Bon Kalindo Ndi Guru lake la Malawi first ayankhura izi pamene anapangitsa press conference lero

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 27 авг 2024

Комментарии • 172

  • @user-mg5yy5hk9t
    @user-mg5yy5hk9t Месяц назад

    Anganga Alula malawi fist member all the way from mangochi mamatiyimilira mr big man keept up mangochi yosaopayo

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Месяц назад +8

    Ndipo athu inuyo tchito mukuigwila mulungu azikusungani ndi moyo maka Mr boni kalindo simutopa mwamangidwa kambili mbili mukanakhala wina bwezi mutatisiya ife athu osauka sikuti ndinu Muthu ovutika ayi koma mumasiya pogona pabwino zakudya zabwino kukagona Malo onyasa chifukwa Cha ife aphawi kuzipeleka m,sembe pokhapo mulungu adzikudalitsani ❤❤

    • @RiyemaDomybusiness
      @RiyemaDomybusiness Месяц назад +1

      Exactly 💯💯 bon amatiyimirila ampwawi

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d Месяц назад

      @@RiyemaDomybusiness sure tidziwapephelela ndithu athu amenewa

  • @VungaQueen
    @VungaQueen Месяц назад +9

    Boni Kalindo munthu wotiyimilira 🔥🔥🔥

  • @Moses51
    @Moses51 Месяц назад +3

    The Dc bon kalindo keep up update 💪💪🇲🇼🇲🇼💯 osawopa

  • @user-ez8uk7py8n
    @user-ez8uk7py8n Месяц назад +3

    That is true it needs all Malawian to vote as long as he/ she is Malawian Mr president keep continue loving your poor people abd our country Malawi proud of you thanks

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj Месяц назад +4

    I respect your Mr nkalindo together with Malawian fest and the cautrry everyone DC is so powerful as well and you are always welcome to our team of Malawi wholld my Allah bless you always about the what happened with Malawian

    • @esaMoha-dm4kj
      @esaMoha-dm4kj Месяц назад

      I am a Malawi but now I'm in the sauth Africa estan about working on

  • @WysonJalamu
    @WysonJalamu Месяц назад +8

    Big up the DC osatopa, osafowoka, osawopa malawi ndi wathu uyu, tili limodzi pa nsewu basi.

  • @user-ml4bl2ll2g
    @user-ml4bl2ll2g Месяц назад +9

    Please please ife TIKUFUNA ufulu wathu wovota a MCP asauchotse ponamizira ma id, aliyense akuyenera kukavota popanda id

    • @Franklifo2217
      @Franklifo2217 Месяц назад

      Nzelu mulibe enanu! Anthu omwe mumalephelesa malawi kutukuka🙌

    • @hudycorex1893
      @hudycorex1893 Месяц назад

      Inu amzeru kwambiri?​@@Franklifo2217

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c Месяц назад

      Anzeru ndinuyo? ​@@Franklifo2217

  • @MussaHassani-zg1hm
    @MussaHassani-zg1hm Месяц назад +1

    This is our president kalindo thanks so much for your help Malawias

  • @DavieBinzih
    @DavieBinzih Месяц назад +1

    More fire mr kalindo we proudly of you keept up we love you

  • @YousufMpunga
    @YousufMpunga Месяц назад +3

    Ndine Yusuf wakumangochi kmnso amalawi amene Ali kumaiko akunja apasidwe mwai wovota kuchokera kunja konko kumene ali

    • @patrickmacheso5062
      @patrickmacheso5062 Месяц назад

      That's true, we need to vote and choose the President that we want not this Manyaka Government, but the problem is Akazembe athu sathandiza or kuwapempha kuti atipatse mwayi ovota.

  • @WezzieChimuzi-ek7bk
    @WezzieChimuzi-ek7bk Месяц назад +1

    Good job my people Ambuye azikutetezelani ndi mwanzi wawo nthawi zonse ..

  • @user-uf4db7im7d
    @user-uf4db7im7d Месяц назад +1

    This government must go

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q Месяц назад +1

    yaa wa mcp ngati akunyasidwa ni boni karindo asavere khani zake ayi chonde ife anthu osauka tiyeni tizimuvera boni koma uzayime iwe boni tizakuvotere

  • @user-uf4db7im7d
    @user-uf4db7im7d Месяц назад

    Every malawian should be in a possession of ID, If the NRB is failing to reach all malawians for ID registration, you should expect Malawi to be on fire, because voting results will not be accepted, People have rights to vote for who they want not rigging.

  • @FrankSpison-o7o
    @FrankSpison-o7o Месяц назад

    The Dccccccc Booooooooon kalindo inu nde anthu oti mzika zamalawi tizikupemphererani kwambili 🙏

  • @NellieKabvina
    @NellieKabvina Месяц назад +1

    Pa ziphatsopo ndie zikudabwitsa zikupezeka kuti anthu ambiri akumadziwa tsiku lokuti akumaliza kupanga ma ID,,,sakulengeza tsiku loyamba anthu ambiri akudandaula

  • @harrisonlowheat6569
    @harrisonlowheat6569 Месяц назад +1

    My president

  • @RemaniNkhoma
    @RemaniNkhoma Месяц назад +1

    boni karindo tingopita mawa bwanji pa sewu kuti agaru awa tiwakhawurise

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 Месяц назад

    Lets presure dem evo!....aluta continua!

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e Месяц назад

    Good move Malawi First ❤

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj Месяц назад +1

    I respect your nkalindo bisid ashankwela and everyone else has been in the path of mcp I don't respect anyone anymore because the people who keep and keeling Malawian people 2025 mashall Allah bless you nkalindo 😮😮😮

  • @ChristopherMadulira
    @ChristopherMadulira Месяц назад

    Congugulations Mr DC ntchito mukugwila anthu inu only God bless you ❤❤❤❤❤

  • @AnussaAlli
    @AnussaAlli Месяц назад

    Big up the DC Bon kalindo continue timakunyadlan❤❤❤❤❤❤🎉🎉

  • @jogechawa6192
    @jogechawa6192 Месяц назад +2

    Bon Kalindo and malawi first our hope basi

  • @dawsonwaya4722
    @dawsonwaya4722 Месяц назад

    Za ziiiiiiiii munthu unalephera kuimirira constituency ndiye ukati amalawi osauka aaaa zangokuvutani Moya, .

    • @robenallie6985
      @robenallie6985 Месяц назад

      Ndizako zimenezo dc number 1

    • @FatimaAyami
      @FatimaAyami Месяц назад

      Vuto ndi bomalo iyeyo amangopanga imprement

  • @OdettaLowrence
    @OdettaLowrence Месяц назад

    Ulemu wanu Mr Born 🙏🙏🙏🙏

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3z Месяц назад +1

    Boni karido ndikatundu

  • @SamKaposa-i5c
    @SamKaposa-i5c Месяц назад

    Viva malawi first Richard mphepo umadziwa kuyankhula more fire dc

  • @Okalekale
    @Okalekale 25 дней назад

    Tikufuna tidziwe kuti ndi ndani amapanga sponsor gulu lanuli Mr.Kalindo?.The nation should know if you claim to advocate for transparence.

  • @BacklinebwanaliBwanali
    @BacklinebwanaliBwanali Месяц назад +2

    Akupatsen moyo was utali

  • @user-dq9oe8sp8k
    @user-dq9oe8sp8k Месяц назад

    Ifetu though tilibe ma ID kma tikazavota
    Angoona kuzinamidza agwapewa
    Fireeee the DC❤

  • @KeftonChimaliro
    @KeftonChimaliro Месяц назад

    Iyayi zonsezitu akupangazi akufuna ndalama mtambo samachitaso chocho anango kuwapatsa zochita ndikungokhala duuu osayakhulaso amalawi anthuwo ndi amodzi Lucia's. Anayimba kale

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer Месяц назад +5

    Wa mcp ngt born kalindo amakunyasa usamaver nkhan Zak iwey ndy opanda zelu ife tikufuna dziko libwerer ngt kal osat mukumakambo shem on you 😢😢😢😢

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 Месяц назад

    Well done guys kpt up

  • @YohaneChitapini
    @YohaneChitapini Месяц назад +1

    Mumakwana ndipo ndinu nokha boss ndagwada ndikumvesela

  • @MikeKoloko
    @MikeKoloko Месяц назад

    Mumatiimilira, big up

  • @usherjamson174
    @usherjamson174 Месяц назад

    Mulungu azikhala namu guy's 💪💪

  • @MercyJohnsonkanchure
    @MercyJohnsonkanchure Месяц назад

    Mr Kalindo Mulungu azikupansani zeru zakuya ngati Solomon ❤

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo Месяц назад

    Never give up guys let's see what happens

  • @ShariffAbdul-m9t
    @ShariffAbdul-m9t Месяц назад

    I salute you

  • @TiyamikeMakande
    @TiyamikeMakande 28 дней назад

    Mumatiuankhulira ndinu bwana ,mutiyankhulireso za ndrama za masiye ku Capital hill Chaka chino nchachitatu ndrama sakutipatsa tikuvutika ndi ana

  • @RanaQari-py4bd
    @RanaQari-py4bd Месяц назад

    Mumakwana guys we love you all the time 🙏🙏🙏🔥🔥🔥🔥

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q Месяц назад

    Malawi first all the best u are representing poor people. To be honest Malawi is the poorest country in the world our leaders are selfish we are going backwards.

  • @AlidWidon
    @AlidWidon Месяц назад

    Wosawopa bon kalindo tili limodxi 💪💪💪🔥🔥🔥👆👆

  • @AndrewNyondo-ut3gk
    @AndrewNyondo-ut3gk Месяц назад

    King David bon kalindo the DC❤

  • @lastonkandiyado4526
    @lastonkandiyado4526 Месяц назад

    Respect 🎉🎉🎉

  • @HarrisonMangani
    @HarrisonMangani Месяц назад

    They need to address those issues other wise Mmmmm panunkha mphira

  • @nelsonmhango7515
    @nelsonmhango7515 Месяц назад

    Inu ndi king

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Месяц назад +3

    Pick up guys chilungamo ndimwano

    • @patrickmacheso5062
      @patrickmacheso5062 Месяц назад

      Ndimayesa ngati mukhala kumbuyo kwa a name anu kkkkkkkk let's fight together, this country is belongs to all Malawians not MCP only.

  • @RanaQari-py4bd
    @RanaQari-py4bd Месяц назад

    🙏🙏🙏🙏🙏 Thnx good work

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 Месяц назад

    The DC ❤

  • @KhalidwePentani-c6q
    @KhalidwePentani-c6q Месяц назад

    Zopanda ntchito izo akalindo mumangofuna udindo ngat mungakwanitse kutumikila dziko aaaa zawumbuli

  • @ImanRashidi-so4oo
    @ImanRashidi-so4oo Месяц назад

    Congratulations mr DC

  • @GodisoneNoel
    @GodisoneNoel Месяц назад

    Asirikali achirendo muzikorathu zichepe mr DC

  • @GetrudeBanda-sd1yf
    @GetrudeBanda-sd1yf Месяц назад

    Only GOd Bless you DC

  • @MuhammedNtaba
    @MuhammedNtaba Месяц назад +1

    ❤❤❤ The DC

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Месяц назад +2

    Akumangeni ngati mwaphwanya malamulo dala mbuli

    • @kenmasta
      @kenmasta Месяц назад

      Ndiye mmene akumamumangamo ndiye akumamupeza ndi milandu yanji,,,,..ndaletu zisakusokonezeni mchimwene andale amabwera amapita koma Malawi adzakhala yemweyu ndiye let's love Malawi.

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Месяц назад

      @@kenmasta mwanena nokha awa asiyeni koma akanalankhula zinthu zambili ndi za against popeza ine ndinapanga nawo compain ndiye sanandipatse udindo awona, zimenezo ndi zabodza,chikuwawe sichimanga dziko amwe awa ndi a ndale musokonekera sayamika ndi ankhwidzi amafuna zawo ziwayendere kalindo akudya makobidi inu mukudya nawo 🤗🤗 ayi so bola yesu

  • @user-dy5bj9ck5e
    @user-dy5bj9ck5e Месяц назад +3

    The DCCC

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli Месяц назад

    Good move bafethu salute you

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 Месяц назад

    Point of correction not guru lake koma Born kalindo ndi guru la Malawi 🇲🇼 first

  • @YohaneChitapini
    @YohaneChitapini Месяц назад +1

    Guys inu musazafe mulungu azikudalisani

  • @PempheroMoleni
    @PempheroMoleni Месяц назад

    Firr the DC

  • @EliasMcray
    @EliasMcray Месяц назад

    Go go ahead

  • @AnockyDavidd
    @AnockyDavidd Месяц назад

    Congratulations to all

  • @gracetjomane-jj3ib
    @gracetjomane-jj3ib Месяц назад

    Kutundu uyu the DC❤❤❤❤❤❤

  • @SueWahna
    @SueWahna Месяц назад

    Big up Malawi first 💪💪

  • @Fridayasani
    @Fridayasani Месяц назад

    Osawopha Bon kalindo tikukupembela kwamulungu Kuti anzikala nawe kwina kulikonse komwe udziyenda

  • @ambeweburton
    @ambeweburton Месяц назад

    Timenyeleni nkhondo please mulungu imvani kulira kwathu

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e Месяц назад +1

    ❤❤❤❤ guys

  • @PetroMatias
    @PetroMatias Месяц назад

    Amarawig fct muri nbi mfunbo zabwini timakuyamikirani

  • @InnocentKavalo
    @InnocentKavalo Месяц назад +1

    Zoona big umakwana dc

  • @Malambia
    @Malambia Месяц назад +1

    Mr kalindo ulemu wanu

  • @ritchardchakuma5725
    @ritchardchakuma5725 Месяц назад +1

    Apomwayikwanisa maiko enasaziwa Chichewa pakufunika ayaluke mbavazi 💯🔥🔥🔥🔥🔥

  • @kurhikhoza8298
    @kurhikhoza8298 Месяц назад

    Tipiya pa sewu akapanda kuyakha

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3z Месяц назад

    Zikomo boni karindo umatiyimilila big Kom amalawi sitimayamika

  • @user-dy4gc2hr5e
    @user-dy4gc2hr5e Месяц назад +1

    Good move

  • @AgnessChiwalo
    @AgnessChiwalo Месяц назад

    Your good man bon

  • @LukaJaulanchirwa
    @LukaJaulanchirwa Месяц назад +1

    You people you thinking harder that is good Diction thank chakwera is not thinking

  • @chikoko-uj2tt
    @chikoko-uj2tt Месяц назад

    Salute 🫡 The DC

  • @ntandokazindzwana3083
    @ntandokazindzwana3083 Месяц назад

    Fire fire tili pa mbuso pa malawi oyambirira

  • @JafaliAjusa-zg2xi
    @JafaliAjusa-zg2xi Месяц назад

    Respect Mr

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm Месяц назад

    The DC'S mwana woooopsa kwambiri chilungamo chiyende ngat madzi.

  • @AgnessChiwalo
    @AgnessChiwalo Месяц назад

    ❤❤❤ good news

  • @shephardlonex3371
    @shephardlonex3371 Месяц назад

    Booooooooni kalindo

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo Месяц назад

    Go konko bwana DC❤

  • @HajaSande
    @HajaSande Месяц назад +1

    Zikomo kwambiri umawona patali

  • @PreciousKARINGANIZA
    @PreciousKARINGANIZA Месяц назад

    Tilikomweko

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj Месяц назад

    Following with all my chidwi

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 Месяц назад

    I'm sure, the government you will grant our request

  • @MaryNgola
    @MaryNgola Месяц назад +2

    Mmene wafikira Malawi alipodi amene akumamuona uyu kt akupanga zolakwika? Iweyotu wa MCP nkana akukubowa

  • @shephardlonex3371
    @shephardlonex3371 Месяц назад

    Munene kuti ife ngati A Dpp

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i Месяц назад

    ❤❤❤💯💯🔥🔥🔥

  • @RitaKainga
    @RitaKainga Месяц назад

    Auzen anthu adyerawo amve ndithu

  • @JoshuaNyirongo
    @JoshuaNyirongo Месяц назад

    Go konko..

  • @user-hr6dj4xc8l
    @user-hr6dj4xc8l Месяц назад

    Koma mukuvutikatu kwambiri, munayambilira muja

  • @user-ru6fc3qy5n
    @user-ru6fc3qy5n Месяц назад

    Zilibwino kwambili osaopa

  • @kashmirmohakashmirmoha8659
    @kashmirmohakashmirmoha8659 Месяц назад

    Ulemu wanu DC😊😊

  • @ShadreckChimaimba-l9y
    @ShadreckChimaimba-l9y Месяц назад

    Kunoso kwachitika zodabwitsa kunkhoma

  • @ShadreckChimaimba-l9y
    @ShadreckChimaimba-l9y Месяц назад

    Osatopa big