Ndimakhurupirira ripompo and bakiri muruzi bas enawa amangokhara kt akhuta mbwanda bad zana romweri atinamiza kt evas mereka wamangidwa chifukwa chanyimbo yomwe anaimba pamariro km guys mmmm ngat mukufuna ku tchuka pezani zina zochita please
NDI A MCP AKUNAMATU KOMA IFE TILI NDI CHIDWI KUYANG'ANIRA KUMVA BODZA LA MCP IFE SITIBALALIKA , MAI KALIYATI OSADANKHAWA MULUNGU ALI KUMBALIYANU , ZIWAVUTA OKHA AGALU AMENEWA,
BEST LEDIO LIMPOPO M'MAKWANA 🙏🙏🙏💪💪💪💪💪❤❤❤
Number one radio
Limpopo station is Station of the moment! I listen every day here in Mozambique.
The best I Limpopo FM
Ineyo mai kaliati ndimamukonda mai olimba mtima zikomo kwambiri ngati akuti zonse ziri bwino .
That's better kuti Hon P kaliyati sanakhuzidwe ndi ngozi iliyose satana achite manyazi popular khan zabodza ndipo ndi wolephere.
Ndege kumvula munthu jeket tai pakhotsi mmmmmmmh 🙌🙌🙌🙌😢😢😢😢
True info!!
Ndimakhurupirira ripompo and bakiri muruzi bas enawa amangokhara kt akhuta mbwanda bad zana romweri atinamiza kt evas mereka wamangidwa chifukwa chanyimbo yomwe anaimba pamariro km guys mmmm ngat mukufuna ku tchuka pezani zina zochita please
Thanks so much Eeee koma anthu muli pa changu mmmmm koma osamanamizira zinthu ngati zimenezi
Koma abale timazifu tsa mafutso kuti chachitika ndi chiyani zikomo potiwiza chilungangamo
Best radio Malawi never had ❤❤
That's great
Thanks for the update comrade
My best radio
Koma anthu muli patchito yopeka mabodza eeeee ai tiziona
It's a propaganda aiming to see if Limpopo is fake or real. Apa ndiye auponda
Best radio ever🙌🙌
The whole malawi tikuvela
More fire Limpopo chilima tidzamulira mpaka kale chakwera ndi Monica Kodi mufalita mukunyasisa dziko
DONT PLAY WITH GOD BECAUSE IT IS YOU WHO MAY DIE BEFORE THESE PEOPLE YOU SEEM TO WANT DEAD
Mayankho abwele poyera me from Kzn ❤❤❤
Best redio lipompo
Umakwana ntanyiwa
My radio limpopo fm
But wy amalawi 😭
Viva best TV ever...much love from cape town Western cape
N1
Makwanila boss man
Kodi tikambe kuti tinayiwala bwanji amalawi kuti udf ndi mcp kunali nkhondo tisamale tiuzeni zoona
Zikomo tayamika kubva kuti Mai Kaliyati ali bhoooo
Mabodza akutulukawa afunikira kwaoonetsa bwino chifukwatu ine ndikukhulupirira kuti zikhoza kutheka kuti mdani wa a Kaliyati ndi Evance Meleka samene mukumuganizirayo koma alipo wangobisala. Akaliyati ndingowalangiza kuti mdani wanu si MCP ayi mdani wanu ali mkhonde mwanu momwemo
NDI A MCP AKUNAMATU KOMA IFE TILI NDI CHIDWI KUYANG'ANIRA KUMVA BODZA LA MCP IFE SITIBALALIKA , MAI KALIYATI OSADANKHAWA MULUNGU ALI KUMBALIYANU , ZIWAVUTA OKHA AGALU AMENEWA,
Atanyiwa khani ya athu anangwina ku 🇿🇦 dzilipati tiudzen
Awuseni big and ifa ya chiwaya zitidaiwale also
Ameeen ndimadabwa,mayesa asnkhidwa ku ministry of mining??
Thank u
Ndiye inuyo antanyiwa mukuyankhula za ngozi ya mayi kaliyati koma mukubwelaso ndi za imfa yachilima zikukhuzana pati kungoti nanuso mumatenga ngati ife amalawi ndife zinsilu zoti china chilichonse chimene munganene ndizowona koma nanuso zambiri mumanama mukuziwa eni ake amene mukuwamenyela kampeni ndicho chifukwa chake simunena zabwino zimene likuchita boma mumango nena zoipa zokhazokha zina zamaboza koma muziwe mulungu si james ngati wati boma limene liripo lizalamuliraso or mutanyoze chotani lizalamuliraso chifukwa timawona kuti zina zimene mukunena zambiri ndinu onama
Radio yachoonad ndiyoopa mulungu ndi yopanda chinyengo ndi radio ya Limpopo FM radio osakonda radio iyiyi ndi udasi ndithu
Bola pamenepo eeeesh
Alemekezeke ambuye atetezele onse atsogoleri a utm
Alemekezeke wa kumitamboyo
Nkhan yabwino kwambili
Zosakhala bwino
No1 radio
Mcp yagwa ndipo,2025 kulowa boma Lina,koma tiyeni tinene zona, nyumba ya mai ili bwino bwino,za mfuti 400 kulibe nkhani imeneyo.tisiye, propaganda.
Great 👍
Mwachita manyazi ndinu zisilu sgalu i u
Wise man
Anakutulukani anthu pano anaziwa kuti ndinu aboza ndinu zisisilu
Ngati lipopo imakunyasa usiye kuvela ifeyo timaikonda
Ife full time pompano kumvela pompano daily
Chisilu ndiweyo
Ndipo zoona munthu wazeru zake sangatengeke ndi izi or ma comments akewo akuwonekaso kuchepa kwake ineyo sindimalizisaso kumvesela mvuuuuu ndadusa zindichedwesa ndi nthawi yolapa ino osati yomvesela mabozawa
Ngati munatuluka inu ife mpaka 2063 wooo
Allah Akbar ntima unawawa komanso ntima unafooka mulungu awatetezele kuzoipa zilizonse zomwe zikukonzedwa