Dziko La Malawi Ndilosauka Kwambili Kuti Tizikhlala Busy Ndi Cybercrime - Samuel Lwara

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 24 июн 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara says, Malawi's level of Socio-econonic development is too low for people and government to be busy with cybercrime laws instead of focusing on development and economic growth.
    Pankhani ya Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara wati chitukuko cha dziko la Malawi pa chitukuko cha chikhalidwe cha anthu ndi chochepa kwambiri moti anthu komanso boma limakhala lotanganidwa ndi malamulo okhudza umbava wa pa intaneti m’malo moika maganizo awo pa chitukuko ndi kukweza chuma.
    #malawi

Комментарии • 94

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 4 дня назад +6

    Malawi has intellectuals like Lwara ,we need people like Lwara the country can do better

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 4 дня назад +5

    Good Messnge Chakwela you mast go watinyasa

  • @JamesMalango
    @JamesMalango 4 дня назад +4

    Chilungamo sir great speech

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 4 дня назад +1

    This is powerful speech i ever heard before from anyone who fighting against this useless government. Chakwera ndimbuzi pamozi ndi anthu ake wose galu yamunthu

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o 17 часов назад

    Powerful message chilima anapanga kale compaign akangolowa kupanda kuganiza zochosa moyo wake koma mau ndi oti chilima sanafe alipo mpaka 2025 MCP isova chipani cha mwazi😢

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 4 дня назад +2

    Sam umalankhula ma points ogwira mtima, keep it up bro, keep on fighting for those whose got a say but they can't talk

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 4 дня назад +3

    Achakwera opusa kwambili wapasako ukuvuna kulimbana ndiandu kusiyakukosa dziko boma lopusa lilibeseluso

  • @user-qg4it7my9n
    @user-qg4it7my9n 4 дня назад +1

    kachilungamo2 ulemu wanu ine pheee!!!! ❤❤

  • @AllanWyson
    @AllanWyson 4 дня назад

    This guys impresses me with his naked truth, may god continue keeping this guy for us so that he must continue speaking for those who cant speak.

  • @jacksonmaster2288
    @jacksonmaster2288 4 дня назад +2

    Samuel Lwara ndiwa nzeru.

  • @user-wf2ii7zx5e
    @user-wf2ii7zx5e 4 дня назад

    Thank you brother, Chilima timulira mpaka tsiku lozavota. Mcp ichoke basi

  • @user-fp5qn5ci2v
    @user-fp5qn5ci2v 4 дня назад +3

    😅😅😅😅 Lwara ai ndithu lero kulibe Bakili Muluzi TV ndipo sindikanagona bwino kupanda iwe anthu ngat inu mukufunika mMalawi muno kwambiri

  • @chikublea8982
    @chikublea8982 4 дня назад +2

    From mangochi mumatha kwambiri

  • @user-iw6cz5ft2l
    @user-iw6cz5ft2l 4 дня назад +1

    Thank you sir

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t 4 дня назад +1

    Very nice mr this goverment is felia

  • @MaxwellMbesa
    @MaxwellMbesa 4 дня назад +1

    Zoona brother

  • @meeksonmkhala
    @meeksonmkhala 4 дня назад

    Well facts presented. Well done Mr Samuel

  • @user-xx3mg2gz5z
    @user-xx3mg2gz5z 3 дня назад

    Achape mutu my brother

  • @StevenAjusugama
    @StevenAjusugama 4 дня назад

    Good talking brother

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr 4 дня назад

    Ndimamva Nanu kukoma abambo a Lwara ndipo izizi mmalankhulazi ziziikidwa ku times radio ku mibawa amalawi adzimva kuti atseguke mitu ndipo chilungamo chimawawa. Koma nde Chilima anali mbambande ndipo anali hope yathu RIP

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 4 дня назад +2

    Muwawuzenso kuti social media ndiya azungu, Twitter, Instagram, WhatsApp, facebook, utube it's from European countries, and enu wake azunguwo akumaposita ma video and photos pa social media, ndeinu a mcp muzitilesa kuposita ma video pa social media, who are you?, peter kalaya , who are you? ,daud suleyman, who are you?, kumkuyu and chimwendo who are you?, zikhale ng'oma and yolamu who are you?.
    Stop intimidating malawians ok?, mxiem 😡

  • @user-ve2ts3yr2n
    @user-ve2ts3yr2n 4 дня назад

    🙌 powerful achoke basi

  • @user-pl8kw3dc9d
    @user-pl8kw3dc9d 4 дня назад

    Zoona zoona brother kuputsa kwa chakwera

  • @afritouch4660
    @afritouch4660 4 дня назад

    Powerful.!

  • @gizzykondwani865
    @gizzykondwani865 4 дня назад

    keep up the good work

  • @LumbaniNeba
    @LumbaniNeba 4 дня назад

    Congratulations brother

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e 4 дня назад

    I salute you sibweni

  • @remsychipani2896
    @remsychipani2896 4 дня назад

    Zamphavu kwabasi more fire big

  • @DavieMakwecha
    @DavieMakwecha 2 дня назад

    Ndipo pafunika kuotcha ma office onse plus magalimoto onse a mcp chitheretu chipani chimenechi mmalawi

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 4 дня назад +1

    Tell dem bro, they don't know de definition of the word CIBER CRIME 😂😂😂😂😂😂

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 4 дня назад

    Cybercrime kunyumba kwako ndi family Yako chakwera,,not Kwa ife amalawi

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 3 дня назад

    Inuyo comrade ndinu mafia Mutha kulowa Malo mwa chilimat inu chilungamo chomwe mukulakhula ZOMWE chilima amafuna zimu wawo SKC uziutsa mumtendere taluzat muthu UJA wapita wamala kwabasaaaaa mwatililisa mcp pachilima ndianthu 9 onse ujatalirat

  • @user-is5dl7np9g
    @user-is5dl7np9g 4 дня назад

    Uku ndiye kulankhula Kwa mzuru bwana Lwara

  • @HafizahHarack-bn3bf
    @HafizahHarack-bn3bf 4 дня назад

    Chakwela ngat uli wa mzelu unakangochoka wenkha pampandopo because watikwana ndikuti Nyasa kwambili.

  • @JohnKayinga
    @JohnKayinga 2 дня назад

    Ndipo izi nane ndinali wodabwa komaso chikudabwisa a police omanga anthuwo akuchokera ku LILONGWE Kodi ku BT ndi ku mzuzu a police kulibeko? MCP government is falling apart koma zomanganazo zikapitilira zitha kubwelesa kusamvana mziko

  • @user-ez8zs1iq9k
    @user-ez8zs1iq9k 4 дня назад

    inetu sindimakuteengerani a lwara pazoyankhula zanu koma ngati zoyankhaula zanu ndi izi nde kuyambira lero ndizikusatani chifukwa umu mwayankhula chilungamo komaso za nzeru kwambiri

  • @blessingsmaloya3570
    @blessingsmaloya3570 4 дня назад

    Shaaaa!!!!!

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p 3 дня назад

    Zoonadi Big

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u 4 дня назад +1

    Amasuleni kuti boma likupita ili kkkkkkk koma Lwara kkkkk anthu osamva awa boma lililamulidwa ndi nduna president of ofoyila kkkk

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 4 дня назад

    Wakumva wave koma agaluwa Chakwera ndi azinzake samba chifukwa ndi ana asatana

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 4 дня назад

    Kkkkkkk inu Mmayankhula bwino kwambiri🔥🔥🔥🔥reality..

  • @user-ww2il4wb8o
    @user-ww2il4wb8o 4 дня назад +1

    😅😅😅😅koma chilungamo chitipha

  • @EdwardSamuel-xj8qq
    @EdwardSamuel-xj8qq 4 дня назад +1

    Zowona

  • @user-lb5gt4uv3s
    @user-lb5gt4uv3s 4 дня назад

    Chilungamo brother

  • @NTHANDOHKHOROMANA
    @NTHANDOHKHOROMANA 3 дня назад

    25 mini zoyakhula za nzeru zokha zokha

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 4 дня назад +1

    Kkkkk wawo wa mcp akuti uza yekha a tavala nsalu yawo amangetu

  • @SibwenzaLevisoni-gm6rv
    @SibwenzaLevisoni-gm6rv 4 дня назад

    Fire dem

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 4 дня назад +1

    Zoona zokhazokha mbambande

  • @4ourcusworldwide426
    @4ourcusworldwide426 3 дня назад

    💪💪💪💪💪

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q 3 дня назад

    Kkkkkk chakwera watikwana kwambiri nichifukwa ni lazar wa zironda

  • @martinnyirongo2892
    @martinnyirongo2892 4 дня назад

    Aaaa kwathu kumzimba no chitukuko Kayama mps aliko ndkukaika, mzimba to eswazini, mzalangwe, kafukule upto ekwendeni mseu unayamba mnthawi ya bingu mpaka pano sunatheee ndikunena pano mcp government inachotsa contractor, mwachidule tinene kuti anasiya kumanga since chakwera anatenga boma mu 2020 ndiye ine ndikudabwa kuti mafumu amuboma lamuzimba akulephera bwanji kumuuza chakwera zamuseu imeneu chifukwa ena mwa mafumuwa ndikwawo kumeneku komaso akugwiritsa ntchito mseu omweu eeeeee abale kumzimba anthu akuvutika nthawi ya mvula mayendedwe,,

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2ki 4 дня назад

    Mr lwara you are genuine comrade may God continue to bless you! Tell these idiots the truth.

  • @tasmania527
    @tasmania527 4 дня назад

    Imwe muli wa chindele imwe, nzeru kuchuluka.

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h 4 дня назад

    Samuel from the bible tiyeni nazo osamakhala ndimantha ngati ndinu obwela tell them truth mantha satithandiza

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 4 дня назад

    Ndipo live chilungamo kuwawa chakwera watiphera msogoleri wathu

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 4 дня назад

    Ndipo live sukunama chakwera saziwa kanthu ndipo ndale saziziwa ata 😂😂😂😂

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 4 дня назад

    Nde mwati mwazi wachilima utani big

  • @user-os7qt6lw2c
    @user-os7qt6lw2c 4 дня назад

    Iwe nde akumanga..

  • @JerryChain-cz8ru
    @JerryChain-cz8ru 4 дня назад

    Awuze kuti onse ndamphawi tikuvutika

  • @fatshooter87
    @fatshooter87 4 дня назад

    S
    Tell them boss Lwara

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 4 дня назад

    😮😮😮😮

  • @margetjustin7170
    @margetjustin7170 4 дня назад

    Zoona apange resign onse felliar minister

  • @ChimwemweHenry-uw1bq
    @ChimwemweHenry-uw1bq 4 дня назад

    Live talk ulemu wanu

  • @MustafaAbdullah-pb5zv
    @MustafaAbdullah-pb5zv 4 дня назад

    Chilungamo biggy

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 4 дня назад

    Lwala iwe ndi wazelu kobas ulemu wako

  • @ebenezerkamanga6016
    @ebenezerkamanga6016 4 дня назад

    Waying'alura momveka bwino aseh 😂😂😂

  • @user-kj6qj1md5e
    @user-kj6qj1md5e 4 дня назад

    Amakambilana zaupandu afiti awa

  • @MilikaKilion-tn1bn
    @MilikaKilion-tn1bn 4 дня назад

    Sumapita kuchimbuzi ukadya question 😅😅😅😅

  • @user-fq4kv8dj4t
    @user-fq4kv8dj4t 4 дня назад

    Presdent uyuyu nde ayi panja penipeni Chakwela lazalo

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 4 дня назад

    Kapen asimti usachaniso agaluwa

  • @Philipmantchombe-bb5dx
    @Philipmantchombe-bb5dx 4 дня назад

    Komatu ndiemwayankhulabwino bolamusasinthekusogoloku pajatu kunali laitoni mangochi

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 4 дня назад

    Why u were quiet for the whole last month bro?

  • @stellakaluluma8241
    @stellakaluluma8241 4 дня назад

    Bingu came with helicopters from China, where are these helicopters ?

  • @user-pl8kw3dc9d
    @user-pl8kw3dc9d 4 дня назад

    Mnthu kuchoka ku church kukankhara mutsogoleri wadziku kkkkkkk malawi ife kumbwambwana kukatsankha nkhumba

  • @CharityMhone-uk9ym
    @CharityMhone-uk9ym 4 дня назад

    😂😂😂😂😂🎉🎉🎉 mtumbuka iyoo

  • @user-um6yo6nc3e
    @user-um6yo6nc3e 4 дня назад

    Cybèrspace 😢

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 4 дня назад

    Kkkk apatu apatu watokota dziedi lwala ti amva pena pake akuti a boma akupasini bazi ayiiii bodza anthu ngati inu ndimene mulungu adzikupatsani moyo wawutali anthu ankhadza mulungu adziwachepetsela moyo wawo chifukwa ngati a MCP akumanga anthu ndiboma lopaaidwa ndi malemu chilima mwalo mothokodza ndikumuphatso ufiti wanji abale nde awine 2025 malawi tafa basi chuma chiwakanika kukodza nsono akufuna amalawi adzatiiani kodi iiii mulungu simunthu achite nanu a MCP

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 4 дня назад

    Another freedom fighter is here guys 😂😂😂😂

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 4 дня назад

    Guyz!, sam rwala is here kkkkkk😂😂😂😂😂

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 4 дня назад

    MCP rest in peace

  • @JumaKachala
    @JumaKachala 4 дня назад

    Kkkkkkkk keep it up

  • @AmusedDimSum-hd5yp
    @AmusedDimSum-hd5yp 4 дня назад

    ipaseni moto fada empty head chakwera

  • @JackMvura-ik2td
    @JackMvura-ik2td 4 дня назад

    Olira sitimamutseka pakamwa chakwera bomaaa sanje akulu awa akalamba mwachangu kuipa mtima zedii utopa ndikulankhula chakwera sudzamuona kuyankhapo zopusa ngati izi very stupid massage to Malawians tikuuze tsono chakwera adzawina with landslide ukuonanso dikira

  • @ClementKamwendo-ti4vi
    @ClementKamwendo-ti4vi 4 дня назад

    😢😂😂😂❤

  • @HarryKandani
    @HarryKandani 4 дня назад

    😂😂😂 koma yeah

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 4 дня назад

    😂😂😂❤❤

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 4 дня назад

    😂😂😂😂😂😂😂🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 4 дня назад

    Is dat true that you recieved the money from dis cruel and useless crocodile party?

  • @InnocentMlowoka-ew4lo
    @InnocentMlowoka-ew4lo 4 дня назад

    Ii

  • @user-xx3mg2gz5z
    @user-xx3mg2gz5z 3 дня назад

    Kkkkkkkkkkk

  • @HakeemJossam
    @HakeemJossam 4 дня назад

    kkkkkkk