VICE PRESIDENT MICHAEL USI AZIZIMUTSA OGWILA NTCHITO KU CHIPATALA.17 July 2024

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 28 авг 2024

Комментарии • 504

  • @EnossDzuwa
    @EnossDzuwa Месяц назад +44

    Zomwe wayamba kupanga Ussi ndi zofunikira kwambiri ndipo zithandiza anthu kumagwira ntchto zawo moopa lamulo kmaso kufika ku ntchto mu nthawi yake, Big up VP

  • @FrankKambwani
    @FrankKambwani Месяц назад +24

    Well deserve Usi, bola lisakhale sewero koma pakhale solution cfk ma doctors ndiye amatiwonjezadi

  • @noelmithi7848
    @noelmithi7848 Месяц назад +12

    That's the way to go , well done our VP Michael usi

  • @vitumbikochinguwo6227
    @vitumbikochinguwo6227 Месяц назад +3

    Kind of leadership we have been waiting God bless you

  • @LemarSmith123
    @LemarSmith123 Месяц назад +10

    Excellent ❤❤❤❤❤❤ imeneyi ndentchito imene ikufunika muno dziko la MALAWI

  • @JoyceNkhokwe
    @JoyceNkhokwe Месяц назад +3

    Keep it up bwana mudzayenderenso nthawi yogulitsa feteleza wamakoponi anthu amavutika amalipiritsidwa ndalama yapamwamba muzipangapanga l like it

  • @francislimbani-jd7ft
    @francislimbani-jd7ft Месяц назад +3

    The type of leadership I have always prayed for to my country. ❤

  • @stanleykumwembe4719
    @stanleykumwembe4719 Месяц назад +5

    Uyuyu aliza athu uyu😢, guy’s, Big up Dr Michael Usi, thawi ndi ndalama guys, maiko amzathuwa akutuyukuka njira zake ndi Izizi guys.

  • @marthachapepa2692
    @marthachapepa2692 Месяц назад +2

    If Malawian leaders of government departments will work like what Mr V P did, I hope there shall be no laziness and corrupt people in our country . I salute this team spirit.

    • @itubiz1501
      @itubiz1501 Месяц назад

      This guys knows what he is doing and others will not even like him cause of his good works, only God can protect and guide him...well done Mr Vp

  • @ngwilasephron7197
    @ngwilasephron7197 Месяц назад +1

    That'll help so much ,the same as John pombe Magufuli was doing in Tanzania, I really appreciate it

  • @user-px9gd6fc6w
    @user-px9gd6fc6w Месяц назад +2

    Wow that's a Great move bamboo asikono 🤔 our VP so much ❤️ you from Lusaka Zambia 🇿🇲 one of followers

  • @ShakilaChagwa
    @ShakilaChagwa Месяц назад

    Congratulations 🎉Mr VP, Good work

  • @umalimaganga
    @umalimaganga Месяц назад +3

    Koma kumeneko 😅😂😂 that's the spirit. Ineyo I work overseas we don't play jokes about time.

  • @user-jl9yk8jd6g
    @user-jl9yk8jd6g Месяц назад +2

    I can see other hospitals afraid that which one will be next!??🤣🤣🤣🤣🤣🤣 It's your hospital of course!!!🤣🤣🤣🤣🤣... Big up Mr VP

  • @EllenChabwera
    @EllenChabwera Месяц назад +3

    This is good Malawi akozeke izizi ndiye zofunika kwambiri thanks bwana VP matiganiziladi amalawi🎉

  • @LovenessLester
    @LovenessLester Месяц назад +2

    Keep it up mr VP, DR Manga more 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @clementgama-u5p
    @clementgama-u5p Месяц назад +4

    Well done Mr VP kwathu kwa gaga HC kuli Ambulance yopanda mafuta ofwala amagula okha mafuta ngati akufuna kugwiritsa ntchito ambulance

  • @AlliSaiti
    @AlliSaiti Месяц назад +5

    We need this kind of readership

  • @AffectionateGondola-cv7qj
    @AffectionateGondola-cv7qj Месяц назад +1

    I love that and I had no doubt with this guy keep up mr VIP

  • @ChristopherKanzere
    @ChristopherKanzere Месяц назад +2

    Go ahead Mr VP don't flashing
    Anthu akumudzi akadwala amavutika amafika ku chipatala muthawoyake koma MA doctor amabwela nthawi yomwe afuna

  • @JacobBanda-s1f
    @JacobBanda-s1f Месяц назад +1

    Bwana mwabwera,this is beautiful dziko lathu liziyenda bwino

  • @YahayaUndiya
    @YahayaUndiya Месяц назад +1

    This is so interesting Mr vp❤❤

  • @ApocheC.
    @ApocheC. Месяц назад +1

    Real definition of Manganya 🔥🔥🔥

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 Месяц назад +2

    Congratulations Mr VP, ukuku ndiye kutumikira ziko komwe mumafunika please continue

  • @WestonMsani
    @WestonMsani Месяц назад +1

    Keep it up Mr VP ,,,,,anthu akalowa muboma amatayilila kwambili thawi sasamala ntchito

  • @ChristyBauleni
    @ChristyBauleni Месяц назад +1

    If this coninues our country can be transformed
    Those Who will be caught not working must face the law

  • @OZIELBLESSINGS
    @OZIELBLESSINGS Месяц назад +2

    Sanje sumana, ganizo lopambana kwambili Mr vice president ❤❤❤❤

  • @user-hq2io8nk7s
    @user-hq2io8nk7s Месяц назад

    Thanks very much Mr VP, this is a good work you have started .Keep it up and it is my appeal to ask you travel hospitals because many deaths occur because of hospital staff wickedness. You have also plan to visit other government departments

  • @LoydKameza
    @LoydKameza Месяц назад +3

    Great work Mr VP ❤

  • @PiliraniDanielDaniel
    @PiliraniDanielDaniel Месяц назад

    Keep it up until my country Malawi is changed

  • @officemoyenda-rj2hz
    @officemoyenda-rj2hz Месяц назад +1

    The spirit of SKC

  • @grenanakhozwe3735
    @grenanakhozwe3735 Месяц назад

    Well done Mr Vice President ❤️❤️

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 Месяц назад +1

    Michael usi weldone apose kugwira ntchito a president, ali busy iwowo kuba ndalama, zikakhala cho ndizakuvotela ine

  • @humphreysidie4747
    @humphreysidie4747 Месяц назад +1

    He was supposed to fire the DHOvfrom the spot coz it can't b that the head of the entire hospital is not in the office at 8, we have so many educated ppl who can do that job so well.... Many ppl would have learnt from this

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v Месяц назад +1

    That's good work Mr vice president ma doctors ambiri amajaira kwambiri

  • @phillgwedera3755
    @phillgwedera3755 Месяц назад

    this is what we call the calling of a leadership. be blessed the VP

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850 Месяц назад

    Good start Mr. VP, keep it up for the betterment of Malawi, anthu m'bomamu akugona kwambiri.

  • @stuartswirase7en977
    @stuartswirase7en977 Месяц назад

    The small things matter, one step at a time it's possible to fix things big up our VP

  • @clementlukhele9551
    @clementlukhele9551 Месяц назад

    This is awesome Mr vp💪🏻💪🏻💪🏻❤❤

  • @HappyChipozi
    @HappyChipozi Месяц назад

    This is so good

  • @EliasDzoole-js8vx
    @EliasDzoole-js8vx Месяц назад

    I can see chilima in him well done bwana ussi

  • @RonaldKanyimbo
    @RonaldKanyimbo Месяц назад

    That's what's up a vp.....am loving this

  • @FynessChikadza-y8h
    @FynessChikadza-y8h Месяц назад

    This is good approach,big up Dr VP

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Месяц назад

    Bravo bravo good work Mr vice president we silute you for what you have done❤❤❤❤

  • @user-gs5mu2px7z
    @user-gs5mu2px7z Месяц назад

    Well done👏👏

  • @YamikaniLiyenda
    @YamikaniLiyenda Месяц назад

    I support this idea and this plp are so stupid

  • @IshueBaneti
    @IshueBaneti Месяц назад

    What I like most about this government is akuphunzisa mmalawi kuti osangwira ntchito asadye Malawian are lazy izizi bwana pitilizan do it whole heartedly for the people and not for votes plz sir

  • @user-kn9jz4qp9h
    @user-kn9jz4qp9h Месяц назад

    This is beautiful Bwana VP

  • @DaynaKalimanjira-kj2gw
    @DaynaKalimanjira-kj2gw Месяц назад

    Nice Mr usi

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 Месяц назад

    This is very good Mr. VP

  • @JamesChiphwanya-tb3tq
    @JamesChiphwanya-tb3tq Месяц назад

    For the first time VIP president to do this thanks so much.anthu ongwila ntchito zipatala za boma amaonjeza kwambili amangwila ntchito 2 ours

    • @NovassTambala
      @NovassTambala Месяц назад

      This is first time kumalawi Vic president kuyedela zipatala guys big up

  • @user-fs5gr8iv5s
    @user-fs5gr8iv5s Месяц назад

    Zikomo kwambiri Ambuye akutezeni anthu akuvutika bweraniso kuno ku ofesi ya DC kuno kukasungu DC CHIDAKWA

  • @FumbwaLyson-3710
    @FumbwaLyson-3710 Месяц назад

    Big up ndinzomwe tikufuna usii uyuu ndi katundu he come to deliver❤❤❤❤❤

  • @nowachiumia3716
    @nowachiumia3716 Месяц назад

    Good work Dr usi Kip it going forward

  • @DalisoulMwale-wu1bf
    @DalisoulMwale-wu1bf Месяц назад

    Big up Malawians

  • @MercyChimaliro-fi6mv
    @MercyChimaliro-fi6mv Месяц назад

    Keep it up our Vp.in so doing you will carry majolity

  • @EugeniaNgoyi
    @EugeniaNgoyi Месяц назад

    That's lovely Mr Vp

  • @pettersen2717
    @pettersen2717 Месяц назад

    That's what I expected of manganya... 🇿🇲🇿🇲🇿🇲

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Месяц назад +2

    So you have to go also to migration, ma passport sitikuwaona

  • @GloryShaba
    @GloryShaba Месяц назад

    This is the way to go❤❤❤

  • @isaacgmc
    @isaacgmc Месяц назад

    Zosezo mwayamba ausi mwachedwa mwayamba ndawi yosaenela . Komaso atu sangagwile chito opanda malipilo abwino

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z Месяц назад

    Respect Vp

  • @UlayaInan
    @UlayaInan Месяц назад

    Mwaiyamba bwino avice president ntchito

  • @peterbyson6269
    @peterbyson6269 Месяц назад

    This is the way we should lead❤

  • @liffawazili2840
    @liffawazili2840 Месяц назад

    It's necessary, people in government office to be working as if they are in private sector. When it's 7:00 it's exactly 7:00 coming late you have to write a report or else advise your immediate supervisor that your won't report in time.. Let's embrace it , Malawi can completely change. IN ADDITION, we should have the spirit of serving our people. Tisaiwale Tinkaisaka nthcito imeneyo, mulungu anatipatsa, tiyen nafeso titumikire whole heartedly. God bless Malawi

  • @jelsonmlowoka8611
    @jelsonmlowoka8611 Месяц назад

    Servant leadership proud of you Mr vice president

  • @user-iq5xk6ju7y
    @user-iq5xk6ju7y Месяц назад

    Excellent move Bwana VP ❤❤❤

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb Месяц назад

    Well done vp.kip it up

  • @MosesSolomoni
    @MosesSolomoni Месяц назад +1

    Ndye mpakana TV ayesa tikufelanji et?

  • @PetroKachingwe-jf7dh
    @PetroKachingwe-jf7dh Месяц назад

    That's good work VP Continue

  • @yahayaomar7077
    @yahayaomar7077 Месяц назад

    First time kuyamba kuona Vice president akupanga zimene Dr Michael usi apanga anthu ogwila ntchito m'boma amapanga ulesi kwambiri chifukwa choti palibe owayang'anila and they respect time thank you Mr Usi tikufuna atsogoleri ngati inuyo, vote for Michael Usi

  • @FarooqPias1625
    @FarooqPias1625 Месяц назад

    Even it looks like show off but I love it, i hope vp his doing this with good intention, not only to show off. we need our government with real solution.

  • @mkupabanda-nd2vb
    @mkupabanda-nd2vb Месяц назад +1

    zabwino kumayamika
    Great job bwana usi

  • @MachitidweYobu
    @MachitidweYobu Месяц назад

    Mostly all the government hospital they do not know time management they take this for granted lero aziona

  • @PraiseMitton
    @PraiseMitton Месяц назад

    Amalawi musapusisike ndizomwe akupanga a VP awawa ali kale mbali ya chakwera asakuphimbeni mmaso ndizabwino zonse zimene azipanga panopa Amalawi kupusa aaaaaa pilizi 😭😭

  • @officemoyenda-rj2hz
    @officemoyenda-rj2hz Месяц назад

    Thank you very much bwana Vice President

  • @mrsmkjb2411
    @mrsmkjb2411 Месяц назад

    Let’s hope this will continue and is just not a “starter show”!

  • @elizabethmapira2773
    @elizabethmapira2773 Месяц назад +1

    Ndipo muwauze a Vice president kuti chipatala Cha Chikwawa amalipilitsa anthu kuti anthandizidwe,MOTi anthu ena amabwerera asapatsidwa chinthandizo chifukwa chosowa ndalama yopereka Kwa manesi ndi madolotala

  • @giftmwale8475
    @giftmwale8475 Месяц назад

    Our able vp keep it up

  • @ChikondiLikapa
    @ChikondiLikapa Месяц назад

    ❤❤❤❤i love you mr vp tapitilizani izi musaleke ayi yendelani kuma office onse aboma 🎉🎉

    • @user-bi6pb5gc8t
      @user-bi6pb5gc8t Месяц назад

      Uyende mwambiri ngakhaleni mumakampani muone nyansi zimene zikuchitika ndimene anthu ogwila ntchito akuvutikila komanso utifufuzileko Kuti amene anakagula fetilaiza kubushala ndindani chidukwansotu mavuto enawa mukuwabwelesa ndiinu anthu amaudindo mukuba kwambiri misonkho yathu

  • @justinmadeya
    @justinmadeya Месяц назад

    Pitilizani ndithu a VP chifukwa athu amaluza miyoyo chifukwa cha kuchedwa kwa thandizo . Well done ❤

  • @Rometcma
    @Rometcma Месяц назад +1

    Anduna alikuti a azaumoyo amalawi umbuli unakula this is not his duty inu munaonapo vp from other countries kumapanga zimenezi 😂😂😂😂😂😂😂

    • @LukaThawe
      @LukaThawe Месяц назад

      Kodi iye wayenda Ngati nduna ya zaumoyo Kodi president sanayendepo kuchipatala mwaganiza bwanji man cadet

  • @AshimayeGama
    @AshimayeGama Месяц назад +1

    Zaziiiiii nanga makwhala alikuti mbiliyako

  • @user-rc3ze2oi7u
    @user-rc3ze2oi7u Месяц назад

    BWANA V.P MWAYAMBA BWINO KWAMBIRI ZIMENEZO NDIZIMENE TIMAFUNA KUWAPANGA ANTHU KUTI AZIGWIRA NTCHITO 🎉🎉🎉
    MUSALEKERE POMWEPO MUZIFUNSASO MAKHWALA ALIPO?

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 Месяц назад +2

    Ndie bola ukanapanga zimenezi ku immigration tu osati ku hospital tufuna ma passport

    • @ChikondiLikapa
      @ChikondiLikapa Месяц назад +1

      Man odwala akufa ndiye ayambe ku immigration inu ndiaja ongosusa aja eti

    • @mavmsusa1310
      @mavmsusa1310 Месяц назад

      Ku hospital nde kofunikilako. Bwana kkkk

    • @PriscahChikaonda
      @PriscahChikaonda Месяц назад

      Anthu Ena amangozindikira alankhula.

  • @emilymwale2596
    @emilymwale2596 Месяц назад

    Good development

  • @user-nz9ty3ih1v
    @user-nz9ty3ih1v Месяц назад

    akoma saname mavayisiwa ntchito anayidziwa uja wapita ujaso samafuna zachibwana uyuso sakufuna zachibwana akanati president so azigwira mene amagwirira ma vasiwa bwezi zikuyenda bho

  • @StevenMjMbama
    @StevenMjMbama Месяц назад

    Apitilize ndinthu Mr vp great job ndipo zizimutsani ma office aboma ambiri plz

  • @MfipaKapwera
    @MfipaKapwera Месяц назад

    Mwapanga bwino A v p mulayendeleso a NRB palibe chomene akupanga kumupoto kuno ambiri sanalembese.

  • @rabisonpias5131
    @rabisonpias5131 Месяц назад

    Bwana MANGA , Osawaiwalatu a Bro.. bwezi akumadzakulondolerani njiraa mumaona popondapo.

  • @frankfrankb8461
    @frankfrankb8461 Месяц назад

    Malawians you are easy to be deceived don't you know that this One is campaign for chakwera

  • @MichaelKachiboo
    @MichaelKachiboo Месяц назад

    Thats good koma mankhwala nzipatalamu ndie mulibe

  • @RaymondPhambala
    @RaymondPhambala Месяц назад

    People of Malawi, Kodi chifukwa chani sitichedwa kupusitsidwa...uyu wakhala minister Kwa dzaka 4, wapanga chani ku dziko lino ?
    Zonsezi ndi zabodza kufuna kupusitsani and izizi a MCP anadana ndi Chilima chifukwa ndiye amene amachita izi but behind the camera, so izi ndi set up, work up Malawi, you know the truth !!!!

  • @user-nn9ow8rn8w
    @user-nn9ow8rn8w Месяц назад +4

    Ku Malawi izizi zimaonjeza mupedza madokotala onse alipa Lunch...... Ma patient ma petient angokhala Komanso nthawi ya lunch yo imapitilira
    Bwanji osagawana ena atenge lunch 12- ena 1 o'clock
    Komanso pachipatala 1 hour is too much 30 minutes is enough.... South Africa that is the system ngakhale pa lunch anthu amathandizidwa and ndi 30 minutes lunch

  • @jonnahobammah6967
    @jonnahobammah6967 Месяц назад

    Well done Mr Vice president 💚💚💐💐

  • @GeorgeKambwiri-xr9ri
    @GeorgeKambwiri-xr9ri Месяц назад +1

    Zomwe tikufuna ife ngat amalawi ndizimenezi

  • @user-kr8th5oh7b
    @user-kr8th5oh7b Месяц назад

    Good start a VP , bingu mutharika ankapangaso choncho

  • @EmmanuelNkosi-ts8bn
    @EmmanuelNkosi-ts8bn Месяц назад

    This way to go Mr VP

  • @user-ww4ei5fb7d
    @user-ww4ei5fb7d Месяц назад

    Well done, civil servants need improvement

  • @AlbertEngelbercht
    @AlbertEngelbercht Месяц назад

    Wayamba bwino usi,onse asogoreli azitero bwezi Malawi alipatali,osangokhala Ku sanjika