ZOMWE AYANKHULA PA MASO PA A PRESIDENT PA MWAMBO WA ZAKA 60 INDEPENDENT 🙌🙌

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 27 авг 2024

Комментарии • 145

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Месяц назад +23

    Amen munthu wa Mulungu achakwera ndi nduna zanu a chimwemdo kunkuyu zikhale ng'omayo mukaka zisakhale ndwiii ziziva mawu a Mulungu ndizimene zikupangisa Malawi kukhala wawumphawi ndalama akuziononga basi.

    • @EmmanuelNauli
      @EmmanuelNauli Месяц назад

      😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😮😅😊

  • @quoniemagalasi9123
    @quoniemagalasi9123 Месяц назад +9

    This man is one of men sent by God to deliver ❤

  • @user-nt5cx3qj4m
    @user-nt5cx3qj4m Месяц назад +5

    Powerful words. We don't need to curse our nation due to painful situations. God will heal our nation

  • @EmilyKamzoole
    @EmilyKamzoole Месяц назад +2

    Amen, very powerful message. God bless you, God bless Malawi.

  • @LeyahPhiri-sd9xj
    @LeyahPhiri-sd9xj Месяц назад +3

    Munthu wamulungu wayankhula, wakumva amve zomwe Mulungu akuyankhula. ❤❤❤

  • @user-kw8tx1wm2i
    @user-kw8tx1wm2i Месяц назад

    Amen Abusa, Yehova ndithandizeni kuti ndizipanga zomwe chi Khristu chimanena, Amen.

  • @CharlesPhiri-ds1rk
    @CharlesPhiri-ds1rk Месяц назад +4

    Munthu wankulu....powerful massage Glory to Jesus🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @HildaKumwenda-ho8vz
    @HildaKumwenda-ho8vz Месяц назад +3

    Powerful message God bless you pastor ❤

  • @user-ey5wx1eu5y
    @user-ey5wx1eu5y Месяц назад +5

    ABUSA alalikira osati zomwe ayankhula ndipo ndi phunziro kwa tonse osati a President okha
    Tiyeni tisiye zonse mmanja mwa Mulungu popeza Iyeyo adziwa zonse bwino koposa mmene tidziwira❤❤❤

    • @user-kt5bq2wg6v
      @user-kt5bq2wg6v Месяц назад +1

      Mwayamba bwino zedi mbale. Anthu tonse tikanamaganiza choncho tikabakhala nidziko lantendere

    • @chimwemwendalama6260
      @chimwemwendalama6260 Месяц назад

      Yes, inenso ndimmene ndavela ulalikiwu ukupita kwa aliyese ndipo ukumpuzitsa kuti tizikhala okhulupilila koma ma comment ndikuwaona ine apa eeee pakuti kumalawi kuno mmodzi atagoyamba ndi negative comment aliyense alemba zomwezo

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Месяц назад +2

    Strong massage this is a lesson to the politicians who pushed a Malaysian people who's dying with hunger poverty

  • @tomasvinkhumbu7487
    @tomasvinkhumbu7487 Месяц назад

    Greatest message pastor God bless you

  • @odalachimphepo5257
    @odalachimphepo5257 Месяц назад +2

    For the first time seeing a preacher without recognizing POLITICIANS 😂😂

  • @nathannbanda3345
    @nathannbanda3345 Месяц назад

    This eas beautiful and powerful sermon, great 👍💯

  • @wonganilungu6352
    @wonganilungu6352 Месяц назад +5

    Abale ndi alongo timaseva zithu zopanda pake mmafoni athu. Zichotsenimo zoipazo komatu sevani uthengawu waphamvu muziwubwereza×10 kuposa zinazo. Tidzapeza mpumulo woyankhidwa kwa Yehova tonsefe tikawutsatira ndi kuwupempherera uthengawu patokha patokha

  • @VungaQueen
    @VungaQueen Месяц назад +3

    Mawu uphudzitsa ndipo achilimbikitso tingavutike motani titsataye chinkhulupiro yehovah ndiye zotse zanthu👏👏👏👏

    • @user-kt5bq2wg6v
      @user-kt5bq2wg6v Месяц назад

      Zoona m bale mulungu ndiye yanko tisanyozane pamene takumana nimavuto

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h Месяц назад +6

    Chakwela yekha ndamene akutikhomelela Malawi siziko losauka chakwela must go

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms Месяц назад

    Indeed powerful preaching God bless you

  • @WILFREDBANDA-o3r
    @WILFREDBANDA-o3r Месяц назад +1

    Powerful message ❤God bless Malawi

  • @HildaKamfose
    @HildaKamfose Месяц назад +1

    Powerful massage amen

  • @florence500
    @florence500 Месяц назад

    My favorite scripture... book of Job

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r Месяц назад +5

    Amene akukondwera ndi utsogoleri wa Mr Chikangawa ndiye kuti Mutu wake suyenda bwino

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад +4

    Koma azanga mbusa uyu mulungu amupatse moyo wautali

  • @serakillo8668
    @serakillo8668 Месяц назад

    Ayi zkm man of god thank for good msg ❤❤❤

  • @SalatielMathews
    @SalatielMathews Месяц назад +2

    Rev Yasinami Gamma,Mwatiphuzitsa Ambuye akudalitseni kwambiri,

  • @Albertngwira-vy3th
    @Albertngwira-vy3th Месяц назад

    Amen i love this man of God 🇿🇲🇿🇲

  • @BerthaManyika
    @BerthaManyika Месяц назад

    Powerful man of God, uthenga wamveka

  • @NellieMbisa
    @NellieMbisa Месяц назад

    Great message Pastor.......God bless you

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d Месяц назад +1

    Kuyakhula mopanda matha respect abusa a Gama

  • @Zeka46
    @Zeka46 Месяц назад

    🤣😂 God bless you Gama

  • @feywellkapala7093
    @feywellkapala7093 Месяц назад

    Powerful message man of GOd

  • @user-wx7pw8xg6x
    @user-wx7pw8xg6x Месяц назад

    Wat a wonderful preaching

  • @phelantunikapikule4624
    @phelantunikapikule4624 Месяц назад

    Amene ali ndi khutu la uzimu uthengawu wawuva koma amene ali ndikhutu koma osamava, ndiwo ma comment ambiri tikuwawonawa. Amen pastor

  • @gomesavirgo3987
    @gomesavirgo3987 Месяц назад

    Y.G is the greatest Reverend of all time

  • @vukanifracksonchinkonde7324
    @vukanifracksonchinkonde7324 Месяц назад

    Wonderful preaching

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад

    Chonde amalawi tisatembelele dziko lathu chonde mau akulu ochokela mkamwa mwa abusa yasini gama amen

  • @RobertCosmas-bo1uo
    @RobertCosmas-bo1uo Месяц назад

    Ulaliki mbambande yobu mwayenkha munali kulimba mtima ndkukhala nacho chikhulupiriro chozama amen

  • @chipiesato-ut7hx
    @chipiesato-ut7hx Месяц назад

    Powerful message ❤❤❤amen and amen

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 Месяц назад

    Big up brother man!!

  • @LytonMfuni
    @LytonMfuni Месяц назад

    I knew my rev: never go wrong.🇿🇲

  • @khamakhwiliro4093
    @khamakhwiliro4093 Месяц назад

    Powerful Preaching

  • @RalphZambezi
    @RalphZambezi Месяц назад

    Ndipo zobvuta Zambiri zikubwela sakunama

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 Месяц назад

    Powerful message ❤❤❤❤❤😊

  • @MikeMakaww
    @MikeMakaww Месяц назад

    Great great great apstor of the year

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 Месяц назад +1

    May God bless His Word through you moderator and may He also plant a heart of philanthropy and patriotism in all political,traditional religious, and legal authorities in Malawi to be once again a Godfearing nation. Amen

    • @RaphaelLudaviko
      @RaphaelLudaviko Месяц назад

      malawi wathu ndipamene takhalapo. Amen abusa

  • @richardarmittage1693
    @richardarmittage1693 Месяц назад

    Amen and Amen !!!!! Mau omveka bwino kwabasi

  • @gabiembuhagondwe3629
    @gabiembuhagondwe3629 Месяц назад

    Yassin gama ndiwaku 49 mama ccap church nt ku 25

  • @hajisonzanditha1246
    @hajisonzanditha1246 Месяц назад

    Great preaching

  • @eunicesaiti
    @eunicesaiti Месяц назад +1

    Happy 60th independence Malawi and Long live.❤

    • @user-lz4kc5ob1t
      @user-lz4kc5ob1t Месяц назад

      Akulu mwati happy chani kkkkk kumalawi kulibe za happy mganize bwino

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 Месяц назад

      Eeee zako zili.pabwino Pali malawipa nkumati happy kakaka

    • @eunicesaiti
      @eunicesaiti Месяц назад

      60th independence and ufulu.

  • @georgealabih8979
    @georgealabih8979 Месяц назад

    True facts in life, ndaukonda uthengawu

  • @SkevaMustapher
    @SkevaMustapher Месяц назад

    Amen amen kuying'alula abusa

  • @eliasmpaso2978
    @eliasmpaso2978 Месяц назад

    Powerful massage

  • @LinessStafordsauti
    @LinessStafordsauti Месяц назад

    Amen man of God

  • @user-bi6pb5gc8t
    @user-bi6pb5gc8t Месяц назад +1

    Nkazi wopusa Ngati Mayi gotani hara

  • @BornwellChipango-s9m
    @BornwellChipango-s9m Месяц назад +2

    Koma anthu amalalika

  • @bernadettechoma
    @bernadettechoma Месяц назад +1

    Hallelujah!🎉🎉🎉🎉🎉

  • @HendrinaWalani
    @HendrinaWalani Месяц назад

    Amen so powerful

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 Месяц назад +1

    Osayelekeza kuwapha awa ,taneneratu

  • @mablemathuso3903
    @mablemathuso3903 Месяц назад

    Powerful message

  • @AtnessBanda
    @AtnessBanda Месяц назад

    Amen amen

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki Месяц назад +2

    A malawi sindimakumvetsani koma zowona after all what MCp has done to you in 3 weeks ago mwayiwala kale, kukuyitanani ku msinkhano inu nkupita,, mumati mukamvako chani chatsopano,,a oposition you guys are sleeping to much 😮h munayenela kukana osapezeka nawo pa chikondwelerochi,a MCP akukondelera their successful mission of killing chilima and the other 9, nchifukwa chake lero ali wokondwa,a malawi ndinu anthu osawona,how can you be invited for prayes to pray for the lives lost in chikangawa by the same man who orchestrated their death😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢 Malawians are you nomal ⁉️⁉️⁉️⁉️⁉️

    • @EllinaBitto
      @EllinaBitto Месяц назад +1

      Ndipo inu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

    • @NatashaBema
      @NatashaBema Месяц назад

      Zosayenda

  • @ChikumbutsoTsalangu
    @ChikumbutsoTsalangu Месяц назад +1

    Awa nde anadalitsika ndinthu

  • @HusseinMoffatt-mi1fl
    @HusseinMoffatt-mi1fl Месяц назад +1

    Ayasin ndi mbambandetu ndi weniweni

  • @ThokozanKanyerere
    @ThokozanKanyerere Месяц назад

    Amen

  • @NDIZOTHEKABANDA
    @NDIZOTHEKABANDA Месяц назад

    Amen paste!!!!

  • @desiremlewa
    @desiremlewa Месяц назад

    Kutumikila mulungu mwachindinje, pamalawi panga pano palibwanj?🎉 Hellooooooo

  • @MosesKhobiri-pr4hg
    @MosesKhobiri-pr4hg Месяц назад

    Ndiyitana padzina lanu yenkhova

  • @SanhedrinMasauli
    @SanhedrinMasauli Месяц назад

    M'busa ameneyu ndi wandale, ananyozapo zipani zina ndikuyamikila mcp,

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 Месяц назад

    Uthenga wabwino koma amaopako pangono a kambiri munthawi ngati iyi anaungalura uthenga .😂😂 a pule osawafunanso kkk.

  • @kadongolakadongola
    @kadongolakadongola Месяц назад

    My reverend

  • @user-dg5pc6rz1b
    @user-dg5pc6rz1b Месяц назад +1

    Eeeeeee ulaliki ogwila mtima

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 Месяц назад

    Chakwera akuzinyoza yekha aise😂😂 and inuyo mukugwira ntchito yanji if I may ask😂😂😂

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад +1

    Amalawi bvuto ulesi ndichikwa chake mtsoleli aliyese akakhala paudindo timati ndioipa akachoka wabwino kodi zooona atsogoleli onse. alamulilandziko linowa angakhale oipa ?

    • @chipi892
      @chipi892 Месяц назад

      U might not mean what you want to say

  • @BerthaChisoni2
    @BerthaChisoni2 Месяц назад

    Man of God

  • @user-kt5bq2wg6v
    @user-kt5bq2wg6v Месяц назад

    Wuthenga wabwino ambuye akudakitseni.

  • @PempheroAlufandika
    @PempheroAlufandika Месяц назад

    Ayasini inu ndi munthu wa mulungu ndipo ndinu mlangizi

  • @MikeMerecah
    @MikeMerecah Месяц назад

    Shehe uja amatinamiza koma uyu,

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z Месяц назад

    Malawi is not poor country

  • @LovemoreUlayazulu-ne3id
    @LovemoreUlayazulu-ne3id Месяц назад

    Abusa a ku 49 ku nvama ccap church fumbi gheeto

  • @PempheroAlufandika
    @PempheroAlufandika Месяц назад

    Ayasini inu zitigairani mau amulungu anthu munawasitha

  • @MercyMakhala
    @MercyMakhala Месяц назад

    Amen and Amen

  • @DevisonHala
    @DevisonHala Месяц назад

    Muzeni zoona aleke kupha anthu

  • @user-sh2hr2cw8b
    @user-sh2hr2cw8b Месяц назад

    Koma Uyudi anadzonzedwa zedi

  • @MiriamMdumuka
    @MiriamMdumuka Месяц назад

    Amen Amen

  • @user-im4tc9qi4j
    @user-im4tc9qi4j Месяц назад

    Koma abusa Bible munalimvesadi ambuye akudaliseni

  • @StevenBwanausi
    @StevenBwanausi Месяц назад

    Ameen Abusa

  • @user-sx7fg1NEDG
    @user-sx7fg1NEDG Месяц назад

    Amen 🙏

  • @ShidaMfune
    @ShidaMfune Месяц назад

    Amen ❤❤

  • @user-ec3xh4pc6t
    @user-ec3xh4pc6t Месяц назад

    Amen 🙏 🙏 🙏

  • @chiefmitengo
    @chiefmitengo Месяц назад

    Amene akunyoza Chakwera tsoka Kwa iye.uli ndi tsoka iwe onyoza munthu osalakwa, ngati ndi ulesi wakowo ongofuna kulandira go to page House khalamba yanu ikakupasani za ulele. Agalu inu

  • @calvinmalinga1774
    @calvinmalinga1774 Месяц назад

    kumalawi Kuno kulibe akazi opusa

  • @chiletsobisweck5007
    @chiletsobisweck5007 Месяц назад

    Mwangozi

  • @hastingsnamasasu8071
    @hastingsnamasasu8071 Месяц назад

    Amen!

  • @VincentAndrew-jz2gf
    @VincentAndrew-jz2gf Месяц назад

    Khaniyotu ndiyona

  • @lexsonlanjesi2050
    @lexsonlanjesi2050 Месяц назад

    Nde mwati ABUSA aku 25 eti???😂😂😂😂😂😂😂

  • @AmosPhilemon-y5e
    @AmosPhilemon-y5e Месяц назад

    Abusa ndye alalika kut amva tikunena kut zikoli timuchokeramo zikhale

  • @dysonmakhwira2394
    @dysonmakhwira2394 Месяц назад

    Kugunda kugwesa

  • @OweniMalokooweni-es9qx
    @OweniMalokooweni-es9qx Месяц назад

    Chinyora

  • @lusekeronyasulu8610
    @lusekeronyasulu8610 Месяц назад

    Abusa aku 25?

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 Месяц назад

    Nkazi opusa ngati mayi Yolamu, Monica Chakwera, Gotani Hara,

  • @mablemathuso3903
    @mablemathuso3903 Месяц назад

    Mulibvumbulotso mu ulaliki uwu,tiyeni timvetsere bwino ndi khutu la uzimu.Ambuye apitilize kukugwiritsani ntchito abusa.