Комментарии •

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 22 дня назад +15

    Bon Kalindo,Kamlepu Kaluwa,Comrade Ntanyiwa,Wanda Msiska and his friend,Brian Banda and others you are really philanthropic and patriotic. May God bless you abundantly.Religious,political, traditional and social leaders here in Malawi are all ordained to the mentality of cupidity hence very unable to transform Malawi philanthropically and patriotically.

  • @BlessingsMbawa
    @BlessingsMbawa 21 день назад

    Bon kalindo iweyo umatha kulankhula bwino. Chifukwa kulankhula kwako umanena zoona zokhazokha kumvera chisoni amalawi munyengo zowawa zomwe tikudusamo kamba ka utsogoleri olephera wa chakwera. Osafooka , osatopa mpakana satana ameneyi tithana naye 2025 ino. Keep it up wakulu ndimakunyadirani kwambiri

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 22 дня назад +4

    The DC mwana wayankhulira m Malawi mommuno osati mpakana kukabisala ku Zambia ayi chi Bon Kalindo chinatha mantha ndipo sichiopa Unyolo anta more 🔥🔥 Mr president waife anthu osauka😅😅😅😅

  • @ThompsonMakwakwa
    @ThompsonMakwakwa 22 дня назад +2

    Aaaaaaaaaaaaaa@ koma nde zafikapotu mpaka muchenga machende awo ndithu

  • @ChrissySalimu
    @ChrissySalimu 22 дня назад +1

    Sikusinja imweyo kkkkkk taimbaso Mr DC aifeeee❤❤❤

  • @user-gm3cx2xn9o
    @user-gm3cx2xn9o 22 дня назад +1

    Ife si osauka ndipo sitisilira kukhala ndi president osauka😂😂😂😂😂

  • @AfricanKingdom-uv1qb
    @AfricanKingdom-uv1qb 21 день назад +1

    God protect mr DC

  • @JibuzahDrag
    @JibuzahDrag 22 дня назад +1

    Fire Mr president mumayakhula zilungamo zokha zokha

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 22 дня назад +1

    🤣🤣🤣🤣🤣 ngati Malawi ndiwandani Mr DC

  • @ChristinaSinoyakapawo
    @ChristinaSinoyakapawo 22 дня назад +1

    Ndabwereza kawili nyimbo yoooo anaphaa mubale wake gwenembe chifwukwa cha udido

  • @ShafieIdrissah
    @ShafieIdrissah 21 день назад

    Bon kalindo dddccccc❤

  • @ishmaelcassim806
    @ishmaelcassim806 22 дня назад +1

    Mr bon kalindo you are number one. More fire Mr dc❤

  • @AbdulsEdsan
    @AbdulsEdsan 22 дня назад +1

    Mr Kalindo great soldier

  • @hajrazuwaja4993
    @hajrazuwaja4993 22 дня назад +1

    😂😂😂amangidwaso uyu ndithu sikusinja ndi gwenembe koma Mr the DC kkkkkkkk

  • @JohnmarkNazombe-hi9xd
    @JohnmarkNazombe-hi9xd 22 дня назад +1

    Mwana wowopya kwambiri!!!!!!!!!❤❤❤❤❤❤

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje 22 дня назад +1

    We love you the DC

  • @Moses51
    @Moses51 22 дня назад +1

    The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉🎉

  • @julietmussa5103
    @julietmussa5103 22 дня назад +1

    Sikusinja ndi Gwenembe yemweyo....ana amphunzile

  • @user-cg5ml7ym4v
    @user-cg5ml7ym4v 22 дня назад +2

    Tili pa mbuyo panu DC ❤❤

  • @user-qc5lh3xw2h
    @user-qc5lh3xw2h 22 дня назад +1

    Powerful Mr president ❤

  • @AubreyBamus
    @AubreyBamus 18 дней назад

    My vote bn

  • @user-ln5hw7dn9g
    @user-ln5hw7dn9g 22 дня назад +1

    Ndakhalira kuseka😂😂😂😂😂😂 iweyo ndi wani

  • @chrisneySwanepoel-yu5vd
    @chrisneySwanepoel-yu5vd 22 дня назад +2

    God protect mr kalindo

  • @richardkumbambe-tg9qi
    @richardkumbambe-tg9qi 22 дня назад +2

    Great indeed. Let's all rise ip.

  • @user-fd7wj3mg2i
    @user-fd7wj3mg2i 21 день назад

    Mulungu azikutetezera nkhondo mukuimenya

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba 22 дня назад +1

    😂😂😂😂😂 malawi ndife makape timaopa muthu ot tamuvotela tokha

  • @bamusmajawa1619
    @bamusmajawa1619 22 дня назад +1

    Mr Bon Kalindo on fire 🔥🔥💪

  • @shamimmahomed6709
    @shamimmahomed6709 22 дня назад +1

    Bon kalindo yemweyo kuti wawawa!!!

  • @JosephPindani
    @JosephPindani 22 дня назад +1

    Km chakwela watopa m'chenga mpaka nd wa boma kkkkkk😅😅😅😅😅

  • @fatsanibanda5213
    @fatsanibanda5213 22 дня назад +1

    Yes iweeee ing'alure basi😂😂

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl 22 дня назад +1

    Kkkkkk wapolice samwa ambuye nditengeni

  • @WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un
    @WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un 21 день назад

    Bon kalindo tili limodzi

  • @JuvenileDebwe-bv8ow
    @JuvenileDebwe-bv8ow 22 дня назад +1

    kkkk koma chimwana chakwa njedza kkk

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e 22 дня назад +1

    😂😂😂 koma ndaseka DC ayi taa sikusinja Kodi

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9d 21 день назад

    The DC!!!!!!!!!!!!!!!

  • @PeterMoosa
    @PeterMoosa 22 дня назад +1

    More fire mr winiko

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3z 22 дня назад

    ❤❤❤❤smdc

  • @user-dk6yc8pl2m
    @user-dk6yc8pl2m 22 дня назад +1

    The Dc ❤❤❤❤

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 22 дня назад +1

    Make mbuuu mwana mbuuuu 😅😅😅

  • @AlexNkhata-c8n
    @AlexNkhata-c8n 21 день назад

    Zoona akunena B kalindo

  • @thandothando6556
    @thandothando6556 21 день назад

    Super super😂😂

  • @user-sp4kn8rh2j
    @user-sp4kn8rh2j 21 день назад

    Hahaha kwachema 🔥

  • @user-mi3fw1zg8b
    @user-mi3fw1zg8b 22 дня назад +1

    😂😂😂😂 Mr DC

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 22 дня назад

    Tang'alulani the DC kuti atongwe-tongwe a MCP amve bwino lomwe. This Boniiii Kalindo the DC, mlowa mmalo mwa Solobala amene ananyongedwa pa makako nda agalu MCP ya Kamuzu ndi John Tembo

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 22 дня назад

    Bwana apolice atraffic akuonjeza bwerani mnseu wa Bunda every 200m atraffic ndie a area 3 amabwera 3koloko am kuyimba pa mnseu mmmmmmm Malawi

  • @user-mx5cx3gl4h
    @user-mx5cx3gl4h 22 дня назад

    Osafowoka bon kalindo

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu
    @TiyanjaneMkwate-we8gu 22 дня назад

    Kkkkkkkkk koma a Kalindo agogo anu ankakuuzani nthano ya sikusinja mukupita ku nzuzu , ndiye mwati ankakuwerengeranu mu chikangawa? Komanso mwati anaphana chifukwa cha udindo? Ndipaseni page ndiwerenge nawo basi . U are number 1

  • @user-vq6zr4tn8v
    @user-vq6zr4tn8v 21 день назад

    Muma tiimila osatopa

  • @AdiniKhama
    @AdiniKhama 22 дня назад +1

    Mr DC osafowoka

  • @frankdonovanntambira
    @frankdonovanntambira 22 дня назад

    Ndipo Boma Lamanyi ngati ili ine sindinalionepo Aaash!!

  • @griviniakanjaula4456
    @griviniakanjaula4456 22 дня назад

    More fire mbuyanga alomwe alomwe nophiya

  • @user-tm6wl5tt3u
    @user-tm6wl5tt3u 20 дней назад

    Umakwana iweyo

  • @RabsonSabit-nc5ds
    @RabsonSabit-nc5ds 22 дня назад

    Uyu ndi nyoooo

  • @user-ng4ic8jo8b
    @user-ng4ic8jo8b 22 дня назад

    Koma iwe ndigalu kwambili

  • @IssahAluba
    @IssahAluba 22 дня назад

    aaaaa zayambika liti tchega omwewu gati mwatopa nawo phandowo apatseni ena MCP is very nonsense iyaaa

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 22 дня назад

    Ipondeni Fadah

  • @PachaloShaba-pf5vw
    @PachaloShaba-pf5vw 22 дня назад

    Good boy

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu 22 дня назад +1

    Koma ndiye mwafikapo mpaka kulesa anthu kuti asamavuule mchenga really? Nyumba zanuzo munamangila mchenga munakawoda ku America? Silly people

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 22 дня назад

    A opposition zochita zamwo ndi zimodzimodzi

  • @MemoryKamanga-jv4jh
    @MemoryKamanga-jv4jh 22 дня назад

    You are welcome Mr dc

  • @lawrenceblacktealyson8015
    @lawrenceblacktealyson8015 22 дня назад

    I don't want to be Malawian anymore

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 22 дня назад

    Kulephera kuja ndi kumeneku, anthu ndi okwiya kale , atopa ndi boma ili

  • @RichmanNkhoma
    @RichmanNkhoma 22 дня назад

    Mbambande me. Kalindo

  • @van-wykchilapondwa6981
    @van-wykchilapondwa6981 22 дня назад

    Great 👍

  • @Chipilirodaniel1989
    @Chipilirodaniel1989 21 день назад

  • @JohnZyambo-q8h
    @JohnZyambo-q8h 22 дня назад

    ❤❤

  • @JohnZyambo-q8h
    @JohnZyambo-q8h 22 дня назад

    🎉

  • @scoltenroma6240
    @scoltenroma6240 22 дня назад +1

    Kuswa kuswa😂😂 akavote ndiamawo Oh yes 🔥🔥

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt 22 дня назад

    Atsala atigulitsa mphweyaa kwatsala

  • @SilenceChepiano
    @SilenceChepiano 22 дня назад

    DC ndimava kukoma mukatiyimilira

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e 22 дня назад

    Mitu singwiradi.anthu onse anafa aja mwanzi wawo sukhara chete.

    • @JeanKambala-gm1zr
      @JeanKambala-gm1zr 22 дня назад

      Mwazi unja wakuchingawa ukuwayenda Mitu anthu amenewa mchenga wobwela ndibvula 😅😅😅😅

  • @JasperKaleni-dx6nn
    @JasperKaleni-dx6nn 21 день назад

    😂😂the dc

  • @oskidooscar7468
    @oskidooscar7468 22 дня назад

    Koma why sakuyamkhulapo za manganya ku mcp palibe audio olo imoz inakambapo za Mr usi

  • @KennethMchenga-j9c
    @KennethMchenga-j9c 22 дня назад +1

    Pliz a DPP tadzukani kodi mukunafuna amalawi atani

    • @dalitson3558
      @dalitson3558 22 дня назад +1

      Ndipo zomwe akupanga a Dpp akumabowa kwambiri anthu akuzunzika ndi boma Koma aliphee ngati akumetedwa

    • @IbrahimYusufu-z9d
      @IbrahimYusufu-z9d 22 дня назад

      Akufuna tidziwe kut tidapanga mistake.. ankatiuzatu paja

    • @dalitson3558
      @dalitson3558 22 дня назад

      @@IbrahimYusufu-z9d ndiye bola akazaluzanso asazalile chifukwa agalu a MCP akuwatakatu osusawa

  • @Aisha-db6ds
    @Aisha-db6ds 22 дня назад

    Eeeee koma ationjezadi apa ndiye yalakwa,,
    Tipindilana ndenvu mkamwa ulendo wake ndi umeneu

  • @stevejizaremu3396
    @stevejizaremu3396 22 дня назад

    The DC

  • @TapiwaKhwisula
    @TapiwaKhwisula 22 дня назад

    Mo faya mr dc

  • @irenioeugeniosumila6647
    @irenioeugeniosumila6647 22 дня назад

    Ulemu wano A Kalendo

  • @StanleyChirwa-d6b
    @StanleyChirwa-d6b 22 дня назад

    Koma Chaka chamawa tikhapana ndithu

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no 22 дня назад

    Anapha zake chifukwa chaudindo

  • @FrancisChimwaza-t7d
    @FrancisChimwaza-t7d 22 дня назад

    Iswani ndithu man wamkulu ndi mulungu basi

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 22 дня назад

    Kodi achakwerawa mchiyani makamaka zikuyenda koma??

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 22 дня назад

    Bwana ine office kuno ku Lilongwe tikupita kokayang'anira mayeso koma no allowances 😅

    • @PeterChilombo-ou2cd
      @PeterChilombo-ou2cd 22 дня назад

      kkk iwe usandiseketse no what?aa. wabodzaiwe

    • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
      @ChikumbutsoJohn-rs4tt 22 дня назад

      @@PeterChilombo-ou2cd ok u can not believe it,maybe your side, koma kuno tili sanatipasebe za Theory subjects

  • @MecyMalothi
    @MecyMalothi 22 дня назад

    The D C!!!!

  • @SolomonShaibuh
    @SolomonShaibuh 22 дня назад

    Ndkhulupilira kut a Malawi mistake iyiyi sitizachitanso

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s 22 дня назад

    Km inuyo mumakwana kkkkkkkk the Dc

  • @charitykalua8507
    @charitykalua8507 21 день назад

    The DC😂

  • @JamilahChitulu
    @JamilahChitulu 22 дня назад

    😂😂❤

  • @FrankiePangan
    @FrankiePangan 22 дня назад

    😢😢😢😢

  • @phillgatoma4857
    @phillgatoma4857 22 дня назад

    😢😢😢😢😢😢

  • @isaacchiwaula731
    @isaacchiwaula731 22 дня назад

    Ubwino wake a Chakwera omwe mukuwanenawo sakuyankhani nkomwe, mumangobwebwetuka zaziii ngat ufulu omwe mumamenyera anthu osaukawo umathandizapo kalikonse, tikungogonabe ndinjala ngat mumati mukayankhula apa mumatipatsa ndalama, phindu lanu ndichani, ine ndiye nsaname zimandinyasa izizi, palibe chomwe munthu wanzeru angayamikire pazomwe mumayankhulazi, coz maboma onsewa zochitika ndizimodzi palibeso wabwino apa, n zonse izizi zilibe nzeru, nanga mpunga souseg zimenezo zikankhale zoyankhulira anthu osauka kapena zangolowa zidani zanu?? Zopusa

    • @StanleyChirwa-d6b
      @StanleyChirwa-d6b 22 дня назад

      Samayankhatu mosathepo mau ap😅😅😅

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 22 дня назад

      IWEYO ndi opusa kwambiri ndi chakwera wakoyo ngati akutuma cadet mbuzi, ngati iwe ukidya ndi mcp usawanyase AMALAWI AKUVUTIKA , ndiye uzikayankhula mbwerera zako zankutuzo , ngati sizikusangalatsa amakutuma kuti uzimvera ndi ndani ulibe manyazi ? Cadet supit

    • @isaacchiwaula731
      @isaacchiwaula731 22 дня назад

      @@HalisonSolomon ukufuna ndikuyankhe? Born kalindo umamudziwa? Zomwe akumayankhula amayankhulira iweyo, it's wat u think? Ok kavotere amene ukumufunayo n uzandiuze kut zinthu tsopano zilibwino pamoyo wako. Kalindo sankatukwana DPP ndi Peter munthalika? Lero mwaiwala

    • @StanleyChirwa-d6b
      @StanleyChirwa-d6b 22 дня назад

      @@isaacchiwaula731 inu musokosa mungosiya kuverako bas sizokakamiza izi boss

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 22 дня назад

      @@isaacchiwaula731 iwe sungamakhale KUMBUYO kwa mcp ngati sukuona momwe dziko lavundira ndiye kuduka mutu kumeneko , usiyamitse mene chakwera amatenga boma linali motani ndiye pano zilimotani ? Ndiye timusiye chakera alamuleso lidzakhala dziko? Anthu adzakhala ngati ndani, tiyeni tiganizire ana omwe taberekawa tisakhale ngati a police ndi asilikali amene asankha kigwira ntchito ndi chipano malo moteteza malamulo adziko,

  • @RidsonChafulumirah-r2y
    @RidsonChafulumirah-r2y 22 дня назад

    DC

  • @muneeladan8580
    @muneeladan8580 22 дня назад

    Mafia

  • @BudaEarth
    @BudaEarth 20 дней назад

    U na problematic

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 22 дня назад

    DC PANTCHITO IFE WOZIWA ZINTHU WE KNOW KUTI ABONI KALINDO ALIPO PA NTCHITO YOSUTSA CHILICHOTSE NDE MUWONE ALOMWE AVEKERE EEE OOOO UUUU KUKUWA AGALU ACHILOMWE MKUNYA MCP IS GOING NO WAY 2030 WOOOOO CHAKWERA.

    • @JeanKambala-gm1zr
      @JeanKambala-gm1zr 22 дня назад

      Zosantheka Brazil ndipo idzankhala yazikwanje zomwe² mwaphela saulosinever again MCP achimwene

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 22 дня назад

      2030 mcp ikakhala mnyumba mwa kwanu zopusa anthu opanda nzeru ngati akukudyetsani ndiye muphe anthu chifukwa choti mukudya ndi mcp yakuphayo yankhanza zachibwana

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl 22 дня назад

    The DC