Malawi Archbishop Thomas Msusa on Saulos Chilima demise & what happened in Chikangawa with the plane
HTML-код
- Опубликовано: 6 фев 2025
- "Ngozi iyi itachitika inenso ndinali ndi mafunso ambiri ndipo sindinafune kufunsa aliyense! Koma ndinafunsa mboni yeniyeni yomwe inali ku Chikangawa" - Arch Bishop Thomas Luke Msusa
SUBSCRIBE here for more videos goo.gl/aYvIXK
Malawi videos in English and Chichewa
Powerful sermon. Anthu timayembekeza anena munthu amene anaona zose but there was wisdom from holy spirit in his sermon😢
God bless you, Bishop, for the word of wisdom, reconciliation, and peace. Indeed blessed are the peace maker for they shall be.called the children of God. Watching from Zambia. God bless you 🇲🇼
Powerful.....i wish Bishop Zuza came back to life... i have missed his preaching a lot..
Eish sure
Powerful and insipirational message. AMEN🇨🇦🇲🇼
Blessed are peace makers 🙏. A word to heal broken hearts
Blessed are the peace makers. Indeed powerful message our Bishop
Great words, God speaking through his people
Glory to God, for your teaching bishop .
Thank you Bishop for the wise and comforting words for the broken hearts 💔💔💔
Great message of peace and reconciliation and ❤❤
Powerful teachings 🎉🎉🎉
Strong, reconciliation words "ngodala amene amazetsa mtendere" from Capetown.
Nzoonadi chitsime chimaoneka chachitali madzi akathamo, never forget the late right honourable Dr saulos Klaus chilima
Kulira kwa Bishop Thomas Msusa, "Mboni yanga ndi Mulungu"
Powerful,glory be to God
Thank you for the good message sir.
Great preaching
This was powerful 💪
LONG-LIVE PAX ROMANA IN MALAWI
Zoona braza msusa bi up
God is in control
Zoona ambuye nsusa
Blessed are the peace makers
Nkhani ndi mboni 😭😭😭😭
AZIUTSA NDI NTHENDERE AMEN
Timusiye mulungu akhale mulungu coz chirungamo akudziwa ndi ambuye ndipo mulungu samalakwitsa
Odala ndi ati? Jehovah shalomu.
God bless you
Ulaliki wozama amalawi tichite manyazi pazochita zathu sibwino kupereka maumbonl onama pazinthu zomwe sitidaone
Pray hard papa
Amen 🙏🎉🎉
Ndale mu mpingo ayi,chilungamo akudziwa ndi amene anatilenga palibenso wina wakuposa iye
Nthawi zina anthu odalilika ngati awa kumabisa chilungamo zimakaikisa chifukwa ndi amene timawadalira pachilungamo ulaliki uwu uli ndi zokaikisa mkati mwake amalimbana ndikunena mbiri ya a chilima ngati ndi akumbumba so sad
Mwatero get the message violence not
Inu muli nacho chilungamo .......?
Inu nde ambumba? Aaah
Amen
😢😢
Amaonaso mitima yosweka. Misozi ikamatuluka zonsezi amaona
Ndipo ABUSA mulungu akudalitseni kwakukulu ndi mau amphamvu anthu amakonda kuweluza ngati iwowo siochimwa ayiitu eeeee
powerful preaching
Who are you targeting??
Munthu onkhulupirira mulungu samankhumudwa mosweka mtima coz amadziwa kuti imfa simathero azonse
Ameen ameen
Tiwakumbukira Mr chilima mpaka infa yanga
❤
Uyu ndiwankhondo osati opemphera ayi
Uthenga km umenewo
Wadya banz mmbusa uyu
Great preaching
Amen
Amen
Amen
Amen amen
Amen
Amen
Amen
Amen
Amen
Amen