Mr president how many advisor do you have? Is it a speech to tell malawians? That is speechless, am not against with you but as president mumayenera kukhala ndi fundo zogwilika, zopasa chiyembekezo koma mmmmmmm tidabesa amalawi koma Mulungu atichitira chifundo
Mr president,,,,you're responsible to bring the solutions,,,,not asking us the way forward,,,,just command what suppose to be done,,,,adzikupisani mr ussi,,,fundo
Kkkkkk inu kodi ndindani mukamakhala mumati ndini ndani Eliya wabwera Abushiri alipano mukawauze Ambuyanu kuti Eliya wabwera mukamalira Achilima ali apo Achakwera ali apo dziwani kuti aEliya wabwera amanena ndani Bushiri kapena ndani mManganya sazatheka
Andale inu muziyamika chifukwa kuno ndi ku malawi, koma kunakakhala kuti ndi ziko la mkhongo ine ndinakakhala mmgulu lopanga upo okuphani for sure inu nonse ndi mbeu yoipa kwambili.
Chilungamo, kuvotela (Ras Chikomeni Chirwa) munthu wapadela, amene ali ndi mfundo zothandiza dziko la Malawi, Dpp, Utm,Mcp Udf, no more we need new leadership.
Amalawi munansanga wolakwika mbambadi course wochakwela wolibe mfundo nthawi zonse amakalila mawu amodzi please next time we need be very careful pangani yonsanga upule chifukwa ntchito iyi sintchito yamasewela ayi yy😢😢😢😢😢😢😢😢
Mmmmm koma pa chakwela nde tidabetsa basi kuchitakusowa ndi mfundozomwe iiiiii amalawi basi tilibe chiyembekezo? Chakwela ndi panja pa munthu😢😢😢😢😢💔💔💔💔💔
A usi koma muli ndi ku mudzi inu,? Ngat mulinako mmapita koma? Mwayankhula ngat mukukhala kunja kwa dziko linotu, kuyankhula kot akuchemeleleni mabwana anuwo zomwe zili zaziiiiiiii ndizotipsetsa ife mitima
This country we have start war 😢 guyz amene mwakozekha bweran ku Dm tayamba group yomwe tingayambitse force acting komaso u'll get salaries b4 kulowa nchire
Muzizipemphelela nokha ndani amene angamataye nthawi yake ya padela ndikumapanga za inuo ngakhale iweo usi fodya bas uzipemphelele wekha wamva iwe za ugalu basi
Usi ndi team yako yonse ya tonse alliance simukuziwa chomwe mukunena, munataya pangano posachita zomwe munalonjeza God will punish you. Iwe Usi uzikanyadira kuthandizidwa zoona pomwe inu mungoba ndalama xa misonkho??? Shame on you tonse alliance.
Zaziiii okufa nkudzuka yekha ndi amene angamvere za Chakwera ndi Chilima you take Malawians like their dom? not again guys enough is enough to mr Chakwera end Chilima
Mr president how many advisor do you have? Is it a speech to tell malawians? That is speechless, am not against with you but as president mumayenera kukhala ndi fundo zogwilika, zopasa chiyembekezo koma mmmmmmm tidabesa amalawi koma Mulungu atichitira chifundo
Mr president,,,,you're responsible to bring the solutions,,,,not asking us the way forward,,,,just command what suppose to be done,,,,adzikupisani mr ussi,,,fundo
SKC my vote
Usi zinazo wangoyankhulira ntchito koma mwainu mulibe sogolo labwino kuposa kuba kupha ndikuononga
Pp
Ku opposition kumeneko ?
Kkkkkk inu kodi ndindani mukamakhala mumati ndini ndani Eliya wabwera Abushiri alipano mukawauze Ambuyanu kuti Eliya wabwera mukamalira Achilima ali apo Achakwera ali apo dziwani kuti aEliya wabwera amanena ndani Bushiri kapena ndani mManganya sazatheka
Ise tikufuna anyamata president ngati Senegal chilima bomaa
Andale inu muziyamika chifukwa kuno ndi ku malawi, koma kunakakhala kuti ndi ziko la mkhongo ine ndinakakhala mmgulu lopanga upo okuphani for sure inu nonse ndi mbeu yoipa kwambili.
Zoona same like me
Chilungamo, kuvotela (Ras Chikomeni Chirwa) munthu wapadela, amene ali ndi mfundo zothandiza dziko la Malawi, Dpp, Utm,Mcp Udf, no more we need new leadership.
My vote is for apm
Mmene wathera muja? Ndiye kuweramira chitandatu
😂😂😂😂mpaka chitanda
Chakwera my vote. Osati opanda Mano mkamwa uja ngati wadya chimanga chotentha
Mbolo yako
Fundo zapa maliro 2% zandare 89%
Amalawi munansanga wolakwika mbambadi course wochakwela wolibe mfundo nthawi zonse amakalila mawu amodzi please next time we need be very careful pangani yonsanga upule chifukwa ntchito iyi sintchito yamasewela ayi yy😢😢😢😢😢😢😢😢
😂😂😂 utm is not a small. Party it has brilliant brains 😊
Wise saying Dr Utsi we really need to pray for our leaders as good citizens and that has promises attached before God.
Apm my vote
Bwanji Vice president bcz phindu asamayendenawo sindikuona
Powerful message
Which message?
Which message?
Powerful massage
Very few of us know who Eliya is
Mr utsi anatumidwadi ndi mzimu anthuwa tikanawaika mmapemphero pazomwe zachitikazi
Wakumva wamva osamva sanamve zomwe wanena Manganya
Mr Michael usi amatha heavy
Great speaker
Mmmmm koma pa chakwela nde tidabetsa basi kuchitakusowa ndi mfundozomwe iiiiii amalawi basi tilibe chiyembekezo? Chakwela ndi panja pa munthu😢😢😢😢😢💔💔💔💔💔
Inu munthalika mumavapo fundo zanji? Bodzalokhalokha basi
Anthu aku Mulanje angopitilako kut akakuziweni palibe vote ya Chakwera pa anthu onsewo😂😂😂
I can't waste my time honestly,I have important burning issues to pray for, don't provoke me please 😠😠
Usi zining'a mumachulutsa sometimes kungoyankhula straight forward ndibwino, Ena akuwomba mmanja koma sanamve zomwe mwatanthauza pazomwe mwayankhula, #eliya wabwela
True
😂😂😂😂😂
Ndipo live
Ndalezo zikufunako chani kumaliroko
Onse ali ku nsanja uko ndi a ndale amadyera momo
Ukupanga zosankhana mitundu ndi iweyo Chakwela ma udindobonse azibalewawo ndi ana ako
Tidziyankhula zinthu ndikuzichitq
Anthu tizikupemphelelan kt mupange cha, takupemphelelan 4years tapindula chan kwainu
Zachamba eti Kodi odzutsa president samakhala vice mesa
❤
See you next year September guys, you really fooling down any time
Cyclone politics ija yachitikatu tsopano. Kd chakwera ndani?? Ulemu wanu a USI
Palibe chomwe tapidula ife ndi chakwera bola Apm
A usi koma muli ndi ku mudzi inu,? Ngat mulinako mmapita koma? Mwayankhula ngat mukukhala kunja kwa dziko linotu, kuyankhula kot akuchemeleleni mabwana anuwo zomwe zili zaziiiiiiii ndizotipsetsa ife mitima
APM my vote
2 let for mama.2025,kuba mukubaku uku,mudzabvala,ma silipasi okutha.amalawi,alipopaja.
Kupempherera kt asagwidwe pa mulandu wakupha😢😢😢
Ndale ndi kumaliro komwe kma chakwela ndi otsekesa kwambili
Thus very true
Mbomba lija anakonzekela mademo akalindo
Chakwela mbava
Abanja limodzi kodi ena mkudya ena akugona njala‼️‼️ ife ndima opharn bax 😳😳
Kwatsara pan'gono kucha
Oooooooh my bando yawonongeka pazadzi koma galuyu
Komatu anthu Inu panachitikila Freddy paja mukabwere lero,manyazi mulibe
Funso labwino kwambiri, Chakwera Ndi ndani?yankho, Chakwera Ndi mbava 💯 10:42
Apm team we are
Apa sindinanvepo fundo yeni yeni, chakwera alibe nfundo, ndipo sakukwana pa u President ayi. Za ziiiiiiiii! Bola michael Usi.
Osakonda mtendere akunenedwayo ndi Inuyo.Adzwinansotu a Chakwera.
This country we have start war 😢 guyz amene mwakozekha bweran ku Dm tayamba group yomwe tingayambitse force acting komaso u'll get salaries b4 kulowa nchire
Mapephelo ndiwofunika koma ukusokoneza zithu ndi iweyo kusakhana mitundu ndiweyo mwangozazana palipose achigawo cha phakati nokha nokha uziwona thawi ikubwela
Malawi dziko lomvesa chisoni always doing politics very shameful
Mbambande Mr usi
Bwana chilima mukukalambatu
Muzizipemphelela nokha ndani amene angamataye nthawi yake ya padela ndikumapanga za inuo ngakhale iweo usi fodya bas uzipemphelele wekha wamva iwe za ugalu basi
Izi nde za ziiii
Keep the fire burning Mr Usi❤
Mbuzi za anthu
Kkkkkkk
Za ziiiii
Usi zining'a zakozo uzatipweteketsa nazo....nfundo zabwino koma kuzikoletsakoletsa...ma drama paliponse kodi....kumakhala serious koma
Tilibe nthawi yowapemphelera achilima ndi chakwera masataniki nkhati amenewo
😂😂😂 Komatu akulu awa amayankhula mwachidule😂
Pemphelo, loti lipite kuti kwayani lipite kwasatana lazalas ndi nkazake chilima
chakwera ine sindingamupepherere😢
Akupasa chani
Kkkkk watera ndege pompano kkkkk ndie kt chan?
Watipha Lazaro,wawononga dziko
Azapenphelela ndani awusi zaziiii
Usi ndi team yako yonse ya tonse alliance simukuziwa chomwe mukunena, munataya pangano posachita zomwe munalonjeza God will punish you. Iwe Usi uzikanyadira kuthandizidwa zoona pomwe inu mungoba ndalama xa misonkho??? Shame on you tonse alliance.
Ndiye kusowazochita kukhala bize kupempherera chakwera aaaaaaa kusowantchito ? Chani
Uyu sichilima iyi ndindondocha yachilima chifukwa chilima amene timamudziwa Kuti amalankhula ichi ndichikwangwani nchifukwa sichikulankhula chilichonse
Komadi ndi ndondocha
😂😂
😮😮
Chifukwa unadana ndi bon kalindo ulibe mfundo ine ndimaona Ngati Uli ndi mzerutu
Takambaniko zazeru akulu 15:11
😂😂😂 Koma malawi ife tizipephelera achuma mmalo motipephera anthu osaukafe
Michael Usi ndi katundu samaopa 😅
Kkkkkk a usi tidaikatu chikhulupilirotu mwainu koma aaaasa madzi a mphutsi
Chakwela ankaganiza zawembu
Kkkkkkk koma dziko ndi anthu akhe
For what Mbuzi ngati zimenezi
Mr president 😂😂 tandipasani dzina la amene wakulembeni speech😢
Ndipo m’mutu mwachakwera mulidi mphuzi anabwerellanji 😢
Michel usi umatha mwachinsisi kkkk zimenezo ndiye ndale
Ine mau ambiri ndilibe always mau ambiri ndilibe kkkk
Mapephero achani kod? Osamasewera ndi Mulungu anthu àmbiri akuvutika
13:49 kuyankhula KWA nzelu michale usi
Bodza ili usi bwanji samuuze chilima monga Vice President Kut adzutse chakwera zazi
Iwe Siwa yamba NDI iwe zosakhanazo buzi
Anthu oipa awa kobasi amatitenga ngati chitosi
Kuona mtima muyambe inu achakwera chifukwa kuyakhura mumatha koma ndiinu munthu ovensa chisoni kwa mbiri
Iweyo ndipambali penipen
Usi ndimwana wanzeru
Usi amakwana kuyankhula mopanda mantha
Choka iwe galu
Chakwera amaziopa nduna zozisankhira okha .olo zitachita zinthu zoononga amangokhala chete kuziopa
Chakwela amaganizanso ngati Mbuzi kwabasi
Kodi mesa odzutsa president akanakhala achilima?
Zaziiii okufa nkudzuka yekha ndi amene angamvere za Chakwera ndi Chilima you take Malawians like their dom? not again guys enough is enough to mr Chakwera end Chilima