Mtanyiwa,ben longwe ,boooooon kalindo they are not alone ali ndi ife amalawi ndeno bola mungopanga zokonza ziko osamalimbane ndi anthu mukuganiza kuti anthu angakusiyeni ? PATRICIA NG'OMA AKUCHITISA MANYAZI AZIMAYI ENA satana wamkazi patricia
No any country kuno ku Africa inatukuka popanga mgwilizano ndi United states (the west) ngongole imasaukisa misewu ndizitukuko zonse mzungu samabwera kuzama kuno koma ma Chinese, phindu la ngongole zomwe chakwera skubwereka zikumathera mmayumba mwawo kudalila imf dziko la Malawi silizatukuka
This is my favorite Radio station Limpopo FM. Comrade Ntanyiwa my Home Boy. Long live.❤❤❤
We are here in South Africa Mr Ntanyiwa anything happen let's us know we are also dealing with guns 😂😂
Limpopo more fire
Perfect ❤❤. Nkhanga zaona
Mmatiimilila a bon kalindo more fire
Limpopo more fire kt buuu
Big up always, Big man !!
Mtanyiwa,ben longwe ,boooooon kalindo they are not alone ali ndi ife amalawi ndeno bola mungopanga zokonza ziko osamalimbane ndi anthu mukuganiza kuti anthu angakusiyeni ?
PATRICIA NG'OMA AKUCHITISA MANYAZI AZIMAYI ENA satana wamkazi patricia
Koma Hii, Haa, Bon wabwelako.❤❤❤❤
Mumatiimirila aborn kalindo more fire
You're most welcome brother man!!
LIMPOPO FM morefire
Am happy today
Good channel umakwana Kumuledi Mtanyuwa
❤❤❤mumakwana ❤❤❤❤❤❤❤kkkkkkkkkkk
More 🔥🔥🔥🔥 Comrade and Limpopo FM, kuswakuswa, nkhanga zaona, Thank you so much for the beautiful information
Koma lipompo imeneyi inalikut??
Tilinanu Bos
Kkkk koma tanyiwa mau ndilibe ayaluse zenizeni
Tamuuzeni ngomayo apange changu kutumiza anthuwo awone zimene tiwapange kuno akuona ngati kuno kujohn timasangalalanako abwele azatipeza kuno komanso adziwe kuti ayika moyo wazibaleawowo kuno pachiswe chifukwa abale anuwo anthu akuwadziwa samala ngoma
Amatiyimilira boni ndi mlipopo kunena zowona
Ambuye akut menyela nkhondo Malawi
Tangomuchotsani Chakwera yo basi
Zavuta pamalawi anthu aphana kkkk😂😂😂😂
Dzana umati vp ndi wakusanje ukungosemphana nazo ndieno kuzitsutsa kt ndiwe wabodza sukwanisa kuzisusa kut sorry?
Zabwino zose
Ndipo dziko lanthu kunakakhala anthu olimba mtima ngati inu bwenzi lili lokoma koma mikango inayi iiiiiiii ititha
MCP Muli zingawenga zokhazokha mumalo mokoza dziko Muli busy kusaka anthu Kuti muziwampha za chisoni shame on you MCP ndi boma lanu la zingawenga 😭😭😭
Kkkkkkk 🔥 😅
Iwe wabuyi buyi usayaluse chimbedzo ndi nfiti nzako chakwera
Koma eeeeeekuli zithu
Antanyiwa zoti muzazolaso paint pasonkhano wa dpp iwalan muzingolubwa bas😂😂😂😂😂
Why not skip his post to avoid your chest pain
😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅
Kkkkkkkkkkk Eeeeee ANTANYWA ndakomoka ambuye akudaliseni
Dzavuta
Kwavuta ku statehouse 😂😂😂
Bon kalindo ndi dolo koma chakwera ndi kape chinthu chonyatsa Lazarus
akat ii aa born watuluka 😂😂😂
Mumakwana a bon kalindo
Ndale chinkhala kuti saphatikiza ndi satanic bwenzi ambiri atasiya bcs athuwa akuyaluka eeeeeee
Limpopo more fare mumatimvesa kukoma
Mall fare Limpopo
I gave up
No any country kuno ku Africa inatukuka popanga mgwilizano ndi United states (the west) ngongole imasaukisa misewu ndizitukuko zonse mzungu samabwera kuzama kuno koma ma Chinese, phindu la ngongole zomwe chakwera skubwereka zikumathera mmayumba mwawo kudalila imf dziko la Malawi silizatukuka
Nkhangaaaaaaaàaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaasaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaàaaaaaaaaaaassssaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaàaaaaaaazaoooooooooooooooooooooooo oooooooooooooooooooooooona mulibwanji Malawi kulikonse kumene muli Lelo pa 20 MCP musamale mudzayenada uyo uyo mukuna mudzayenada uyo mademo sitisiya tinakapanga mademo sitisiya tinakapanga president wathu osauka munyengo ino watuluka Mademo tinakapanga mademo sitisiya tinakapanga mademo sitisiya tinakapanga tinakapita Ku state house modemo
😳😳🦃🦃🦃🦃🦃🦃