If u stopped by the police officers on the road in ur 🚗 .who is supposed to follow the other? 4me i don't go out to a police office who stopped me coz i had no intention of stopping.u stop me,u come to me &tell me why you stopped me not me coming to ask u
Apolice amaonjeza nkhanza pansewu😢
Zikhale ng'oma ma bombasa wagulakoso 😂😂😂 wausilu iwe
A Traffic police ambiri za miyoyo ya anthu alibe nazo ntchito nde ndizimenezo
Powerful GwedeGwede,,bambo banda
Salute
Live from south Africa cape town
Munadza makosana ❤❤
Chipewa cha khwangwala kuteloko amafuna anyemere kaye kuti adutse ndi mwana wodwala ,utsilu dyera
I salute mibawa
Kkkk chipanda kuyankhula bwezi ali mumaguza omwewo kkkk
Mumakwana guys 💥
Sitidya ndale kkkk ndimakunyadilani kwambiri Mibawa TV
Anduna akutsotsola ulusi pano akuti kuionesa 😂
😢😢😢😢 apolice apamalawi vuto ndi umphawi anthuni
Za police mbuzi zaanthu izi kma kuba ndikupempha
Mwanayo anali ndi 1 month and 3 weeks mgalimoto ndinali MO ine😢
Chakwera mumuudzeso kuti opha nzake afeso chifukwa chakwera anapha chilima my boss he call chakwera bull dog😂😂
Nkaka akulembaso MSCE
Ndipo apolice akumalawi ndinu otembelekdwa ndipo mukulephela kugwila mbava koma kulimbana ndi athu osalakwa
Muli ndi mtopola guyz😊
Kkkkkkkkkkkkkkkkkkk Komatsu dzina izi
Steve ndi Selina mativesa kukoma
Nawo a MCP asatile malamulo a gwirizano wawo kuti apite s Utm asogoleke nawo
Zoonadi apolice amaonjeza
Tisakubisileni apolice alowa chiwewe kusaka ndalama
Madokotalanso ali ndivutolawo munthu akumuwona ali pamzele komakungobwelawinawake wawudindo amakudusila chifukwachani winayusi munthu kodi?
Kkkkkk
Va police palibe vomwe vikuchita vimangodziwa kupempha ndrama pamseu ndikumanga mbava yoti anthu aigwira kare anthu eniake,ndipo vitengelepo phunziro mwina vingayambe kugwira ntchito bwino vipewa va mbalevo
Ku malawi zimathera tikufufuza.
Mbambande mibawa
Futso nkhumati kodi sopano kubako mwathana Nako?
Wanga kufa mwana chifukwa cha wa police wandigwira nayeso adzafera pompo ineyoso natopa nawo mbuzi zimenezo pofunika osamawanyengelera😢😢
If u stopped by the police officers on the road in ur 🚗 .who is supposed to follow the other? 4me i don't go out to a police office who stopped me coz i had no intention of stopping.u stop me,u come to me &tell me why you stopped me not me coming to ask u
Zoonadi Inu muli bwino kwambili
Malawi tingogulisa tigawane ndlama bc