Limpopo kupsa kwa nyumba ya Kaliati zoona zeni zeni izi tamvani bwino bwino

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 8 июл 2024

Комментарии • 59

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge 22 дня назад

    BEST LEDIO LIMPOPO M'MAKWANA 🙏🙏🙏💪💪💪💪💪❤❤❤

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w 23 дня назад +6

    Number one radio

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt 23 дня назад +2

    Limpopo station is Station of the moment! I listen every day here in Mozambique.

  • @augustMag
    @augustMag 23 дня назад

    The best I Limpopo FM

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona 23 дня назад +3

    Ineyo mai kaliati ndimamukonda mai olimba mtima zikomo kwambiri ngati akuti zonse ziri bwino .

  • @MilwardChanza-mr4yr
    @MilwardChanza-mr4yr 22 дня назад

    That's better kuti Hon P kaliyati sanakhuzidwe ndi ngozi iliyose satana achite manyazi popular khan zabodza ndipo ndi wolephere.

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge 22 дня назад

    Ndege kumvula munthu jeket tai pakhotsi mmmmmmmh 🙌🙌🙌🙌😢😢😢😢

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 23 дня назад

    True info!!

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r 23 дня назад +2

    Ndimakhurupirira ripompo and bakiri muruzi bas enawa amangokhara kt akhuta mbwanda bad zana romweri atinamiza kt evas mereka wamangidwa chifukwa chanyimbo yomwe anaimba pamariro km guys mmmm ngat mukufuna ku tchuka pezani zina zochita please

  • @fannyzimba149
    @fannyzimba149 23 дня назад +1

    Thanks so much Eeee koma anthu muli pa changu mmmmm koma osamanamizira zinthu ngati zimenezi

  • @janemvubu7750
    @janemvubu7750 23 дня назад +3

    Koma abale timazifu tsa mafutso kuti chachitika ndi chiyani zikomo potiwiza chilungangamo

  • @LeonardMhone-cg1tk
    @LeonardMhone-cg1tk 23 дня назад

    Best radio Malawi never had ❤❤

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v 23 дня назад +1

    That's great

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 23 дня назад

    Thanks for the update comrade

  • @LameckBeharry
    @LameckBeharry 23 дня назад

    My best radio

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 23 дня назад

    Koma anthu muli patchito yopeka mabodza eeeee ai tiziona

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 23 дня назад +2

    It's a propaganda aiming to see if Limpopo is fake or real. Apa ndiye auponda

  • @CeciliaChibwana-lx9dn
    @CeciliaChibwana-lx9dn 23 дня назад

    Best radio ever🙌🙌

  • @ThokozaniMaulana-oi5hz
    @ThokozaniMaulana-oi5hz 23 дня назад

    The whole malawi tikuvela

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 23 дня назад

    More fire Limpopo chilima tidzamulira mpaka kale chakwera ndi Monica Kodi mufalita mukunyasisa dziko

    • @happymughogho5167
      @happymughogho5167 23 дня назад

      DONT PLAY WITH GOD BECAUSE IT IS YOU WHO MAY DIE BEFORE THESE PEOPLE YOU SEEM TO WANT DEAD

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 23 дня назад

    Mayankho abwele poyera me from Kzn ❤❤❤

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 23 дня назад

    Best redio lipompo

  • @JerseyAlfred
    @JerseyAlfred 23 дня назад

    Umakwana ntanyiwa

  • @user-ul1fb4yn5o
    @user-ul1fb4yn5o 23 дня назад

    My radio limpopo fm

  • @RoseChiphiri-ts8jx
    @RoseChiphiri-ts8jx 23 дня назад

    But wy amalawi 😭

  • @davidcainoiss2762
    @davidcainoiss2762 23 дня назад +1

    Viva best TV ever...much love from cape town Western cape

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d 23 дня назад

    N1

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 23 дня назад

    Makwanila boss man

  • @DevisonHala
    @DevisonHala 23 дня назад

    Kodi tikambe kuti tinayiwala bwanji amalawi kuti udf ndi mcp kunali nkhondo tisamale tiuzeni zoona

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 23 дня назад

    Zikomo tayamika kubva kuti Mai Kaliyati ali bhoooo

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 23 дня назад

    Mabodza akutulukawa afunikira kwaoonetsa bwino chifukwatu ine ndikukhulupirira kuti zikhoza kutheka kuti mdani wa a Kaliyati ndi Evance Meleka samene mukumuganizirayo koma alipo wangobisala. Akaliyati ndingowalangiza kuti mdani wanu si MCP ayi mdani wanu ali mkhonde mwanu momwemo

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 23 дня назад

    NDI A MCP AKUNAMATU KOMA IFE TILI NDI CHIDWI KUYANG'ANIRA KUMVA BODZA LA MCP IFE SITIBALALIKA , MAI KALIYATI OSADANKHAWA MULUNGU ALI KUMBALIYANU , ZIWAVUTA OKHA AGALU AMENEWA,

  • @FrankHaruni
    @FrankHaruni 23 дня назад

    Atanyiwa khani ya athu anangwina ku 🇿🇦 dzilipati tiudzen

  • @sharifujoe7633
    @sharifujoe7633 23 дня назад

    Awuseni big and ifa ya chiwaya zitidaiwale also

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 23 дня назад

    Ameeen ndimadabwa,mayesa asnkhidwa ku ministry of mining??

  • @MecyMalothi
    @MecyMalothi 23 дня назад

    Thank u

  • @SlindiryLoveness
    @SlindiryLoveness 23 дня назад

    Ndiye inuyo antanyiwa mukuyankhula za ngozi ya mayi kaliyati koma mukubwelaso ndi za imfa yachilima zikukhuzana pati kungoti nanuso mumatenga ngati ife amalawi ndife zinsilu zoti china chilichonse chimene munganene ndizowona koma nanuso zambiri mumanama mukuziwa eni ake amene mukuwamenyela kampeni ndicho chifukwa chake simunena zabwino zimene likuchita boma mumango nena zoipa zokhazokha zina zamaboza koma muziwe mulungu si james ngati wati boma limene liripo lizalamuliraso or mutanyoze chotani lizalamuliraso chifukwa timawona kuti zina zimene mukunena zambiri ndinu onama

  • @user-ht7vs3dp2u
    @user-ht7vs3dp2u 23 дня назад

    Radio yachoonad ndiyoopa mulungu ndi yopanda chinyengo ndi radio ya Limpopo FM radio osakonda radio iyiyi ndi udasi ndithu

  • @DKMWALE-ew3lp
    @DKMWALE-ew3lp 23 дня назад

    Bola pamenepo eeeesh

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 23 дня назад

    Alemekezeke ambuye atetezele onse atsogoleri a utm

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e 23 дня назад

    Alemekezeke wa kumitamboyo

  • @user-cp4qt9hs8w
    @user-cp4qt9hs8w 23 дня назад

    Nkhan yabwino kwambili

  • @DorisChatenga
    @DorisChatenga 23 дня назад

    Zosakhala bwino

  • @Biath-m4b
    @Biath-m4b 23 дня назад +1

    No1 radio

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc 23 дня назад

    Mcp yagwa ndipo,2025 kulowa boma Lina,koma tiyeni tinene zona, nyumba ya mai ili bwino bwino,za mfuti 400 kulibe nkhani imeneyo.tisiye, propaganda.

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg 23 дня назад

    Great 👍

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r 23 дня назад +1

    Mwachita manyazi ndinu zisilu sgalu i u

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc 23 дня назад +1

    Wise man

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r 23 дня назад

    Anakutulukani anthu pano anaziwa kuti ndinu aboza ndinu zisisilu

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d 23 дня назад +2

      Ngati lipopo imakunyasa usiye kuvela ifeyo timaikonda

    • @GraceZumazuma
      @GraceZumazuma 23 дня назад +2

      Ife full time pompano kumvela pompano daily

    • @LamseyLazarous-dl5qd
      @LamseyLazarous-dl5qd 23 дня назад +1

      Chisilu ndiweyo

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r 23 дня назад

      Ndipo zoona munthu wazeru zake sangatengeke ndi izi or ma comments akewo akuwonekaso kuchepa kwake ineyo sindimalizisaso kumvesela mvuuuuu ndadusa zindichedwesa ndi nthawi yolapa ino osati yomvesela mabozawa

    • @JhdaLifi-vu9sd
      @JhdaLifi-vu9sd 23 дня назад +1

      Ngati munatuluka inu ife mpaka 2063 wooo

  • @user-lk8kj9zv6x
    @user-lk8kj9zv6x 23 дня назад +2

    Allah Akbar ntima unawawa komanso ntima unafooka mulungu awatetezele kuzoipa zilizonse zomwe zikukonzedwa