Malawi Archbishop Thomas Msusa on Saulos Chilima demise & what happened in Chikangawa with the plane

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 6 фев 2025
  • "Ngozi iyi itachitika inenso ndinali ndi mafunso ambiri ndipo sindinafune kufunsa aliyense! Koma ndinafunsa mboni yeniyeni yomwe inali ku Chikangawa" - Arch Bishop Thomas Luke Msusa
    SUBSCRIBE here for more videos goo.gl/aYvIXK
    Malawi videos in English and Chichewa

Комментарии • 61

  • @paulinekayuni1621
    @paulinekayuni1621 7 месяцев назад +13

    Powerful sermon. Anthu timayembekeza anena munthu amene anaona zose but there was wisdom from holy spirit in his sermon😢

  • @anniechisanga246
    @anniechisanga246 7 месяцев назад +4

    God bless you, Bishop, for the word of wisdom, reconciliation, and peace. Indeed blessed are the peace maker for they shall be.called the children of God. Watching from Zambia. God bless you 🇲🇼

  • @henrymalepula2934
    @henrymalepula2934 7 месяцев назад +3

    Powerful.....i wish Bishop Zuza came back to life... i have missed his preaching a lot..

  • @rosebymunthali7505
    @rosebymunthali7505 7 месяцев назад +4

    Powerful and insipirational message. AMEN🇨🇦🇲🇼

  • @Phukira
    @Phukira 7 месяцев назад +3

    Blessed are peace makers 🙏. A word to heal broken hearts

  • @hildahchiluba6702
    @hildahchiluba6702 7 месяцев назад +1

    Blessed are the peace makers. Indeed powerful message our Bishop

  • @JustusSNkhata
    @JustusSNkhata 7 месяцев назад +3

    Great words, God speaking through his people

  • @AugustineChilongo
    @AugustineChilongo 7 месяцев назад +1

    Glory to God, for your teaching bishop .

  • @mirriamphiri7032
    @mirriamphiri7032 7 месяцев назад

    Thank you Bishop for the wise and comforting words for the broken hearts 💔💔💔

  • @leonardzchavula3139
    @leonardzchavula3139 7 месяцев назад +2

    Great message of peace and reconciliation and ❤❤

  • @LucianoMtima
    @LucianoMtima 7 месяцев назад +2

    Powerful teachings 🎉🎉🎉

  • @Andrew-u5i8n
    @Andrew-u5i8n 7 месяцев назад +2

    Strong, reconciliation words "ngodala amene amazetsa mtendere" from Capetown.

  • @JereChimwemwe
    @JereChimwemwe 27 дней назад

    Nzoonadi chitsime chimaoneka chachitali madzi akathamo, never forget the late right honourable Dr saulos Klaus chilima

  • @JoelTchuma-g3s
    @JoelTchuma-g3s Месяц назад

    Kulira kwa Bishop Thomas Msusa, "Mboni yanga ndi Mulungu"

  • @CleverChaphamnkhwani
    @CleverChaphamnkhwani Месяц назад

    Powerful,glory be to God

  • @WilfredYekha
    @WilfredYekha 7 месяцев назад

    Thank you for the good message sir.

  • @arnoldchikopa2611
    @arnoldchikopa2611 7 месяцев назад

    Great preaching

  • @nathannbanda3345
    @nathannbanda3345 7 месяцев назад

    This was powerful 💪

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 7 месяцев назад +1

    LONG-LIVE PAX ROMANA IN MALAWI

  • @SenzoAyati
    @SenzoAyati Месяц назад

    Zoona braza msusa bi up

  • @ChancyMaphuza
    @ChancyMaphuza 7 месяцев назад +1

    God is in control

  • @NdumbaMurora
    @NdumbaMurora 7 дней назад

    Zoona ambuye nsusa

  • @DIVASONMAKIYI
    @DIVASONMAKIYI 7 месяцев назад

    Blessed are the peace makers

  • @REXCHARLESKAJAWO
    @REXCHARLESKAJAWO 7 месяцев назад +1

    Nkhani ndi mboni 😭😭😭😭

  • @ChristinaNkwanda
    @ChristinaNkwanda 7 месяцев назад +1

    AZIUTSA NDI NTHENDERE AMEN

  • @FaithJimm
    @FaithJimm Месяц назад +1

    Timusiye mulungu akhale mulungu coz chirungamo akudziwa ndi ambuye ndipo mulungu samalakwitsa

  • @JoelTchuma-g3s
    @JoelTchuma-g3s Месяц назад

    Odala ndi ati? Jehovah shalomu.

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 7 месяцев назад

    God bless you

  • @CharlesBanda-kv8bh
    @CharlesBanda-kv8bh 7 месяцев назад +4

    Ulaliki wozama amalawi tichite manyazi pazochita zathu sibwino kupereka maumbonl onama pazinthu zomwe sitidaone

  • @ZondoChirwa
    @ZondoChirwa 7 месяцев назад

    Pray hard papa

  • @StainNkandawire
    @StainNkandawire Месяц назад

    Amen 🙏🎉🎉

  • @JohnKamkwamba
    @JohnKamkwamba Месяц назад

    Ndale mu mpingo ayi,chilungamo akudziwa ndi amene anatilenga palibenso wina wakuposa iye

  • @AugustineMwamadi
    @AugustineMwamadi 7 месяцев назад

    Nthawi zina anthu odalilika ngati awa kumabisa chilungamo zimakaikisa chifukwa ndi amene timawadalira pachilungamo ulaliki uwu uli ndi zokaikisa mkati mwake amalimbana ndikunena mbiri ya a chilima ngati ndi akumbumba so sad

  • @AgnessSilungwe-x1n
    @AgnessSilungwe-x1n 7 месяцев назад

    Amen

  • @ChauncyKampayi
    @ChauncyKampayi 7 месяцев назад

    😢😢

  • @ChancyMaphuza
    @ChancyMaphuza 7 месяцев назад

    Amaonaso mitima yosweka. Misozi ikamatuluka zonsezi amaona

  • @cosmaskhonje
    @cosmaskhonje 7 месяцев назад +2

    Ndipo ABUSA mulungu akudalitseni kwakukulu ndi mau amphamvu anthu amakonda kuweluza ngati iwowo siochimwa ayiitu eeeee

  • @FaithJimm
    @FaithJimm Месяц назад

    Munthu onkhulupirira mulungu samankhumudwa mosweka mtima coz amadziwa kuti imfa simathero azonse

  • @AdbossKusweje
    @AdbossKusweje 7 месяцев назад

    Ameen ameen

  • @HappyLuhanga-f8g
    @HappyLuhanga-f8g 2 месяца назад

    Tiwakumbukira Mr chilima mpaka infa yanga

  • @rodglae6657
    @rodglae6657 7 месяцев назад

  • @NkalakathaPanje
    @NkalakathaPanje Месяц назад

    Uyu ndiwankhondo osati opemphera ayi

  • @NtopeLucias
    @NtopeLucias Месяц назад

    Uthenga km umenewo

  • @RodgersCalenNYIRENDA-yg8rg
    @RodgersCalenNYIRENDA-yg8rg 7 месяцев назад

    Wadya banz mmbusa uyu

  • @arnoldchikopa2611
    @arnoldchikopa2611 7 месяцев назад

    Great preaching

  • @SamsonGondwe-ut7mk
    @SamsonGondwe-ut7mk 7 месяцев назад +2

    Amen

  • @joelgondwe2983
    @joelgondwe2983 7 месяцев назад

    Amen

  • @nicholasmweghama5062
    @nicholasmweghama5062 7 месяцев назад +1

    Amen

  • @estawilson9998
    @estawilson9998 7 месяцев назад

    Amen amen

  • @martinkasamba1576
    @martinkasamba1576 7 месяцев назад

    Amen

  • @FezHenz
    @FezHenz 7 месяцев назад

    Amen

  • @madakabichi2251
    @madakabichi2251 7 месяцев назад +1

    Amen

  • @racheldongolosi2252
    @racheldongolosi2252 7 месяцев назад

    Amen

  • @KilembeAtuganile
    @KilembeAtuganile 3 месяца назад

    Amen

  • @GertrudeKaipa
    @GertrudeKaipa 3 месяца назад

    Amen