A Thabo Chakaka Mupangitsa Manyazi Dziko La Malawi - Concerned Citizen

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 6 июн 2024
  • On Nyasa VoiceBox, a concerned citizen says Attorney General Thabo Chakaka Nyirenda is embarrassing the country by giving the President poor legal advice.
    Pa Nyasa VoiceBox, mzika yokhudzidwayi yati loya wamkulu wa boma Thabo Chakaka Nyirenda akuchititsa manyazi dziko popereka uphungu wolakwika pa zamalamulo kwa mtsogoleri wa dziko lino.
    #malawi

Комментарии • 101

  • @FranklinNdovi
    @FranklinNdovi 22 дня назад +7

    Why did President Chajwera remove Dr chikosa Silungwe? Dr chikosa Silungwe is a competent lawyer who has had worked in the Malawi Government for long long time with vast experience but because he advised the government accordingly.
    Mr Thumbo chajaja Nyirenda is an incompetent lawyer he occupied that seat because of political reasons and nothing else. somebody in the MCP had just favoured him yo become the Attorney General of the Malawi Government. Shame on you the president and his politically appointed Attorney General Thabo chajaja Nyirenda. He had never won cases in the Court of law for the RBM and his other clients before.
    Therefore the President should now terminate his fake appointment on that post of the Attorney General and give it to the rightful competent lawyers with vast experience. He is as incompetent as the former DPP before Dr Kalua.

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 22 дня назад +3

    Abambo awa akukalipa zoon, Thabo Chakaka sakukwana kulangiza boma, moti akuwononga ndalama za boma pochita zonsezi. Amuchotsepo paudindo.

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v 21 день назад +2

    Chakwerayonso ndi mbuzi yamunthu galu

  • @FunnyBasketball-er3vc
    @FunnyBasketball-er3vc 22 дня назад +3

    The problem is ,the president advises the attorney general

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll 22 дня назад +5

    Chakwera, ana mchosa silungwe, kadaulo pazamalamulo, ankafuna oti aziba naye, komanso kuphinja Malawi

  • @Moffat-oi4yx
    @Moffat-oi4yx 22 дня назад +2

    Mwapangitsa manyazi atumbuka anzanu ngati anthu osapita kusukilu mbuli zoyendetsa ziko.

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 22 дня назад +2

    Akulu awa ayakhula bwino kwambiri koma vuto lonse ndi Chakwela chifukwa sogoleri azikhala wadzelu ndiwonganiza bho

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 22 дня назад +5

    Chakaka nyirenda chisiru cha munthu akumusochelesa president nkhani ya streight forward then why wasting kumakatenga chileso. Are you pleasing president for wat?? Are you quolified?? Anakutenga kuti??.

  • @jamesgondwe6669
    @jamesgondwe6669 21 день назад +1

    Thabo is just an honour's degree holder.

  • @GrecianWyson
    @GrecianWyson 21 день назад +1

    Vuto NDI osewa amwene no sense chakwera 😊

  • @GogomphatsoSinosi
    @GogomphatsoSinosi 11 дней назад +1

    Kulankhula kolankhuliratu 😅😅😅

  • @khoviwaedward
    @khoviwaedward 22 дня назад +2

    Ulamuliro ochitisa manyazi mu mbiri ya southern Africa. Embassy ya dziko la kunja kupereka visa pomwe dziko lako kupereka fake passport dzoona?

  • @user-zg7iw8kq4r
    @user-zg7iw8kq4r 21 день назад

    Ameneyi si attorney general ndi mbuzi kwabasi tsiku lina pofunika kuzamugenda miyala galu ameneyu

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 20 дней назад

    Dr Chakwela akanatha kumayendesa bwino ziko la Malawi koma vuto anthu omwe amuyandikila president ali ndi njiru kuti president azioneka oipa pomwe ndi wabwino.

  • @amiduclement2142
    @amiduclement2142 22 дня назад +2

    Komaso ameneyu ndi wa mcp?

  • @CassimMbalaka
    @CassimMbalaka 22 дня назад +1

    Akudxiwana wosewo alilimodxi mmesa adamusakha yekha chakwerayo

  • @user-ql8nf2vb8s
    @user-ql8nf2vb8s 22 дня назад +2

    Awuze bwana uyu ndi waunsilu

  • @Ngwangwa-ej4rs
    @Ngwangwa-ej4rs 14 дней назад

    Dzikoli laola kuposa nthawi ya Mutthalika izi ndiye zolopa zenizeni

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 22 дня назад +1

    Experience matters!!!!

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 22 дня назад +1

    They are busy breaking the law

  • @ManesKamtambo
    @ManesKamtambo 20 дней назад

    More fire big man you are talking

  • @JimmyKapunza
    @JimmyKapunza 22 дня назад

    This is powerful iwe thabo chakaka futsek

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 5 дней назад

    We want One Malawi One love, And this iz not Old Malawi, all the malawians know the truth people are crying and suffering Under the rule of MCP, and Chakwera the killer Man fake pastor panyini pa mawo both of them but what they should know is that, this is not Old Malawi, this cruel people must know justice of Malawian people One Day, and justice will come out One Day

  • @user-iu6mr5xu6r
    @user-iu6mr5xu6r 4 дня назад

    Munthu iwe Mulungu akudalise pa masomphenya ako

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q 22 дня назад +1

    Wauza bola anve koma ngati sanva tumizani Ina audio apange manyazi

  • @jonathanmunthali8500
    @jonathanmunthali8500 21 день назад

    Ndi a Nyirenda akuti wosaphuzira 😢

  • @user-cv3zw9ic6d
    @user-cv3zw9ic6d 21 день назад

    Athabo chakaka akalowelera bwanji za ku immigration popeza si office yawo komakuti ma guy aku immigration agenda galu mwini wagalu waoneka poti akupangira ma passport kuchipinda munya muona 2925 dpp boma wokavota ndi ife tatopa kulamulidwa ndi gule

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 21 день назад

    Aaaaa MCP simamva zaanthu kuyambila kele mvuto mtima wachipani chimodzi chakaka alibe mvuto mvuto chakwela ndi MCP

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 22 дня назад +1

    Zoona amasureni athabo aaonjeza

  • @mathiasmastepe2873
    @mathiasmastepe2873 21 день назад

    Chomwe akuyankhula mkuluyu sindikukuchimvetsa. Who is to blame? Thabo chakaka ndi wabwino kwambiri. Koma anthu omwe amaunikiridwa ndiwo amene Ali ndi vuto. Ask ur president kuti Kodi AG amamuza chani?

  • @user-rk4ch1ly3z
    @user-rk4ch1ly3z 21 день назад

    Muthile moto kumene, mwana opusa kwambiri akuwona ngati,,zikoli lawyer alipo yekha mwana opusa kwambiri,,mukalipileni dziko akuliwononga ma guyz watu.

  • @AckimMhango
    @AckimMhango 21 день назад

    President ndiye akufuna munthu woti atsamulangize ndicho chifukwa anachotsa Chikosa Sulungwe poti akufuna zomwezo

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 22 дня назад

    Komanso apule anamuchotseranji lawyer oyamba uja, kuyika Thabo Chaka ka nyirendayo

  • @Ngwangwa-ej4rs
    @Ngwangwa-ej4rs 14 дней назад

    He is after money not rules nao apresident aganize bwino za advisor wawo failing which mmmm

  • @PiterDeleza
    @PiterDeleza 22 дня назад

    A Chembe intelligent yake ndiye yotibweresera nkhalambayo.

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n 21 день назад

    Osaona kuyendesa dziko mbuzi za anthu izi

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n 21 день назад

    Anaphunzira kuzunza anthu basi, asatana achabechabe awa

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 22 дня назад

    Pajatu anthunu munkati atumbuka ndiodzindikira kwambiri nanga izi nchiyani ? Anthuwa anasankhidwa ndi Chakwera ndipo amukhaulitsanso Chakwerayo nanga pamenepa a Chakwera zinthu ziwayendera ?

  • @BernadFlackson
    @BernadFlackson 22 дня назад

    Chiwudzeni chikuwononga dalaa

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki 22 дня назад

    Osewo ndi zisilu zidude zakuba

  • @JamilahMaluwa
    @JamilahMaluwa 21 день назад

    Onsewo nzitsiru retired abwelera bwanjinso mboma?

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 22 дня назад

    Muuzeni galu ameneyu ndi chitsilu

  • @joebrown1158
    @joebrown1158 22 дня назад

    Noone is above the laws

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk 22 дня назад

    Manyaka enieni adindo opanda nzeru

  • @FaisonLukiyo
    @FaisonLukiyo 21 день назад

    Mzowonad tiyamike kulankhula kwa abwanawa.

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 22 дня назад

    Ngati ogwira nthito zaboma ziri zitini ofoyira oyamba ndi omusankha .

  • @JimmyKapunza
    @JimmyKapunza 22 дня назад

    Madala mwayankhula this is very powerful iwe chakaka futsek 😂

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 22 дня назад

    Akulitenga ngati dzikoli ndilambuyake

  • @BMadhlopa
    @BMadhlopa 12 дней назад

    That Thabbo is the most failed is running away from the truth!

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 22 дня назад

    Zangokumana zisilu zokha zokha pamenepo ka awapange abwino kmaso cnanga ndi mbamva anakatani kubelako akubelako limozi ndi mcp 😂😂😂

  • @user-jd9yz5hp7y
    @user-jd9yz5hp7y 21 день назад

    NKHASA adayimba NYIMBO YONENA KUTI TINASAKHA ORAKWIKA izi lero zikuyikira uboni nyimba imeneyi ya PHUNGU JOSEPH NKHASA
    NAWONSO ACHAKWERA NDI UMBULI WAWO AKUGOPITILIZA KUSAKHANSO ORAKWIKA ZOMVETSA CHISONI DZIKO LATHU

  • @KasimIbbu
    @KasimIbbu 22 дня назад

    Ndiwesilu kwabas apage mayaz kumene puleziditi wo

  • @wayafrank2405
    @wayafrank2405 21 день назад

    Kamwana kameneka udindoo wamukulila

  • @yohanedaudi1740
    @yohanedaudi1740 22 дня назад

    Anthu oputsa ,Koditu ine Ngati mmalawi mukamati anthu ambiri akupoto NDI ophunzira ine ndimaletsa Koma chomwe ndimadziwa ndichoti anthuwa amangolowetsana potengera kochokera tribelisim

  • @user-is5dl7np9g
    @user-is5dl7np9g 22 дня назад

    Thabo Nyirenda ndi kape kwambiri

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n 21 день назад

    We need chikosa silungwe back

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 22 дня назад

    Ndipo chakwela tizamukumbukila osati ku zabwino ayi koma ku zowawa zomwe chakwela wativetsela kuwawa ndipo sitidzamuiwala

  • @LukaAron-el5qh
    @LukaAron-el5qh 22 дня назад

    Thabo chakaka ndi Attorney general wa chakwera kalpana wamcp osati wa boma lamawi

  • @AbdulrahimoMassamba
    @AbdulrahimoMassamba 20 дней назад

    Musamuchemerere mdalayu ndiwaganyu uyu.akukoma mkamwa akufuna 1kg ya sugar uyu

  • @AbdulrahimoMassamba
    @AbdulrahimoMassamba 20 дней назад

    Musalimvane ndi Athabo, bwanji mukudusa m'mbali? Kweni kweni muli mbali iti inuyo Apule ndiwo chizete chotheratu inunso mwagudwa timawaxiwa omwe akutimenyera nkhondo tsekani chimbuzicho mukutinunkhitsa kuno

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 22 дня назад

    Chisilu cha munthu ichi kaya ndiwakuti munthu wopepela ngati ameneyi ....akuti pamenepa akufuna kusamgalasa president

  • @user-sw2rn3xn3g
    @user-sw2rn3xn3g 22 дня назад

    Zosayenda

  • @joebrown1158
    @joebrown1158 22 дня назад

    If we speak of incompetent means Razarus Chakwera is incompetent.

  • @user-hl3vl9nt1b
    @user-hl3vl9nt1b 22 дня назад

    Nawe iwe chembe tamata kuchimbuzi kwakoko naweso ndiwe kape paja

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 22 дня назад

    Kumasiyanitsa Mlangizi wa boma ndi wa banja

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m 22 дня назад

    Achoke

  • @jeffchikwapata6933
    @jeffchikwapata6933 21 день назад

    This guy he called himself atoney General is useless

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 22 дня назад

    Kodi munthu ameneyi anakamutenga kuti ......kungotengana zisilu zokhazokha

  • @amiduclement2142
    @amiduclement2142 22 дня назад

    Zikozakuteka kuti ndi wa udf

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 22 дня назад

    Komadimtu Sona🤔

  • @user-bg7ur1gw1q
    @user-bg7ur1gw1q 22 дня назад

    Auze anve

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o 22 дня назад

    Ndinamva kuti ndi m'bale wawo wa a Chakwera uyu

  • @Ngwangwa-ej4rs
    @Ngwangwa-ej4rs 14 дней назад

    He is not suitable for apresident he must go back to be apastor

  • @user-oq5rg5mz7q
    @user-oq5rg5mz7q 22 дня назад

    Chakwela ndi athabo chakwaka ndi 🐕‍🦺 kwambili

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 22 дня назад

    RUclips yaphweka kumalawi.

  • @PhillspicJere
    @PhillspicJere 22 дня назад

    Ngakhale ku thyolo kumachoka Bingu komaso Peter koma umphawi osayamba agalu inu

    • @Zelinakhisswell
      @Zelinakhisswell 22 дня назад +1

      Nanga zugwirizana bwanji ndi main nkhani yomwe ikukambidwa, mesa umphwawi wasefukira chifukwa Cha president wako ongodziwa kugwetsa ndalama ndi kuba moti azilimbikira kupanga zinthu zoti apeze forex

    • @MarthaMalopa-kw9xw
      @MarthaMalopa-kw9xw 22 дня назад

      Zomwe zikuonongeka ndi zakuThyolo kapena dziko lonse? Tiyeni tidzuke aMalawi ndikusiya kaganizidwe kodana ndi anzathu

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN 21 день назад

    Chichosen pampandopo musazachiyikeso pa mpando uliose chimenecho aaa chandikwana msaname, and
    Which pelezideti instead of president you talking about ,not we don't have a leader in malawi,I shall show you a really president of malawi in 2025!!!!

  • @garnetphiri
    @garnetphiri 22 дня назад +1

    Im Garnet J K Phiri, im here to comment on this audio, mzika zokhumudwa they are100% right,to tell our gaverment muli mbuli zosaona zokha zokha paja amati osaona salondolelana njila munthu sungatenge masanzo ndikuwabwezelesa mmimba kachiwiri ,mukutenga munthu wa retired wosanzidwa put back in gaverment Achakwela mutual wanu umagwira bwino ntchito or you are just enforced by some .Nyirenda ,attorney,are you a real qualify loyar?or you are there like a sign post that you don't know what you are doing?Even you Chakwela and your friend Chilima you can't feel shame to how how people are struggling on passports issue? Simuchita manyazi anthu kumabwezedwa pa immigration for sake of fake passport , Chills i thought you're brilliant but you are coward plus Chakwela too

  • @user-sw2rn3xn3g
    @user-sw2rn3xn3g 22 дня назад

    Kkkkkkkkk

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i 22 дня назад +1

    Angokumana okhaokha,...ubwino wakenso ma passport wo akuvutika nawo okha.....ife timangoyendatu olo opanda passport ..crossboarder😂😂😂😂😂😂

    • @SameKaposa
      @SameKaposa 22 дня назад

      😂😂😂😂😂😂

  • @ChembeWaimba
    @ChembeWaimba 22 дня назад

    Chakaka Nyirenda very interigent, iwe do you know behind this mess, do you know that Kalumo is fighting corruption at immigration hence this and yet supporting corruption, inu munakhalapo kuti attorney general??¿???

    • @PhillspicJere
      @PhillspicJere 22 дня назад

      Sakudziwa awa zambiri Ku DPP ndizitsiru zomwe akumazipasa bundle kumangolankhula zopanda mutu agalu awa

    • @eliffagondewe8214
      @eliffagondewe8214 22 дня назад +1

      Fake passport, fake president, kkkkkkk 🔥🔥🔥🔥boma lofoyila ili

    • @SameKaposa
      @SameKaposa 22 дня назад +1

      Akuthana ndi corruption? Koma akumapanga ma passport a fake nkhani yochititsa manyaz musamuikile kumbuyo nanu😢😢😢

    • @user-to5of3ks3g
      @user-to5of3ks3g 22 дня назад

      Fake govement passport fake

    • @user-hd7wq2yc6m
      @user-hd7wq2yc6m 22 дня назад +1

      Pali zanzeru pa chakaka nyirenda apa? Iwe mbizi eti khoti laweriza bwino bwino iwe nkumanena kuti sizilibwino opanda nzeru iwe khala chete malamulo simuwaziwa Inu boma muziyendetsera unkhungu ,.kuba chitsiru iwe ndi usapota wako wauchitsiru

  • @PhillspicJere
    @PhillspicJere 22 дня назад

    Thabo chakaka Nyirenda ndi dolo koma zisiru ngati inuyo a DPP ndiamene mukumuona ngati palibe chomwe akudziwa, mwaiwala kuti munali ndi mhango lawyer wa mutharika emwe samadziwa kanthu? Mwaiwala kuti kunali Mai Jane Ansah wa DPP koma Peter anakhala chete? Ndiye nzeru zomwe mulinazo inu Ndiye ziti zotibwelesera nkhalamba kuti izalamulese? Agalu inu zisiru Ku DPP kwanuko musaone ngati akakupasani ma bundle wo a DPP Anthu Ndiye asintha kuvotera nkhalamba? Chitsiru iwe ndi ufulu otengera nkhani Ku court lina mbuzi iwe sudziwa kanthu galu

    • @Zelinakhisswell
      @Zelinakhisswell 22 дня назад

      Anthu ukuwatchurao munthaw Yao zinthu zimayenda ngt Pali zomwe amalakwitsa kma sizinafike ngt apa pokhotesera Dala malamulo Ali clear, ufune usafune 2025 gule kwao abwelere kudambwe

    • @JamesLongwe-qz9fd
      @JamesLongwe-qz9fd 22 дня назад

      Takhala chete naweso Malawi wavunda naweso ukuyankhula mbwerera

    • @user-hd7wq2yc6m
      @user-hd7wq2yc6m 22 дня назад +1

      Ndichifukwa chake iwe ukusapota chiboma ichi uli chindere nkhani yachiziwikile iyi iweyu kuyamba kuyamkhula za DPP palizeru apa? Iwe zeru ulije kwali ndiwe wa mcp ulichindere chomene DPP ungafanizire ndi mcp, DPP inayendesa bwino boma kusiyana ndi mcp yakoyo mcp kuba,kulemba nthito pa chibale, kikondera chigawo chimoza, kulembana ntchito pa mpingo wa Assembles of God pama boma ghose agho takhala nagho since democracy 1994 this is the worst of the worst government munthu iyo wakusapota boma ili kulongola kuti mutu wake ngwakufuntha mahala walije chindere foseki

    • @vytwistthelion98
      @vytwistthelion98 21 день назад

      Mwana wanjoka seka pachombuzi pakopo chifukwa suziwa chomwe ukunena

    • @richardbanda9997
      @richardbanda9997 21 день назад +1

      Izizi musazitengere Ku ndale. Time zoona pano Ku Immigration kwaola. You mean you can't see. Kapena inuyo mukapita Ku Immigration, mukuthandizidwa? Tamaganizani osati chifukwa Choti mukudya nawo nde basi kumangotsutsa pomwe Pali chilungamo. SHAME MCP.

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 20 дней назад

    Ameneyu anali mulimi sakuziwa za ndale vuto akumasankhilana chibala ndichifukwa akumakanika kuyendesa dziko akumasiya anthu okhala ndi experience ya kuyendesa boma zamanyanzi Malawi