Inuyo simunawauze bwanji amzanuwo kuti asakwele ndege coz kuli chivungacho hahahahaha nde tsopano mwayamba kutsutsana ndi Michael Usi? Mmesa Chilima amati ayamba kuyimba bell tsopano
Crook ya munthu iyi ngati pali ma minister anaba ndrama za boma she is one of them. She could even use a Government truck to buy goods from Tanzania uyu.
Zakumpoto ndiye musanene Mai ndiboza limenelo amene Azusa mpoto ndi chakwera. Ndiye akuziwa Kuti ku mpoto ndikumalawi not mbuzi inu ndizanu Peter machende anu
Kaliat anakonza mai wochenjera kwambiri Mmalawi muno atapezeka azimai awa awiri kungabvuti zedi umatha Pati i love you❤❤❤❤❤❤❤
Tili nao koma amaopa apasaneni ma boord gurdz 😅😅
Koma Kaliati ndi machine opangila machine anzake 🤗😂
Aaa adatha uyu
Ndi machine zoona
Kaliati wadya ndalama from 2006 thawi ya bingu koma ndalama sikhutika respect madam kaliati proud of you 😂😂😂
Iweyo Patricia kaliat unabwera kuzakhala pa ndale keep it up
Chakwera ndi Kaliati apikitsane pa debate eeeeeeee Chakwera akhoza kudwalatu😂
😂😂😂
Kkkk
PK you deserve to be the president of utm and Malawi nation
As it is, I vouch for mai Kaliti for UTM president. Go for it mama. Obwerawa asatinamize
What a strong woman ever seen . Proud of you keep it up
Never trust politicians onse ndiamozi amangofuna kutiyuza
Exactly. Anthu opusa andalewa ndithu
A utm ndikhalidwelawo lonyoza komwe akuchokera. Pitani kwinako nukayese ngat mtendere uliko. Zisankho simuwinaso agalu.
My brother Salambula mumatiyimilira
❤❤❤❤my name
Akuti CHIKANGAWA😂 siinetuuuu osandisakasaka ai
Manifesto ya UTM akanaikwanitsa ndi Chilima yekha basi no one else
Exactly and I don't trust these people
Mcp boma 2050 woooo
Kape iwe
❤ Unity with love all of Malawian people and activities with faith thanks for every one
Usi better kaliyati....wangowona kunkhala zimayi....
Usi is indeed not amember to UTM. Even ma speech onse amasonyeza ndithu kuti ndi wa mcp. Koma akungofuna chabe kubalalitsa anthu mitu
You are the best mama at UTM
Mama ndinu one
Monga wachinyamata ti vote pati UTM oyeeh
Mama awawa ndikatunduuu
Nsaluzo zituluke kuno ku South. Tikukufunani pa Njamba
Very unforyunate speech
More fire kaliyati
Kabambe wabwera kudzaba UTM. Ma factory ikuyika MCP. osatinamizapo apa. Mwadziwa liti a Kabambe kuti UTM ndichipani chabwino.
Kaliat wa bodza ufuna utinamizepo apa a mtsogoleri wanu nd amene anangoculutsa kulonjeza km osakwanilitsa chakwera my vote
Ur super mama
Akaliyati azinamiza ana ama 2000, mpoto wake uti munamudzutsayo🤣🤣
you just talk too much without principles. Chikagfawa issues will not give you votes rather the truth.
Inuyo simunawauze bwanji amzanuwo kuti asakwele ndege coz kuli chivungacho hahahahaha nde tsopano mwayamba kutsutsana ndi Michael Usi? Mmesa Chilima amati ayamba kuyimba bell tsopano
Tell people what you will do to improve the economy madam provide alternative leadership
Kaliatii umatha iweyo.
Skc anasankha Mai olingalila
Kaliyati anatha anthu anasiya ukukhulupilila
Crook ya munthu iyi ngati pali ma minister anaba ndrama za boma she is one of them. She could even use a Government truck to buy goods from Tanzania uyu.
Nanga osamumanga bwa? Kupusa
@@tingamasi106amangidwa bwanji when oyenera kuchita ntchitoyo are corrupt like any other politician?? Palibe wandale yemwe azatukule dziko la Malawi
😂😂😂😂😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Zakumpoto ndiye musanene Mai ndiboza limenelo amene Azusa mpoto ndi chakwera. Ndiye akuziwa Kuti ku mpoto ndikumalawi not mbuzi inu ndizanu Peter machende anu
SKC RIP
Aaaaaa athila kuwiri inu mesa mumkat tambala nde dzichan idzi hiyaaa dpp boma
Aaaaa Patricia pena umasongoneza zinthu
Akabambewa mulibe mfundo muli ziiii awa ndiye achita kutumidwa
Kabambe chavuta chizungu proboka pro eish limbikilani Chichewa chomwecho basi
Ubwino wake a Malawi anatsekuka maso.
It's up to them to decide in 2025.Talk is cheap.
Ku gender kumakunkharani mama
Mayiwa adayenera kutsogolera chipani utm
Same lies
Koma a kaliati😂😂😂😂😂
Kodi mmesa utm inalindi ma mp 4 okha
Koma kumeneko mwamuminitsa usi wanyaaa manyii
Kkkkkkkkkkkkklkkkk😅😅😅
Koma mukuziwa kuti ena ali ku Israel 🇮🇱 Chipani chanuchii timachikonda apa nde mwanyereratu takutulukani ndinu anyapapi apapa 😢
😂tizasiya katangale according to kabambe,and utm believes him
True
Michael Usi akulakwa zedi ayenela kuchotsedwa
Abiti makandulo yauzimu mukutokota heavy
Iwe ndoomvesa chisoni chikanakhala Kuti mu ndege munali mbale wake am sure sukanalankhula matuzi akoo
Akwen kachaso bibida too much
Fodya wake eeeeiiiishshsh
A before jesus christ 😂😂😂😂
Chonde osavotera Dr chikangawa chonde munthu oipa
Uku nde kung'alulatu
Tamuwuzani usi asiye kunyoza chilima please
A LUTA CONTINUWA koma amalemba A LUTA CONTINUA....
ZIKUNDISANGALASA ZA NFUNDO YA UTM NDITI KU MOÇAMBIQUE NDIE KUATO MAPUTO
Zomwezi zoweta agaluzi mpaka kukondela
UTM moto usi apanika ndi chitseko Yudasi
NDIKUFUNA KUKUWUZANI IZI PLESASE OSAMULOLA MAGANYA KU UTM CHIFUKWA CHOTI MANGANYA SIKUTI NDI WA UTM AI MOWOPA MULUNGU IZI NDIKUNENA MOWOPA MULUNGU AKUFUNA KUKUPUsiTSANI KUTI CHAKWERA apeze mpata wakupha anthu amene ndinu wodalilika ku chipani chanucho komaso mukuwoneratu kuti ndamene anapanga ma pulani wamupha Achilima pamodzi ndi gulu lachakwera nsimukutha kuwona pamenepa nokha manganya ndichitdilu kwambili
Kwabasii
Phavu osatakgwanika nigalu usi
Makaliati zukani pano ndifundo zanu zili bwino
Kabambe ndi zero EQ
Kodi akabambewa adziwa liti kuti UTM ndichipani chokoma?
Namga chilima anaziwa bwanji kut mcp inali ya bho ndale us dirty game
Yongo wayongo anali chipani chanji?
Mcp
Musarore kubwerara kuthiko
True fact asatipusise manganyà
zaziii😂😂😂
Ndinyambo akufuna kukola msomba tikamadzazinfikila madzi afika nkhosi
Zaziiiii numadziwa kuti mukhala pa kaliyala ,ndikumayankhula zoti kudya katatu,komanso fertilizer otchipa,lero mukuti samaimba belo, hahaha malawi wake siwalero,muname zina,izo ayi,anzanu ayendetsa boma movutikira chifukwa cha manifesto anu abodzawo ,shut up ,patricia
Choka iwe ukunyoza Mai Kaliyati Kaliyati akunena zoona otsutsana naye ndi nfiti mwazolowera kupha anthu inu
Ndipo zoona anthu akupha inu...Mukumunyoza kaliati kuti watani zopusa basi mukhara choncho afiti inu