Это видео недоступно.
Сожалеем об этом.

Kusumira IMF? Uyuyu ndi Future President

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 5 июл 2024

Комментарии • 116

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 26 дней назад +13

    Azungu amakonda dzisilu monga chakwera

    • @AustinChiyembekezo-cx4mz
      @AustinChiyembekezo-cx4mz 26 дней назад +1

      Ndipo nzungu Amazonia zisilu kwambili powagwilitsa ntchito mwauchisilu like chakwela

  • @user-cq7zi3xu5l
    @user-cq7zi3xu5l 21 день назад +1

    Palibe chosatheka,ndizotheka ndithu kusintha malamulo amenewo before 2025.ndizotheka ndithu let's give support him.

  • @GiftKananji
    @GiftKananji 22 дня назад +2

    Ine ndiye ndamukonda

  • @victorykaminjolo4635
    @victorykaminjolo4635 22 дня назад +1

    DENIS MAHATA ndi Thomas Sankara wa malawi 🇲🇼

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 26 дней назад +7

    Zoonadi brother munthu ameneyo alibwino alibwino ndipo chakwera samaziwa nthandauzo la ( IMF )

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 25 дней назад +2

    Malawi has a lot of intellectual people and mostly very talented and like late sk they knew that he was wise but was polluted with his mind with corrupt money at the time he was very desperate for saving enough money to use for his upcoming UTM campaign and unfortunately he was assassinated bcoz the other party knew he was getting equipped to severed his relationship with Tonse but the problem was that he also knew that the very ruling party at this moment also stole the same am of money and even more than him. He knew what was under the scrotum of his opponent and he was done and finished, ndale za usiku. Greetings from UK.

  • @vivianmkwate8536
    @vivianmkwate8536 24 дня назад +1

    we need young smart men like him look at Ibrahim very young but smart he took over the country couple months the country has been changed. why not us let him be a president and bring changes to our country

  • @vivianmkwate8536
    @vivianmkwate8536 24 дня назад

    He’s young, however super smart, genius, talented young men,he knows how to improve our country being land locked country.

  • @PeterChalechale-pz2bp
    @PeterChalechale-pz2bp 21 день назад

    Captain Ibrahim Traore 36yrs wasinthiratu dziko lake panopa dziko lonse likusapota Traore koma zisiru za ku Malawi kuno zosakonda dziko lathu lino limangogwadira imf pomwe ndiyokuba

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 26 дней назад +3

    Ndizoonadi azungu samafuna kuti africa ipite pa tsogolo ndinkona amabweretsa ngongole zawozp

  • @blessingmanda
    @blessingmanda 26 дней назад +3

    lets welcome him

  • @AudettaYohanie-fl3oc
    @AudettaYohanie-fl3oc 23 дня назад +2

    Ndili pambuyo pake , and zikangotheka zoti aimile u president watenga vote yanga sure

  • @SyilesChebomba
    @SyilesChebomba 25 дней назад +1

    ❤❤❤❤❤ .koma uzamasionese ngope ata kukupanga chiwembu chimwene

  • @Realbaaadman
    @Realbaaadman 26 дней назад +5

    Tiyeni tipange ma demo atsitse zaka akulu akuluwa atitopesa

    • @innocentmusuli7380
      @innocentmusuli7380 24 дня назад +1

      Any time any day any week any month from now tiwone zomwe sitinaziwone a chinyamata azuka

  • @PeterChalechale-pz2bp
    @PeterChalechale-pz2bp 21 день назад

    Uyuyu ndiwoganiza, zitsiru zimangovomera zina zili zonse IMF ndiyokuba koma ife a Malawi timagwadira azungu kupotsa

  • @omanm2919
    @omanm2919 23 дня назад +1

    Wachinyamata ndi amene akufunika ngati president wa Bukina fanso

  • @LessonMnelemba
    @LessonMnelemba 24 дня назад

    I know this Dennis. He was our university president. He is strong.❤

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 22 дня назад +1

    Kwambili azungu amakonda zitsilu kwambili koma amwene kwathu kuno mmmmmmmm

  • @kestenlemucha8316
    @kestenlemucha8316 21 день назад

    he is a supper hero

  • @Realbaaadman
    @Realbaaadman 26 дней назад

    Munthu wa nzeru ameneyi, ati Denis Thanthwe Nkhang’a Mahata Eeh 🔥🔥

  • @user-du8jv9oi5e
    @user-du8jv9oi5e 26 дней назад +1

    Munthu ameneyo abwele bas 😊

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 26 дней назад +3

    IMF kuthandauza kuti freemasons members intentional .koma Satanic mauwa amawabisa ndizolinga zao ndechoti muziwe ndalama ija akakupasa simumapindula zosatilake ndimavuto monga njala kugwa kwandalama yanthu kukwera mtengo kwazinthu ifa pafupipafupi Ngozi zonsayembekezera

  • @PatrickMwamcheka
    @PatrickMwamcheka 22 дня назад

    Inu mayiko onse muwaunawa otukukawa ali ndi ngongole zambiri mbiri ku chokera ku IMF for example south Africa zambia Nigeria just to mention a few

  • @user-nd9cm3yl7e
    @user-nd9cm3yl7e 25 дней назад +1

    Sumaona bakili muluzi tv amakationetsaso mapick omwe achimene akuyakhulacho katundu bakili muluzi tv

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di 26 дней назад +1

    Koma nde mwatilongosolera bwino. Great improvement bro. Kp it up

  • @user-dc7qq9yz3v
    @user-dc7qq9yz3v 24 дня назад

    Ndi chigayo Mr Mahata

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 26 дней назад +2

    Zopanda tchito zimenezo munthu aliyese akakhala kunja kwa boma amaoneka ngati azelu

  • @afonsolucias9339
    @afonsolucias9339 22 дня назад

    But he should be careful coz azungu safuna anthu okuda kom Ali anzeru...

  • @salafinamhone-rd1ku
    @salafinamhone-rd1ku 24 дня назад

    Yes Thomas njala was 29 from Burkina Faso, Abraham Tiro from South Africa was 28 but he asked un comfortable questions to these lolonial masters

  • @runkenkasale4057
    @runkenkasale4057 22 дня назад

    Kwa ine uyuyu ndi munthu wofunika kwambiri muno mmalawi same like kabambe

  • @InnocentThamangani
    @InnocentThamangani 20 дней назад +1

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 26 дней назад +1

    Ndimaganizo abwino potengelanso kuti alikunja kwaboma ,
    Nkhope yeniyeni yamunthu imaoneka akakhala president wadziko , palibe amadziwa kuti uyuyu alipoyu ndi mwini umbava ndi umbanda ,

  • @staprickskilled8589
    @staprickskilled8589 26 дней назад

    Tili pambuyo pake 🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @nafejonga972
    @nafejonga972 26 дней назад +1

    Tell him, he is welcome tinve zomwe akufuna kupanga

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 26 дней назад

    Mwasowatu boss

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 26 дней назад +1

    That's true

  • @user-ie5pc4ox8i
    @user-ie5pc4ox8i 20 дней назад

    Nokha mukumuyamikila nokhaso mukut ndindan alibe dzina aaàaaa😂😂😂😂😂mwatani kod

  • @khwimashawa9040
    @khwimashawa9040 21 день назад

    ❤ tilipa mbuyopake

  • @MorrisMapiri-d6z
    @MorrisMapiri-d6z 23 дня назад

    I have loved him most

  • @stephenkasusubanda3550
    @stephenkasusubanda3550 23 дня назад

    Izitu ndi zoona ndipo ine ndi zomwe ndakhala ndikumaganiza koma poti tiribe kuthekera kothandizira kusinthako. Anthu oganiza chonchiwa (let's support them)

  • @cynthiataulo5211
    @cynthiataulo5211 23 дня назад

    Akhale careful with prayers and wisdom. Azungu ngakhalenso mbava zandale kumalawi zimusowesa.

  • @talentfreshfoods4607
    @talentfreshfoods4607 25 дней назад +1

    IMF sikakamiza ngongole. Timapita tokha kukagwada. Wamwa Ambuye mtengeni ameneyo.

  • @charlesdaisi616
    @charlesdaisi616 24 дня назад

    Bola azipanga zakezo mwanzelu, sikuonpa koma moziwa chomwe anguchite akaziwa ndekuti udolo wake ukhaladi odalilika zikomo

    • @charlesdaisi616
      @charlesdaisi616 24 дня назад

      Umakhala ndi nzeru zabwino koma ukazitulusa ndikumakhalabe mokhulupila aliyense umaphedwa nde azikhala oziwa. Tikufuna anthu oganiza zanzeru chocho koma azichenjela , osangoganiza then kufa aaa.

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 22 дня назад +1

    Koma muthu amwene ndi dolo kwambili

  • @kestenlemucha8316
    @kestenlemucha8316 21 день назад

    NRC Natural Resources College-Tikuchidziwa bwino chipani chmenecho...😅😅

  • @user-mf8fi8wt5d
    @user-mf8fi8wt5d 24 дня назад

    Chakwera ndi puppet wa azungu and thats why you see kuti ndalama za IMF zija amati Extended Credit Facility zakhala zikubwera since Chakwera became President and amatiuza kuti their govt has trust of the donors komano on the ground chomwe tikuwona ndi umphawi okhaokha

  • @MemorieMwasinga
    @MemorieMwasinga 22 дня назад

    The great achievement

  • @andrewBwanaisa
    @andrewBwanaisa 20 дней назад

    Mwana uyu ndi katakwe

  • @TraverMbewe
    @TraverMbewe 21 день назад

    Mmmmmmmm brz sadasumile km amangowaunikila anthu

  • @tiyaselemani4203
    @tiyaselemani4203 19 дней назад

    Dziko la pansi limadani ndi anthu ozindikila take note

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 22 дня назад

    Ngati kuli Anthu akuba kwambili pa dziko ndi IMF fiti za Anthu

  • @williamhami1243
    @williamhami1243 26 дней назад +1

    Are countries forced to borrow money from IMF??

  • @user-cy9zp4fb2m
    @user-cy9zp4fb2m 26 дней назад +1

    Za zakazo zikumphinja kwambr look at Burkina Faso president zaka zake 35 akukwanisa kumene km izi zoti president akhala wazaka 35 above szoona zmnezo

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  26 дней назад

      That's true bro za zakazi azioneso bwino

  • @JustinLipipa
    @JustinLipipa 26 дней назад

    Mmmmmmm atha kukhala president kwakanthawi kochepa, azungu atha kumupha

  • @ophlexmkondowe8107
    @ophlexmkondowe8107 22 дня назад

    Vuto si IMF koma amene amapita kukatenga ngongole kumeneko

  • @AminAbbass-xc4qk
    @AminAbbass-xc4qk 26 дней назад +2

    🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @HaliJana
    @HaliJana 23 дня назад

    TIMUVOTELA KUSIYANA NDI MANYI ACHAKWERAWO MBOLA YOPINDIKA YA CHAKWERA, MFANAYO TILINAYO PA MBUYO BOLA ASAMUPHESO

  • @BakaliAdam-d3j
    @BakaliAdam-d3j 26 дней назад

    Kamer❤❤❤

  • @alexanderlipenga1330
    @alexanderlipenga1330 26 дней назад

    Malawian cameras mwabwera inuyo, ask him akupasenso video ya press briefing yomwe anachititsa some two years ago around July 18/8. Ada awawa has what it take to be a leader except the so called age. Ngat presidential age ili open kwa gogo ikhalenso open kwa mwana.

  • @salafinamhone-rd1ku
    @salafinamhone-rd1ku 24 дня назад

    And we need other kind of education,

  • @user-um6ob9sf3g
    @user-um6ob9sf3g 26 дней назад

    Vuto ndi asogoleli amafuna za IMF cholinga agawane

  • @georgezikabuma9396
    @georgezikabuma9396 22 дня назад

    Bwanji sanasumire a president anthu? Mwawona tsopano kuti president mmangompaka zinthu zoti sizimukhudza. Mesa Inu mmati president ndi amene amatsitsa kwacha? President alibe chifukwa anthu mmangomunena popanda chifukwa.

  • @user-xd2iz1yx4z
    @user-xd2iz1yx4z 24 дня назад

    Amwene mumvereni Denisyo mofatsa ndiye mubwerenso ndi presentation ina.

  • @JhdaLifi-vu9sd
    @JhdaLifi-vu9sd 26 дней назад

    Tell them

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 26 дней назад

    Chakwera ndi mbuzi kodi ameneyi timakamutenga kuti mbuzi yosaziwa chilichonse

  • @user-wk9zh1qc5b
    @user-wk9zh1qc5b 26 дней назад

    Okay

  • @EmmanuelMoyo-hy5ni
    @EmmanuelMoyo-hy5ni 26 дней назад

    Malawi akufunika anthu ngati awa gwenembe amangovomelera chili chonse..

  • @user-ox4fh8pw9z
    @user-ox4fh8pw9z 26 дней назад

    Kd Mesa ndalama za ku IMF timakapempha tokhaa?

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 26 дней назад +1

    Munthu ameneyu Kodi chakwera samupha chifukwa chakwera mmmmmm palibe kalikose. I

  • @MadalitsoChinkhonyo
    @MadalitsoChinkhonyo 24 дня назад

    Palibe zosatheka man bwanji kodi

  • @alickmodi6449
    @alickmodi6449 20 дней назад

    Ndidolo mfanayo😂

  • @user-nd9cm3yl7e
    @user-nd9cm3yl7e 25 дней назад

    Dolo ndiyemweuja bakili muluzi tv bas km iweyo mani palibeso umalankula zogwila ntima kaya umaona ngati timazikonda umakambazi umazinamiza zd bola ungosiya umataya thawiyo zd

  • @MustapherDavie-su3nk
    @MustapherDavie-su3nk 26 дней назад

    Tili Pambuyo pake

  • @PatrickThomson-p9u
    @PatrickThomson-p9u 26 дней назад

    Ali bho ameneyo

  • @joelmakwinjakambalame9652
    @joelmakwinjakambalame9652 24 дня назад

    Kodi chilima nayeso mumati ndi wanzelu. Nzelu nsi ku school chifukwa zomwe timamphunzula ku school ndizoti ena analemba or they experienced it

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x 26 дней назад +1

    Ali bo kwambili tamulandila

  • @hissimajohn965
    @hissimajohn965 26 дней назад

    Komano iyeyo Ali nazo ndalama?????

  • @AaronzoAaron
    @AaronzoAaron 20 дней назад

    Owo

  • @sallymahata4376
    @sallymahata4376 25 дней назад

    🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 26 дней назад

    Anawo ndie ali bwno km kunoko ndie eeeee sizingatheke

  • @user-ln5hw7dn9g
    @user-ln5hw7dn9g 22 дня назад

    Ndamukonda uyuyu

  • @BlessingsNyirenda-ru7ss
    @BlessingsNyirenda-ru7ss 26 дней назад +1

    Tamulandila ife

  • @PatienceMhone-n5w
    @PatienceMhone-n5w 26 дней назад

    Your talking zoveka zokha zokha

  • @AyamMkango
    @AyamMkango 25 дней назад

    Abwinowa akumaphedwa chonde asamale mwanao

  • @ritchardchakuma5725
    @ritchardchakuma5725 26 дней назад

    Tayipangani muve

  • @Thembokatuli
    @Thembokatuli 24 дня назад

    Amupha ngat chilima uyu

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 26 дней назад

    Eeeee ndi mwanadi ameneo kma ndi wa mzeru ka bwanji Ibrahim traole ndi mwanaso osakwana zaka 35 km bwanji akumukonda kwaoko ndie anawo amzeruwo kusiyana ndi akulu akuluwa ka

  • @user-oc1uc6gz3w
    @user-oc1uc6gz3w 26 дней назад

    Ndindanikwenikweni

  • @user-nd9cm3yl7e
    @user-nd9cm3yl7e 25 дней назад

    Komaso iweyo aseyee ndiwe kape zd umakambs zaukape ulibe zelu zd

  • @user-xc2zm9bu1i
    @user-xc2zm9bu1i 26 дней назад

    Amwene chakwera ndi wamkulu kwambirii, computer saikudziwa zangovuta Chilima uja
    Taonani 4 yrs yatha kuno ku Ntcheu wapanga chiyaniii
    Nsewu opita ku Dzunje panopa zoopsa kwambirii
    MCP sikuona kuti paground palibwanjii
    Ine siwandale,zithu zakwela kwambirii
    Dzikoli likufunika anyamata oganiza mwakuya not malilime
    Fertilizer mmmm zafikapa boma likadangonena kuti mafumu ayambeso kulamula anthu awo basi
    Boma lalephera
    Katangale mmm
    Kuvetsa chisoni mafana oganiza bwino akupitaso mmm

  • @HamidavioletYassin
    @HamidavioletYassin 26 дней назад

    Biseni chakwela asamuone asowatu kkkkk

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  26 дней назад +1

      @@HamidavioletYassin 🤣🤣🤣🤣🤣 muli ndi Lawyer?

    • @alexanderlipenga1330
      @alexanderlipenga1330 26 дней назад +1

      ​@@MalawianCamera hahaha musiyeni nzanu alire mwamtendere kkk

  • @user-nd9cm3yl7e
    @user-nd9cm3yl7e 25 дней назад

    Ndesudziwaso kulondolalozakhani

  • @JohnPusi-c9f
    @JohnPusi-c9f 22 дня назад

    Bola asasowesedwe

  • @FlorahBanda-fl4vf
    @FlorahBanda-fl4vf 26 дней назад +1

    Ali ndizaka 32 not 29

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 24 дня назад

    Akhalise Malawi tankonda

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o 26 дней назад

    Big lie alipo ena atha kusintha Malawi

  • @husseinmponda
    @husseinmponda 24 дня назад

    Kkkkkkkk zachabe

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 26 дней назад

    Kodi sheikh mufuti madengo Ali kuti nkhani imeneyo amailongosola bwino ndithu ine ndimamusatila maulaliki ake Osati masheikh anawa satanizm

  • @user-kj4kd1jo1z
    @user-kj4kd1jo1z 26 дней назад +1

    Ayambe kaye u MP then next tym azaimile u President

  • @AudettaYohanie-fl3oc
    @AudettaYohanie-fl3oc 23 дня назад

    Ndili pambuyo pake , and zikangotheka zoti aimile u president watenga vote yanga sure