Комментарии •

  • @kadijachilwan967
    @kadijachilwan967 21 день назад +5

    Apolice amaonjeza nkhanza pansewu😢

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 21 день назад +1

    Zikhale ng'oma ma bombasa wagulakoso 😂😂😂 wausilu iwe

  • @giftmasenti5732
    @giftmasenti5732 21 день назад +1

    A Traffic police ambiri za miyoyo ya anthu alibe nazo ntchito nde ndizimenezo

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 21 день назад +2

    Powerful GwedeGwede,,bambo banda

  • @B1Chitatata
    @B1Chitatata 21 день назад +3

    Salute

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282 21 день назад

    Live from south Africa cape town

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 21 день назад

    Munadza makosana ❤❤

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 21 день назад +1

    Chipewa cha khwangwala kuteloko amafuna anyemere kaye kuti adutse ndi mwana wodwala ,utsilu dyera

  • @mathewsmdzanja3276
    @mathewsmdzanja3276 21 день назад

    I salute mibawa

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk 21 день назад +2

    Kkkk chipanda kuyankhula bwezi ali mumaguza omwewo kkkk

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 21 день назад

    Mumakwana guys 💥

  • @MerryWayson
    @MerryWayson 21 день назад

    Sitidya ndale kkkk ndimakunyadilani kwambiri Mibawa TV

  • @ishmaelchirwa9303
    @ishmaelchirwa9303 20 дней назад

    Anduna akutsotsola ulusi pano akuti kuionesa 😂

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 21 день назад

    😢😢😢😢 apolice apamalawi vuto ndi umphawi anthuni

  • @SurprisedDrumKit-ql7rj
    @SurprisedDrumKit-ql7rj 21 день назад +1

    Za police mbuzi zaanthu izi kma kuba ndikupempha

  • @user-gw2zb8pf7n
    @user-gw2zb8pf7n 21 день назад

    Mwanayo anali ndi 1 month and 3 weeks mgalimoto ndinali MO ine😢

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 21 день назад

    Chakwera mumuudzeso kuti opha nzake afeso chifukwa chakwera anapha chilima my boss he call chakwera bull dog😂😂

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 21 день назад

    Nkaka akulembaso MSCE

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 21 день назад

    Ndipo apolice akumalawi ndinu otembelekdwa ndipo mukulephela kugwila mbava koma kulimbana ndi athu osalakwa

  • @StevieChikaonda
    @StevieChikaonda 21 день назад

    Muli ndi mtopola guyz😊

  • @HarryMasamba
    @HarryMasamba 21 день назад

    Kkkkkkkkkkkkkkkkkkk Komatsu dzina izi

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282 21 день назад

    Steve ndi Selina mativesa kukoma

  • @LucianoKapepuza-sy9wx
    @LucianoKapepuza-sy9wx 21 день назад

    Nawo a MCP asatile malamulo a gwirizano wawo kuti apite s Utm asogoleke nawo

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z 20 дней назад

    Zoonadi apolice amaonjeza

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 21 день назад

    Tisakubisileni apolice alowa chiwewe kusaka ndalama

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 21 день назад

    Madokotalanso ali ndivutolawo munthu akumuwona ali pamzele komakungobwelawinawake wawudindo amakudusila chifukwachani winayusi munthu kodi?

  • @NaduMbewe-zz6iw
    @NaduMbewe-zz6iw 21 день назад

    Kkkkkk

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 21 день назад

    Va police palibe vomwe vikuchita vimangodziwa kupempha ndrama pamseu ndikumanga mbava yoti anthu aigwira kare anthu eniake,ndipo vitengelepo phunziro mwina vingayambe kugwira ntchito bwino vipewa va mbalevo

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g 21 день назад

    Ku malawi zimathera tikufufuza.

  • @user-jn7bt1uy5s
    @user-jn7bt1uy5s 21 день назад

    Mbambande mibawa

  • @user-bc2mu2ns5n
    @user-bc2mu2ns5n 21 день назад

    Futso nkhumati kodi sopano kubako mwathana Nako?

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 21 день назад +1

    Wanga kufa mwana chifukwa cha wa police wandigwira nayeso adzafera pompo ineyoso natopa nawo mbuzi zimenezo pofunika osamawanyengelera😢😢

  • @OfwaMwambila
    @OfwaMwambila 21 день назад

    If u stopped by the police officers on the road in ur 🚗 .who is supposed to follow the other? 4me i don't go out to a police office who stopped me coz i had no intention of stopping.u stop me,u come to me &tell me why you stopped me not me coming to ask u

  • @AlasonPaulo-ht7zb
    @AlasonPaulo-ht7zb 21 день назад

    Zoonadi Inu muli bwino kwambili

  • @WysonYohan
    @WysonYohan 21 день назад

    Malawi tingogulisa tigawane ndlama bc