AFORD AKUPEPHA UTM KUTI APANGE ALLIANCE- ZOMWE ZAYANKHULIDWA KU NSOKHANO

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 12 июл 2024

Комментарии • 66

  • @RachelDongolosi
    @RachelDongolosi Месяц назад +7

    Amen 🙏 mawu amphavu Mulungu akutetezeleni azitsogoleli amene mukuimila a Malawi osaopa Mulungu alinafe

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga Месяц назад +3

    MTAMBO kakhaleni kunyumba...tinatopa nanu.AFORD SIYINGAWINE MWANA WAWUPANDU IWE..UMVE ZIMENEZI KOMWE ULIKO

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb 18 дней назад

    Utm udf my vote

  • @WatipaCawinga
    @WatipaCawinga 28 дней назад

    Magufuli wathu kupoto

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 Месяц назад +1

    Vyakuyoghoya vya mtambo ni boza lekha😢😢

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Месяц назад

    That's good l dea God be with you we love you pangani gwilidzano Ife tili pa mbuyo Pano

  • @marthaphiri3600
    @marthaphiri3600 Месяц назад +1

    Join hands with all the opposition parties, gawani mipando molingana campaign wisely win 2025.

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Месяц назад

    Alliance tapanga kale ndi UDF musavutike ❤❤❤❤

  • @RobertGoliat-gt2qh
    @RobertGoliat-gt2qh 28 дней назад

    Iwe Mtambo leka bodza unatiputsitsa padzana kulankhula ngt zamzeru kma sitingakhulupilire munthu ngt iwe

  • @johnussenu2848
    @johnussenu2848 29 дней назад

    Utm and udf boma

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 Месяц назад +1

    UTM ikuyenera ibwerele ku DPP ndipo Ife angoni a ku Ntcheu tili ready kudzawavotera DPP Pamodzi ndi UTM ngati alliance

    • @KikaImran
      @KikaImran Месяц назад

      You re very right. Sindinavoteko and if DPP coraborate with UTM i ll vote for them though am 100% sure that andale ndi oipa onse, they re there for their empty bellies

  • @LuwisKaigwaze-gr6cg
    @LuwisKaigwaze-gr6cg Месяц назад

    Musayembekeze kuti mudzalamulira dziko lino aford

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Месяц назад

    Bomo ylo ❤

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Месяц назад

    Chihana is my vote

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Месяц назад

    Yambani zomwe mukunenazo musanalowe muboma ,kenako Anthu adzakhulupilila Kuti mukufuna kutukula dziko. Anthu Andale inu mumangotizunza,Anthu wovota kumabvutika inu Ana anu akuphunzila kunja

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o Месяц назад

    Munthu oyipisitsa mtima Timothy sitingakumvere

  • @IshmailDukuturu
    @IshmailDukuturu Месяц назад

    Mbuzi iyi Timothy

  • @WanangwaMfune
    @WanangwaMfune 28 дней назад

    Join

  • @PeterPhiri-u7h
    @PeterPhiri-u7h Месяц назад

    MuKufuna alliance mukuopa chani

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e Месяц назад +1

    Amen 🙏

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Месяц назад

    Utm & UDF Boma 2025 ❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 Месяц назад

    Wabodz uyu
    Mumater mukamafun mavot
    Mumakhal ngat anthabwino
    Chilimanso amater
    Chakweranso amater

  • @JumaGadaff
    @JumaGadaff Месяц назад

    Mulungu wamakamu kanthani onse omwe adzunza nzimu wa skc lest in peace ndipo chauta langani ndithu

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Месяц назад

    🫡🫡🫡🫡🫡🫡

  • @Dickies-mk8cd
    @Dickies-mk8cd Месяц назад

    Tiyeni tikavote mwanzeru mcp must go.

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga Месяц назад

    Mtambo NDI MBUZI...mavuto alipo panowa,anyani akulamulira panowa..mesa anawathandizila kukhala pampando ndi iyeyo😂😂

  • @jamessoko9480
    @jamessoko9480 Месяц назад

    Aaaaaaa....,ndimo mukuyowoyela mwa wandyale. Pa mupando khale waka,kujikuzga kwake uko,mwaluwa ivyo mukapangana.

  • @josephgabriel1016
    @josephgabriel1016 Месяц назад +3

    Timothy sangatinamize for the second time.....

  • @ntombiunice8637
    @ntombiunice8637 Месяц назад

    Mtambo ndikhuluku...u minister unamurephera

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel Месяц назад

    Zimenezo2 zithera konko mwene

  • @BwanaGD
    @BwanaGD Месяц назад

    Komatu mtambo munthawi ino ukanankhala chete kaye munalumbwa kwabili nthawi inja ife kukopeka nanu lero munagopita kukamuphetsako chilima inu kumabwerako ndiye muliena nthawi inoyo mukanadenkha kuyamba kulingalira pazomwe munachita aaa

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Месяц назад +1

    I don't trust NTAMBO ,NTambo vuto nngosamudalila Komanso nkovuta kumukhulupilila uyu . Ife aMalawi mukanakhala Ngati Bingu ,mmali ndi munthu wosavuta ,kungomupangila njira ya chakudya basi ,President ameneyo adzakhala WA muyaya. Ngati dziko Lili ndi chakudya ,ma business amayenda BWINO .Koma aaaaa uyuyu ayi mwina

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 Месяц назад

      Ngakhale banja limayenda bwino ngati chakudya chikupezeka. Zovala ndi zina zimaphweka kugula.

  • @user-rg9zc6eo2q
    @user-rg9zc6eo2q Месяц назад

    My vote afod

  • @alickkachepa3801
    @alickkachepa3801 Месяц назад

    Move

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Месяц назад

    Chipani cha UTM chija ayamba kuchikanganirana. Chizungu chake SCRAMBLE FOR UTM. Ena apita kwa Aford, DPP ndipo ena atsala ku MCP. Thats my opinion. You got yours take it or leave it.

  • @user-bv8wo2fn4e
    @user-bv8wo2fn4e Месяц назад +1

    I hope if all mupoto must vote for AFORD

    • @yassinn5634
      @yassinn5634 Месяц назад

      Mtamboyu akunena zoona nthawi Chihana Senior UDF imamunyengerera chifukwa Chihana anali ndi MP ambiri anali ndi mphamvu koma chifukwa chakugawanikana alibenso mphamvu

  • @Syakinongwa
    @Syakinongwa Месяц назад

    Team up and cartel leadership positions within your team. Otherwise forget individual-party leadership as there is no way you can beat MACOPA.

  • @BestonChagala
    @BestonChagala Месяц назад

    Regionalism inamkanika chihana ,you can't win the national presidency without people from other regions.Nthawi zina musanayankhula mudzikhala Kaye pansi nkuuzana kuti kodi izi ndizoyenera kudziyankhula pagulu?Mukuti unduna simukuufuna chonsecho mukudziwa kale kuti simungadzawine u president wa 2025.Ngqkhale iwe mtambo pa ticket ya AFORD sungawine kuchitipa u mp ,nthawi imene munali nduna palibe chomwe munawathandidza anthu aku chitipa

  • @BestonChagala
    @BestonChagala Месяц назад

    Koma a Enock muchenjere ndi mtambo,mugawana zida 2025 isanafike chifukwa aliyense akuyankhula ngati ndi president payekha.Nanga mmene akuyankhulira mtambomo akuyankhula ngati vice president wa chipani ngati?Akudziwa kuti kupatula Ku hrdc sangayambitsenso gulu lina lotchuka paokha,nchifukwa chake asankha AFORD.Akuti safuna mpando chonsecho amayankhula ndi zodiak kuti afuna Udindo ngati platform yoti adzikhala influential

  • @HappyAntenna-sf9qx
    @HappyAntenna-sf9qx Месяц назад

    iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela

  • @user-wk7ut7ld1x
    @user-wk7ut7ld1x Месяц назад

    Mtambo you are Malawian julias malema and your party aford you get 9% of the votes that is my prediction

  • @user-jn9tz3li3v
    @user-jn9tz3li3v Месяц назад

    Mtambo mpaka kumuziwa Mulungu kkkkkkkkk ndale ndizovuta

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h Месяц назад

    Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk

  • @emmanuelsambo1158
    @emmanuelsambo1158 Месяц назад

    It was only SKC

  • @Donnex-gn2sf
    @Donnex-gn2sf Месяц назад +2

    Aford akuwona kuti ku UTM kulibe utsogoleri komabe sizingatheke chifukwa a Aford akufuna mpando and UTM nayo yikufina mpando 🤣🤣🤣🤣

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Месяц назад

      Ife tapanga kale ndi UDF musavutike 😂😂😂😂😂

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h Месяц назад

    Koma chaka chino ziliko ndithu.

  • @MosesNyalugwe-ll8hh
    @MosesNyalugwe-ll8hh Месяц назад

    Maloto achumba

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 Месяц назад

    Kkkkk mtambo sungatunamize adah ndife a utm we are together with DPP

    • @spargomw
      @spargomw Месяц назад

      I agree with you 100%❤❤

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 Месяц назад

    Ili ni lirombo yayi 😂😂😂😂

    • @VungaQueen
      @VungaQueen Месяц назад

      Kkkk😂😂😂😂😂

  • @BestonChagala
    @BestonChagala Месяц назад

    Vuto ndiloti ena pa imfa ya chilima afuna kutchukirapo.Aford yakhala zaka 30 but no progress koma pano they are claiming to be friends of chilima just to capitalise on the direction less supporters of utm.Ku AFORD kuli ndani odziwa ndale kuposa kaliati?And in terms of popularity utm ili pa mwamba kwambiri kuyerekeza ndi AFORD

  • @chrisgremu740
    @chrisgremu740 Месяц назад

    Ndiye Chakwera akawinaso 2025 Mutani?

  • @TiyesNayuma
    @TiyesNayuma Месяц назад

    Chitsilu iweyo you failed as a minister

  • @BrightNyoni-yd4ip
    @BrightNyoni-yd4ip Месяц назад

    Mumakwana a hot 265 watching you from lusaka Zambia twatotela sana

  • @user-eh1gn1nj9d
    @user-eh1gn1nj9d Месяц назад

    Kodi imfa ya Chilima mukupangira campaign Mulungu akukanthani ndithu

  • @HappyAntenna-sf9qx
    @HappyAntenna-sf9qx Месяц назад

    iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h Месяц назад

    Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk