Zitsiru ndi azibusawo, povomeleza ma instructions akupelekwdwao. Kumeneko ndikupembeza munthu osati mulungu ayi. Ndiye kuti m' awa ku tchalichi kumeneko mulungu wao akhala Chakwera. Koma dziwani kuti nzimu wa mulungu ukangochoka mawa lino pa tchalichi chimenechi, basi subwelelanso chifukwa mulungu sangamapikisane ndi munthu. U can only serve one Master.
Mizimu yalusa mpingo wa CCAP ndi wake osapita ku Assemblers of God kwawoko bwanji chitsiru cha president wayaluka basi galu ameneyu dzikoli lamalawi lamuchepera akubisala mbatata nsana ukuonekera mumva kuwawa bwana😂😂😂😂😂😂
Ndpu wasiyilanji kupita ku church kwake kt akamuchose ma demons amene Ali naye..walowa chiwewe sanati, kupha mnzake ngati garu anthu angamukonde chitsiru Cha munthu
😂😂😂😂 wayamba ndiye kukhala ndi udindo waukulu?? Zinachitikapo kt zimenez ngt ndi udindo mku politics konko not kumpingo, mulendo safika mkulamulira eni khomo achuruka nzeru mpingo umaendesedwa ndi malamulo a Mulungu not a politics
Monga ine wa ccap woopa Mulungu mulendo sangandiuze zochita pa khomo panga. Iyeyo ali ndi church lake ndikumene skapange zimenezo. And iyeyo si Mulungu wa ccap Mulungu wa ccap ali kumwamba asatenge ulamuliro waluchipani kwake kapena wakuboma or waku church kwa iye ndikubwera nawo mumupingo wathu ayi mupingo umayendesedwa ndi malamulo a Mulungu. Ndiye a tsogoleri athu a ccap musalole zimenezo opani Mulungu. Osaseka pa khomo aliyese phone asazimise ndindani iye akuyesa amaposa Mulungu wamambwa kodi? Ngati ali ndizifukwa ndi anthu ena asabwere ku mupingo wathu please ziko opani Mulungu wosati olengedwa
Aaaaaaaa nde zichani zimenezi? Zinayamba zachitika liti, nde zodabwitsa tu akufuna adzagawe ndlama paja ali nazo zogawatu koma chonsecho mankhwala mzipatala mulibe shame
Ankapembedza Satana ameneyu. Ndiye pano mwadziwa kuti sanali opemphera koma ofuna chuma. Mwana wake akuba ma passport. Akugulitsa ma passport a fake. Inu a Zambia tangotengani dziko la Malawi boma la Malawilalephera kutukula dziko
Be careful people of God,something will be happen there take care
Chakwera anapha president wa assembles of god musazapite ndi chigawenga ichi ndi kale anayamba kupha anthu
Chakwela the life of Malawian matters alot
Aaaaaaaah! Uchimo wamela mphondo Chakwera, bwanji osapemphera kunyumba kwake komweko ndi security yakeyo. Chitsilu cha President.
Musadzapiteko nonse!
Mapwala Ake ameneyo
Oipa athawa yekha,afuna agawe ndalama ameneyo komatu ndalama zimenezo tizitafunadi koma vote ndiye ndi ija munakakwilira ku nsipe ija,sitikusinthaso chiganizo,pitani akhristu mukamuonere pafupi wakuphayo.
Church ndichanu osawopa osatopa osafooka vuto asogoleliso aku church dyela
Ndagwilizananawe
Chakwera ndiwe galu kwabasi, tapitani ku mpingo wanu mwayamba kusokeratu, inu mumkaona ngati mwakhoza kupha chilima hahaha chilima uja sanafe alipo, olo munamupha koma anthu sitikukufunani🎉🎉🎉
Iyai auzeni kut asabwele church si chao apite Ku church kwao
Zitsiru ndi azibusawo, povomeleza ma instructions akupelekwdwao. Kumeneko ndikupembeza munthu osati mulungu ayi. Ndiye kuti m' awa ku tchalichi kumeneko mulungu wao akhala Chakwera. Koma dziwani kuti nzimu wa mulungu ukangochoka mawa lino pa tchalichi chimenechi, basi subwelelanso chifukwa mulungu sangamapikisane ndi munthu. U can only serve one Master.
Chimo limadzuza olo anapeleka yesu uja anazipha yekha uyu siyeni azaseke ziseko zotse inu musade khawa koma lizasala khomo limodzi la mulungu sazakwanisa kuseka khomo limenelo ndilimene lili loopsa kwambili azisamala popanga zithu
Mizimu yalusa mpingo wa CCAP ndi wake osapita ku Assemblers of God kwawoko bwanji chitsiru cha president wayaluka basi galu ameneyu dzikoli lamalawi lamuchepera akubisala mbatata nsana ukuonekera mumva kuwawa bwana😂😂😂😂😂😂
Azimagililatu ameneyi ndikilani muzandinkhululupilila
Muletseni ameneyo ndi nyumba ya mulungu siyoseweletsa mulendo sapelela lamulo pa nyumba yaweni
Koma Mahule enawa paja muli mtundu uliwonse wa tchimo eti bodza momwemo eeee
Osapita ku assembles koo bwaa mesa ndikumene anachokera musamulore akuphani galu yoooo
Bas nonse mumapemphela kumeneko muzakhale osaptakonso akhaleko ndi zikhalenhoma wakeyo
Pita Kaye ukamine usatipangitse nseru
Osapitako kumeneko something will happen there osalola zimenezo
Komatu galu iwe president wamanyi usatizolowere ndikupha kwakoko
Zimenezo kuchislam sangapange
Koma ichi nditsilu kobasi amazitenga ngati ndani 😢
Kkkkkkkkkkkk azakupa inu eeeeeeeeeeeee mavuto😅😅😅😅😅
Osapitako akhristu akapemphere ndi abusa,mayi oyendela komanso akazawo aabusa kkkk abwere kuno ku MAKATA CCAP izamuimbile chitsitsimutso mutu wanyimbo CHIFUNGA
all the best mr president God help you
mmene wanenera comrade mtanyiwa... kut musazapiteko. Azapemphere ndi azibusa awoo.. Ku Limpopo yafika kale kkkkkkkkkkkk
Akuona ngati nayenso azathilidwa poison? Kkkkk
Vuto ndiazibusawo Adya zambili
Kkkkk kodi chimenechi chikufuna chani kweni kweni
Malamuro awusatana basi kkkkk
😂😂😂😂😂😂 wa satanic wasowa mtendele mzimu wa chilima ukumusausa wanya uona machende ako
Chimo kuzunza kupha anzako ukuyesa suzafa , anthu ayeza usogoleri wako chakwera walephera
Ndpu wasiyilanji kupita ku church kwake kt akamuchose ma demons amene Ali naye..walowa chiwewe sanati, kupha mnzake ngati garu anthu angamukonde chitsiru Cha munthu
Osapita kumeneko amalawi chikumbutima chimupha oyo
Chikangawa chakwera sunakhuthe nyama za anthu.
Khalani tchelu mamembala nonse olo kakhaleni kunyumba nose akapemphere yekha galuyo
Chilipo chachikulu kukapanga kumeneko, pajatu muthu akalowedwa ziwanda amavuta mmm
Palibe chimene mwalakhula chazeru mayi, zingowonetsa kuti inuso mulibe zimu wachidziwitso kapena kuti inuso ndale zidakuwonongani.
Zikomo kwambiri madam taziwa n busa ameneyo ndi street wasatanic azingopita kumeneko kuli nzake akubisalawo koma muvumbuluka tikuziwani ponpano Nzimu wachilima ukumuzuza uona sizinati akanakhala kuti alibe ndalama bwezi tikuti wayamba misala poti wandalama akuti Ali pamwamba palamulo keep it up sister 🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏
Mama musapiteko kuntchalichiko tiponyako bombaa kumeneko😂😂😂😂
Abusa akazapora manyii .asazatyrukeso mmmmm
Nde mapephero ake abwanji amenewo
Galu ameneyu alesedwe asapiteko malamulo akapereke ku mpingo wKe kuja anaphako yemwe adamupeza eeee wooipa uyu asogolleri a mcp 3/4 owoneka obadwa mopotoka nkhope komanso ndi mitima yomwe alephera amenewo
Mukanamukanira Galu wachiwewe uyu
Chakwera ndi satana kwabasi
Musamale naye ameneo mumusiye apiteko yekha zake ndi zakumidima kkkk ati galu ameneu kkkkk koma chikangawa eish
Mulendo kubwera ndikalumo kakutwa
Vuto inuyo simuli molalika uthenga. Muli mowona matchimo amunthu. Kusowa choyankhula inu. Kwanuko kukabwela alendo wopemphela simulankhula pano mukulengeza pamenepo simukuziwa kut uyu ali ndi udindo wa ukulu. Nanga mumene mungalandilile mwana wa bale wanu ndi abusa akumpingo malandilidwe ake angafanane
😂😂😂😂 wayamba ndiye kukhala ndi udindo waukulu?? Zinachitikapo kt zimenez ngt ndi udindo mku politics konko not kumpingo, mulendo safika mkulamulira eni khomo achuruka nzeru mpingo umaendesedwa ndi malamulo a Mulungu not a politics
😂Kumpanjeeko nkoonkoma kwambili
😂😂 anthu a mcp ndi iyaluka manyazi ndi umunthu alibe Inu pitani mungoima papemphelo lomanga zoipa zakezo ndalamazo agawe ndithu voti ili muntima aziwona 2025 ameneyo
Mukapemphelele pakhomo osapitako
Chakwera Chikangawa Congress party
Apenga mkuluyitu ndikuti ndikaona,,mizimu yakwiya ya a Malawi.
Nde mwati ndan ameneyui 😂
Mumuuze Chakwerayo kuti ndi mbuzi ya ma president yoti sitinakhalepo nayo kumalawi kuno ndiponso siyizapezekaso
Kma chakwera akuzioona ndithu 😂😂
Wafa wafa imeneyo
Monga ine wa ccap woopa Mulungu mulendo sangandiuze zochita pa khomo panga. Iyeyo ali ndi church lake ndikumene skapange zimenezo. And iyeyo si Mulungu wa ccap Mulungu wa ccap ali kumwamba asatenge ulamuliro waluchipani kwake kapena wakuboma or waku church kwa iye ndikubwera nawo mumupingo wathu ayi mupingo umayendesedwa ndi malamulo a Mulungu. Ndiye a tsogoleri athu a ccap musalole zimenezo opani Mulungu. Osaseka pa khomo aliyese phone asazimise ndindani iye akuyesa amaposa Mulungu wamambwa kodi? Ngati ali ndizifukwa ndi anthu ena asabwere ku mupingo wathu please ziko opani Mulungu wosati olengedwa
Musapiteko akakhaleko ndi ndunazakezo bass
Abale imvani ichi samalani, mukapusa ndi ma church mutha nonse, Musapiteko please amalawi
Apenga misala ameneyo zimu wachilima ndi abale anthu Ena aja wina Anya awo a chitsilu cha president
Msayiwale kt munthu ochimwa amakhala ndi mantha chifukwa samayenda ndi Yesu... Nde chichakwera ndicha satanic ndipake kukhala ndi mantha.
Fiti fiti ndithu
Mayi pitani mukagone mwadwala chifine.
Mmmmmmm koma inu
Inuyo musapite ku church ko mukapatsa anthu chimfine
A Malawi ndinu dzitsiru, mumafuna president OTAN i?mumafuna president adzikuseserani m'makomo kapena adzikuvulilani Kodi?
Musamale ampingo akulimbana ndaazibusa poison ameneyo samalani mufa
Chakwela nd galu ameneyoo kwabasi
Aaaa zavuta ku mpanda basi
Ndalama idyani
Ku chalichi kwake bwanji osapita kodi iyeyu ndi Mulungu? Wafikapotu Chakwela koma uziwe kuti Mulungu amatsisa mafumu ku mipando ndikakawasiya ku tchire mkumakadya udzu ngati chinyama ask mfumu Nebuchadnezzar
Musapiteko apiteko ekha
Mwayankhula bwino koma mwachimwanso potukwana kuti galu ameneyi
Mukuzawapembeza iwowo
Komatu mulindi time
Musalole a C.C.A.P zausataniki zaozo asakutaiseni yesu
That day will not day for worship God, better to pray at your home.
Kod ndi mulungu ameneyu KAPENA 😢😢
Chenjerani akhristu ndi mneneri onyengayo
Asiyeni ma members a church abwere even atachedwa don't stress about that criminal chatsika
komatu guys ziwanda za uyuyu za chikhamu zija zikuchepera, coz chamudimbayi nde wapengeratu apapa
Mmmm koma muli busy ndimabodza a Malawi, kodi mkamapeka nkhani zanuzo mumapedzapo chani?? Ine ndimapemphera pompano izozo kulibe, ukudwala mnthu komano busy kunama iiiiiii.
😂😂😂😂 iwe unajomba ku church uli ndi udindo wanji umafuna akuyimbire foni kt udziwe ngt ndiwe secretary
Iweyo nde wabodza musatinamize nkhani yi olo limpmpo yanenso kumapemphera kuti mwana Wa njoka iwe kagwere
Aaaaaaaa nde zichani zimenezi? Zinayamba zachitika liti, nde zodabwitsa tu akufuna adzagawe ndlama paja ali nazo zogawatu koma chonsecho mankhwala mzipatala mulibe shame
Hmmm this man called chakwela
Akuphelani komweko musamulole ndiopusa akufuna akuphelani mukanizeni akayangane kwina kopemphera
Osamulola osamunyengerera akuphani satana chikangawa
Komatu mutipatsira chimfine.....,😢
Kd iwowa afika pomadzimva ngati mulungu?ngati akuluakulu avomereze zimenezo onse muwaukire coz sizoona ayi asamalikatu achakwera eti za ubusa zija adazitaya chi khristu anavula akulamulidwa ndi winauja.
Ngati ndi zoona ndye kuti sizapingo ayi
Machende ake
Ufiti ,,afuna chani
Wamisala Chakwela
Muziona inu a chalichi sinanga chalichicho ndi chake
Ok chikangawa titsalandila ndalamaso
Musapiteko
Adzapempereko yekha ameneyo
Iyeyo ndikandani kodi??
Za ziii
Zimamina osamina bwanji iwe ngati zakunyasa ungokhala basi ndwe chisilu galu ndiwe ndipo ulibe yesu
😂😂😂
😂😂😂😂. Eeee yabayatu akuulurani ndipo simunati mupenga zenizeni
Chitsiru ndi iweyo mwana Wa njoka 😂😂😂😂😂
Kkkkkk
Mafoni tinagula na machen amak galu
Ankapembedza Satana ameneyu. Ndiye pano mwadziwa kuti sanali opemphera koma ofuna chuma. Mwana wake akuba ma passport. Akugulitsa ma passport a fake. Inu a Zambia tangotengani dziko la Malawi boma la Malawilalephera kutukula dziko