CRUISE 5 WITH MICHAEL MANGANYA USI

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 5 фев 2025
  • Michael Manganya Usi is a man of many talents. Comedian, Actor, Producer, Singer, Social Commentator. He currently works for ADRA as the Executive Director (to retire soon). He met Joyce Banda former Malawi President and told her that her government was corrupt. He is currently promoting a political philosophy - Odya Zache Alibe Mlandu.

Комментарии • 91

  • @JimmyKamkusa
    @JimmyKamkusa 7 месяцев назад +10

    Anyone else who is watching this in 2024

  • @kassimjuma8822
    @kassimjuma8822 4 года назад +2

    Uncle mukunena zoonadi mukabwela kumudzi kumulanje kwa gorden kuchem'kwanda mumathandiza aliyense mumakwana DR usi stay blessed God bless you big

  • @colleinbham1955
    @colleinbham1955 5 лет назад +2

    Malangizo a bwino abro Manganya. Problem with our Country is selfish and greedy leaders. 🇲🇼👏👏👏👏

  • @AbdulAziz-qf4qe
    @AbdulAziz-qf4qe 6 лет назад +1

    Mr Usi keep the Chitenje for me pliz.....am coming there next year...kuti tiyende limodzi ndi odya zake alibe mulandu.....

  • @bupemhango6876
    @bupemhango6876 4 года назад

    Uncle Usi, may God continue blessing you and I praise God for giving you such a good heart... Much love

  • @ShekelengDavid
    @ShekelengDavid 7 месяцев назад

    More 🔥 Dr Michael Usi.

  • @kaitanokagalu
    @kaitanokagalu 7 лет назад +1

    This is great Dr Micheal Usi, i like the way you always do your things, you have great things to the country especially on leadership.

  • @GraceMaylMayling
    @GraceMaylMayling 7 месяцев назад +2

    Such a genius

  • @JamesGuevara-jz9fk
    @JamesGuevara-jz9fk Год назад

    Ure the Best mr usi..all the best inuo mmakwanitsa kobasi

  • @AbdulAziz-qf4qe
    @AbdulAziz-qf4qe 6 лет назад +2

    Mr Usi keep it up.....go ahead one day you will be a president of Malawi.....am watching from Kuwait.....more fire kuti buuuu......🔥....

  • @jamesmatabwa9949
    @jamesmatabwa9949 7 лет назад +3

    Mr usi my home boy he is genius indeed and I know that one day he will become the president of MALAWI manganya he is a game changer believe that

  • @sakaladickson2389
    @sakaladickson2389 4 месяца назад

    He sounds visionary leader.....

  • @felixchikumbutsochapita9194
    @felixchikumbutsochapita9194 6 лет назад +1

    Michael Usi has a lot of constructing points. He is a guy who is focussed. Other people speak because they just want to speak something but Usi speaks because he has something to.... I like him and I owe him my total support

  • @chimwemwechimwaza7512
    @chimwemwechimwaza7512 7 лет назад +1

    Manganya ndimamusata coz amaziwa kuvutika ka amalawi...koma khani za ku malawi zinafika sondiwawisa mutu chifukwa anthu ake ndiwongokoma mkamwa, komano kut asithe zinthu ngat achitira mayiko ena samatha. Maiko ambiri mu Africa akutukuka ndithu pomwe Malawi palibe chanzeru chikuwoneka Mmitu mwangozaza mamina okhaokha basi...Watching fro Yokohama, Japan

  • @joelmatchindu1738
    @joelmatchindu1738 7 лет назад +1

    Thanks Joab that's marvellous and Mr usi matiimirila

  • @flacksonnkhoma1895
    @flacksonnkhoma1895 6 лет назад +1

    These guy is so genius. .so sweet

  • @SulimanAdams-u8o
    @SulimanAdams-u8o Год назад

    Wow manganya

  • @juliamvula7163
    @juliamvula7163 4 года назад

    Very enlightening interview

  • @yamikanichinganyama6607
    @yamikanichinganyama6607 5 лет назад +1

    Dziko lino silingapite kuli konse bwanawe, we don't have a dream that shapes us... Until we get to know what we do need boom our way to ho

  • @kingsleybanda8360
    @kingsleybanda8360 7 лет назад

    koma nde alipo nigwiranugwiranu nofumu..makoponi avuta..like the songs by Katwell and phwanyaphwanya boys

  • @emmanuelkaomba7064
    @emmanuelkaomba7064 2 года назад +2

    This man is wise...what an influence!!!

  • @xanderdambe4174
    @xanderdambe4174 2 года назад

    i missed this

  • @issahwaphee8361
    @issahwaphee8361 7 лет назад

    is so amazing keep it up joab

  • @francismtonga7360
    @francismtonga7360 4 года назад

    Nice music

  • @evelynmakhaya2756
    @evelynmakhaya2756 7 лет назад

    Am proud of you Mr Manganya. More fire!! Koma nsaluyo nane ndikuifuna.

  • @emiliezambezi8287
    @emiliezambezi8287 7 лет назад

    Eee koma Mr ussi mumandisangalatsa Chimodzimodzi simufuna kukamba zoipa kumbali I like it

  • @joelstephensongebujr5916
    @joelstephensongebujr5916 7 лет назад +4

    The interview I was waiting !!
    please Mr chankhaza I wish you host Andrea Thonyiwa (Mr Jokes)

  • @lishancastillodzowa9667
    @lishancastillodzowa9667 7 лет назад +2

    That was exclusive interview with my boy usiman manganya dembele

  • @geoffmajawa9413
    @geoffmajawa9413 7 лет назад

    Great interview ...

  • @AlexKaunda-x3p
    @AlexKaunda-x3p Год назад +1

    So za azimayi anakuphuzisa ndani kuti uziti ndi yamwe chokozela

  • @ChikuSteven
    @ChikuSteven 10 месяцев назад

    Masikono

  • @dziwanipaul2418
    @dziwanipaul2418 7 лет назад +3

    Usi is absolutely right. I don't like current DPP leardership though but if we as malawians need to change a party we really need to examine it. What new can MCP bring to Malawians? What about UDF, Aford etc?

  • @DUNCANJANUARYBANDA-vk7bg
    @DUNCANJANUARYBANDA-vk7bg Год назад

    Wandilimbikitsa manganya

  • @sungenimaloya8174
    @sungenimaloya8174 Год назад

    Michael Usi is smart

  • @oswardmulenga2350
    @oswardmulenga2350 7 лет назад +5

    Who else has noted? Mdidi by faith mussa preferred by most guests of cruise 5

    • @joabfrankchakhaza
      @joabfrankchakhaza  7 лет назад +1

      OSWARD MULENGA That's true. It's a favourite for many, Patience Namadingo as well.

    • @kazimilebanda9643
      @kazimilebanda9643 6 лет назад

      I think Madam Mary chilima chose the same song !!!!!!nyimboyi inaimbidwa jealous down!!!!!!!!!

  • @stephenlupanga1970
    @stephenlupanga1970 5 лет назад

    Joab kkkkkk ukutinamiza zakuoneka kwako before kkkkkk like kapuku

  • @andy4christ991
    @andy4christ991 7 лет назад

    This has been so sweet

  • @mussakapalamula1990
    @mussakapalamula1990 Год назад

    Foreigner Manganyayu

  • @maggiemariwu7360
    @maggiemariwu7360 7 лет назад +1

    Mr Manganya wodya zake alibe mulandu kkkkkkkkk nsaluyo tikuyifuna

    • @beautyphiri7513
      @beautyphiri7513 7 лет назад +1

      Zowona mr usi, l respect you ndipo ma president athu akanakhala anthu ozindikila ngatinu bwemzi tilipatali

    • @ivykampala6295
      @ivykampala6295 7 лет назад

      Ambuye akutsogolereni. Awotu sanabvutikire mpandowo anangolandira.keep on brother.

  • @isaacjoven8671
    @isaacjoven8671 6 лет назад

    Muli fundo akuluwa.

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 4 года назад +1

    But Manganya amakaliila anthu kuntchito akamuitana kuti mangaya now akuvomera coz akufuna upresident, whats that

  • @macphersonnchessie5101
    @macphersonnchessie5101 7 лет назад

    The bass guitar is great

  • @kaitanokagalu
    @kaitanokagalu 7 лет назад

    Kikkkkk the last questions seems the same you asked Dr Lazarus Chakwera

  • @paulnkhama3621
    @paulnkhama3621 3 года назад +2

    Chimene chimawononga dziko NDI chifukwa chozikonda

  • @brightgenesisbamusi4427
    @brightgenesisbamusi4427 7 лет назад

    KATIWELO & PHANYAPHANYA BOI LIVE PERFEMANCE ILI BHO,KUMENYA DZIDA MWASILIYASI KIPI ITI APU

  • @LookmaniIshmael
    @LookmaniIshmael 10 месяцев назад

    Manganya amakwana

  • @JessieVeggie
    @JessieVeggie 7 месяцев назад

    manga wakublawayo kkkk

  • @tkhasan713
    @tkhasan713 7 месяцев назад

    It's me here 😂

  • @trustbanda6577
    @trustbanda6577 7 лет назад

    Michael Usi is such genius

  • @andy4christ991
    @andy4christ991 7 лет назад

    nice cruise 5 team

  • @aishatawakali9017
    @aishatawakali9017 7 лет назад

    Manganya ali ndi nzeru kwambiri koma akanangonena kuti he's contesting 2019 ino

  • @paulnkhama3621
    @paulnkhama3621 3 года назад

    Joyce Banda wakubayu amafuna kunkumenya wayaskanya joyce

  • @pempheropharaohphiri3634
    @pempheropharaohphiri3634 7 лет назад

    nice

  • @charlesstephano7836
    @charlesstephano7836 7 лет назад

    Joyce banda imformer president

  • @arthurmwagomba7256
    @arthurmwagomba7256 7 лет назад

    wasala winiko

  • @ReginaDandize
    @ReginaDandize 9 дней назад

    Odya zake alibe mulandu party 😂

  • @jameskavina197
    @jameskavina197 6 лет назад

    Aaaa manganya atizuza askhale president ndithu kkkkk kuumira

  • @SarahM-vj2ou
    @SarahM-vj2ou 6 лет назад

    You so much sound like uli ndi ubwenzi kwambiri ndi azungu zomwe zili zosakhala bwino.

  • @OmegaChingamuka
    @OmegaChingamuka 2 месяца назад

    Palibe akukufuna iwe ungovutika kupita ku chisankho sukawina zipita ku MCP konko

  • @preciousmagaleta7576
    @preciousmagaleta7576 6 лет назад

    Mr Usi please send me one nsalu .Im in Zimbabwe

  • @judyemmanuel8435
    @judyemmanuel8435 7 лет назад +1

    vuto amalawi presdent mumafuna kaya akuvulireni akuonetseni kumatakoko kwake kaya aliyense azadya thukuta lake

    • @dziwanipaul2418
      @dziwanipaul2418 7 лет назад +1

      Kwinaku a m'boma akuba zomwe wina wake akugwirira ntchito ? Your reasoning is pathetic and cheap though.

  • @dennisimedi5347
    @dennisimedi5347 7 лет назад

    wamasewela sakudziwa chomwe akufuna

  • @paulnkhama3621
    @paulnkhama3621 3 года назад

    Ndiye munaona kuti dzipewa ndi salu m'malawi zamukwana umphawi watha kkkkkkkk mulindisoka

  • @blessbakili
    @blessbakili 7 месяцев назад

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 lero muli ku boma mukupanga chiyan

  • @elastoleonardmankhwala711
    @elastoleonardmankhwala711 6 лет назад +1

    Anthu andalenu masomphenya anu amakhala abwino koma mukalowa kuti muzichite iiiiii Kodi nanga tisonkhe ndani??

  • @timothyeweldone9781
    @timothyeweldone9781 7 лет назад +1

    Joab Frank Chakhaza r u politician or Journalist???????? plz stop boring people OKY

  • @Thebloodline365
    @Thebloodline365 7 лет назад +1

    ziko LA Ku Malawi lafikapa chimozimozi kukhala opanda purezideti. chifukwa palibe chikuwoneka

    • @judyemmanuel8435
      @judyemmanuel8435 7 лет назад

      Nixon Patrick amalawi umphawi ndi ulesi kumalimbqna ndi president zopanda mphindu ukhala choncho lwe kape opanda nzeru

  • @timothyeweldone9781
    @timothyeweldone9781 7 лет назад

    aaaaaa broh u boring me serious r u politician ????

  • @issahwaphee8361
    @issahwaphee8361 7 лет назад +1

    is so amazing keep it up joab