Chakwera watutumuka zomwe wanena wa Catholic mosaopa pa imfa ya Chilima

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 5 сен 2024

Комментарии • 459

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Месяц назад +39

    I hope bishop mwatumidwa ndi mulungu ❤❤❤❤

  • @YamikaniMwale-bo7cv
    @YamikaniMwale-bo7cv Месяц назад +36

    I will vote next year because of chikangawa accident witnessed by my naked eyes,rest well my handsome VP SKC

  • @EdenEreneo
    @EdenEreneo Месяц назад +16

    Tsoka kwaiye anatengako mbali pa ifa imeneyi sazaona mdalitso Amen 🙏

  • @YamikaniMwale-bo7cv
    @YamikaniMwale-bo7cv Месяц назад +35

    Powerful message,,,we silute you,,,, keep on doing this please

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu Месяц назад +39

    Amen amen amve Mr chikangawa fiti

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Месяц назад +33

    Mawu amphavu kulakhula mosaopa munthu koma kowopa mulungu

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Месяц назад +25

    Mmmmmmm, koma a Bishop inu mwamaliza zonse, ndipo kumene aliko mutu waima Chakwera ndi boma lake la MCP. Tili pa mbuyo panu Bishop, osafowoka, osatopa .❤❤❤❤

  • @MaxwellChiwaya-tv7kn
    @MaxwellChiwaya-tv7kn Месяц назад +27

    Ine mpakana lero sindikumvetsabe kuti Biyeni anamwalira mmmmmmmmm only God knows

  • @user-xm1ic3nr9w
    @user-xm1ic3nr9w Месяц назад +12

    Tiyen tipitilize kuyatsa ma kandulo iziwapweteka daily mpaka kampen wao azakhare opanda mphamvu Amen🙏

  • @JoyceChaima
    @JoyceChaima Месяц назад +13

    Ambuye Mulungu odziwa kuweluza.... aweruze ndithu. MZIMU WA CHILIMA usowetse mtendere aliyense amene anatengako gawo pa infa imeneyi😢😢😢

  • @Hellenistic109
    @Hellenistic109 Месяц назад +6

    Thank You very much Bishop for the Wise Preaching,I Salute You..😢😢😢

  • @chinomwephiri1183
    @chinomwephiri1183 Месяц назад +5

    Amen, and powerful
    SKC, may your soul rest in peace

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma Месяц назад +3

    Powerful massage father,mwatiyankhulira ndipo chakwera am sure wamva ndipo akudziwa kuti next year zake zada or atatani ndi manganya wakeyo mfiti zokupha zimenezi zikapume

  • @MirriamChakanza
    @MirriamChakanza Месяц назад +10

    Powerful message, wakuva wamva. Amen 🙏

  • @EstherChibwana-lp3gx
    @EstherChibwana-lp3gx Месяц назад +8

    Abig message to malawians I salute u bishop

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Месяц назад +12

    Ndipotu zoonadi ambuye kudziwike kuti kuli mulungu pa ifa ya athu amenewa ikhale panutu Pao ndipo china chake chichitike ndithu ❤❤

  • @HashimNyirenda
    @HashimNyirenda Месяц назад +43

    Uthengawu nde ndiwankaka ndi uchi

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Месяц назад +15

    Mathembelelo akhale pamutu pa onse amene anakhudzidwa ndi imfa ya a Chilima ndi anthu 9 mwadzi wawo ukhesedwe pamitu pawo omwe anapanga izi Mudzina la Jehovah's...Amen..

  • @jjhollyland4918
    @jjhollyland4918 Месяц назад +7

    We need this everyday. Men of God come out and preach the truth 🙏

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf Месяц назад +10

    chakwera wazimvera yekha ma umboni apose apo chakwera ndiwe chigawenga ndithu

  • @user-hq2io8nk7s
    @user-hq2io8nk7s Месяц назад +1

    Very very powerful , may God continue giving you fearless speeches for Malawians to know the truth of God.

  • @LuskaMoses
    @LuskaMoses Месяц назад +3

    Ambuye yesu akudakitseni Fathar😢😢😢choonadi chimamasura

  • @Creslevison-vj2sl
    @Creslevison-vj2sl Месяц назад +2

    Aaaa yes bishop watokota chilungamo uyu eshiii i lv the way he cud articulate the whole story fearlessly amidst mr chikangawa eshiii

  • @SildaKatundu
    @SildaKatundu Месяц назад +14

    Uthenga of the year ,2024

  • @MaryAaron-nn8ec
    @MaryAaron-nn8ec Месяц назад +8

    😂😂😂😂Amen pastor and thank u for reminding us that we don't have a president 😂😂😂😂

    • @EstherDebwe
      @EstherDebwe Месяц назад

      Iiiih koma abale😂👐

  • @NeemaMatewere
    @NeemaMatewere Месяц назад

    Powerful gospel,imfa yowawa ngati ya Yesu Christu,ngati yaa Martini Aku Uganda,ngati yaa Postoli
    Mtima woyera WA Yesu,mutichire chisoni,a Martini Aku Uganda mutipemphelerw Ife,woyera ose akumwamba mutipemphelere ife.
    Kuyankhula kulalika zomveka .Amen

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Месяц назад +8

    Achita bwino kulankhula ku tchalichi,,atidyenawo akwiya kuteleku,,koma ali mbuu,,

  • @user-er7ub4ug7y
    @user-er7ub4ug7y Месяц назад +1

    God bless you bishop the power of message

  • @misoMoyo
    @misoMoyo Месяц назад +5

    Munthu wa mlungu wayankhula mosaopa nae ndi okhumudwa ndi IFA ya bambo Biyeni

  • @Hellenistic109
    @Hellenistic109 Месяц назад +1

    Bravo Bishop Bravo tell them..They should know that people are watching..RIP SKC 😭😭😭💔

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Месяц назад +7

    Amen. Pastor uthenga wamveka uyu opanda chilema

  • @user-gd2kl1fx1q
    @user-gd2kl1fx1q Месяц назад +1

    Once catholic always a catholic and our tears for our vp skc will never end until justice prevail

  • @WisdomPupweeMwalilino
    @WisdomPupweeMwalilino Месяц назад +4

    Our God will do it and make us move forward with grace.

  • @user-db5wf7pd7i
    @user-db5wf7pd7i Месяц назад +3

    Uthenga usu ngati Chakwera sanawunve pls mutumizileni awunve.
    Tony Momadi.
    Johannesburg, RSA.

  • @ifristathope1131
    @ifristathope1131 Месяц назад

    Amen bishop🙏🏿 chatsika blood on his hands. God gonna answer our tears. Osaopa osatopa n osafooka we need better Malawi for all not za sikusinjazi

  • @stevenfrancism3638
    @stevenfrancism3638 Месяц назад +2

    mzina la Dada nalamwana Nala mzimu utuwa . Amen.

  • @petroszgambo9949
    @petroszgambo9949 Месяц назад +3

    Still can't believe our Biyeni is really gone forever 😢

  • @user-tw9nl6ks9d
    @user-tw9nl6ks9d Месяц назад +5

    Panopa zomabisa chilungamo zinatha mau awa ndawakonda kulakira kwabwino ndithu Bishop

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h Месяц назад +1

    ❤❤❤❤ bishop anga akutetezeni Yehova choona chidzatimasula ndiye ndiinuyo abusa, a bishop, onse kuunikira anthu anu amen

  • @ChristopherChimbalanga-ez5he
    @ChristopherChimbalanga-ez5he Месяц назад +6

    Indeed chakwera next year azipita bas

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 Месяц назад +2

    We love u bishop .......sitikhala chete ai paka mcp ichoke

  • @AndsonYusufChiwamba-jw3vl
    @AndsonYusufChiwamba-jw3vl Месяц назад +3

    Powerful message to Malawi 🇲🇼

  • @AmosKayira-y1m
    @AmosKayira-y1m Месяц назад

    Amen, that's why am proud of Catholic bishops! 🙏🙏 may his blood be like those of Martyr RIP SKC

  • @IanAllstal
    @IanAllstal Месяц назад +2

    Pachilungamo palibe Mantha ; osaopa .osafooka. osaopa . Koma tizafela mbendela iyiiih 👉🇲🇼🇲🇼🇲🇼

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s Месяц назад +6

    🔥🔥🔥🔥🔥 Mr Chikangawaa uveee ndithuuu

  • @SangwaniNkosi
    @SangwaniNkosi Месяц назад +2

    Amen mtumiki wamulungu,chilungamo mwanena ndithu

  • @DoYouKnow3838
    @DoYouKnow3838 Месяц назад +1

    What a powerful message 😢❤

  • @fannyzimba149
    @fannyzimba149 Месяц назад +4

    Amen indeed 😭😭😭😭😭 timenyereni nkhondo mulungu kumwambako

  • @EmmanuelNgambi-y6h
    @EmmanuelNgambi-y6h Месяц назад +4

    Mbusa wachilungamo ,,,,,,,,mulungu akudalitseni abusa

  • @IgnatiousFote
    @IgnatiousFote Месяц назад +6

    kkkkkkkk anthu akufuna chilungamo mantha palibe

  • @TonyMhone
    @TonyMhone Месяц назад +2

    Amen. Munthu wa Mulungu walalikira mopanda mantha.

  • @liz9425
    @liz9425 Месяц назад

    Lord protect this pastor for us we want more of them to come out . SKC ❤

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwela Месяц назад +2

    Amen,mafunso alipo nmitima mwathu ambuye okha akudziwa

  • @martinnyirongo2892
    @martinnyirongo2892 Месяц назад +4

    Amen and amen chauta akalange azibusa ena amene a kupanga nawo katangale muboma limeneli amen

    • @EmmanuelNgambi-y6h
      @EmmanuelNgambi-y6h Месяц назад +1

      Amen

    • @user-ec4jo9cu4d
      @user-ec4jo9cu4d Месяц назад +1

      Amen " Katangaleyo olo atamapanga km ine chikundipweteka imfa ya my favorite mzimu wake uwuse mumtendere mpaka kale😭😭😭😭😭💔💔

    • @GraceMwase
      @GraceMwase Месяц назад

      Ndipo akawafulatile asakawamverenso chisoni

  • @ShabaniKuswere
    @ShabaniKuswere Месяц назад +2

    Koma akuluakulu anthu akatopa amakhala atopa ndaona😂😂😂

  • @lameckmbeza6532
    @lameckmbeza6532 Месяц назад +1

    Straight to the point amen 🙏 prist

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Месяц назад +3

    Chakwera ndi mbuzi yachabe chabe ..ndichimunthu choipitsitsa pa zolengedwa zonse...matembelero a Mulungu,angero ,komanso onse amene amadziwa kutembelera akhale kwa chakwera oipa kwambiri😏😏😏😏😏

  • @MATTHEWSANDREWMANDUTU
    @MATTHEWSANDREWMANDUTU Месяц назад +4

    Mmmmmm achakwera muzivere nokha akuti tilbe tsogoleri nanga inu ndindani kodi?awa akutemberelani mufune musafune simuzalamulanso dziko lamalawi

  • @RuthMasamba-ms2di
    @RuthMasamba-ms2di Месяц назад

    Amen and amen, kma2 kudziwike ambuye kt mumatha

  • @user-ml4bl2ll2g
    @user-ml4bl2ll2g Месяц назад

    Very powerful message indeed Ambuye akudalitseni father

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 3 дня назад

    Kuiponda fadah. Kuipatsa Fire. OSAOPA, OSAFOOKA,OSATOPA.

  • @chipiesato-ut7hx
    @chipiesato-ut7hx Месяц назад +2

    Amen Amen powerful message ❤❤❤🎉

  • @NedsonMatia
    @NedsonMatia Месяц назад +2

    Amen amen ntumiki anve zimenezi oyipau nfiti

  • @Gwedeza-oz3jv
    @Gwedeza-oz3jv Месяц назад +1

    6:52 Kulankhula mosaopa osati enawa. Amalekeza wakuphayo chigawenga kamba Koti wapatsidwa ndalama , uwu ndiye utsogoleli osati abusa ndi asheikh ena Aja aaa anangoziwikiratu Kuti akugulitsa mawu aMulungu Kwa chikangawa (chakwera) ndi ntengo wotsika mukankhanthidwa patsiku lomaliza ndipo mukasowa kothawila ndalama mubazo sizikakuthandizani chifukwa kuzakhala kulibe,

    • @GraceMwase
      @GraceMwase Месяц назад

      Azibusa ena mzimu ndi mphamvu za Mulungu zinawachokela kalekale angokhala zitsiru kumakalandira ndalama kwa chakwera chigawenga chouma mtima ngati chimenechi chisatana

  • @thomasbotha9790
    @thomasbotha9790 Месяц назад +1

    Powerful preaching mau Amphamvu

  • @user-ec4jo9cu4d
    @user-ec4jo9cu4d Месяц назад +2

    Chilima Rest well 😭😭😭😭imfa yokhumudwisa kwambili

  • @CathrineBizza
    @CathrineBizza Месяц назад +3

    Chikablngawa ipangitsa kuti ena aluze Zisankho ndipo zoxhitika

  • @user-ml4bl2ll2g
    @user-ml4bl2ll2g Месяц назад

    I love the Catholics they stand on the truth may God bless you all

  • @SabeehaIbrahim-h1y
    @SabeehaIbrahim-h1y Месяц назад +3

    Amen Man of God

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q Месяц назад +3

    Uthenga uwu umufikire chakwera nimumene anamuphera chirima

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa Месяц назад +3

    Nenaso kuti chakwela ndi fit wakupha anthu MCP ndi anthu oipa kwambili

  • @BwanaGD
    @BwanaGD Месяц назад +3

    Chibaluwa chawelengedwa kupita kwa babo chikangawa zivele mtoloooooo kuchikagawakooooo

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v Месяц назад

    The Catholics are very powerful 🔥🔥🔥🔥

  • @user-wq8ul6tu5t
    @user-wq8ul6tu5t Месяц назад +1

    Powerful massage

  • @mussamapira801
    @mussamapira801 Месяц назад

    Mwamvatu a chakwera ngakhale mukubisa umboni anthu akutopelani poti chilungamo nchowawa kuyamba kumanga koma mwa Allah mwini chisoni ndichifundo Ali nafe Ameen mwa Allah

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete Месяц назад +3

    Akatolika aying'alura nawo kuno tamvani 😂😂😂

  • @JustinaKadammanja-u1z
    @JustinaKadammanja-u1z 29 дней назад

    Powerful words chilungamo ichi

  • @AlifeChiwanda
    @AlifeChiwanda Месяц назад

    Amen ndipo mulungu akudalitseni Muthu uyu chilango alandila ndithu mulungu sagona

  • @AubreyThipa-zc6vs
    @AubreyThipa-zc6vs Месяц назад +4

    Ulaliki umafuna amen wamphavu uwu😂😂😂😂😂😂

  • @lukepangani1373
    @lukepangani1373 Месяц назад

    If there's change let's change for better Us Malawian

  • @CheGuevarraAbubaker
    @CheGuevarraAbubaker Месяц назад +3

    Eya umeneondiye ulaliki abusa osamaopa osafoka osatopa

  • @JonathanMsiska
    @JonathanMsiska Месяц назад +2

    Chowonadi chiwoneke abusa thank you.

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 Месяц назад

    I salute you bishop 🙏🙏🙏🙏🙏🙏

  • @user-ko1lk3br4r
    @user-ko1lk3br4r Месяц назад +3

    Pajatu ngakhale wandale amapitaso ku church

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j Месяц назад +4

    Bambo mfumu Anga samanyengerera kuzuzula

  • @user-nm7wm1ew1k
    @user-nm7wm1ew1k Месяц назад +2

    Am proud to be a Catholic

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Месяц назад

    Zowona, i really surprised how people should go for rest while people are missing, my first time

  • @ratkillermusic8482
    @ratkillermusic8482 Месяц назад +3

    Koma ulaliki uwu ulibwino heavy

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg Месяц назад +2

    Zimangondimvekera ngat ali penapake SKC mpaka lero,

  • @MosesKamtndo
    @MosesKamtndo Месяц назад +2

    Zoona zimakhala zowawa that's y people usually say chilumgamo ndi mwano

  • @PaulineKamwana
    @PaulineKamwana Месяц назад

    Popangira vn ndipati abale amzanga?Km chikangawa chakwera wazimva izi ?SKC rest in peace 💔

  • @MaryKhoropa
    @MaryKhoropa Месяц назад +3

    Amen, wakumva amve, osamva akhale?

  • @PidoMaganga
    @PidoMaganga Месяц назад

    Zandinvesa chisoni nkatolika kulilila mwana wake SKC😢😢😢😢😢😢

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Месяц назад +3

    😂😂 chakwera warepera udindo amtulepazi dziko waliono nga

  • @user-qq1uj7ct6n
    @user-qq1uj7ct6n Месяц назад

    Kulalika mosaopa. Koma chilungamo chokha chokha. 🇲🇼🇲🇼😭😭😭😭😭😭

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu Месяц назад

    Osawopa.... kuyankhula koma uku osawanyengelera awa aziuzidwa chilungamo evil people Ambuye achite nanu

  • @elsiekandiona7321
    @elsiekandiona7321 Месяц назад

    Uthenga okhathamira bwino Amen

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 Месяц назад +2

    Ulaliki koma umenewu ndinthu.......

  • @user-pc7hj7hs5v
    @user-pc7hj7hs5v Месяц назад

    Mmmgh am intoxicated with this message

  • @successm-vt3dx
    @successm-vt3dx Месяц назад +4

    amen and amen