Imfa la Saulos Chilima. Kulira kwa niece wa Bingu, Abiti Wiliam Dawood.

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 26 авг 2024
  • SUBSCRIBE here for more videos goo.gl/aYvIXK
    Malawi videos in English and Chichewa

Комментарии • 169

  • @ProphetessEzinass-qu4ir
    @ProphetessEzinass-qu4ir Месяц назад +2

    Iam not politica but this is the truth and awesome people chose to save gods and no justice . Continue to put sense in malawias God bless you

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx Месяц назад +25

    Michael usi alibe chilungamo and ndidamuona chilima akuzengedwa mlandu olo tsiku limodzi sadapite

  • @OwamThoko
    @OwamThoko Месяц назад +1

    Powerful massage,I'm a man but you make me feel pain like I'm in labour to gv birth to a baby ,100 % I agree with you,GOD protect you from this ng,ona,n bless you,you are the angel of malawians,keep it up❤❤❤❤ 25:47

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 Месяц назад +5

    Abiti ndi Deal, long live Sis

  • @user-sz2wg7ug8i
    @user-sz2wg7ug8i Месяц назад +1

    Asis speech yanu it's powerful 👏 🙌 a Malawi 🇲🇼 tiyeni tichose matha amene tili nawo dziwani kuti onena chilungamo adzaona mwayi pamapeto amoyo wake

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 Месяц назад +4

    You make me cry also ma'am,,, God is watching Malawi and whatever is happening in Malawi God is there 😢

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms Месяц назад +1

    Powerful message mom god bless you indeed it was painful.

  • @josephchitsulo5882
    @josephchitsulo5882 Месяц назад +3

    You make me cry too 😢

  • @victorauwana7258
    @victorauwana7258 Месяц назад +4

    So sad ... Mcp people are not sleeping anymore

  • @elvienyirenda-ln3dm
    @elvienyirenda-ln3dm Месяц назад +2

    Mai zoona zokhazokha mukukambazi. I wish you were here, muthandizane ndi Bon Kalindo.

  • @AbuBakrIqrah
    @AbuBakrIqrah Месяц назад +2

    😢😢😢 sister indeed you made me cry a lot

  • @josephgabriel5941
    @josephgabriel5941 Месяц назад +8

    I absolutely agree with you. Nothing to subtract or add. You have said it all

  • @MaxwellMbesa
    @MaxwellMbesa Месяц назад +1

    GOD bless you Sister power full keep on sharing what ever is coming from our party

  • @memoryziyaya2593
    @memoryziyaya2593 Месяц назад

    i love the blief dear sis...what a plain tuth ..wow!!i salute u love💥🤝

  • @andreabanda7838
    @andreabanda7838 Месяц назад

    Thanx so much madam. This is great for local Malawians.
    As you keep keep advocating for change. Please factor in the perspectives of the manifesto - such as freedom education, in secondary schools, even in the universities. Eradication of corruption. Change of some elements of sections constitution such as why the VP without real jobs descriptions.
    Kulira kwanu tonse tikulira. UTM please be strong. It’s only some 13 months to go. People don’t want this MCP thing.

  • @ishmaelsiffah9900
    @ishmaelsiffah9900 Месяц назад +7

    Tipemphe anthu aku Chilimba asamupatse manganya vote, munthu ameneyu ndi traitor sure

    • @laurentchisambi4984
      @laurentchisambi4984 Месяц назад

      Nayeso tsiku lake lizakwana,mulingo womwe umayesa nawo nzako naweso mulungu azakuyesa nawo.

  • @user-cy3js1sf2u
    @user-cy3js1sf2u Месяц назад +2

    Mcp bolaosamusowetsatu mayi you akulila malilo abwana ake 😢😢😢

  • @CathreenKadwala
    @CathreenKadwala Месяц назад +1

    Abiti God bless you, zitiyankhulirani plz tikanena ife atimangatu

  • @HanifMoses
    @HanifMoses Месяц назад +7

    MCP singawineso

  • @user-te3ps3kf2t
    @user-te3ps3kf2t Месяц назад +1

    l agree with you sister,your are tolking the truth, Molingana ndimmene mwafotokozelamu musalolere kukhalabe pa mngwilizano ndi mcp chifukwa a Bwanawa Sanali ku chipani cha UTM ,mubwelele ku gwilizano pokhapokha ngati malemu Saulosi chilima angadzuke kumanda kudzapitiliza mngwilizano ndi mcp not Bwana usi chifukwa akuoneka ngati anali a independent, according to your statement.

  • @TressLuka
    @TressLuka Месяц назад +3

    You make me cry tòo Aunt 😢😢😢 . Pipo ayi zikomo chikondi palibeee😢😢😢😢

  • @FrancisDay-br7xb
    @FrancisDay-br7xb Месяц назад +3

    Mzimayi akulira

  • @user-mf8fi8wt5d
    @user-mf8fi8wt5d Месяц назад +2

    Koma Ku UTM Ku Kuli azimayi okongola heavy...SKC ndi idea for sure mama

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Месяц назад +2

    Mwazi wa saulos supita pachabe ai..... Ndipo mulungu sangalore kuti mizimu ya anthu 9 isabale zipatso

  • @MiliamManda
    @MiliamManda Месяц назад

    Or aphee adadi wioo komabe tivotela My alipo a my Mrs Mary Chilima siazawinaso a Chakwera 2025 UTM yiwinakale takozeka ife kuwapanga sport My Mary Chilima❤❤

  • @WitnessPhiri-zr9uf
    @WitnessPhiri-zr9uf Месяц назад

    😢eish zopweteka ndinthu God bless you sister

  • @user-ul5hh3cz8z
    @user-ul5hh3cz8z Месяц назад +2

    Powerful massage sister kumalawi kwaza afiti mudzipanimu there not have future anthu anapita school zakamuzu alibwe kuti mawa kubwelanji

  • @LanceLance-mj4kc
    @LanceLance-mj4kc Месяц назад

    We are all crying,& others we don't believ that he is gone for gud

  • @EmmanuelZiba-qz6ug
    @EmmanuelZiba-qz6ug Месяц назад

    😢😢😢😢😢 or Zambian 🇿🇲🇿🇲🇿🇲 we are crying 😭😭😭

  • @user-yc3ik9dq3x
    @user-yc3ik9dq3x Месяц назад +1

    TRUE WORDS SISTER 😢

  • @doreenKamwendo
    @doreenKamwendo Месяц назад

    Facts dear

  • @burtonamin5913
    @burtonamin5913 Месяц назад +1

    Congratulations sister

  • @umalimaganga
    @umalimaganga Месяц назад +4

    I like you ndinu wolimba mtima Mayi👍🔥

  • @arnoldkaikenkayange
    @arnoldkaikenkayange Месяц назад +1

    Powerful

  • @MiliamManda
    @MiliamManda Месяц назад +1

    Mkunena zowona auntie zikolanthu lili ndimatha kwambiri

  • @user-do9of5uo6s
    @user-do9of5uo6s Месяц назад +1

    Kkkkkk wandiwaza kufazafaze kukoko basi

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Месяц назад +1

    Amene muli nchipani cha UTM munvere uthenga uwu mulungu alowelelepo

  • @MphatsoMhoney-xn2ft
    @MphatsoMhoney-xn2ft Месяц назад +4

    Zuka malawi

  • @lindamalunjika6581
    @lindamalunjika6581 Месяц назад +1

    powerful

  • @dingim1234
    @dingim1234 Месяц назад +2

    Zodanwitsadi zikuchitika ndi Michael Usi.
    Money root Of evil.
    POLITICS is a dirty game.
    Malawi opposition is wealth.
    Anankhumwa ankati a Chakwera asiye udvinding, later zoo anagulidwa anatseka pakamwa.
    But who is fearless to

  • @AliceChitaukali-e5q
    @AliceChitaukali-e5q Месяц назад +1

    Why us 😭😭

  • @IanAllstal
    @IanAllstal 21 день назад

    Kunamveka kufuura kupempha thandizo Koma olo ndi moziyemwe otulukira mmm my Biyeni

  • @sakalameck
    @sakalameck Месяц назад +1

    Manganya is an opportunist.

  • @user-tm9el7tj7h
    @user-tm9el7tj7h 19 дней назад

    Truth is always bitter

  • @Agin2pex-ms3di
    @Agin2pex-ms3di Месяц назад

    Am touched 😢

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee Месяц назад +2

    Komatu nde mwayakhula chilungamo,mwa chapa anthu oyipa mitima ngati ngati awa sinamvepo,

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z Месяц назад +1

    Nai warila uyu mmmmhhhh ndalira

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne Месяц назад +3

    Chakwera ndi wopusa and misara yake

  • @WestonGawaza
    @WestonGawaza Месяц назад +1

    UTM mwana wake ayimilile u president, mayi chirima akoza kuyima pa president or Brayani Banda to bepresident ku UTM MCP yakupha kuyambira karekale

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo Месяц назад +2

    Powerful enough

  • @sayidimisessa
    @sayidimisessa Месяц назад +1

    Zoona azimayi nanu onesani nkwiyo

  • @EdnaSiyan
    @EdnaSiyan Месяц назад

    Very powerful

  • @corretabanda7685
    @corretabanda7685 Месяц назад

    Im really behind you cc. Michael usi aliko okha ku MCP komwe aliko

  • @wonganimwase9881
    @wonganimwase9881 Месяц назад +4

    Those 9 people were murdered in cold blood.

  • @JoyousDaveson
    @JoyousDaveson Месяц назад

    Ndipo ife tikulira everyday for SKC kufa imfa yowawa inuuu

  • @FredKanyerere
    @FredKanyerere Месяц назад

    Thats true cc.

  • @ZogoZeko
    @ZogoZeko Месяц назад

    Pano ndithawi yokonda utm

  • @MiliamManda
    @MiliamManda Месяц назад +1

    Koma atiphera sogolo lanthu kwambiri chifukwa Malawi pano ai siwalibwino ai

  • @fairkabambo6386
    @fairkabambo6386 Месяц назад +1

    zikuveka bwino ndife amasiye

  • @user-jn3bg6tj1q
    @user-jn3bg6tj1q Месяц назад

    Namwera ❤

  • @JoyceNkhokwe
    @JoyceNkhokwe Месяц назад +1

    Mayi palibe kuloza mukuyankhula bho ndiye poti chilungamo chimapweteka go deeper maah

  • @dingim1234
    @dingim1234 Месяц назад +1

    Zodanwitsadi zikuchitika ndi Michael Usi.
    Money root Of evil.

  • @Franklinclothingcarpentry
    @Franklinclothingcarpentry Месяц назад

    I cant even believe up yo now that he is nomore

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili Месяц назад +1

    Tikavotera Apm basi

  • @JONAHMWALUGHALI
    @JONAHMWALUGHALI Месяц назад

    koma imfa ya Bingu wa mthalika how did it go?

  • @user-nm8gp1du2m
    @user-nm8gp1du2m Месяц назад +1

    MUNTHU OGANIZA BWINO SANGAVOTERE MCP.. AMISALA OKHAOKHA NDI AMENE NGA VOTELE MCP.

  • @PreciousChisale
    @PreciousChisale Месяц назад

    pandiwadza ndiapapa eti pa TANZANIA zikuwayendera ndi munthu wamai pachiongolero pamene ife ndi bambo ,malawi vuto ndi chani

  • @user-iz1qi3db2g
    @user-iz1qi3db2g Месяц назад

    Yes komadi awudzeni amenewo athu avetse

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s Месяц назад +1

    Izo ndiye zoona acc Mcp ndiyankhaza

  • @Agin2pex-ms3di
    @Agin2pex-ms3di Месяц назад

    😢so sad

  • @user-ky4ce9gb6j
    @user-ky4ce9gb6j 25 дней назад

    Zomvesa chisoni kwambiri mmm

  • @user-tw1jo5xu9r
    @user-tw1jo5xu9r Месяц назад

    Thats true

  • @JoannaMbando
    @JoannaMbando Месяц назад

    Madam you are talking.

  • @BlessingsMakalani
    @BlessingsMakalani Месяц назад

    💯 Dzoona zake izi

  • @MichaelWilliamsNyirenda
    @MichaelWilliamsNyirenda Месяц назад +1

    Si aphunzitsi okha police, mw Army' ndi Anthu wovutika kwa basi koma pano munthu kuyankhula za boma eti ndikumanga that's nonsense of them

  • @josiahgarley3824
    @josiahgarley3824 Месяц назад

    Amen

  • @user-do9of5uo6s
    @user-do9of5uo6s Месяц назад

    None munjigale mwejiiii kkkkk

  • @OsmanAyatu
    @OsmanAyatu Месяц назад

    Basi siyani kulira tonse tidzafa

  • @IsaacSemu
    @IsaacSemu 4 дня назад

    Iwe sungatipangire maganizo athu pangazako

  • @MiliamManda
    @MiliamManda Месяц назад

    Apa bola apesani a my Mrs Chilima u president osalimbanasi ku ku vote ai a my alumbiluseni basi Chakwera achoke wabakwakwana

  • @chrispinekaludzu864
    @chrispinekaludzu864 Месяц назад +2

    Ku America mkokoma amai

    • @user-dm2fs6hf1b
      @user-dm2fs6hf1b Месяц назад

      What do you mean apa mayiwa akuyankhula za mzeru tsono what does it mean ku America mkokopa please yankhulan za nzeru athu tikulira imfa ya chirima

  • @GrinTemboh
    @GrinTemboh Месяц назад

    Tiyenayo ku fasefaze yachiyawo yeleyo

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Месяц назад

    Sister mukulankhula zowona zokhazokha, mcp alongside usi ndang'azi agule ozola manyi kudambwe.
    Do me a favour please our beloved sister, mmene mwayamba kubwera chomchimu , pitilizani musasiye ayi , menyani nkhondo imeneyi mothandizana ndi Limpopo FM with comrade Mtanyiwa , Bakili Muluzi tv, Bon Kalindo and others please.
    Poyamba ndimkawona ngati amalawife ndiofasa koma it's not dat kufasa as such!, amalawi ndife anthu opusa kwambiri , timayang'anila zinthu zikuonongeka pamaso pathu

  • @JamesZanelo-iv1wb
    @JamesZanelo-iv1wb Месяц назад

    Usi is an opportunist,he has Never been a member of UTM.

  • @ELLENKANJERE
    @ELLENKANJERE Месяц назад

    Tiyeni nazo amayi mwalakhura ndithu sindinu Mai mwatumindwa ndimzimu ghoyera ndiumene ukulakhura zikomo pitilizani

  • @MatemboGondwe
    @MatemboGondwe Месяц назад

    ❤❤

  • @eliaskachali-xn2ve
    @eliaskachali-xn2ve Месяц назад

    Bwanji a UTM ,asankhe mukazi wa chilima akhale presedent wa UTM , Anthu ife tikamuvotere?

  • @gaddiemkandawire6436
    @gaddiemkandawire6436 Месяц назад

    Malawi anthu ndia manthandi

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx Месяц назад +1

    2025 ndikuona kuchedwa kt tichotse mcp and chakwera

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Месяц назад

      Komanso chakwerayo akafere kundende ...he will never be allowed out.komanso Ma boarder onse tidzatseka ...tidzamuvula zovsla adzakhale pa mphepo ngt mmene adapangira chilima

  • @user-jn3bg6tj1q
    @user-jn3bg6tj1q Месяц назад

    MHSRIP

  • @ZogoZeko
    @ZogoZeko Месяц назад

    Manngqnya musiyeni angwa nayo mcp yakupha kuyambiira kale chilima atipwetekesa kugwilizana ndi mcp

  • @KereeditseMotsetse
    @KereeditseMotsetse Месяц назад

    Muthu akavoteledwe okufa iwe galu eti

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete Месяц назад

    Chilima akanakhala kuti amatikonda ife amalawi bwanji sanachoke ku mcp ataona kuti zimene amafuna sizimachitika personal he was a good guy political zero for me

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Месяц назад +1

    Usi is a hypocrite, ndinthira kuwiri amene anampereka chilima mmanja mwa zigawenga za crocodiles dancer mcp patty and dat we know for sure.
    I had request sister, i need a capital please, der's no one whom I can ask apart from u sister, zinthu sizilibwino mdziko muno

  • @augustMag
    @augustMag Месяц назад

    Mulungu apitilize kukusogolerani cct Chilungamo chokha chokha ku Malawi matha ndiwo timawayika pasogolo ndi chifukwa dziko lino tikukumana ndi mavuto ufulu tikuugulisa ndi ndalama Usi wapala kwaoko anthu zasankondanso ngati azawine andifuse ndithu

  • @ZintleSotshange
    @ZintleSotshange Месяц назад

    Anatigulisa ku mcp ukulele chani iweso unalu momo ziyipe lero sukudya nawo

  • @eliaskachali-xn2ve
    @eliaskachali-xn2ve Месяц назад

    Sorry sister , Chakwera galu yeniyeni. Amalawi no vote for MCP.

  • @Shadrick-lq6oj
    @Shadrick-lq6oj Месяц назад

    Mahule awa akulila Poona kuti ntanji wavuta

  • @pierrebanda1176
    @pierrebanda1176 Месяц назад

    Kadzibwerani mudZatule Malawi osamangotukula kaniwake tidzawone luso lanu Mai osangolole kwaniwake

  • @gersommalama
    @gersommalama Месяц назад +1

    Why do people want all of us to feel sorry for their loss. All of us knew Chilima and we also know that he passed on. Death is final you can't expect us to moun him forever. Accept that God allowed it. Please don't insult us by calling us cowards. Don't expect us to fight your battles. You and your relatives gang up and fight your battles don't use our poverty for your benefit. Leave

    • @frankjolijo
      @frankjolijo Месяц назад

      God allowed what!!?!... wake up from your sleep and slumber....... Politicians are thieves, crooks and murderers