KU CHIKANGAWA NDIYE KWACHEMA UKU / ZINTHU ZAKE ZOVUTA🙌🙌

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 5 июл 2024

Комментарии • 392

  • @RiannahKaliat
    @RiannahKaliat 10 дней назад +28

    Pempho langa ndilakut ngat chilima anaphedwa ndi anthu ndikut mzimu wake uwakathe ndipo asowe mtendere mpaka kare uwakathe

  • @RiannahKaliat
    @RiannahKaliat 10 дней назад +35

    Imfa ya chilima mpaka lero ikumandivetsa mutu 😢Rip legend

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r 11 дней назад +64

    The problem with Comrade Timothy Mtambo is that He's after Money so He has nothing to do with the development of this Country. He started as an Activist while His aim was to benefit something.

    • @sithandanechirwa6376
      @sithandanechirwa6376 11 дней назад +8

      I also don't trust Timothy but if I overthink about the dearth of SKC makes me think that maybe Timothy lost direction because of the ruling gvnt. His mouth was shut by other elites who takes Malawi to their own hands

    • @HamiltonwaNamuwah
      @HamiltonwaNamuwah 11 дней назад +5

      Ndi galu kwabasi ameneyi Timothy Mtambo

    • @MarthaJafali
      @MarthaJafali 11 дней назад +3

      Timothy mtambo is a betray cos he was betrayed the who malawians some years ago I really don't like this gu

    • @user-nw6ie3xx8b
      @user-nw6ie3xx8b 11 дней назад +2

      I love this brother but dyela

    • @user-zk7jw9up6m
      @user-zk7jw9up6m 11 дней назад

      Zikomo mtambo

  • @emmanuelmukondia3568
    @emmanuelmukondia3568 11 дней назад +16

    THE best way is you to prepare yourself with God. So that you are right with God.

    • @jamesgondwe6669
      @jamesgondwe6669 10 дней назад

      God, how many times have we consulted God? How come that God fearless countries are more progressive than Malawi? Do you think we really survive death to claim heaven?

  • @jogechawa6192
    @jogechawa6192 10 дней назад +6

    For the first time I agree with Mtambo .Sitimayenela kusangalala 6th July. Palibe chikukoma

  • @HarlodAndrewbanda-vf2rd
    @HarlodAndrewbanda-vf2rd 11 дней назад +10

    We're still crawling to get there!! Rest in peace Dr SKC, UTM is a movement

  • @mishecksipolo7153
    @mishecksipolo7153 11 дней назад +13

    That's too bad,and it's evident kuti chilima anachita kuphedwa,it just needs the youth to clean up this mess

    • @AbelSinoya
      @AbelSinoya 10 дней назад +1

      Khala chete God knows ungatenge tsoka😂😂

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 11 дней назад +12

    Mtambo thanks for the vital words.
    We now needs actions against these idiots in the government

    • @rexphiri6951
      @rexphiri6951 10 дней назад +1

      powerful words Mr Mtambo

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 10 дней назад

      Only stupid people with commend the selfish and greedy Timothy Mtambo

  • @EdoJohn46
    @EdoJohn46 11 дней назад +17

    Antambo 😂😂😂 ndikukutengeni ngati ndinu amene mudasongezera dzikuni dzamoto kuti tipse Malawi muno ndiwe galu kwabasi

    • @ThomasShuga
      @ThomasShuga 10 дней назад

      Very true 😢😢

    • @MatiasMbaula
      @MatiasMbaula 9 дней назад

      Very true

    • @MaggieCement
      @MaggieCement 8 дней назад

      Ndipo Inu alibe umuthu uyu za ziiii mesa iye emweyi ndiamene anapangitsa kuti tilowe mudima akuonapanowo galu zedi

    • @wakisamsukwa9918
      @wakisamsukwa9918 7 дней назад

      No matter how long you have gone the wrong road, turn back.
      Turning back isn't an offence

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 10 дней назад +10

    Amtambo...ngat mukufuna kut ife tikukhululukireni ...pitani ku mademo mutibwenzere dziko lathu...anthu akuopa mademo chifukwa alibe support...mabungwe onse chakwera adasiya abale ake mmaudindo

    • @LOKAMJ
      @LOKAMJ 10 дней назад

      Exactly

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 10 дней назад +1

      DPP could have finished us . He did the right thing to rescue some of us from DPP. It was oppressing us

    • @InnocentMmanga
      @InnocentMmanga 10 дней назад

      😂😂😂

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 10 дней назад +1

      @@ancientnkhata1137 oooooh ...May the curse of Almighty befall who is a lier...and make them the wood of hell fire

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 10 дней назад +5

    SKC forever in our hearts 💔🔥 powerful words Comrade Mtambo Osafooka kms Osaopa Dziko ndi lanthu ife kuno Ku Ntcheu tili mbali yanu...

  • @dhaoudhiabedinegomaseko2363
    @dhaoudhiabedinegomaseko2363 5 дней назад +1

    Mtambo mseu wa Rumphi Nyika Chitipa munawukana mesa munkaguba nkumaphwanya zinthu kuti musinthe utsogoleri

  • @user-ro1pl7rv7z
    @user-ro1pl7rv7z 3 дня назад +1

    Sometimes I wish Bakili Muluzi to come back again....
    Ligongo apano indu yayi itupile Draft kwabasi. 😅😅 Yangajenda Ata panondi

  • @user-zf9xs3zj9b
    @user-zf9xs3zj9b 10 дней назад +4

    Wakuba mtambo akutiona ngati amalawi ndife galu anthu mwa sandutsa ndale ndi maliro a Dr saulos chilima 😂😂😂

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 11 дней назад +9

    Ndikakumbukila ifa yaathu amenewa mtima umawawa

  • @user-te4ii6sz2v
    @user-te4ii6sz2v 10 дней назад +5

    We quote more political speeches than prayers. This was not a political rally

    • @JosephHill-fy1bb
      @JosephHill-fy1bb 10 дней назад

      Ntambo is not a pastor.... Just watch pastor's preaching time...

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 11 дней назад +5

    Mtanbo akuyakhula za ndale zikugwilizana bwanji ndi mwambowu

  • @user-ub1mw7ce5p
    @user-ub1mw7ce5p 10 дней назад +4

    Well spoken, comrade Mtambo.

    • @KondananiNjakwa
      @KondananiNjakwa 9 дней назад +1

      He has missed the trail. Uyu watha. Ndipo akamati ngati wina amawona ngati wayimisa agenda, atanthawuza kuti munthu wina anachita kuphedwa? Kulankhula kopanda nzeru

    • @KondananiNjakwa
      @KondananiNjakwa 9 дней назад

      Nanga munthu angati anyamata oganiza bwino akumanena wena Lwarwa aaaah guys Mtambo anaganiza bwanji?

  • @JohnSingano-f1p
    @JohnSingano-f1p 11 дней назад +2

    The voice of a lion always brings confusions

  • @YohanePatrick-lc2lq
    @YohanePatrick-lc2lq 11 дней назад +4

    Man ife amalawi tikufuna dpp enawa abodza ngati iweyo Timothy anakuchosa ku mcp chifukwa cha katangale

  • @SakanjiraRose
    @SakanjiraRose 10 дней назад +1

    I'm getting confused, he is the man who mobilized people to fight a government that was to me far much better than the this one he helped to form.

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 11 дней назад +8

    mtambo walankhula za mzeru kuposa namachende chakwera

  • @DannielOnions-fy3dc
    @DannielOnions-fy3dc 10 дней назад

    Thanks so much 🙏 keep it up please we need people like 👍 u

  • @user-bq5ev7de1l
    @user-bq5ev7de1l 11 дней назад +4

    Apm my vote ✊

  • @TnmMpamba
    @TnmMpamba 11 дней назад +1

    Watching live from Salima, Khombedza

  • @jonathanmalanda7742
    @jonathanmalanda7742 10 дней назад +1

    A Mtambo ikani za mapemphero kuti mzimu wa skc uuse mumtendere

  • @SteveKumwenda-t3d
    @SteveKumwenda-t3d 10 дней назад +2

    Chitsiru ichi, ndiponso uku sikumapemphero

  • @emmanuelmukondia3568
    @emmanuelmukondia3568 11 дней назад +11

    Idol worship

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 11 дней назад +9

    More fire mtambo chakwera machende ako😂

  • @LloydLuwis
    @LloydLuwis 11 дней назад +4

    Keep morefire mr tman

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 11 дней назад +3

    That's true they is nothing to celebrate 60 years, it's like we help chakwera, kumkuyu ndi zikhale ng'oma kudya mitsonkho yanthu. Ayi momwemo 😂

  • @ConfidenceBanda-g8k
    @ConfidenceBanda-g8k 11 дней назад +4

    Koma ndipo poletsa kupepherapo ndie nduchitsiludi,mobwereza amene amaletsa kupepherayo nchitsiru

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 10 дней назад

    Well spoken comrade mtambo criticism singalephere as Malawian we were born like that, keep it up comrade

  • @LunnahMtambo
    @LunnahMtambo 10 дней назад

    More fire bro ,love from ccter namtambo cp

  • @AndrewLanken-v3u
    @AndrewLanken-v3u 10 дней назад +1

    He has got nothing to give malawians never

  • @ChiletsoChembe
    @ChiletsoChembe 8 дней назад +1

    Amalawi please! Let's pray to God forgive us and punish those who mudder saulos chilima

  • @JosephJosab
    @JosephJosab 10 дней назад +4

    Mtambo ndi kape

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 10 дней назад +2

    A ndale ndabodza kumene. Ndi chifukwa chake olo akuba ndalama zambiri-mbiri akavala amangokhala ngati avala chithumba chaku chigayo

  • @arthurmanyozo1289
    @arthurmanyozo1289 11 дней назад +2

    Give your life to Jesus.The owner of your soul is Jesus

  • @WisdomMaseko-fi5sv
    @WisdomMaseko-fi5sv 11 дней назад +9

    Koma tizikukhulupirirani ndithu a Timothy???

    • @DeliaKaduya
      @DeliaKaduya 10 дней назад

      My question too 😢😢

  • @RitaKainga
    @RitaKainga 10 дней назад

    Zikomo Inu nonse amene mwalimbabe mtima kupanga mwambo uwu though asatana akutchinga,Mulungu wathu ndwabwino,sanalepherepo,imfa iyi ndyovuta kuiiwala

  • @LulezLele
    @LulezLele 10 дней назад +2

    Kapolo uyu guyz akulubwa chani, mesa udapanganso ufitiwo at dat time kape

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 10 дней назад +1

    Osaoopa ai......ku Malawi kulibe president

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 10 дней назад

    Good Messnge Mr Mutambo

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso 8 дней назад +1

    Ndipo ngati chilima anachita kuphedwa ndi anthu adzakhala osowa ntendere mpaka Ndipo ngati mizimu imakantha yakanthe anthu amenewa

  • @AndersonChiponola
    @AndersonChiponola 6 дней назад

    Mtambo ndamene anapangitsa zonse izi palibe chomwe angayankhule Mutu wake sumayenda bwino ameneyo chifukwa anamuchotsa unduna wagwa nayo Mbuzi iyi

  • @user-ie5pc4ox8i
    @user-ie5pc4ox8i 6 дней назад

    Ada awawa bwenz Ali MUNTHU wapamwamba kwambir kma Anapanga zausiru ngat akufuna timukhulukire ayambise mademo

  • @WiscotDzombe
    @WiscotDzombe 5 дней назад

    Uku ngat kunari kumapemphelo ngat uyu anari compain amtambowatu safuna Bata Malawi koma kusokoneza

  • @EdwinMakwangwala
    @EdwinMakwangwala 9 дней назад +1

    Only God is our rest not this politicians. God help Malawi

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 10 дней назад +2

    LUWALA ANGASINTHE CHANI MBAVA YA MNTHU

  • @AbdulKhan-j2h
    @AbdulKhan-j2h 10 дней назад +1

    Mpava iyi atidye bawo bwanji Sumatuluka uli nduna pano abakuchosa ukufuna kodwela amalawi timaiwala

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 11 дней назад +1

    Antambo vuto chinthu chimozi mumafuna ndalama Chonde muzikhala ngati Born Kalindo chifukwa amati pavute pasavute asayimira amalawi ndipo akuti imila amangidwa amangidwanso pomwe enanu mumatifuna pomwe zakuvutani tikukukuwerenganitu INEYO NDIKUCHALENJA zoti wina aliyese aime payekha kuyambira Apita. Tupele. Raz. Nankhumwa. Shahana. Osati Chakwera Amayi Joyce banda ndi phulezdent Kalindo. Ndiye tikavote masankho mawa mwachilungamo mopanda kubela angawine ndi Kalindo chifukwa ndi amene akuoneka kuti angatithandize osati Ena inu 😁😁😁😁😁😁😁😁😁

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 11 дней назад

      Inuyo

    • @user-ww4ei5fb7d
      @user-ww4ei5fb7d 10 дней назад

      Kalindo ndiolimba mtima, ofunika kumuvotera. 😂

    • @JohnAsendi
      @JohnAsendi 10 дней назад

      @@user-ww4ei5fb7d zoonadi sister osati enawa akuoneka ngati akuti konda koma mmitima mulibe chikondi

  • @AustinBornface
    @AustinBornface 10 дней назад +1

    Malawi timakhala ngati tili pa stage tupanga drama kma ayi ndithu ndi action

  • @vinceynyone6693
    @vinceynyone6693 10 дней назад

    Viva mtambo Viva🔥👏👏

  • @VincentAndrew-jz2gf
    @VincentAndrew-jz2gf 9 дней назад +1

    Atambo ,Ulibe Zelu unaphetsa Athu Ambili

  • @taombeedward5026
    @taombeedward5026 8 дней назад +1

    The biggest problem mtamboyu

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws 11 дней назад +2

    Vote yanga yikupita kwa afford

  • @markjames-v1f
    @markjames-v1f 5 дней назад

    Chomwe mkukanikila kutiyimilira ndichan boss wanga

  • @user-wz1or9ud9i
    @user-wz1or9ud9i 10 дней назад

    Mzimu wa chilima awasowetse mtendere anthuwa mpaka anfe amene anapha chilima.

  • @GibsonBakha
    @GibsonBakha 10 дней назад

    Andale inu musamatiwawitsemutu muma gofuna ndalama agalu inu

  • @ChilangoNdalama
    @ChilangoNdalama 10 дней назад +2

    Big mtambo timakunyadiran

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 10 дней назад

    Exactly Andale akale achoke boma achinyamata alamulire dziko nkhalamba ndi mfiti komaso ndiankhaza

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 11 дней назад +1

    Akulesa bwanji ma pephelo akuopa chani tiyeni nazo pephelo ndi chida

  • @surgeon1621
    @surgeon1621 7 дней назад

    Malawi has become a very sad country. Everyone is just fighting for their own stomach. A person like Mtambo shouldnt be applauded like that as if he wasnt a minister in this government. What achievement can he show malawians to prove he is a better man for malawians. A lot of people want to use Chilimas death to gain points for themselves and yet they have no substance themselves. Too much sentimentalism without constructive knowledge

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso 8 дней назад

    Imfa yachilima ine sinfidzaiwala mpaka pano ndikulirabe ngati kuti anali bambo wanga amene anabereka ine koma sichoncho Ndipo mzimu wachilima ukuyendayendabe pakati pathu mzimu wachilima ambuye muulandire kumpando wanu wakumparadise

  • @YahayaUndiya
    @YahayaUndiya 10 дней назад +1

    Mpira amauona ndi akunja big bolani osaiwala zimene mukuyankhulazi antambo

  • @MagretIdimu-u7w
    @MagretIdimu-u7w 6 дней назад

    We're heart broken 💔 SKC still remains in our hearts 😢😢😢

  • @WilliamChopika
    @WilliamChopika 6 дней назад

    God is our side nthawi zonse

  • @CharityKangulero
    @CharityKangulero 11 дней назад

    ❤❤❤ Exactly

  • @LimbikaniMakwandu
    @LimbikaniMakwandu 10 дней назад

    Only chilima not you mtambo RIP CHILIMA

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso 8 дней назад

    Munayambira kukonaza dziko mudzamaliza liti komanso palibe chimasintha mumaona ngati umphawi wamalawi ndiye podyera panu komanso polemerera panu palibe chanzeru chkmwe wayankhula mtambo apa

  • @SaeedHurzrut
    @SaeedHurzrut 10 дней назад

    chilima wakuba ngati amwalira sangakhale wabwino Ife tonse tikuziwa zimenezo aphana pa gwilozano wawo

  • @user-qs2tx7wt6g
    @user-qs2tx7wt6g 10 дней назад

    Achinyamata ake ati angavele iweyo pathako Pako iweyo unakakhala wa mzelu unakakana undunaaa

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 10 дней назад +1

    Dziko la Malawi likuyenda cham'mbuyo

  • @HenriqKwilasi2022
    @HenriqKwilasi2022 10 дней назад

    Iwenso ndi mfiti chifukwa ukupanga za ndale mtambo

  • @AngellachifundoMwale
    @AngellachifundoMwale 9 дней назад

    Mumatipangisa ndinu omwe muli ndikuthekela kolamula dzikoli koma chonsecho simutithandiza and iwee ntambo uli nkuyankhula koma osakwanilisa mxiii unduna uja unali pheeeee ife tikuvutika pano fukwa cha nzerru zomwe unatilimbikisa ife kuti tikavotere mcp yet lero ukuti usintha ziko mub 2025 yet wakanika zaziii

  • @Josehimba
    @Josehimba 8 дней назад

    More fire comrade

  • @alexbanda9052
    @alexbanda9052 8 дней назад

    Awawa ndiovesa chisoni, akungosaka ndalama basi.

  • @PeterThomas-lw3io
    @PeterThomas-lw3io 10 дней назад

    Rest in peace 🕊️ chilima anagwira chito yaikulu DPP mu
    2014 ikanafela giya komano chilima anapanga zotheka kuti Peter akhale tsogoleri muchomwechotso mu 2020 wayigwira ntchito yathangata kumuyika Crazy Chakwera akulamulila koma njilu ndikupanga mission plane yakumupha yooohhh Chakwera ngoyipa

  • @MACKDADFFDANIEL
    @MACKDADFFDANIEL 7 дней назад

    Vuto athu kumalawi safuna kumenyela athu ovutika kom mimba zawo zomwe akuyakhula uyu ntambo ngati Ali ndi nzeru chonsecho momwe anali nduna samayakhula PAno anamuchotsa wayamba kuwalalatila athu omwe anawasiya a kugwila ntchito mbuzi ya muthu uyu ndipo ndipo ndiyemwe anapangitsa kut athu azivutika mpaka lelo

  • @MarriamBakalie
    @MarriamBakalie 9 дней назад

    Mtambo ndiwe galu kwabasi usamawapusise a 🇲🇼 anthu anakuona kale galu iwe zako zinada kale machende ako osavinidwa mbudzi

  • @kamangamathias2001
    @kamangamathias2001 11 дней назад +2

    What's the reason of kuwaletsa anthu ku phiri. Kiphiri kuli chani?

  • @VincentAndrew-jz2gf
    @VincentAndrew-jz2gf 9 дней назад

    Timothy panyopako ,Unapitsa Athu ambili

  • @Patricenkhoma09Tricia
    @Patricenkhoma09Tricia 9 дней назад

    Imfa yachilima imandidwalisa Bp daily😢

  • @OFG-th3st
    @OFG-th3st 10 дней назад

    Ngati bodza😢za Chilima

  • @user-ok7bq9es3y
    @user-ok7bq9es3y 9 дней назад

    Timothy unali ndi molaro kale iwe because of Msundwe barracks, size yako ndi Chimwendo. Ulibe faz iwe

  • @anoldkapolo4493
    @anoldkapolo4493 6 дней назад

    Kkkkkkkk aMtambo mabodza ndipo zikatere timati zawo zinaona kungolo, bwanji Mtambo osango gawa chakudya kwa anthuwo kapena muwamangira nyumbazo. . Kufuna ndalama kumeneko , osangopita kukapanga dimba . Chakwera akumenyera nkhondo ife alimi ndipo 2025 ndiboma choncho A Mtambo akunama

  • @SylvesterHarry-n7c
    @SylvesterHarry-n7c 10 дней назад

    Timothy mtambo adali momwemo adagwiramo ntchito palibe chimene adapanga nduwadyera uyu

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 10 дней назад

    no no anthu mzimvetsa zinthu u know very well kuti 6 july ndisiku la padara kumalawi ufulu omwe mkulankhupa lero nkhani yake ndi 6july nde mmafuna asiye za 6july apange za ma candle aa imfa si ya chilima yekha ati anthu akufa dairy .

  • @user-zf9xs3zj9b
    @user-zf9xs3zj9b 10 дней назад

    Pali chani chomwe mtambo anakupangila lweyo

  • @user-lz4kc5ob1t
    @user-lz4kc5ob1t 10 дней назад

    inetu ndimangokuveran anyamata a mcp ndimaziwa kt simunakumane nazo uyo mtambo ngat ndinu madolo kkkkk

  • @MorrisMapiri-d6z
    @MorrisMapiri-d6z 8 дней назад

    It's not over until it's over. We shall shut up when we will be satisfied.

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI 9 дней назад

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 10 дней назад +1

    Mtambo 💥💥💥💥

  • @GoodluckMwenifumbo-dk8jk
    @GoodluckMwenifumbo-dk8jk 10 дней назад

    Anthu ambiri osutsa pano ndi a MCP
    Zoona mpaka kuwaopseza amipingo,a MCP mwafikapotu

  • @YasinAmidu-b7b
    @YasinAmidu-b7b 10 дней назад

    The problem with us is that we are the ones that took evil to lead us

  • @KulinjiGoodsonnkhoma
    @KulinjiGoodsonnkhoma 8 дней назад

    Iwe ntambo khala pansi palibe angakumvele

  • @omarajibu860
    @omarajibu860 11 дней назад

    Ndipo takonzeka kuchotsa masewerawa

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 10 дней назад

    Amtambo naye ine ndinakhumudwa naye ndipo ndinataya chikhulupiriro mwaino mwatulukirano nthawi yonseyi munali momwemotu mu Timbaland wakudayo ndiye pano mukutinamizaso chani apaa iyaaa😊

  • @stevenchirwa5028
    @stevenchirwa5028 10 дней назад

    Unatinamiza ndiwe tuu kut MCP 2019