KU HOT CURRENT KWATENTHERATU

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 6 июл 2024

Комментарии • 45

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 10 дней назад +4

    Hee bwanji pamaliro achilima munalephela kusegula mlomo chochi bwanji simunena kuti chakwera ali ndi dyela loipa mpaka kupha munthu sure chifukwa cha 5years😢😢😢 machende ake

  • @user-lb6ek3ee6d
    @user-lb6ek3ee6d 9 дней назад +2

    Malawi ndi chitsazo chabwino cha kusauka koma zikukhala zovetsa choni kwambiri mpaka pano ma President adakalibelabe a Malawi ndi President yekhayo yemwe amandisangalatsa Professor Dingu wa Muthalika zimu wawo ukuse mu ntendere adasitha zithu kwambiri osati izi tikuziona panozi manyaka enieni the must go out stupid Government

  • @stevenchirwa5028
    @stevenchirwa5028 10 дней назад +3

    Don't just talk we need action to change Malawi 🇲🇼

  • @yusufbakali
    @yusufbakali 10 дней назад +3

    Nduna zaboma zosezakuba zimangidwe it only one way katangale akhoza kuta akamangidwa no belo ndende basi akagwire

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h 10 дней назад +1

    Kkkkkk anyamata inu leroli ndakupatsani 100 pa 100 ❤❤❤ guys iyiyi ndiye hot current

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 10 дней назад +2

    🙏🙏🙏🙏🙏🙏Anyamata lero muli bwino kwambili 🙏🙏🙏🙏🙏🙏

  • @ahmedmsume1489
    @ahmedmsume1489 9 дней назад

    Akuonesana zikwanje inu lero mwatasa 😂😂😂😂

  • @JustinChiwale
    @JustinChiwale 10 дней назад +1

    Khoswe akakhala pakhate sapheka Malawi we can't fight against corruption

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl 10 дней назад +1

    Talk guys we are together but don't eat baz from chakwera

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 9 дней назад

    Vuto ndale zanthu zimapatsa mphanvu president.koma democracy parliament ndiyomwe imakhala ndi mphanvu yolemba ACB director azipanganso report Ku parliament basi

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 10 дней назад +1

    Abida mia wapelekera bwino kwachakwera😂tiona dzinthu yakumbuyo😂😂

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 9 дней назад

    Kumalawi tili ndivuto katangale sangathe. Chifukwa ndi culture. Katangale ngati mukufuna kuti athe choyamba president akhale oopa Mulungu komaso akhale osanama chachiwiri azikhala ndinthawi yotendera ma office mwazizuzi osawawuza anthu ogwira ntchito. Chachitatu a police a traffic army ikhale yachilungamo ndipo asavere boma pankhani za katangale. Simungathane ndikatamgale pamene oteteza ziko ndi amene akuchita katangale ndiye mukugani anthu angasiye katangale

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 10 дней назад +1

    Lelo mwayakhula zokomela athu osaukano. Osati zachamba zanu zinja.

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 10 дней назад +2

    Kuti katangale kuti athe muphe chakwera ndi chimbava choipa kuchokela kumpingo that's why he kill chilima

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 9 дней назад

    Nkhani ya police kuti alibe uniform sapata zili bwino ngati akuvutika choncho chifukwa apolice wo ndi amene akumanga anthu akamazuzula boma so azivutika motero

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr 10 дней назад

    Ajona mwamvatu malango anga kkk cz ndeumabowa bolako lero ❤

  • @SaukaniMbiliyawanda-ur7zb
    @SaukaniMbiliyawanda-ur7zb 10 дней назад +1

    Amene sanachimweko ayambe kumugenda miyala

  • @AustinNkhula-j6y
    @AustinNkhula-j6y 10 дней назад

    Ttv awunikileni anthu aziwe zenizeni tatopa ife ndianyapapiwa

  • @TarPoor-ye9jx
    @TarPoor-ye9jx 8 дней назад

    Lero ndaziwa kut anthu chilungamo akuchziwa koma mantha mcp ndi chakwera anthu atopa nawo kkkk 😂😂anthu amaba koma tonse yalepera pazonse kuba kuli pa high too much

  • @g_forcemusician4242
    @g_forcemusician4242 10 дней назад +2

    2025 we choose wisely

  • @StevenMjMbama
    @StevenMjMbama 9 дней назад

    Guys big up kwinako muzitchulako mayina aaaanthu amene akumapanga katangale

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o 9 дней назад

    we shall be singing like this for how long

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 10 дней назад

    Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 10 дней назад

    Ambuye mulungu wanga mudapereka mwana wanu modzi yekha yemweyo kufera ifeyo ochimwa kudzuzika yesu chifukwa chaife , kodi ngat mudalora mwana wanu modzi yekha kufera ife ,simungalore yehova wina osakhala mwana wanu kuti angofa yekha kutulo osadwara ai kuti afere ifeyo amalawi tatopa naye ndiy skhale Chakwerayu ambuye ndimvereni mbuye wanga Chakwerayi atifere ife chifukwa wanyañya tikumvutika musadzuze ndimatenda ai akangogona apitilirekonko kuti tipume mbuye wanga ndimvereni yehova chskwerat akutidxuza musakhare chete yehova akhoza kumayesa ngat mulibe phamvu ngat safera kutola koma afeeee chakwera kuti nduna zake ziziwe kuti inuyo mdinu owopsa yehova

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 10 дней назад

    Bon kalindo anayakhula kt aku prison akudandaula kt iwo palibe amapita muziwaganizila km mukati wamisala

  • @user-wx1jt5fd2j
    @user-wx1jt5fd2j 10 дней назад +3

    We need to change this leadership

  • @HarryMsudzula
    @HarryMsudzula 10 дней назад

    Sinanga ntchito zina akanatha kugwira aprison like kugadira mayeso ameneb anaipereka ku mdf omwe sizimayenera kutero malinga ndi nature yantchito yawo

  • @Austinyonah
    @Austinyonah 10 дней назад

    Kuyankhula kwabwino

  • @DalitsoulNchengah
    @DalitsoulNchengah 10 дней назад

    Ulemu wanu

  • @Moses51
    @Moses51 9 дней назад

    Chakwela ndigalu kwabasi

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 10 дней назад

    Aona nyekhwe 2025

  • @Moses51
    @Moses51 9 дней назад

    Aphana 🤣🤣🤣🤣

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 10 дней назад

    Lelo maimatu pachilungamotu kunenachoona chomwe ngakhale ife akumudzi tikuziona masomu boma ili linangolowelamo Kuba basi, chifukwa chilima anangomunamizila kuti apeze mphata Obama bwino, after kuona kuti bodza anapangila chilima kunamizila Kuba, anaona kuti kubako otsogolela anali chakwela chifukwa anatetsa mulandu cholinga amuphe chifukwa anadziwa kuti chilima amadziwa zonse. Chakwela chakwela iweyo mulungu azikupangila za bwino

  • @user-wx1jt5fd2j
    @user-wx1jt5fd2j 10 дней назад

    Anthu ena anagontha ku makhutu chifukwa cha matemberero

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 10 дней назад +1

    Kikikikiki

  • @KanjoIsaac-u1w
    @KanjoIsaac-u1w 9 дней назад

    Kkkkkkkkkkkk

  • @SandramKambalame
    @SandramKambalame 10 дней назад

    Boma ilili ili ndi manyaka

  • @MusaManati-ho4zf
    @MusaManati-ho4zf 10 дней назад

    😂😂😂😂😂😂😂

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 10 дней назад

    In Malawi we consider corruption as a problem.It is not a problem but the result of something.Therefore,to end corruption in Malawi we must list down main causes of corruption and get rid of them.

  • @giftmwango3214
    @giftmwango3214 9 дней назад

    You don't know what you are talking about

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 10 дней назад

    Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 10 дней назад

    Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe