Это видео недоступно.
Сожалеем об этом.

KUZUKUTA NKHANI ZOMWE ZACHITIKA.UKU KWATENTHA 🔥🔥🔥🙌🙌

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 25 авг 2024

Комментарии • 100

  • @CHRISSYBALALIKA
    @CHRISSYBALALIKA Месяц назад +12

    Mukaona munthu akuti MCP my vote ameneyo ndi wa family ya chakwera mwina ndi ankolo ake kapena chakwera anakwatira pakwawo which means phindu la chakwera akuliwona ameneyo wachita zolozeka kwawoko

  • @macdonaldmunthali9895
    @macdonaldmunthali9895 Месяц назад +9

    Very wrong decision,the end of utm.chilima was the only leader with great vision and calmness, you can't make decision out of anger.

  • @user-nc4vi1jt5g
    @user-nc4vi1jt5g Месяц назад +3

    Kabambe afunampando ku utm koma autm samalanaeni mtsogoleli wanu autm sankhani kaliati ndiponso pamasankho adzawina anthu tilinae ndichikhupililo enawa tawaesa akanika

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Месяц назад +1

    Nkhani ndiyomweyo mwamva bwino zikomo kwambiri pamibawa.. God bless you two guys... Mamakutu wava koma wopanda makutu mawa wazakuwawani

  • @lifayohbenson1994
    @lifayohbenson1994 Месяц назад +3

    Ku utm kulibe mphungwe mpungwe
    Winayo chipani chake ndi odya zake alibe mulandu

  • @user-io2uw2me9f
    @user-io2uw2me9f Месяц назад +1

    Anapha dala chilima cholinga anthu abalalike koma mulungu ndiwadongosolo a utm osafooka osatopa osaopa

  • @SharifChibwana
    @SharifChibwana Месяц назад +5

    Bakili Muluzi tv ndi katundu

  • @user-nv3rf7bl7r
    @user-nv3rf7bl7r Месяц назад +2

    Uku nde kuyankhula kopanga umodzi that's y ndimakukondani amibawa chifukwa mumayankhula chilungamo

  • @DavieChiwale
    @DavieChiwale Месяц назад +1

    Apa a UTM Mukapanda kumva zanu izo

  • @PeterTembo-zj5jk
    @PeterTembo-zj5jk Месяц назад

    Dpp moto❤❤❤

  • @ManzyNgoleka
    @ManzyNgoleka Месяц назад

    vuto inu akulu mukukocha ndale mwachidule nanu mulikuseli kwa enaake

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g Месяц назад +2

    MCP my vote ❤❤❤❤❤❤

  • @JazzdMonga-v6e
    @JazzdMonga-v6e Месяц назад +1

    Kumupeza wina akuti mcp my vote
    Amalawi ndichani

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn Месяц назад +2

    Khondo Yochita kutiponyera Mcp kumupanga usi
    LET HIM BE THERE WILL MAKE CONVENTION SOON

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Месяц назад

    Aaa manganya ngati mutu mwake dziyendamo bwino ayi musiyeni ku MCP koko afela nayo limodzi

  • @VincentMbeye
    @VincentMbeye Месяц назад +1

    Yalakwa UTM kuchoka msanga ....awonesa umbuli kwambili

    • @Aqiec09
      @Aqiec09 Месяц назад

      Ndipo usavage wa athu ophunzira umakhumudwisa

  • @daviskamonde4882
    @daviskamonde4882 Месяц назад +2

    Don't lie to us.
    You support MCP.

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Месяц назад +1

    Njawala number one, kaluati number two be careful ndi anthu awiriwa ndi anthu oyipa mutima kwambiri
    We love utm kwambiri koma isakhale ya munthu

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Месяц назад

    Zoona zake anganidze mofasa sure ❤❤❤❤❤

  • @JaphetSakala-pq4fl
    @JaphetSakala-pq4fl Месяц назад +2

    UTM motomoto osadandaula

  • @MosesNanchinga
    @MosesNanchinga Месяц назад

    Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj

  • @TonykalicheloKalichelo
    @TonykalicheloKalichelo Месяц назад +1

    Inu ngat mwin wake amafuna kusazika ndiye mukufuna omusatila atan

  • @lyiemax
    @lyiemax Месяц назад

    Proper narration, big up guys ❤❤❤

  • @RegistermoseskashonKashon
    @RegistermoseskashonKashon Месяц назад +1

    Inu nde munabwela kudzauza amalawi tchutchutchu osat akapilikon enawa ongokamba zinthu zopanda kumutu

  • @user-rf4br1fv2z
    @user-rf4br1fv2z Месяц назад +2

    Mwawathandiza ulemu

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl Месяц назад

    Skc ankafuna kutchoka after kusalemekdza mgwirizano omwe unalipo ndiyeno kutchoka it's a good move komano to agree with ndikutenga mnthu kunja that's wrong indeed

  • @EdsonNjonjo
    @EdsonNjonjo Месяц назад +1

    Munthu uyu akunena zoona

  • @AlliSaiti
    @AlliSaiti Месяц назад +5

    Athu akuda ndife opanda nzeru

  • @OsmanMasamba-ck4mo
    @OsmanMasamba-ck4mo Месяц назад +1

    Manganya iwetu wagulidwa ndichisilu chinzako

  • @FloraBanda-w7t
    @FloraBanda-w7t Месяц назад

    Koma selina 😂😂😂akut kod akabambe akulowela kut 😂😂😂😂

  • @user-ux9ik4zr5x
    @user-ux9ik4zr5x Месяц назад

    Probably the best program

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi Месяц назад +1

    Ndibwino kt atengane okhaokah

  • @StevieTaiza-r9j
    @StevieTaiza-r9j Месяц назад

    Mulungu azikutete bro

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r Месяц назад +1

    Akumatibera zathu zomwezi zamisokho

  • @EstherManda-ex3bc
    @EstherManda-ex3bc Месяц назад +1

    🤣🤣🤣🤣 nkhani zake

  • @Aqiec09
    @Aqiec09 Месяц назад

    Yea that's very true and I see it ku utm utsogoleri unali wa chilima ena onsewa mavuto bola ku MCP komweko mudziwa bwanji mwina the death of chilima was planned with those who are on top blaming MCP for the death yets amafuna mpando wachilimawo why so early kutuluka mugwilizana without solid proof that is MCP guilty , ine unless pa social media muzabwerese real proof how you saw the killing happen that's when I will find them guilty

  • @ChiyembekezoPhiri-sv8nw
    @ChiyembekezoPhiri-sv8nw Месяц назад

    Njawala ndi kaliati mutiwonongera chipani chathu ndakwiya Nanu heavy kuno kuntheu mutisamale awirinu

  • @Ishriss1999
    @Ishriss1999 Месяц назад

    Ma prophet watu koma atilankhilitsa pambali mxiiiiew

  • @mzeewandembonyirongo2972
    @mzeewandembonyirongo2972 Месяц назад

    Gwende u have fairly advised

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w Месяц назад

    Kkk😂😂😂😂😂😂😂😂 anzanga afumu owuka

  • @SabinaNkhoma-sf7kz
    @SabinaNkhoma-sf7kz Месяц назад

    Mmmmm km mcp yaonjeza,zot amalawi akuvutika sakuganizako

  • @user-rx7cc7tc6b
    @user-rx7cc7tc6b Месяц назад +1

    MCP 💥💥💥❣

  • @GiftKaunda-f8j
    @GiftKaunda-f8j Месяц назад

    Analysis yanzeru zozama koma imeneyo?

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga Месяц назад

    anthu atamalankhura ngati mmene ukuyankhulira lweyo anthu akhoza kumachitazinthu mwanzelu

  • @ChrispinKashosha
    @ChrispinKashosha Месяц назад +2

    Mcp ya wina kale

  • @user-he5ol5or7f
    @user-he5ol5or7f Месяц назад

    Gwede is the best

  • @dysonmasiye5736
    @dysonmasiye5736 Месяц назад

    Nduna zomwe zikugawa ndalamazo akumatibera misonkho yathu yomweyi...ifetu maso athu tikuona ndipo tilankhula chaka cha m'ma chino....40million plus just for one meeting business yanji imene akupanga? Apapa zaonekeratu kuti andale amatibera pomwe anthu akufa ndi njala. Ambuye akukuonani ndithu

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 Месяц назад

    Pamaliro wandale athamangitsidwe

  • @JasonMailos
    @JasonMailos Месяц назад

    😢😢😢😂 ozuka kumandao
    Eeeeee kusokonezatu kkkkkkk

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 Месяц назад

    First to comment

  • @MasaukoNyirongo
    @MasaukoNyirongo Месяц назад +1

    😂😂😂😂😂😂😂 koma zinaz abale kkkkkkk kuthamangitsa masiket mudzi kkkk

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c Месяц назад

      😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂Koma abale

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Месяц назад

    Kuwechetamwangajimbilambali

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Месяц назад

    Aaaaa
    Malawi

  • @ZioneMkangadzula
    @ZioneMkangadzula Месяц назад

    utm igawana zida zafikapa angonamizana

  • @chrisgremu740
    @chrisgremu740 Месяц назад +5

    MCP 🔥🔥🔥🔥

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Месяц назад

    Umakwana

  • @PociahMack
    @PociahMack Месяц назад

    Kma nkhani ya a pro andiseketsa bwanj😂😂

  • @PhiriChitani
    @PhiriChitani Месяц назад

    Ndinu a Mcp chokani apa mukuyiwala kuti UTM idayamba yokha without mcp

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Месяц назад

    Usi ndi munthu yimodzi yomwe mwini wa UTM

  • @SprianoJeke
    @SprianoJeke Месяц назад

    Kugawa ndalama Koma ma servants ndee ka salary ka mmanja

  • @SprianoJeke
    @SprianoJeke Месяц назад

    As government I think abalalika ndithu

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga Месяц назад

    vuto amalawi timasapota vitsilu kali ndi ........

  • @user-gk4nu4xr8r
    @user-gk4nu4xr8r Месяц назад

    Of course

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад +2

    akuononga chipani cha utm ndi mai kaliati ndi azao filex njawala anthu awawa ndithu amaliza chipani cha utm samalani

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda Месяц назад

    Ntchindi mulije mu utm

  • @user-kj7hr2jf1l
    @user-kj7hr2jf1l Месяц назад +1

    Zowona utm yisatenge munthu wakunja

  • @atupelemposa4786
    @atupelemposa4786 Месяц назад

    😂😂😂

  • @MayesoKulea-sh8xd
    @MayesoKulea-sh8xd Месяц назад +2

    MCP ☑️

  • @YohaneMotison
    @YohaneMotison Месяц назад

    😂😂😂😂😂😂

  • @PulayaKalaka
    @PulayaKalaka Месяц назад +1

    Mcp mooootooooooooo

  • @user-cb5gh9md4i
    @user-cb5gh9md4i Месяц назад

    Kodi ntchentche zikutanipo pamibawapo

  • @YamikanAbubakary-my4ie
    @YamikanAbubakary-my4ie Месяц назад +1

    Ambuye mulungu daritsani chipani cha mcp 🇲🇼❤️
    🙏🙏

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Месяц назад +1

      Ndiwe opembedza mafano
      Mulungu wa Abraham sangadalitse MCP...siwachisokonezo ngat Chakwera wakoyo...usamutchule Mulungu pachabe...ungaone tsoka

    • @user-px6kt8rx2p
      @user-px6kt8rx2p Месяц назад

      Ukunama ukadakhumudwa mcp chiyembekezo cha Malawi ambiri

    • @robertkalima874
      @robertkalima874 Месяц назад

      @@user-px6kt8rx2p MCP chipani chafuko

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c Месяц назад

      Usatchule dzina lamulungu wako pachabe chome iwe

  • @MosesNanchinga
    @MosesNanchinga Месяц назад

    Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Месяц назад

    Abwenza ndalamazi...eni ake akutuwa kusowa sopo...akuoneka a fumbi lokha lokha km ena akuononga mosaopa Mulungu...ayi tiona posachedwapa....nafe tikudikira

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Месяц назад

    Aaaaa
    Malawi