Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI”

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 9 июл 2024

Комментарии • 81

  • @user-ix2ux5ss1b
    @user-ix2ux5ss1b 21 день назад +5

    More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji 21 день назад +1

    Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏

  • @EversDman
    @EversDman 20 дней назад

    Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯

  • @LuyoloTlhapane
    @LuyoloTlhapane 14 дней назад

    A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila

  • @PeterKasiya
    @PeterKasiya 20 дней назад

    Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili

  • @MomeryPhiri
    @MomeryPhiri 20 дней назад

    ❤❤❤❤❤❤❤ love it

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k 21 день назад +1

    bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo

  • @user-xm5cq1fb8g
    @user-xm5cq1fb8g 20 дней назад

    Ulemu wanu big❤❤❤❤❤

  • @user-dj6rc3lc4t
    @user-dj6rc3lc4t 21 день назад

    Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana

  • @UthmanKapungu
    @UthmanKapungu 21 день назад

    Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife

  • @neemahkapatamoyo9563
    @neemahkapatamoyo9563 21 день назад

    Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @AffickChaona
    @AffickChaona 18 дней назад

    ❤❤❤❤❤

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp 20 дней назад

    😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi

  • @FarookRaphael
    @FarookRaphael 21 день назад

    More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 21 день назад

    Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂

  • @FlorryVugy
    @FlorryVugy 20 дней назад

    A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂

  • @user-wm4rs4kd7d
    @user-wm4rs4kd7d 21 день назад

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w 21 день назад +1

    Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira

  • @user-hq8fw5hz2l
    @user-hq8fw5hz2l 21 день назад

    Awa ndie mawu

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem 21 день назад

    Big up bro

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j 21 день назад

    Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima.
    Agalu a anthu ndithu

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 21 день назад

    😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 21 день назад

    Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @FwasanMwenefumbo-zq7sg
    @FwasanMwenefumbo-zq7sg 21 день назад

    The DC 🔥

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 21 день назад

    Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂

  • @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa
    @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa 21 день назад

    Ambuye akudalitsen

  • @PeterMaulana-qk5uq
    @PeterMaulana-qk5uq 21 день назад

    Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!

  • @NdawaPhillipfortunePhakatie
    @NdawaPhillipfortunePhakatie 20 дней назад

    Motor 💥 kalindoooo

  • @user-zt3gv7md6x
    @user-zt3gv7md6x 20 дней назад

    Zoona amwene

  • @FrankMilias-og3js
    @FrankMilias-og3js 21 день назад

    Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko

  • @BernadettaTengula
    @BernadettaTengula 20 дней назад

    Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂

  • @JoyceChitsulo-mw7wg
    @JoyceChitsulo-mw7wg 21 день назад +1

    Makosana apa nde mwapita

  • @ericlarks8165
    @ericlarks8165 21 день назад

    ,🔥🔥🔥🔥

  • @benjulius6070
    @benjulius6070 21 день назад +2

    😂😂😂😂😂😂

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 20 дней назад

    Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza

  • @user-kx4cj7iu9q
    @user-kx4cj7iu9q 21 день назад

    Dc

  • @D.RJALLI-qo6yd
    @D.RJALLI-qo6yd 21 день назад

    Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa

  • @VincentMalika-w7x
    @VincentMalika-w7x 21 день назад +1

    Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi 21 день назад

    Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi

  • @RamseyWasi
    @RamseyWasi 21 день назад

    Blasa,
    Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC)
    My opinion:
    Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.

  • @SmartMoles
    @SmartMoles 20 дней назад

    Zofunikila kulangura mwayangure kumene

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 20 дней назад

    Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha

  • @ChisomoamitoniSauzandeamiton
    @ChisomoamitoniSauzandeamiton 21 день назад

    bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu

  • @JuliusMunthali-z7j
    @JuliusMunthali-z7j 21 день назад

    Awuzeni

  • @directorkfuture118
    @directorkfuture118 21 день назад

    Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂

  • @gerrardgladstone2473
    @gerrardgladstone2473 21 день назад

    Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣

  • @user-dm6xq6cp1m
    @user-dm6xq6cp1m 21 день назад

    Ai zikomo 🥱

  • @HendersonDziwa
    @HendersonDziwa 21 день назад

    Dzelu zachepa kkkk

  • @maxwellcaptain3937
    @maxwellcaptain3937 21 день назад

    Kalindo samaopa😂😂

  • @TshepoModise-xs4qu
    @TshepoModise-xs4qu 21 день назад

    Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee

  • @user-tw5iw7gf2v
    @user-tw5iw7gf2v 21 день назад

    😂😂😂😂 mpaka muchenga license

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward 20 дней назад

    Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 21 день назад

    Ati kutitola kapena chani

  • @DaudiAbdullah-o5l
    @DaudiAbdullah-o5l 20 дней назад

    Mumatiyimilila

  • @nicholasmutano6017
    @nicholasmutano6017 21 день назад

    Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?

  • @user-yl3lg5fk8f
    @user-yl3lg5fk8f 21 день назад

    Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious

  • @PeterGrant-ih1sr
    @PeterGrant-ih1sr 21 день назад

    Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 21 день назад

    Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk

  • @ikmusic-s9f
    @ikmusic-s9f 21 день назад

    koma nde eeee mpaka licence mchenga

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 18 дней назад

    😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp

  • @user-ls5zj8qn6k
    @user-ls5zj8qn6k 21 день назад

    Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya8577 21 день назад

    Bigiliman naweni

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-2001 21 день назад

    Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo

  • @YonaMartin-kb3do
    @YonaMartin-kb3do 21 день назад

    😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe

  • @AaronLitete
    @AaronLitete 21 день назад

    Kkkkk boma lopusa

  • @user-ky8us1ff5b
    @user-ky8us1ff5b 21 день назад

    😅😅😅😅

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 20 дней назад

    😂😂😂😂😂 koma DC

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko4534 21 день назад

    😂😂 kung'alulatu

  • @user-vn1wq6wg6i
    @user-vn1wq6wg6i 21 день назад

    K.K😂

  • @YohaneMbewe-u4k
    @YohaneMbewe-u4k 21 день назад

    😂😂😂😂

  • @AnthoniohMazengera
    @AnthoniohMazengera 20 дней назад

    Hahahahahahahahahaha😂😂😂

  • @Aluwenkareem-ev3ro
    @Aluwenkareem-ev3ro 20 дней назад

    😂🤣😂🤣

  • @PhillipMtonga-g7o
    @PhillipMtonga-g7o 21 день назад

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance

  • @GiftKulture
    @GiftKulture 21 день назад

    🤣🤣🤣🤣 mipunga

  • @BenjaminKayembe-j7j
    @BenjaminKayembe-j7j 21 день назад +1

    km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km

  • @Kachelephiri
    @Kachelephiri 21 день назад

    Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam 21 день назад

      Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam 21 день назад

      Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe

  • @user-wz6jy3re8n
    @user-wz6jy3re8n 21 день назад +1

    😂😂😂😂😂😂

  • @myheartforkids2876
    @myheartforkids2876 21 день назад

    😂😂😂😂😂