MTAMBO WAYAMBA KUNG'ALURA ZA INFA YA ACHILIMA KU MSONKHANO KU MZUZU |

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 27 авг 2024

Комментарии • 68

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 Месяц назад +3

    Ntambo thanks my Brother for your bravest speech.

  • @JacksonKanjanga
    @JacksonKanjanga Месяц назад

    Thanks for powerful speach

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu
    @TiyanjaneMkwate-we8gu Месяц назад +3

    Opusa uyu, mavuto tikuwaonawa anatipalia ndi iyeyo. May GOD punish him.

  • @JamesChiphwanya-tb3tq
    @JamesChiphwanya-tb3tq Месяц назад +2

    I wish to see change for Malawian with alliance for democracy god bless you

  • @Nganya96
    @Nganya96 Месяц назад +1

    Talk is free, mvura ikagwa kumachuluka zolilalira😂😂😂😂😂😊

  • @user-ve4zn2ne1k
    @user-ve4zn2ne1k Месяц назад

    Big up bro mumakwana ndinu big wa ma biggy ife tilindi inu even wina afune asafune munthu wakulu kwambiri mutambo❤❤❤❤

  • @Marymahendra
    @Marymahendra Месяц назад +2

    I want to see Malawi and change the present state like Chikwara is not doing well enough in four years time he killed 18people so please don’t be chose him may god bless Malawi xx

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Месяц назад

    Chomwe chinapha chilima ndi opposition yonse because ndi amene akudziwa zonse kuposa boma ndiye akudziwapo kanthu amenewa kuphatikizapo mtambo

  • @jestinanamkonda1495
    @jestinanamkonda1495 Месяц назад

    Afford = Chakufwas son
    UDF = Muluzis son
    DPP = Bingus Brother
    PP = JB
    MCP = LMC
    Where is Makawi heading? Dyela too much

  • @DevisonHala
    @DevisonHala Месяц назад +2

    Adapha chilima nayeso aphedwe osamunyengelera ameneyo ndale zophana zinatha

  • @user-un8yq1gg2i
    @user-un8yq1gg2i Месяц назад +1

    Fetilizer yo ayi, tikufuna biochar ife zinthu zotchipa zosavuta kupeza komanso zogwira ntchito nthawi yayitari, komanso biogas, gas wachilengedwe ndicholinga chofuna kuteteza mitengo yathu,

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon Месяц назад

    IMPHAWI ONSEU , MAVUTO ONSEWA , KUZUNZIKA KONSEKU AMALAWI AKUVUTIKA NDI WEYO GALU MTAMBO USAPUSITSE ANTHU NDIWE UNAPANGITSA ZONSEZI STUPIT NDIWE GALU KWABASI

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Месяц назад +1

    Good Messnge ❤

  • @FrankMkandawire-tl8gf
    @FrankMkandawire-tl8gf Месяц назад

    Only Jesus is honest

  • @ChifundoChiwanda-ru3pg
    @ChifundoChiwanda-ru3pg Месяц назад +2

    Osaopa! Mtambo kuti moto buuuuuu

  • @ellennchambalinja484
    @ellennchambalinja484 Месяц назад

    Aaaa uyu nde pomukhulupililq panadutsa 2019 tinkaipatsa moto

  • @CharityGondwe-bw9gs
    @CharityGondwe-bw9gs Месяц назад +1

    Unapanga khaza adadi iwe oipa iwe tambo😢

    • @FrancisNyayi
      @FrancisNyayi Месяц назад

      Ndipo live ine nnakaponya pompa ine coz of izi adadie abale

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x Месяц назад

    Katundu 🔥🔥
    Confidence 🎯

  • @Faithnsini
    @Faithnsini Месяц назад +1

    Bilimangwe pa malo oyela amakhala oyela 😂

    • @joebrown1158
      @joebrown1158 Месяц назад

      Kodi iweyo wutawona mzako amene wukuyenda naye akupanga zoipa kodi wungapitilizebe kumayenda naye?bilimamkhwe ndi iwe.

  • @JohnJohn-og8rt
    @JohnJohn-og8rt Месяц назад +1

    Nkondo ilipo apa ukuvunika dpp kapena UDF afodi tikwavuna koma apapa ayi sangate

    • @masalinodovu1705
      @masalinodovu1705 Месяц назад

      😂😂😂😂😂😂 koma yaaaa anthu mumath

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 Месяц назад

      Silipo sindu sambiri somwe mwanena. Soninso inkuwechetayo isyesyene.

  • @McphersonMsulira-zx2lj
    @McphersonMsulira-zx2lj Месяц назад

    Chipani chimombole malawi

  • @FaraiMatandika
    @FaraiMatandika Месяц назад +1

    Mtambo ndikamamuona mtima umandisiya siya munthu oipa uyu

    • @joebrown1158
      @joebrown1158 Месяц назад

      Kodi iweyo wutawona mzako amene wukuyenda naye akupanga zoipa kodi wungapitilizebe kumayenda naye? Woyipa mtima ndiwe osati mtambo

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Месяц назад +2

    Tiyen nazo mtambo osaopa

  • @MilwardMalunga
    @MilwardMalunga 6 дней назад

    Unduna wa ku MCP uja bwanji simunaukane??

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw Месяц назад

    Mawu anu bwana chakwera achoke

  • @kensonmbewe6692
    @kensonmbewe6692 Месяц назад

    We Malawians are tired of you people, mukametana kuseriko mumabwera poyera kudzapangana black mail, timakidziwani ma politicians a Ku Malawi. Now we need a new blood, a new gene, we want someone selfless and bold to help Malawians not you people

  • @SaulosKacheche
    @SaulosKacheche Месяц назад

    Mtambo ndiwe galu kwabasi, chibilimangwe

  • @VacksonPhiri
    @VacksonPhiri Месяц назад

    Musapuse naye Mtambo ndi nazikambe kapena kuti bilimankhwe

  • @MosesMsiska-x2n
    @MosesMsiska-x2n Месяц назад

    Chihana and his fellow are the one Who made all these messes we are in deed

  • @JohnFrank-cg1yh
    @JohnFrank-cg1yh Месяц назад

    Izi ndi zoona anthu akale andale must go chifukwa ambiliwa ali ndi magazi m'mazi ndie zazitukuko sizingatheke, koma azingoganiza zothana ndi ana asogoleri am'mawa

  • @AshimayeGama
    @AshimayeGama Месяц назад

    Ife sitidza khululupilaso andale ayi Bola dpp sina gwetsepo ndalama ayi

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem Месяц назад

    Bilimangwe Ali pa mpando wa blue tsopano

  • @EdwardKachinjika-c8q
    @EdwardKachinjika-c8q Месяц назад

    Mose wake uti naweso usanamize wanthu iweyo

  • @temwarachaelkhonje3733
    @temwarachaelkhonje3733 Месяц назад

    Bravoooooo

  • @VacksonPhiri
    @VacksonPhiri Месяц назад

    Ndi ndege

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Месяц назад

    Unalipilidwa kale mtambo wadyera

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Месяц назад

    Aford 💙💙💙

  • @MayorKachali
    @MayorKachali Месяц назад

    Mwasowa
    Cholakhula
    Fundo
    Zatha
    Mukangoyamba
    Kumpha
    Mbewa
    Komaso
    Satanic
    Yakoyo
    Ife
    Ayi

  • @user-jw2vy8sr7i
    @user-jw2vy8sr7i Месяц назад

    Kugwa Kwa ndege jekete,lamba,sapato ,kolona mpaka miyendo mmapaxi kuthyoka,ma phone kupangika wipe 😂? Aaaaaa guys ambuye akukamtheni

  • @OliviaFour-rk9ir
    @OliviaFour-rk9ir Месяц назад

    Unatipussa iwe MTAMBO chikkhulupililo paiwe tinataya

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Месяц назад

    Maloto achumba antambo kkkkkkdpp woyeeeeee

  • @GLABELMW
    @GLABELMW Месяц назад

    Ndizoonadi kafukufuka achitikedi tive zoona zake

  • @GraciousFrank
    @GraciousFrank Месяц назад

    Nde kuli gulu la anthu ngati ine a duuuuuu nobody knows which side we are vote ndi mu ntima

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Месяц назад

    Mtambo mbuzi

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba Месяц назад

    😂 koma awa unduna mmesa anaulawa madyela bas 😂😂😂

  • @CharlotteMushimiyimana-g6b
    @CharlotteMushimiyimana-g6b Месяц назад

    Zona

  • @SusanaMakanga
    @SusanaMakanga Месяц назад

    Zazii bilimankhwe weniweni iwee

  • @tuzijachaba-zl6pm
    @tuzijachaba-zl6pm Месяц назад

    Tikawina akale wonse azatuluke ziko litha kukhala bwino

  • @MsaMtonga-wo1nb
    @MsaMtonga-wo1nb Месяц назад

    Very stupid info iyeyu analiko komwe ngoziyo ikachitikira matako ake

  • @GeraldGunde
    @GeraldGunde Месяц назад

    Aaaaaaa! Zabwino sayitanira

  • @zolozaifilipe5940
    @zolozaifilipe5940 Месяц назад

    Wamasukat ntambo

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj Месяц назад

    Kodi Chilima ndi chida choyakhulira zandale kodi abale

    • @johnbullyohanittokasikizim7127
      @johnbullyohanittokasikizim7127 Месяц назад

      Kodi munamupha ndinu?

    • @joebrown1158
      @joebrown1158 Месяц назад

      Iwe mwana wanjoka

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 Месяц назад

      Simwamupha dala cholinga tikhale mchonena

    • @joebrown1158
      @joebrown1158 Месяц назад

      @@inessmsiyambiri8517 you need someone to interpret for you people will not gonna stop to speak about chilima until the truth must prevail ngati wuli mvali yomweyo ya kupha nawo ndiwe watsoka

  • @FridayKasto
    @FridayKasto Месяц назад

    U was bigy at first
    But now mmm little trust 😢

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw Месяц назад

    Mawu anu bwana chakwera achoke