Agape khombe amandibowa bwanjii eish!, i dont feel good wen i heard names like agape, kumkuyu, chimwendo, chakwela, zikhale, yolamu, vetino phiri, pter kalaya, billy malata, layitoni mangochi, ben longwe too many to mention
Mulungu akuulura chinachilichonso ku dziko langa koma vuto dziko langa linasankha kusamva koma limamva china chake chitachitika...Ambuye athandize Malawi
Amalawi let’s gather together and fight like our fell Kenya’s bakili tv and Limpopo fm thy are doing there parts ife tonse tikutani kapena yathu ija ya Ulemu???
Eyetu ameneyo nde mulungu inuyo ngati mukukwanitsa kutseka anthu pakamwa ndindalama ndiomwewo opusa osusuka achina yudasi Ana anjoka inuuuuu Malawi mizimu yambiri ikuzunzika kusowa chisamaliro zinthu zinakwera kuli okalamba Ana amasiye nzipatala kundende ndi anthu onseee mdzikomu ofuna zabwino koma ayi zikuvuta kwacha mwagwetsa mwagwetsanso ma million mukukhonyolera m'matumba mwanu kukhutisa mimba zanu Nde pemphero la olira ovutika Mulungu samalisiya amayankha mwachangu nde anthu ayamba kugwidwawa nchiyambi chowululika zinsisi zanu I'm repeating all most each and every day kuti you will pay one by one I'm not just taking this is prophetic word Mulungu ndiokwiya nanuuuuuu anthu amagazi m'manja inu
Koma ntanyiwa. Respect to you May the almighty God protect you wherever you will go
Keep up the good work comrade 💪💪
Ulemu wanu comrade Ntanyiwa.
Munandisangalasa yomweo chikangawa❤️❤️❤️🇿🇦🇿🇦🇿🇦🇿🇦 osavera Riiimpopo ndi ndimakhala ngati ndataya kofunikila
Ndipo kwambiri tu mmm
Salute comrade ntanyiwa,we love you and all Limpopo FM
Limpopo FM live from south Africa Durban Pietermaritzburg auzeni zoona amenewa
Panopa ine ndinasiya kuvela ma redio ena panopa ndili limpopo yokha basi
Ulemu wanu big mani mmatimvesa kukoma kwambili god bless you all the time ❤❤❤❤❤❤
Ntanyiwa and your fellow comrades excellent well done, and keep it up for the battle you are fighting for Mw nation
Respect bwana Ntanyiwa 🔥🔥🔥
Ine mchifukwa chake ndinakana ntchito ya usilikali ndiyapolisi coz fans ya madepartiment amenewa ndiyombwambwana kwambiri, zigawenga zaku Israel and Ruanda zikungolowa mdziko mwathu ngat zikulowa mmanyumba mwawo, chomvesa chisoni kwambiri ndichoti asilikali ndi apolisi angoti vyooooo , vyooooo , osapangapo kanthu
Dzitsiru
My brother your number one keep it up
Mtanyiwwa ulemu wanuw mulungu asinkuphasa moyyo wabwinno ndawi sonse I pray for you all the time amalawi tili phamoto 🤲🤲🤲🙏🙏🙏mulungu dalisani Malawi
Agape khombe amandibowa bwanjii eish!, i dont feel good wen i heard names like agape, kumkuyu, chimwendo, chakwela, zikhale, yolamu, vetino phiri, pter kalaya, billy malata, layitoni mangochi, ben longwe too many to mention
Antuwo zisilu kwabasi ...Antanyiwa gwilani nchito blo❤
Chifukwa iyeyu..akupanga zinthu zomwe south African ikhoza kukwiya nanzo.zomwe zingaikidze miyoyo yanthu ife amalawi pa chiswe😢
Tikuziwa zambiri GUYS mmmm Limpopo FM ndikatundu number 1
Mtanyiwwa osawopha mulungu adalise inuyyo mulungu adalise inuyyo nosse
Limpopo inabwera kuzakhala
May good God knows everything and palibe chingabisike Mulungu ateteze malawians
Ndili pambuyo pako mtanyiwa
Ulemu wanu from Limpopo south Africa 🇿🇦
Wailesi yokhayo yomwe ambiri akuikonda kunvera panopa
Ndikuuza girl
God's good always Amen
Mulungu akuulura chinachilichonso ku dziko langa koma vuto dziko langa linasankha kusamva koma limamva china chake chitachitika...Ambuye athandize Malawi
Mulungu wayitenga nkhondo imeneyi kukhala yake ndipo palibe yemwe angamenyane ndi MULUNGU.
OKHA OKHA A MCP AMENYANA NDIPONSO AWULULANA POSACHEDWAPA. IFE TINGOTI PHEEEEEE KUDIKIRA
Tafika ndithu kuzamvera our very own limpopo Fm
Comrade ntanyiwa mulungu azikupasa moyo wautali azikusogolera ndipo mupitiliza kuti pasila choona chamalawi Allah azikuteteza kulikose ukuyenda Limpopo FM ndimanyoya nayo ndikamavera
Mumatiimirira acomrade timakunyadilani❤
I salute you comrade, you are genius
God bless you ❤
God bless you comrade
Buddy Ntanyiwa ‼️
Always proud of you ♥️🔥
It's only champion station in limpopo fm
Musalimbane ndi manyi woo aaaa muti asilikali alikuti??
Agalu osaziwa ntchitowo? ntchito zigololo bas.
ife tiibe ma ninja mmalawi muno aaaa
🔥🔥🔥🔥Ana Wachepa awa Zina amangoziyambadi...
Tinakusowan Mr Mtanyiwa muli bwanji kumeneko kuno tili bwino ndithu
Chakwela sawina wapangila ena kapeni
Ndipo kwambiri tu mmm
boma la zitsiru apolice army chakwera mitumbo ya chamanu
Chikangawa Ali madzi😅😅😅
Kkk
Mutitumizire zithunzi za anthu omwe agwidwa ku South Africa.
Mcp ikupanga zinthu zoopsyeza kwambiri ndipo zamdikwana mmmh
LIMPOPO FM PALIBESO IFE TINGOTI NYADU
Kkkkkkkkkk yomwe mwaiputayo chakwera ikuphulikikani
Even Tv,Radio stations in Malawi are getting lessons though they are silent bravo
Yomwey gulu iwe
Pangolin ..ntanyiwa ....
Tchimo limayitana Lin,zache
Yomwey galu iwe umakwan
Osasiya kunena zowona
Zigawenga zosadziw dziko akadziwe munthu ali kudimba zoon
Achita bwino 😂😂😂arirata😂😂
Guz Malawi ndiwatu if anyone ali okudzidwa ndikulephera kwa Chakwera tiyen paunsewu tonse pa 10 July
Zoonadi brother mtanyiwa ifetinapanga mistake kuvotera Chakwera ndigululake komano chakwera aziwekuti wasalandi madzi amodzi
Mcp mulungu walange ndinthu ndipo apange kanthu mudzina layesu akutitenga ngat chisiru ndinthu
Pa 10 akuchoka bas
Koma braz mumakwana athawa a mcp
Respect to you bro nthanyiwa keep the 🔥 buuuuuu
Ndipo anapa chilima ndi ameneyo lelo chikuza mawu ndi iyeyo aziwona ndithu atule pasi udindo
God bless you mr ntanyuwa ❤❤❤
Amalawi let’s gather together and fight like our fell Kenya’s bakili tv and Limpopo fm thy are doing there parts ife tonse tikutani kapena yathu ija ya Ulemu???
Not ulemu as such bro, amalawife ndombwambwana kwambiri man, mtanyiwa and bakili muluzi tv alongside bon Kalindo are doing their part for sure
We need some more teachings brother man !!
Be blessed
27:11 ❤❤❤❤❤
😂😂😂😂😂😂😂musandikomole antanyiwa ine lero Koma kulizithuuuu 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Kodi agapeyu ndindani nanga tundu wanji wamunthu ku malawi kuno agalu kwabasi ndi MCP yawoyo
Walemphela udindo
Chakwera wamupa chilima kuvuna akhale president galu kwabas
Mumakwana ntanyiwa
Respect for you
Limpopo FM is number one
Bambo mu mtanyiwa ulemu ndi wanu mulungu apitirize kukuyang'anirani
🎉🎉🎉 to Limpopo FM
Ntanyiwa more 🔥🔥🔥🔥🔥 fire
Mumakwana ❤
Koma athu aku mcp mulungu achitepo kathu
Be protected sir
Limpopo fm ❤
God be with u brother
Ulemu wanu Comrade ❤
Great Job Ntanyiwa
Comrade umakwana bigup
Limpopo ndi katundu uyu😂😂😂😂
Eyetu ameneyo nde mulungu inuyo ngati mukukwanitsa kutseka anthu pakamwa ndindalama ndiomwewo opusa osusuka achina yudasi Ana anjoka inuuuuu
Malawi mizimu yambiri ikuzunzika kusowa chisamaliro zinthu zinakwera kuli okalamba Ana amasiye nzipatala kundende ndi anthu onseee mdzikomu ofuna zabwino koma ayi zikuvuta kwacha mwagwetsa mwagwetsanso ma million mukukhonyolera m'matumba mwanu kukhutisa mimba zanu
Nde pemphero la olira ovutika Mulungu samalisiya amayankha mwachangu nde anthu ayamba kugwidwawa nchiyambi chowululika zinsisi zanu
I'm repeating all most each and every day kuti you will pay one by one
I'm not just taking this is prophetic word
Mulungu ndiokwiya nanuuuuuu anthu amagazi m'manja inu
Komatu ndiye nyama ya malemu Chilima mwasavuka nayo afiti inu muyaluka simunati akanyimbi
Ipaseni moto nkulu
Inde bwana wathu❤❤❤
Ife kuno ku South Africa kungochotsedwa chifukwa Cha zomwe akupanga chakwela😢azaona konko ku Malawiko zomwe tizapange
Auze zoona a Malawi iwe umakwana ndipo ndimachita kukuika PA Bluetooth kut maneba amve nawo kkkkkk
😂😂😂😂😂
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
umachita bwino
Our channel Malawian channel we love you comrade together with your people ❤❤❤
Namu bwana mumata ❤
Koma a mcp dzikoli ndiye mwalipezelera bwanji pasana panu nonse a mcp ndi masapota anu nonse zitsiru za anthu inu
@@EdwardMathuwa Ndipo mbalame zokhazokha
Kkk koma ntanyiwa usazamwalire uzangosowa mumat tsegula maso ndikutichosa khawa ndikavera mtima kut miyaaah
My channel ❤❤❤
South Africa ikangomuphulisa wagule uja basi, walowa mkati mwana wang'ona ameneyu
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Chakwera woyeeeeeee! Mutu waima, ndipo a Malawi tisalole zopusa
😂😂😂
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Amuchita bwino kumuthyola msagwadazo on top of dat mapwala ake , atilakwisapo apaa kafucheche ameneyuu eish
No matter anyone to hate but the truth i talk.
Yomweyo chikangawa
Inuyotu mumakwana palibenso