AMENE WAULURA ZA CHINSISI CHA JOYCE BANDA NDI LAZARUS CHAKWERA LIVE LIVE PA NSOKHANO WA PP UJA UYU

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 9 сен 2024

Комментарии • 113

  • @JeanKambala-gm1zr
    @JeanKambala-gm1zr Месяц назад +25

    Sangasiyane ngwilizana wawo ndi wamaganzi kuteloko mayi Joyce Bandah ,,ngankhale muli akulu Anga Koma lmfa yachilima mudziwapo kanthu inuyo ,,

    • @PhillspicJere
      @PhillspicJere Месяц назад +2

      Mutu wanu ndiobonga amai Inu, mgwilizano wa DPP ndi UDF siwamagazi?

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 29 дней назад +3

      @@PhillspicJerechokani inu mulibe mzeru palibe chomwe mudziwa mmutu mwanu mwangodzadza manyi umuuzeso chakwera kuti machende ake anapha chilima

    • @PhillspicJere
      @PhillspicJere 29 дней назад

      @@Musa1828-l5d Ndiwe mwana phone ndiyako koma uziona Zotukwana komaso owatukwana

    • @chippakaribafox2865
      @chippakaribafox2865 28 дней назад +1

      Obvious....she can do anything for money shame

    • @ThokoLungu-tq6pw
      @ThokoLungu-tq6pw 10 дней назад

      Akuziwadi kwambili mmayi oipa uyuuuuu alape

  • @charlesnankumba9991
    @charlesnankumba9991 8 дней назад

    Those that think that Dr. Joyce Banda is a spent force in Malawian politics are cheating themselves and at the same time misleading others. Dr.Joyce Banda is and will still continue to be a highly respectable force in Malawian politics. There are so many good and great things Dr. Joyce Banda has done for Malawians and continues to do which Malawians of good will and sound reasoning will never forget. Long Live Amayi!

  • @EvanceLumeyo
    @EvanceLumeyo Месяц назад +8

    Asatanic okhaokha ndi Mr chikangawa iyah..

  • @AustinBornface
    @AustinBornface Месяц назад +9

    Ndiye china nkumati Mutharika wakula? ifetu tikungofuna fertilizer tizidya nthalo yambiri

  • @SophiaKalonga
    @SophiaKalonga Месяц назад +3

    I love this man eeshhh

  • @WisemanMunthali
    @WisemanMunthali День назад

    Titamakhala ndi anthu ngati awa mziko olankhula chilungamo bwedzi ziko likuyenda bwino

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr Месяц назад +2

    Komatu zomatenga amalawi ngati nyape zanuzo ife timadya nawo musatitole osaukafe musamale,,,,kulankhula kwabwanji uku? Timve ziti? Muona ngati ndi nthawi zopusitsana panoso?

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope 29 дней назад +1

    Joyce Banda osavotera ndikape ndi munthu mmodzi safunira amalawi zabwino mutayeni

  • @andrewchiyembekezadimba7173
    @andrewchiyembekezadimba7173 Месяц назад +1

    Akuluwa nzeru mulibemo. Iye akuti mgwirizano sunathe pamene amai ananena kuti anauzidwa MCP ikalowa ku convention ndiye kuti mgwirizano watha

  • @ShaidaJackson
    @ShaidaJackson 7 дней назад

    Agalu inu asatanic okhha okha,tikumana 2025

  • @ElizaLabson
    @ElizaLabson 8 дней назад

    Adadiiii moto buuu!!¡

  • @ClementsKamanga
    @ClementsKamanga 9 дней назад

    Chokhacho achimwene mwauponda mcp ndimbola

  • @user-qv4yu2ir2k
    @user-qv4yu2ir2k Месяц назад +2

    Cashgeti people's paty

  • @Kamwachale
    @Kamwachale Месяц назад

    Politics at its best. PP is still with MCP. This is a strategy of dividing votes in the south. Amalawi akupenya masiku ano sangapusitsidwe

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w 29 дней назад

    Moonse NDinu amane mukuzunza Malawi ,vote Kwa Dadie basi

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 21 день назад

    Inu palibe chanu chipani cha satanic chakwela palibe za vote

  • @AshimayeGama
    @AshimayeGama Месяц назад +1

    Gashiketi yokhayokha kulibetu ndege yogulitsa kumalawi anagwetsa chakwela ndiye akadzawina maiwa

  • @EmanuelFundudwa
    @EmanuelFundudwa 3 дня назад

    Nkhani yabwino hvy

  • @innocentlipita3630
    @innocentlipita3630 Месяц назад +1

    Anthu ngati pa msonkhano wa fumu wa macopoun

  • @user-ld8gb9xm7v
    @user-ld8gb9xm7v Месяц назад +1

    Mmphuno mwako

  • @user-ld8gb9xm7v
    @user-ld8gb9xm7v Месяц назад +1

    Ndimwe wa tonse alliance mavwele yinu

  • @stewart.mwamughunda
    @stewart.mwamughunda 21 день назад

    Kondwani Nakhumwa chikapeta Chakwera bwana mkonzeke kukalowa Ku state house 2025

  • @amoschisisi2070
    @amoschisisi2070 Месяц назад

    It only happens in a federal government

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Месяц назад +1

    😂😂😂😂😂😂 Inu munaziyipisila mu trauser chifukwa cha tonse alliance simuzawinanso agalu inu😂😂😂😂😂

  • @Martinmkapangakapanga
    @Martinmkapangakapanga Месяц назад +1

    koma ambuliwu amalawi changamukani

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Месяц назад

    Zinawakanika awa analamulira dzaka za Bingu ziwiri basi koma Bambo uyu wakhura za nzeru Koma mai athuwa akuba

  • @PatienceHarry-z7h
    @PatienceHarry-z7h 16 дней назад

    Mcp zake zada basi

  • @user-jb5yb9wq3y
    @user-jb5yb9wq3y Месяц назад

    Mabindi (masanje) APM my vote

    • @damianokachingwe3531
      @damianokachingwe3531 Месяц назад

      Kutaya vote my friend kumeneko think nicely

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga Месяц назад

      Kagwere uko mufuna muphe tonse ndi chifunga tikakuviterani ​@@damianokachingwe3531

    • @tamalangoma2765
      @tamalangoma2765 Месяц назад +1

      Eti munthu wanzeru zoona angavotele Peter kkkkkkkkk

  • @user-ww9rj2wx8d
    @user-ww9rj2wx8d Месяц назад

    Zamanyi basi mesa Joyce Banda yo ndi mfiti anatigulisa kwa chakwela yo hiyaaaa

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Месяц назад

    Kuonekerathu kuti muri pamodzi ndi Mcp mkufuna kunamiza amalawi muona pa 2025

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 Месяц назад +1

    Kodi mukadali ku mcp eeeti?? Ayi tamva

  • @KensonMsiska
    @KensonMsiska Месяц назад +1

    😂,,,😂😂 palibepo Cha nzeru apa

  • @user-ku3gk4fz5i
    @user-ku3gk4fz5i Месяц назад +1

    Ingotulukani ku mcp inu

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Месяц назад

    Inu muli ku Mcp musatiputsitse kuteroko nde kuti kutsogoloko chachiziwikire midzapanga mgwirizano ndi mcp

  • @kondwanichirambo7797
    @kondwanichirambo7797 Месяц назад +3

    Bakili muluzi TV yokha nde ya nzeru zinazi zimakhala ngat mwa chiphwilikiti

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma Месяц назад +1

    Mfundo za ziii

  • @happynyirenda8790
    @happynyirenda8790 29 дней назад

    Kanyamata aka boza ngati katsikana ka 15 yrs old

  • @FlywellThengo
    @FlywellThengo Месяц назад

    Kunena zoona mulamuliro wanu amayi zinthu zimaenda km ife tili pambuyo panu mai 2024 moto kt buuuuuuuuuuiiiiiiiii

  • @MangaDamiano
    @MangaDamiano Месяц назад +1

    Mwasowa chochita Kodi ?

  • @EddenKamanga
    @EddenKamanga 19 дней назад

    Chasowa chochita inu

  • @faidaceciliaYekha
    @faidaceciliaYekha Месяц назад +1

    Kkkkkk kuiyang'alura😂

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 18 дней назад

    AGALU kwabasi inu mbavu satanic nokha nokha simungawinenso afiti inu ndi chikangawa wanuyo

  • @user-rv7tk8cv2q
    @user-rv7tk8cv2q Месяц назад +4

    Your Back ground music ndibwino kuyichosa zizimveka boh boh

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Месяц назад +1

    kodí zílimótero et

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 Месяц назад

    Zilombo za chakwera

  • @ednanamboyachilambe6901
    @ednanamboyachilambe6901 3 дня назад

    Hahaha koma ndale kkk

  • @tobiousmtenje139
    @tobiousmtenje139 Месяц назад

    Ubwino wake mwavomereza kuti mafumu akuvutika.Mavutowo ndye akuta wina aliyense

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn Месяц назад +1

    Kod chilipo chipan ichi et

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g Месяц назад

    ATUMIDWA KUTAPA MA VOTE A KUMMWERA A DPP.

  • @LovelyAntenna-jh8yh
    @LovelyAntenna-jh8yh Месяц назад +1

    Kuyankhula kwamanyi uku nkotani

  • @lastonekaponya7675
    @lastonekaponya7675 16 дней назад

    Salu zikugawidwa koma sakuvala mudzifuse

  • @henrymwale8994
    @henrymwale8994 Месяц назад

    Koma timvereni ma followers anu background sound yo muchotse ikumatisokoneza

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona Месяц назад

    Mai Joice banda imfa ya chilima akuidziwa

  • @godrickmapepu2754
    @godrickmapepu2754 Месяц назад

    A Joice Banda tazisiyani izi. That time you had that opportunity because of death and you can't win your dreams.

  • @SpiweJambo
    @SpiweJambo Месяц назад

    Zee one films

  • @RoseChiphiri-ts8jx
    @RoseChiphiri-ts8jx Месяц назад

    Moni kwa mr Chikaonda ku chipani kwanuko 😂😂😂

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g Месяц назад

    ❤❤❤❤❤ 50 +1

  • @voicedumathindwa
    @voicedumathindwa 20 дней назад

    Joyce chipani chako ndi chakwanu konko ndi zisilu zakozo

  • @user-nj4pn8gx7y
    @user-nj4pn8gx7y Месяц назад

    50+1🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @CassimMbalaka
    @CassimMbalaka Месяц назад

    Zaziiiiiiii tixivaso za mcp pano

  • @MaggieCement
    @MaggieCement Месяц назад

    Za ziiiiiiiiii kwanu kunatha Inu limbani mtima

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m 27 дней назад

    Musapepelese anthu Mai inu

  • @johnkambala692
    @johnkambala692 Месяц назад +1

    Aimed basi

  • @SmilingFishingRod-zc4wx
    @SmilingFishingRod-zc4wx Месяц назад

    Kkkkk koma anthu akafuna kum'bera wankulu eeeee amanama koopsya. M'bereni Ali ndi ndalama zomwe anaba kuzera mu Caschgate tuyeni naoni musamukhumudwise m'beleni

  • @IgnatiousFote
    @IgnatiousFote Месяц назад

    chivunde ali nd mfundo mbambande koma chipanichi chamuchepela kwmbr

  • @PrinceTaibuBanda
    @PrinceTaibuBanda 29 дней назад

    Good

  • @grantkangombe6804
    @grantkangombe6804 Месяц назад

    Ndiye ngati akukayikirana kuba chitenje what more ndalama za boma?

  • @IgnatiousFote
    @IgnatiousFote Месяц назад

    Kod chivunde first name ndindan

  • @Martinmkapangakapanga
    @Martinmkapangakapanga Месяц назад

    mukuwapusisa amalawi awuzeni Zoona

  • @MoreenHussein
    @MoreenHussein 22 дня назад

    Tinadzidzukadi zoona Ng,alulula basi ,tachika nacho kutali

  • @esaumtambo-d3h
    @esaumtambo-d3h 22 дня назад

    Anthuwa atiwonjeza ife ovota atifuna pompano

  • @WisilamuSaid
    @WisilamuSaid Месяц назад

    Musezeseni katundu muzakana kumutura pasogolo

  • @ShaibuAmeck-z5w
    @ShaibuAmeck-z5w Месяц назад

    Aaaaa awa ndi anthu okuba

  • @user-yq1mc3nm1f
    @user-yq1mc3nm1f 29 дней назад

    Kkkkk Joyce banda amakhala mu fernbrook estate muno pa Stage wood street apa ife tinali kumuona tsiku ndi tsiku and olo amufunse anena kuti zoona. Ku America Joyce adakhalako liti ? Joyce amakhala mu fourways/ Johannesburg Fernbrook estate - kenako anasamukila ku Dainfern ndikomwe anamumangila kuti abwelere ku Malawi zaku America mukuzitenga kuti agalu inu

  • @aliemohammed5853
    @aliemohammed5853 25 дней назад

    Achakwela mundu jwamatama

  • @BEATRICE-t7k
    @BEATRICE-t7k 12 дней назад

    Mhuu!!!

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 Месяц назад

    Awa angomasuka basi atulukamo mu gwilizano wa Tonse alliance

  • @CatheySichari
    @CatheySichari 29 дней назад

    Tikuvoteran may tavutika mokwana

  • @AlihAmdulillah
    @AlihAmdulillah Месяц назад

    Zaazii kuti ziveke bwanji inuyo

  • @PatienceHarry-z7h
    @PatienceHarry-z7h 16 дней назад

    Koma ndiye mutimatiza

  • @user-hx6jd4yy4u
    @user-hx6jd4yy4u Месяц назад

    Hi

  • @kearabetswemashego3084
    @kearabetswemashego3084 Месяц назад

    Hhhh kom inu mupangisa kuti chakwira awine hhhh

  • @YobuMbawa
    @YobuMbawa 26 дней назад

    Kkkkk kwachema ku pp

  • @JosephKandapako
    @JosephKandapako Месяц назад

    Ulemuwanu amai ine ndichisanzo chabwino ulamulilowanu unatisithadi achinyamata mmalawimuno munasitha dziko lamalawi masiku owelengeka amalawi tiwakumbukile anapangazabwino❤

  • @JusticeKalemba
    @JusticeKalemba Месяц назад

    Vinyo watha

  • @BridgetZingani-gb8yf
    @BridgetZingani-gb8yf Месяц назад

    Kutereku zolinga zao nzimenezi? Mwayaluka. That's why speech ya mai sikumveka mutu wake kkkkkk

  • @StainMlamba-x5e
    @StainMlamba-x5e 25 дней назад

    Amapocholol

  • @KaungaYawaka
    @KaungaYawaka Месяц назад +1

    😂😂😂😂

  • @TimothyKabumbuKendrix
    @TimothyKabumbuKendrix Месяц назад +1

    😅😅😅😅

  • @esaumtambo-d3h
    @esaumtambo-d3h 22 дня назад

    Chaka cha mawa chakwera no vot

  • @GrealishMulimah-y5i
    @GrealishMulimah-y5i Месяц назад

    Ine vote yanga ilikwa may

  • @MaggieMuhone-r7m
    @MaggieMuhone-r7m Месяц назад

    Kkkkkkk Kkkkkkk Kkkkkkk