Mr president anthu awuphawi palibwino ayimile u president waziko pasogolopa tizawona kusitha ulemu Mr president born kalindo chonena chimandisow mulungu azikudalisani thawi zose
Koma kodi kodi chakwera ndi munthu kapena chiwanda Malawians gather here to help me...akuoneka kut satana uja Mulungu anamusiya kut malawi...apa Mulungu watiyesa mayeso ....zoona maiko onsewa ,satana akagwere kwathu kuno..Allah transfer this devil please...throw it in a country which does not prays You...as for malawians..we pray
NDIPO sinaone duna za bomadi zikulipira misokho olo amalowetsa zithu ulele ndipo Mr DC mau Anu ndi moto km amalawi akupusa masiku ano bwanji apa boma likuonjezatu
Ngati kuli munthu upusa chisilu chindere chizereza ndimunthu amene akudya zaulele koma akuzuza amamene amamudyesa chaulerezo. Nyumba galimoto petrol magesi school fees ya ana zose zaulele koma anthu amene apakupasa zimenezo mdikuwatenga ngati zisilu atsogoleri atundu anji mra mukuputa chiteze dala chizakuyabwani ndi boma lanulo
Lá em Malawi tem muito mais Ladrão,burladores, governo de burladores, isso acontece aonde? you must do like Kenyan people,tamu thama ngiseni, Chakwera muku mu sekerera ,if I fiñish here My training and back there, some of bastard people gonna chora, stupid government, siku limodzi Chakwera and savage police he use will see amazing things any citizen must wake up
Kwacha yagwa kangati? Katundu tikugura pa rate yopoira ,win palibepo timapanga business kungoti nanga titani poti ntchito zikusowa.tiganizireni a business 😢chonde.
We love you Mr president you fight for us poor people
Bonnnnn Kalindooooo the DC chimwana cholimba mtimaaaaaa😅😅 love you more!
Kungotipela Born Kalindo achakwera sazagona ku state house 😮😮 ndipo malawi wina aliyeze sazagona izi nde mudziwe achakwera 😊😊😊
Kuyakhula chilúngamo Bon akuigwira ntchito more than zipani zotsusazi. Big up Bon, kaya anthu anve or asanve better wayakhula💪💪
Komatu the DC amalangiza Chilima Ali moyo kuti atuluke mu tonse then Chilima ananyalanyaza mapeto ake anaphedwa.
Mtsinje wa timkanena udathera mu siizi😢😢😢
Brave man we're very appreciated
🔥 kulavula moto big boss kalindo ❤fire 🔥
We absolutely appreciate the DC, THE DANGEROUS PERSON.
dziko la Malawi likukhala ngat nyanja yoti aliyese akhoza kusambiramo ndi kutuluka. anthu ali m'boma nsaname akusambira paliponse
Good news mr brother ♥️♥️♥️♥️ bon kalindo 💪💪💪💪💪💪💪✊✊✊✊✊✊✊
Mumatiyimirira akalindo God bless kalindo❤
Kkk achikulile olimba mtima
Wise man the DC❤
Kalindo his DC indeed akupanga masewera aboma
Ulemu wanu mr Dc timenyeleni nkhondo basi mwina ifeso tsiku lina tizakamba zokoma tikudya katatu patsiku
Maina wo muwawulure bas DC akamuna fire on duty keep it up
Mr president anthu awuphawi palibwino ayimile u president waziko pasogolopa tizawona kusitha ulemu Mr president born kalindo chonena chimandisow mulungu azikudalisani thawi zose
Boooooooon kalindooooooo the DC mumatiimilila mulungu azikutetezani
Zomadinda ma stikcer pa boder zija zathanso 😅 more fire boni kalindo
Keep it up MR BK DC were under you Mr
Namu Dc ❤❤❤❤ wi love to ❤ kuswa kuswa basi chakwera machende ake
Bwanawathu wathu the DC chimwana Chopanda matha❤❤❤❤❤❤
The DC ❤❤❤❤❤ Koma uyundye mamuna eeeeee
The last man standing 🔥🔥🔥
Booooooooooon kalindo 💪💪🔥🔥🔥🔥🔥
Mumakhwana munthu wamkulu🎉🎉🎉🎉
Bon kalidoo sakunama tilikoko,🔥🔥🔥
More 🔥 📛 🔥 fire
Kuno Kumalawi Tendendele tilibe dzimakhala zonvesa chison ponva kuti ndife anthu opemphera koma tili chabe
Tikumva kuwawa kwambiri a malawi
Ndizamanyid zimenezo iyya
U r indeed the pangolin.contunue fight for malawians,we are at your back
Zoonadiitu Mr bon kalindo bomaili ndi lamanyi lauchitsilu zikuchitikazi ndi za manyikobasi
We apriceate our president more fire.
😂😂😂😂the DC kusakaniza nkhanitu, mwana wooopsaa kwambiri osaopa
Ife wathu ndi born kalindo ✌️
Kikikikiki, chipangolini sopano. Auze amazolowela agalu amenewa.
More fire 🔥 big man
THE Dcc much respect to you
Za power Mr kalindo
Zimenezo ndipo bwana bon kalindo mukunena zoona
Kkkkk Koma kalindo, akuti akukondera
The legend one 💥💥 DC
Akunena zowona akalindo ziko silikuyenda abakili ana pangapo border free anali ndindalama anthu kuvaratso bwino anthu wose azimayi zikomo sport kalindo paster w
Dziko la Malawi lafika pothesa m, zelu ambuye bwelani
The DC mwana oooooopsa kwambiri ❤
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥
The first here❤❤❤❤
Koma kodi kodi chakwera ndi munthu kapena chiwanda
Malawians gather here to help me...akuoneka kut satana uja Mulungu anamusiya kut malawi...apa Mulungu watiyesa mayeso ....zoona maiko onsewa ,satana akagwere kwathu kuno..Allah transfer this devil please...throw it in a country which does not prays You...as for malawians..we pray
Kwatsala roadtraffic tsopano.Akupanga zopusa kwambiri
DC mwana wohipa apule zamagona tulo
Mulungu akudalitseni ABON anthu akufa ndi njala plz
Boma la Chakwera kwake ndi kuba kupha ndi kuononga
Kod Border free ija inali pa manifesto ilikuti ?
Malawi is about to rise.!🧑⚖️
Our big man
Pangolin
Kalindo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥💯
❤❤❤❤ Bonnnnnnn Kalindoooooo
Zikom kwambili bon kalindo komaso ndi zoona
Apapa zafikapa ikanangobwelapo ziwonesero ngati zaku Kenya zija
I love you mr DC
Zoona boma la cakwera ndi lokuba komanso loipitsitsa mbiri ya dziko lamalawi
More fire boss
More 🔥🔥🔥
mwana owopsa kwambiri dziko tiwotche bas kkk
😂😂😂😂😂 umakwana
The DC ❤❤❤❤
Mwana ooopya kwambiri the DC
NDIPO sinaone duna za bomadi zikulipira misokho olo amalowetsa zithu ulele ndipo Mr DC mau Anu ndi moto km amalawi akupusa masiku ano bwanji apa boma likuonjezatu
Machine kalindo
Ngati kuli munthu upusa chisilu chindere chizereza ndimunthu amene akudya zaulele koma akuzuza amamene amamudyesa chaulerezo. Nyumba galimoto petrol magesi school fees ya ana zose zaulele koma anthu amene apakupasa zimenezo mdikuwatenga ngati zisilu atsogoleri atundu anji mra mukuputa chiteze dala chizakuyabwani ndi boma lanulo
The D.Ciiiiiiiiiiiiii!! Ifetu tili kumbuyo kwako ndipo sitingakusiye wekhayi!! Apresident anthu achakweka pomwe zafikapa chonde mukanangosiya kupanga zomwe mukupangazo chifukwa mukukwezabe mkwiyo wa amalawi! Pamwamba pamkwiyo omwe ulipo kale! End chomwe mungaziwe palibe chanu ku 2025 ndipo mukanakhala ena mukanatula pansi udindowo before election!!
The DC. bon kalindo 💪💪💪💪💪💪💪💪💪♥️♥️♥️♥️♥️♥️♥️♥️💥💥💥💥💥💥💥💥🫂🫂🫂🫂🫂
Mumakwana aboni kalindo mupitilize zimenez amalawi tikuvutika😮
Truth
The D.C. ❤❤❤😂😂
The DC sakuyamkhulapo za manganya ku mcp why
Thanks boss mn
The diccc❤❤❤❤❤
Lá em Malawi tem muito mais Ladrão,burladores, governo de burladores, isso acontece aonde? you must do like Kenyan people,tamu thama ngiseni, Chakwera muku mu sekerera ,if I fiñish here My training and back there, some of bastard people gonna chora, stupid government, siku limodzi Chakwera and savage police he use will see amazing things any citizen must wake up
Koma chakwelaiwe pamako wamva
Kwacha yagwa kangati? Katundu tikugura pa rate yopoira ,win palibepo timapanga business kungoti nanga titani poti ntchito zikusowa.tiganizireni a business 😢chonde.
🔥🔥🔥🔥
Akuti agula mifuti 400 Monika chakwela ndiye akugawa mifuti 😂 yophela anthu oyankhula Za imfa yachilima.
😂😂😂😂😂 mpaka pepe kaley
Kalindo always amanena zoona zokha zokha. And ife anthu sitikusintha dziko lathu chifukwa choopa boma let's do more together
❤❤❤
Mumatiimilila BG 💪🏿💪🏿💪🏿
Apule mutu sikugwira nanga mpaka kuphwethula ndi okaoder akhululupirila bwanji kuti katunduyo ndiwabwinobwino
Tiyeni tisaope aboma coz aboma akuononga mopanda chisoni
Go konkoooooooooooooooo
Koma dziko ili 💔💔💔💔💔
The DC..... pangolin
The DC iyi nd nthaw yot ndod ituluke
Tellem
umatiyimilira
❤
The DC 😅😅
Mcp woye 😂😂😂😂😂
😂😂😂 Mr DC
Tingopanga zakukenya basi asatitopese anyaniwa