Bon Kalindo,Kamlepu Kaluwa,Comrade Ntanyiwa,Wanda Msiska and his friend,Brian Banda and others you are really philanthropic and patriotic. May God bless you abundantly.Religious,political, traditional and social leaders here in Malawi are all ordained to the mentality of cupidity hence very unable to transform Malawi philanthropically and patriotically.
The DC mwana wayankhulira m Malawi mommuno osati mpakana kukabisala ku Zambia ayi chi Bon Kalindo chinatha mantha ndipo sichiopa Unyolo anta more 🔥🔥 Mr president waife anthu osauka😅😅😅😅
Tang'alulani the DC kuti atongwe-tongwe a MCP amve bwino lomwe. This Boniiii Kalindo the DC, mlowa mmalo mwa Solobala amene ananyongedwa pa makako nda agalu MCP ya Kamuzu ndi John Tembo
Kkkkkkkkk koma a Kalindo agogo anu ankakuuzani nthano ya sikusinja mukupita ku nzuzu , ndiye mwati ankakuwerengeranu mu chikangawa? Komanso mwati anaphana chifukwa cha udindo? Ndipaseni page ndiwerenge nawo basi . U are number 1
@@HalisonSolomon ukufuna ndikuyankhe? Born kalindo umamudziwa? Zomwe akumayankhula amayankhulira iweyo, it's wat u think? Ok kavotere amene ukumufunayo n uzandiuze kut zinthu tsopano zilibwino pamoyo wako. Kalindo sankatukwana DPP ndi Peter munthalika? Lero mwaiwala
DC PANTCHITO IFE WOZIWA ZINTHU WE KNOW KUTI ABONI KALINDO ALIPO PA NTCHITO YOSUTSA CHILICHOTSE NDE MUWONE ALOMWE AVEKERE EEE OOOO UUUU KUKUWA AGALU ACHILOMWE MKUNYA MCP IS GOING NO WAY 2030 WOOOOO CHAKWERA.
Bon Kalindo,Kamlepu Kaluwa,Comrade Ntanyiwa,Wanda Msiska and his friend,Brian Banda and others you are really philanthropic and patriotic. May God bless you abundantly.Religious,political, traditional and social leaders here in Malawi are all ordained to the mentality of cupidity hence very unable to transform Malawi philanthropically and patriotically.
Bon kalindo iweyo umatha kulankhula bwino. Chifukwa kulankhula kwako umanena zoona zokhazokha kumvera chisoni amalawi munyengo zowawa zomwe tikudusamo kamba ka utsogoleri olephera wa chakwera. Osafooka , osatopa mpakana satana ameneyi tithana naye 2025 ino. Keep it up wakulu ndimakunyadirani kwambiri
The DC mwana wayankhulira m Malawi mommuno osati mpakana kukabisala ku Zambia ayi chi Bon Kalindo chinatha mantha ndipo sichiopa Unyolo anta more 🔥🔥 Mr president waife anthu osauka😅😅😅😅
Aaaaaaaaaaaaaa@ koma nde zafikapotu mpaka muchenga machende awo ndithu
Sikusinja imweyo kkkkkk taimbaso Mr DC aifeeee❤❤❤
Ife si osauka ndipo sitisilira kukhala ndi president osauka😂😂😂😂😂
God protect mr DC
Fire Mr president mumayakhula zilungamo zokha zokha
🤣🤣🤣🤣🤣 ngati Malawi ndiwandani Mr DC
Ndabwereza kawili nyimbo yoooo anaphaa mubale wake gwenembe chifwukwa cha udido
Bon kalindo dddccccc❤
Mr bon kalindo you are number one. More fire Mr dc❤
Mr Kalindo great soldier
😂😂😂amangidwaso uyu ndithu sikusinja ndi gwenembe koma Mr the DC kkkkkkkk
Mwana wowopya kwambiri!!!!!!!!!❤❤❤❤❤❤
We love you the DC
The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉🎉
Sikusinja ndi Gwenembe yemweyo....ana amphunzile
Tili pa mbuyo panu DC ❤❤
Powerful Mr president ❤
My vote bn
Ndakhalira kuseka😂😂😂😂😂😂 iweyo ndi wani
God protect mr kalindo
Great indeed. Let's all rise ip.
Mulungu azikutetezera nkhondo mukuimenya
😂😂😂😂😂 malawi ndife makape timaopa muthu ot tamuvotela tokha
Mr Bon Kalindo on fire 🔥🔥💪
Bon kalindo yemweyo kuti wawawa!!!
Km chakwela watopa m'chenga mpaka nd wa boma kkkkkk😅😅😅😅😅
Yes iweeee ing'alure basi😂😂
Kkkkkk wapolice samwa ambuye nditengeni
Bon kalindo tili limodzi
kkkk koma chimwana chakwa njedza kkk
😂😂😂 koma ndaseka DC ayi taa sikusinja Kodi
The DC!!!!!!!!!!!!!!!
More fire mr winiko
❤❤❤❤smdc
The Dc ❤❤❤❤
Make mbuuu mwana mbuuuu 😅😅😅
Zoona akunena B kalindo
Super super😂😂
Hahaha kwachema 🔥
😂😂😂😂 Mr DC
Tang'alulani the DC kuti atongwe-tongwe a MCP amve bwino lomwe. This Boniiii Kalindo the DC, mlowa mmalo mwa Solobala amene ananyongedwa pa makako nda agalu MCP ya Kamuzu ndi John Tembo
Bwana apolice atraffic akuonjeza bwerani mnseu wa Bunda every 200m atraffic ndie a area 3 amabwera 3koloko am kuyimba pa mnseu mmmmmmm Malawi
Osafowoka bon kalindo
Kkkkkkkkk koma a Kalindo agogo anu ankakuuzani nthano ya sikusinja mukupita ku nzuzu , ndiye mwati ankakuwerengeranu mu chikangawa? Komanso mwati anaphana chifukwa cha udindo? Ndipaseni page ndiwerenge nawo basi . U are number 1
Avu
Lyton Mangochi bwerani yamanja ija kuno
Muma tiimila osatopa
Mr DC osafowoka
Ndipo Boma Lamanyi ngati ili ine sindinalionepo Aaash!!
More fire mbuyanga alomwe alomwe nophiya
Umakwana iweyo
Uyu ndi nyoooo
Koma iwe ndigalu kwambili
aaaaa zayambika liti tchega omwewu gati mwatopa nawo phandowo apatseni ena MCP is very nonsense iyaaa
Ipondeni Fadah
Good boy
Koma ndiye mwafikapo mpaka kulesa anthu kuti asamavuule mchenga really? Nyumba zanuzo munamangila mchenga munakawoda ku America? Silly people
A opposition zochita zamwo ndi zimodzimodzi
You are welcome Mr dc
I don't want to be Malawian anymore
Kulephera kuja ndi kumeneku, anthu ndi okwiya kale , atopa ndi boma ili
Mbambande me. Kalindo
Great 👍
❤
❤❤
🎉
Kuswa kuswa😂😂 akavote ndiamawo Oh yes 🔥🔥
Atsala atigulitsa mphweyaa kwatsala
DC ndimava kukoma mukatiyimilira
Mitu singwiradi.anthu onse anafa aja mwanzi wawo sukhara chete.
Mwazi unja wakuchingawa ukuwayenda Mitu anthu amenewa mchenga wobwela ndibvula 😅😅😅😅
😂😂the dc
Koma why sakuyamkhulapo za manganya ku mcp palibe audio olo imoz inakambapo za Mr usi
Pliz a DPP tadzukani kodi mukunafuna amalawi atani
Ndipo zomwe akupanga a Dpp akumabowa kwambiri anthu akuzunzika ndi boma Koma aliphee ngati akumetedwa
Akufuna tidziwe kut tidapanga mistake.. ankatiuzatu paja
@@IbrahimYusufu-z9d ndiye bola akazaluzanso asazalile chifukwa agalu a MCP akuwatakatu osusawa
Eeeee koma ationjezadi apa ndiye yalakwa,,
Tipindilana ndenvu mkamwa ulendo wake ndi umeneu
The DC
Mo faya mr dc
Ulemu wano A Kalendo
Koma Chaka chamawa tikhapana ndithu
Anapha zake chifukwa chaudindo
Iswani ndithu man wamkulu ndi mulungu basi
Kodi achakwerawa mchiyani makamaka zikuyenda koma??
Bwana ine office kuno ku Lilongwe tikupita kokayang'anira mayeso koma no allowances 😅
kkk iwe usandiseketse no what?aa. wabodzaiwe
@@PeterChilombo-ou2cd ok u can not believe it,maybe your side, koma kuno tili sanatipasebe za Theory subjects
The D C!!!!
Ndkhulupilira kut a Malawi mistake iyiyi sitizachitanso
Km inuyo mumakwana kkkkkkkk the Dc
The DC😂
😂😂❤
😢😢😢😢
😢😢😢😢😢😢
Ubwino wake a Chakwera omwe mukuwanenawo sakuyankhani nkomwe, mumangobwebwetuka zaziii ngat ufulu omwe mumamenyera anthu osaukawo umathandizapo kalikonse, tikungogonabe ndinjala ngat mumati mukayankhula apa mumatipatsa ndalama, phindu lanu ndichani, ine ndiye nsaname zimandinyasa izizi, palibe chomwe munthu wanzeru angayamikire pazomwe mumayankhulazi, coz maboma onsewa zochitika ndizimodzi palibeso wabwino apa, n zonse izizi zilibe nzeru, nanga mpunga souseg zimenezo zikankhale zoyankhulira anthu osauka kapena zangolowa zidani zanu?? Zopusa
Samayankhatu mosathepo mau ap😅😅😅
IWEYO ndi opusa kwambiri ndi chakwera wakoyo ngati akutuma cadet mbuzi, ngati iwe ukidya ndi mcp usawanyase AMALAWI AKUVUTIKA , ndiye uzikayankhula mbwerera zako zankutuzo , ngati sizikusangalatsa amakutuma kuti uzimvera ndi ndani ulibe manyazi ? Cadet supit
@@HalisonSolomon ukufuna ndikuyankhe? Born kalindo umamudziwa? Zomwe akumayankhula amayankhulira iweyo, it's wat u think? Ok kavotere amene ukumufunayo n uzandiuze kut zinthu tsopano zilibwino pamoyo wako. Kalindo sankatukwana DPP ndi Peter munthalika? Lero mwaiwala
@@isaacchiwaula731 inu musokosa mungosiya kuverako bas sizokakamiza izi boss
@@isaacchiwaula731 iwe sungamakhale KUMBUYO kwa mcp ngati sukuona momwe dziko lavundira ndiye kuduka mutu kumeneko , usiyamitse mene chakwera amatenga boma linali motani ndiye pano zilimotani ? Ndiye timusiye chakera alamuleso lidzakhala dziko? Anthu adzakhala ngati ndani, tiyeni tiganizire ana omwe taberekawa tisakhale ngati a police ndi asilikali amene asankha kigwira ntchito ndi chipano malo moteteza malamulo adziko,
DC
Mafia
U na problematic
DC PANTCHITO IFE WOZIWA ZINTHU WE KNOW KUTI ABONI KALINDO ALIPO PA NTCHITO YOSUTSA CHILICHOTSE NDE MUWONE ALOMWE AVEKERE EEE OOOO UUUU KUKUWA AGALU ACHILOMWE MKUNYA MCP IS GOING NO WAY 2030 WOOOOO CHAKWERA.
Zosantheka Brazil ndipo idzankhala yazikwanje zomwe² mwaphela saulosinever again MCP achimwene
2030 mcp ikakhala mnyumba mwa kwanu zopusa anthu opanda nzeru ngati akukudyetsani ndiye muphe anthu chifukwa choti mukudya ndi mcp yakuphayo yankhanza zachibwana
The DC