"Bwato satsitsirana pakati pa nyanja" Dr Michael Usi kusambwadza MCP pa mwambo okumbukira Kamuzu.

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 15 май 2022

Комментарии • 58

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 19 дней назад +3

    A Michael Usi mwamugulisa mzano, mwaphesa chilima ndinu

  • @moosamapira9182
    @moosamapira9182 2 года назад +6

    ali ndi makhutu afe good speech DR USI 100%

  • @Seche204
    @Seche204 2 года назад +3

    Malawi 🇲🇼 akufunika anthu ngati awa osangoti yes yes zili zonse

  • @andersonmaster8055
    @andersonmaster8055 2 года назад +2

    Well said

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Месяц назад

    Good Message ❤

  • @pansigaleta3438
    @pansigaleta3438 2 года назад +2

    Kod zoti yona anamutsitsila pakat pa nyanja sanawelengeko

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 3 месяца назад

    Goog Message

  • @CholapitsaSamson
    @CholapitsaSamson 9 месяцев назад

    Good speech

  • @chekiamaabdul5083
    @chekiamaabdul5083 2 года назад +2

    Allah knows best

  • @enockthomasloyidi4914
    @enockthomasloyidi4914 2 года назад

    👍👍

  • @nananambela5525
    @nananambela5525 2 года назад

    Yaaa neeee Mr usi

  • @charlesgunda1873
    @charlesgunda1873 2 года назад

    This is true

  • @leonardjika2100
    @leonardjika2100 2 года назад +1

    A NEW VERSION WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD WE WILL END ALL NONSENSE GARBAGE FOOLISHNESS HAPPENING TO OUR LAND

  • @JMB804
    @JMB804 16 дней назад

    Awa zowayenera nzomwe zija ku masewero not izi ayi adzingopeleka azinzao nchimbuli mbuli

  • @simonpaul6567
    @simonpaul6567 2 года назад

    michael usi you have to be our president ,cause you know exactly what malawians want

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 3 месяца назад

    Zoona ❤

  • @mcpreciousnyangulu1501
    @mcpreciousnyangulu1501 2 года назад

    100% my president

  • @hamischikalimba6626
    @hamischikalimba6626 4 месяца назад

    Mau abwino okonza dziko Dr Michael Usi

  • @mathewsmbaluko8522
    @mathewsmbaluko8522 2 года назад

    Ausi mumatiimilila kumauzadi zowona anyozele okha achakelawo akazaluza azakhale okha chifukwa chosamva kwao 👍

  • @williammhoni5729
    @williammhoni5729 2 года назад +1

    a usi kumeneko ndiko kulankhula kwamphavu takunyadilani more fire 😂😂

  • @lucymanjolo9288
    @lucymanjolo9288 2 года назад

    A usi mwaiwala chimodzi muzikumbukira nkhani ya Yona muchombo muja zinthu zikavuta sitimasankha katundu oponya mmadzi ai muziwe zimenezo Hon USI

  • @user-ws1ov4se5u
    @user-ws1ov4se5u 5 месяцев назад

    Wandale ndi munthu omuyamikila, ndiye utsiluwo Kodi a Malawi mudzachangamuka liti???? Anthu olilitsa inu😭😭😭😭

  • @frankkamunde4575
    @frankkamunde4575 2 года назад

    yes bwana yes bwana cholinga kufuna kuononga dzina lanu

  • @frstyhavoc6678
    @frstyhavoc6678 2 года назад +1

    Yona komatu anamutsitsa zitavuta apatu zinthu zavuta 😀😀😀😀

  • @hassammaulana4529
    @hassammaulana4529 2 года назад

    Dr usi amanveka motelomo

  • @user-gd6zb2bv8f
    @user-gd6zb2bv8f 7 месяцев назад

    Amakoma asanalowe udindo koma akasakhidwa amasitha

  • @griphinmtonga411
    @griphinmtonga411 2 года назад

    No comment yet

  • @josuahkachali1489
    @josuahkachali1489 2 года назад

    Kkkkk true

  • @PaulKaunda-lj8vr
    @PaulKaunda-lj8vr Месяц назад

    Siku lachigawenga muchizungu amati chigawenga day

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Месяц назад

    Kuswa kuswa basi kkkkk

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 2 года назад

    Bwato likamamira sitimaona chotsitsa. Mwambi otsutsana nawo

  • @user-db2xl7zw9l
    @user-db2xl7zw9l 5 месяцев назад

    Anayakhula koma osamanamizana chekwera anazivera okhatu apa

  • @janenkhoma6447
    @janenkhoma6447 2 года назад +1

    Lelo asiya kuyankhula kut muboma muli mbuz zokha zokha kkkk ndale icant follow

  • @anafieintuka8090
    @anafieintuka8090 Год назад

    Makape awa

  • @mbirinyirenda176
    @mbirinyirenda176 2 года назад

    Amenentchito sakugwira achosedwedi akuyipisa mbiri chakwera wanuyo

  • @henrymbalame222
    @henrymbalame222 2 года назад

    Zanveka ndithudi munthu wankulu ndithudi!,,,

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 2 года назад

    Chilungamo ndi chimenechi

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 2 года назад

    Zoona zake manganya muuze Chakwerayo mbuzi yamunthu

  • @kamwendoderek6567
    @kamwendoderek6567 2 года назад

    NDIMAONA NGATI THABWALA AKULU MUNASIYATU KKKKKKKKKKKK AYI NDITHU ,ITS NOT ALL UNITY THAT STAND WHICH IS OUT SIDE THE TRUTH OR JESUS CHRIST

  • @geoffreymgundo5322
    @geoffreymgundo5322 2 года назад +1

    Kkkk mawu mawu abwino kwambili

  • @KozekaniNowa
    @KozekaniNowa 13 дней назад

    Ngalu

  • @jimmysingano799
    @jimmysingano799 2 года назад

    Ndipo musayelekeze kutsika. Mumira.

  • @hassanyahayatahirotahiro1126
    @hassanyahayatahirotahiro1126 2 года назад

    Kumeneko ndiye kulangula

  • @cosmasnkanda8193
    @cosmasnkanda8193 Год назад

    Koma malawi walero ndi nyatwa!😆

  • @kassimjummah3018
    @kassimjummah3018 2 года назад

    Zonazake mbwiyache

  • @nditumenichagunda4192
    @nditumenichagunda4192 10 месяцев назад

    Zopepela zanuzo osamagwilisa ntchito baibulo

  • @RajabWhite
    @RajabWhite 7 месяцев назад

    Koma Mkulu uyu 😂😂😂😂😂

  • @muhammaddaimon5294
    @muhammaddaimon5294 2 года назад

    Iwe mbuzi munthu wopanda nzeru iwe chitsilu boma lake liti lakuthaithalo

  • @alexanderkaunda9554
    @alexanderkaunda9554 2 года назад

    Kamuzu wakupha anthu uja

  • @mrr.a.l.s752
    @mrr.a.l.s752 Год назад

    😂😂😂😂

  • @isabelmartin4299
    @isabelmartin4299 2 года назад

    Madzi achita katondo 😂😂😂

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 Месяц назад

    Kkkk usi mukukana kusika bwato? Kkkk mumila limodzitu chifukwa ndie APM akulowanso mwatinamiza tinakuvotelani kwatha amalawi anachenjela sitingamvelenso bodza lanuli bola ki Egypt than ku bagamoyo

  • @reubenbambe9101
    @reubenbambe9101 2 года назад

    Chili Ndi mutu muli dzeru

  • @harrisonmwanga9812
    @harrisonmwanga9812 Год назад

    If ndiye timasitsila pakati popo iyaaa asambila ngati satha aona plan

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 2 месяца назад

    Good Message ❤