NKHANGA ZAONA

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 8 фев 2025
  • tidziwe tv

Комментарии • 105

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 Год назад +8

    Mwaswela bwanji nonse amene mumamvela pa nkhanga zaona.ngati mulibwino dzikomo

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 Год назад +1

    Mwaswela bwanji abale anga pa nkhanga zaona,ineyo kuno ndilibwino

  • @DoricaGoweka
    @DoricaGoweka Год назад

    More fire broo osaopaaaa kunena chilungamo.

  • @khalifacalvinajass9998
    @khalifacalvinajass9998 Год назад +2

    Limpopo FM more fire

  • @AliajoeAliajoe-vv1wo
    @AliajoeAliajoe-vv1wo 5 месяцев назад

    More fire 🔥

  • @CharlesNtasa-k2n
    @CharlesNtasa-k2n Год назад

    More fire Limpopo

  • @gracemnenula2518
    @gracemnenula2518 7 месяцев назад

    More fire kt Buuuuuuu!!!

  • @Yoxym
    @Yoxym 7 месяцев назад

    Also were waiting for bakili tv thanks you guys

  • @OmegaChingamuka
    @OmegaChingamuka 6 месяцев назад

    Limpopo FM radio ndi one 🔥🔥🔥🔥💪💪💪💪

  • @Medson-u7n
    @Medson-u7n 4 месяца назад +2

    Zoona koma lipopo mbambande

  • @AlomweAndrewLastonMagwira
    @AlomweAndrewLastonMagwira Год назад

    More fire no fear comrade go go go!!!!!!

  • @peterphir2250
    @peterphir2250 Год назад +1

    Atsogoleri tikuyamikireni koma nkhani zanu simukumaliza mukaziyamba ngati mukunena kuti ntchito zomwe akugwira anthuwa ndi malipiro pa zomwe achita powotcha wa police ku Nsanje kutanthauza kuti anatumidwa ndi abomawo, ndiye a bomawo akuuzani chilungamo chotani? Inu mukadaulula zifukwa zomwe adamuwotchera wa police kuti womutumawo adziwe kuti abisala mmbatata musamangochulukisa kuseka ndi kamangoyimba nyimbo ayi, ifeyo timamvetsera ndi chidwi kuti nkhanga zaonanji tidziwe koma mumango nena molumpha lumpha ngati kuti zomwe mukuwulusa ndi zongopeka so please help us we love you

    • @SheenahMwalabu-iz3pr
      @SheenahMwalabu-iz3pr Год назад

      Ndipo message yomwe imasowa muno ndeiyiyi kkk kumatambasula bobo ngati muja apangila DC Kalindo, otherwise zikumavuta kuzitsatatu. Love you ❤❤

    • @TimothyBilly
      @TimothyBilly Год назад

      That's true muzimalizisa nkhanizo kut tiziziwa zoona zenizeni wr real love you mr Comrade

  • @Rameck-z4z
    @Rameck-z4z 7 месяцев назад

    Iipopo fm mukutiimilira keep it up to

  • @SamuelSamuelJemus
    @SamuelSamuelJemus Год назад

    Mukutiyimirira kumred go go go km ndikufuna nyimboyi yoti chakwera watipweteka anayimba ND ndan

  • @DanielMjasten
    @DanielMjasten 6 месяцев назад

    Ine ndili pheeeee vela limpopo fm

  • @KenedyJolamu-rs9xx
    @KenedyJolamu-rs9xx Год назад

    Mbambande nkhanga zaona❤️🔥

  • @TawandaDzama
    @TawandaDzama 3 месяца назад

    Mumatilankhulira mukukhonza ndithu Limpopo

  • @JOHNDIMA
    @JOHNDIMA 7 месяцев назад +1

    Keep giving us updates

  • @AndrewMdala
    @AndrewMdala 8 месяцев назад +1

    Live from south Africa
    Muyaluka chaka chake ndi chino

  • @ChiwamboThomas
    @ChiwamboThomas 7 месяцев назад

    Nice song

  • @MagretMvula
    @MagretMvula Год назад

    Tikuthokozeni ntciito ndi yayikulu mukugwila more fire mulungu aikepo zanja tione mphumulo mumalawi

  • @SalimMeer-fk9do
    @SalimMeer-fk9do 7 месяцев назад +1

    Zana amayi asanka chifanti malunga ngati vice koma pano ndi opposite ndi zambiri zomwe amalankhula za boza

  • @AnishaMoosa-ej7yr
    @AnishaMoosa-ej7yr Год назад

    Online from Pretoria

  • @TravelodgeMalawi
    @TravelodgeMalawi Год назад +1

    Tiyenazoni ,ife tilipambuyopa tidziwe

  • @Bowa-c7g
    @Bowa-c7g 7 месяцев назад

    Ndipo musasiye mukutisegula maso❤

  • @GiftFrancesco
    @GiftFrancesco Год назад

    Never give up

  • @LyfodKesten-he3fr
    @LyfodKesten-he3fr Год назад

    Lipopo mo faya

  • @AhamdJafali
    @AhamdJafali 7 месяцев назад +2

    Antanyiwa ndakusowani

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 5 месяцев назад

    Sikuti nkuopa bill ya mkadzi ati nkukhwimila anamunamidza Kwa sing'anga akabiba mu toilet apenga a Vaya 😇🤣🤣🤣

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 Год назад

    Mwadza bwanji

  • @PreciousLewis-su2pl
    @PreciousLewis-su2pl 8 месяцев назад +1

    timakunyadilila big man .mtiuzilekoso wa bakili Muluzi tv tawasowa mau ake😢😢😢 guys timakunyadilan

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 7 месяцев назад

    Yomweyo galu iwe Nankhumwa😅😅😅😂😂😂😂😂😅😅😅😅😅

  • @YassinMoffat
    @YassinMoffat 7 месяцев назад +5

    Limpopo fm moto buuuuuu

  • @AdaKalinde-c4j
    @AdaKalinde-c4j 5 месяцев назад

    Apa ndiye mwangarula zenizeni😂😂😂

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule Год назад

    Zoona big man

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw 7 месяцев назад +1

    Timanyadila Limpopo fm

  • @josephcalisto
    @josephcalisto 7 месяцев назад +1

    Limpopo moto kuti buuu

  • @MartinMajola
    @MartinMajola 6 месяцев назад

    Mtaniwa uma kwana

  • @ChristopherAlfred-q9e
    @ChristopherAlfred-q9e 3 месяца назад

    Timayikonda wayiresi imeneyi.

  • @HanifuShaibu
    @HanifuShaibu 13 дней назад

    Umakwan iweyo

  • @BrightonKamwendo-db1ci
    @BrightonKamwendo-db1ci 7 месяцев назад +2

    Osafoka osatopa osawopa

  • @SalimMeer-fk9do
    @SalimMeer-fk9do 7 месяцев назад +1

    Bola bon kalindo ndi bakili mukuzi tv amafufuza mokuya kwambiri

  • @MadalitsoKestern
    @MadalitsoKestern 6 месяцев назад

    Mumakwna alimpompo fm

  • @MatiasPiloti
    @MatiasPiloti Год назад

    Kkkkk koma eeeee

  • @KodwaniMereka
    @KodwaniMereka 7 месяцев назад

    Mulungu azizikuteteza nthawi zonse.

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete Год назад

    ❤ big up brother

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 7 месяцев назад

    Awa ndaboza awa

  • @SalimMeer-fk9do
    @SalimMeer-fk9do 7 месяцев назад

    Uyu ngwa maboza saziwa kufufuza nkhani zoona

    • @robenallie6985
      @robenallie6985 7 месяцев назад

      Ndizzkho zimenezo ife tikumudalira anatiuza kuti onse amu ndege amwalira zinali zoona

  • @ChimwemweJere-v1u
    @ChimwemweJere-v1u 5 месяцев назад

    Ndikufuna kanyimbo Ako please send kamandivesa kukoma heavy ka nyimbo ka zisakho ako

  • @AliAlihasin
    @AliAlihasin Год назад

    Morefire

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 Год назад

    Timakudyadirani our comrade!!

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 7 месяцев назад

    😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅kwagwanji bambo

  • @JamesChiphazi
    @JamesChiphazi 11 месяцев назад

    Kulonjedza nde analonjeza ndikalephela kusitha dzithu kwa dzaka wilili ndizatula pasi udndo Kodi pana pano sanavomeleza kuti alephela kukweza Malawi pano Malawi alipamoto kuposa alamulilo wa muthalika

  • @johnynamano3862
    @johnynamano3862 Год назад

    Zomaotchazi zisiyike chifukwa tsiku lina mudzagwidwa ndiye tidzaona

  • @Maxielyies
    @Maxielyies Год назад +2

    Go deeper comrade, proud of you always 🔥🔥🔥🔥

  • @DysonFly
    @DysonFly 7 месяцев назад

    Mumakwana bwana

  • @CalistoRichard
    @CalistoRichard Год назад

    Yah tamudziwa.....uja ali ndi bukula azibambo

  • @NafeAlie
    @NafeAlie 7 месяцев назад

    Lipopo fm Palibeso ai

  • @smt7036
    @smt7036 Год назад

    fire fire

  • @asiyatujuma5507
    @asiyatujuma5507 Год назад +1

    dyimboyi iilibwinowo😂😂😂😂😂

  • @williamskondowe8795
    @williamskondowe8795 Год назад +1

    Wanunkha malawi

  • @RhodaKalumbi
    @RhodaKalumbi Год назад

    Kkkkkkkkkkkk Sevethday

  • @sharifujoe7633
    @sharifujoe7633 Год назад

    Eisj where are you brah Malawi first we're confused ryt niw so brah plz tell us the truth

  • @chelseajackson3200
    @chelseajackson3200 7 месяцев назад

    Lovely song🎉🎉🎉

  • @SamKaposa-i5c
    @SamKaposa-i5c Год назад

    😂😂😂😂😂 Limpopo fm

  • @MarthaJafali
    @MarthaJafali 7 месяцев назад

    Koma comrede indipha ndi phwete😂😂😂😂😂😂😂

  • @MorganBanda-oc2jx
    @MorganBanda-oc2jx 7 месяцев назад

    kunoku moyo wake ndi osiphina omwewu basi. Malawi zikuoneka kut m'manja mwa atsamunda sitinachokemo ayi

  • @GraceLobart
    @GraceLobart 7 месяцев назад

    Osaopa mulipa bill yanga 😂😂😂

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 7 месяцев назад

    Mundifunsilenso chipatala chakumangochi chimawotchedwa chakandichaka zikukhalabwanji?

  • @SophieKamanga
    @SophieKamanga 7 месяцев назад

    Tilinawe limodzi limpopo Fm mumatiimilila

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 7 месяцев назад

    Koma ambuye kumwambako musatipitirire ku Malawi 😢😢😢

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 7 месяцев назад

    Akut anapengapo Misara kkkkkk amawona ngt amalawi angagwrinse ntchito Misara yakeyo

  • @ImraanJafali-dk7rg
    @ImraanJafali-dk7rg Год назад

    Limpopo fm ndimainyadila kwambli simabisa zigawenge 😂😂😂 more fire nkhanga zaona ife nde malawi olilawo

    • @HOMEOFTECHNOLOGY
      @HOMEOFTECHNOLOGY Год назад

      Mumakwana Limpopo mumatiimirira Ife a malawi potidziwitsa zonunkha za afisi a nkhaza awa tikudziwanao zambiri 😂😂😂

    • @GanieAlidih
      @GanieAlidih Год назад

      Kwan

  • @mcdonaldsitima2107
    @mcdonaldsitima2107 Год назад

    Auze ngozi

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 Год назад

    Achimwene mumanikwana

  • @MarthaJafali
    @MarthaJafali 7 месяцев назад

    Auzeni apite kumangochi aone

  • @AdamYas-ec9oc
    @AdamYas-ec9oc 7 месяцев назад

    Osapa todze ndi amalawi fredom c_to_

  • @FungulanReuben
    @FungulanReuben Год назад

    Mulipo angt,

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 7 месяцев назад

    Opusa iwee ukusochelesa amalawi koma amalawi anapenya zidya drama za muthalikazo ife tikupitax chisogolo ndi mcp bas

  • @WincoJulias
    @WincoJulias Год назад

    Zikachitika timvera kwainu

  • @LimbaniRojha
    @LimbaniRojha Год назад

    avomele zavuta ayimikemaja

  • @patriciacraiton-sf5vu
    @patriciacraiton-sf5vu Год назад

    Kkkkkkkk 😂😂😂😂😂

  • @jossynaitha6863
    @jossynaitha6863 Год назад

    😊

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 Год назад

    😂😂 amangonyera mplastic

  • @DamianoKapachika-ft1ye
    @DamianoKapachika-ft1ye Год назад

    Zamphanvu

  • @JamesKamanja
    @JamesKamanja 7 месяцев назад

    Koma nyimbo zachuluka

  • @Yahiya-wm8nd
    @Yahiya-wm8nd Год назад

    Koma Patricia unaziyamba wenkha kkkkk

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah 7 месяцев назад

    Osafooka osatopa osagonja

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Год назад

    😂😂😂

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Год назад

    😅😅😅😅😅😅😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @RashidBrada
    @RashidBrada Год назад

    Zifukule zose zidziwike❤

  • @AnishaMoosa-ej7yr
    @AnishaMoosa-ej7yr Год назад +1

    Network problem ashh

  • @YassinMoffat
    @YassinMoffat 7 месяцев назад

    Limpopo fm moto buuuuuu

  • @ZioneNyirenda
    @ZioneNyirenda 7 месяцев назад

    😂😂😂😂😂😂

  • @YassinMoffat
    @YassinMoffat 7 месяцев назад

    Limpopo fm moto buuuuuu

  • @YassinMoffat
    @YassinMoffat 7 месяцев назад +1

    Limpopo fm moto buuuuuu