BON KALINDO KUYANKHULA PAMBUYO PA CHIGAMULO CHAKU COURT 10 July 2024

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 8 июл 2024

Комментарии • 65

  • @MuhajirinaSaid
    @MuhajirinaSaid 16 дней назад +4

    Keep it up mr Dc

  • @ForsterThawan
    @ForsterThawan 16 дней назад +4

    Aaaaaaaaa koma kalindo ndi munthu wankulu kwambili ndipo amayankhula saopa kanthu

    • @user-lz5yv4vj6h
      @user-lz5yv4vj6h 16 дней назад

      Kkkkk koma Born aaaa ndi president wanthudi ,l salute you sir

  • @josephinemisomali6840
    @josephinemisomali6840 16 дней назад +3

    Ndimadikira Dc kuti lero atichani apa nditha kukagona 😂😂😂 Boni kalindooooooooo!!!

  • @NelsonbastonMandela
    @NelsonbastonMandela 16 дней назад +2

    Kkkkl mpaka police 200 koma bon kalindo ndimunthu okwiya kwambiri 😂😂😂😂😂

  • @robertchitsulo8006
    @robertchitsulo8006 16 дней назад +3

    Bon kkkkkkkkk akuti aputa milandu yambiri iwe ndi 1 basi kkkkkk

  • @SamfrayGvng
    @SamfrayGvng 14 дней назад

    Eeeee ai ndagonja nanu big up a 🙋DC

  • @user-mk7fh5ml8s
    @user-mk7fh5ml8s 15 дней назад +1

    Mr kalindo ife tidalira inu basi❤❤❤

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d 16 дней назад +2

    Wakumuzi kwenikwenni za pa social media -zi saziziwa kuti inu muma -aimilira

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 16 дней назад +2

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂Nyau kumva pain 😂😂😂

  • @AufiThera
    @AufiThera 15 дней назад

    Kod Aku Germany aja bas angotithera ndalama mosemuja lipot osabwerensa aaaa ndiye angopita kwawo wapas amenewo iyaaa

  • @TougiedaAjam
    @TougiedaAjam 15 дней назад

    It's the Dc keep it

  • @PeterKathewera
    @PeterKathewera 15 дней назад

    Kodi kwanu sanakuvoteren bwanji😢😢

  • @AlickMakunganya-o4w
    @AlickMakunganya-o4w 15 дней назад

    Ichichi sichamasewera Adaaa😂😂

  • @PetroMatias
    @PetroMatias 16 дней назад +2

    🤝🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🤝🤝🤝🤝

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e 15 дней назад

    DC 🥰

  • @EvsonNgurube
    @EvsonNgurube 15 дней назад

    Bon kalindooooooo

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 16 дней назад +1

    Za Imfa Ya Chilima Tisaopsezane, Ngati Simunamuphe Tiuzeni Kuti Chinachitika Ndichani?
    Ku MCP musabise zinthu zoti munapanga nokha, Chakwela Ukhale ndimanyazi Ubusa wake Uti Unkapanga iwe Okupha Nzako Chifukwa Chautsogoleli?

  • @AufiThera
    @AufiThera 15 дней назад

    Wanthu wanthu DC 💪

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e 15 дней назад

    DC ❤

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali 16 дней назад

    Ndodo ija ituluke DC tatopa ndi chakwera ife kkkkkkkkkkk the DC ❤❤❤❤

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-2001 14 дней назад

    Kkkkk chikumvesa kukoma a Malawi ambili

  • @user-fz3gu2ez1o
    @user-fz3gu2ez1o 14 дней назад

    Kkkkkkkk
    Mwana ovuta kulera
    Hehehehe

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 16 дней назад

    Amafuna kukuipisirani Mr DC koma akunama 💪

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 16 дней назад

    Bon Kalindo the DC (The most dangerous child)❤❤❤❤❤❤

  • @GracePhirie
    @GracePhirie 15 дней назад

    Mwana woipa kwambiri😂😂😂

  • @allansili-rc9gc
    @allansili-rc9gc 16 дней назад +1

    🤣🤣🤣🤣 mpaka a police 200 kkkkk

  • @williamchatha6139
    @williamchatha6139 15 дней назад

    The DC salute

  • @ShaibKudzinja
    @ShaibKudzinja 16 дней назад

    The DC, ndipo anthu tizamulilira kwambri mkului nd ntchto yakei akazasamira mkono

  • @ZexNkhoma-p8t
    @ZexNkhoma-p8t 16 дней назад

    The braval child of Malawi, Speak out without fear and favor! Bon kalindo, The DC...

  • @user-mi3fw1zg8b
    @user-mi3fw1zg8b 15 дней назад

    😂😂😂😂😂the DC machine

  • @kondwanimandala4575
    @kondwanimandala4575 15 дней назад

    Winiko the DC pachilungamo sumawopa iweyo umatha

  • @KhalideNerve-mu1eq
    @KhalideNerve-mu1eq 15 дней назад

    ❤❤❤❤❤ more fire 🔥

  • @lazarousnamakhwa6549
    @lazarousnamakhwa6549 15 дней назад

    boni kalindo malawi 😂😂😂😂

  • @IbrahimYusufu-z9d
    @IbrahimYusufu-z9d 15 дней назад

    Bon Kalindo

  • @NorahMangasanja
    @NorahMangasanja 16 дней назад

    Mr Dc mumakwana inuyo tilinanu ife amalawi

  • @HaruunWalusa
    @HaruunWalusa 15 дней назад

    The DC

  • @moseskalande9853
    @moseskalande9853 15 дней назад

    zopanda ntchito zomwe ukulu inu mumalankhula

  • @nafejonga972
    @nafejonga972 16 дней назад

    Chizagwira zipolopolo😅😅 iwe ndi machine, wait to destroy them with you

  • @EmmanuelNgambi-y6h
    @EmmanuelNgambi-y6h 15 дней назад

    Umakwana DC

  • @user-zs6qc9dx8s
    @user-zs6qc9dx8s 16 дней назад

    The DC🔥

  • @user-ql8nf2vb8s
    @user-ql8nf2vb8s 16 дней назад

    It's plezident of poor people

  • @AustinBornface
    @AustinBornface 16 дней назад

    The DC!

  • @ArnoldKamanga-r6k
    @ArnoldKamanga-r6k 16 дней назад

    Uyu yekha timuteteza I swear

  • @PoxisNation-fe1kr
    @PoxisNation-fe1kr 15 дней назад

    The DC 😂😂😂

  • @OnexAliMwale
    @OnexAliMwale 15 дней назад

    Kulankhula wina aliyese atha kulankhula koma kuchita zakupsa...Bwana Bon kalindo akumalankhula koma ndi action yanji yomwe ikuchitika? We need kulankhula ndikuchita namaona progress..Mukatiuza zomwe mwapezazo kenako muzinenanso kuti tipanga izi pothana ndizimenezi...tisamangokhalira kumva mwana oopsa mmalankhulidwe, action nothing

    • @myheartforkids2876
      @myheartforkids2876 15 дней назад

      Inu mene mwayankhulamu mwapanga action yanji? Kkkkkkkkkk

    • @sir-wanton-2001
      @sir-wanton-2001 14 дней назад

      Kkkk mbuli ife timakonda DC

    • @OnexAliMwale
      @OnexAliMwale 14 дней назад

      @@myheartforkids2876 Amene amawatsata omenyera ufulawa atha kudziwa kuti nthawi ya Bingu kunali Mavuto Bamusi ndipo amati akanena amapanga action ndipo Mpaka Bingu anasintha machitidwe azinthu zina, nthawi ya Peter kunali Timothy Mtambo, za amenewu mukudziwa zomwe amachita, Koma Bwana Bon mmmm tiyeni tizingomva Mwana oopsa komanso kung'alura kenako tiseke osaona chisintha...I always appreciate for actions not talking that's why tonse Government tikudana nalo coz nawoso kulankhula amatha koma kukwanilitsa kukuwavuta

  • @RedrawLittleMushutula
    @RedrawLittleMushutula 15 дней назад

    DC mewafika

  • @williamalvis6028
    @williamalvis6028 16 дней назад

    The DC umakwana

  • @phindiswatshibo7101
    @phindiswatshibo7101 16 дней назад

    Chipangoline😂😂

  • @chipanganofackison5185
    @chipanganofackison5185 16 дней назад

    Zamanyi basi kape ndiweyo akanadakhala Ofuna kupha akanampha iweyo umatisokoneka mutu amakutuma ndindani? Umango uwanamizila anthu wosawuka ndidziko lanji lomwe kungapezeke wolemera wose?

  • @moseskalande9853
    @moseskalande9853 15 дней назад

    Even ur voice doesn't sound like a leader

  • @FrankMulola
    @FrankMulola 16 дней назад

    😂😂😂😂😂

  • @samhussen708
    @samhussen708 16 дней назад

    😂😂

  • @brightkaunda920
    @brightkaunda920 16 дней назад

    Ati amangidwe ndamako