Mai inuyo musazafe....ndipo..musazasowe...Ambuye Apitilize kukupasani...mtima wa Chifundo......okonda Amalawi...Azanu ndipo ife... business tinaduka....kare kare kma..pano.tili ndi Chikhulupiliro kuti sikulina..dzuwa liwaraso... Ambuye Akudalitseni....mai..🙏💪
Maonekedwe anu akusikimizila chomwe inu muli..Pokhala Hon koma nkumaonela mwa naturally as if mulibe khobili sichinthu chophweka iyo ndi mbali imodz yomwe ikukamba za kuzichepesa kwanu.....Muzilimbikila kupemphela musalowese ajuju mu machitachita anu..may the good Lord bless youmy dear sister
May navitcha muli ndi fundo zabwino kwambiri ndpo mulungu apitilixe kukupasan moyo wawutali ndpo muzatilamulila muzakhla presidential presidential president waziko la malawi love you mom❤❤
Mayi Navitcha,am very impressed with ur back ground and what it has taken you to be where u are,thanks for the Education foundation u instituted and it has worked and its working for that Child coming from that poor family,May God bless you and continue helping the Less privileged
Nkhaniyi ndiyoona. Adaliyekha kwathu ku Nsanje North. Udzudzu wakwathu sadauope mayi ameneyu. Moti ine ndimadabwa mpaka pano kuti kodi u leader of opposition uja adamulandiranji? Mulungu adampasa mphatso ya utsogoleri mkazi ameneyu. Umboni wina ndi umenewu woti pakanthawi kochepa adabebetsa u Leader of opposition.
Ndizoona Peter Wamuthalika his a good President koma kunena zoona munthu uja wakula kwambiri his 85 nde alamulire zaka 5 azakhala ndi 90 pamenepo ndekuti sitili serious a Malawi ngati 2017 to 2019 amangogona mpakana kumalamulidwa ndi bodyguard Bambo a Chisale mpakana kutisakhila Bwana Chimulirenji kutathauza kutha kwa nzeru akanapeleka udindo kwa munthu wachichepere ndikumamupanga guide, zithu momwe zikuyendera panopa padziko lapansi khalamba ngati imeneyo singakwanitse tiyeni tikonde dziko lathu a Malawi
@@AlfredMatthew-v4h Pali zoyakhula zina aziyamba aganiza polakhula chifukwa palibe amene sakuziwa chilungamo ndiposo Palibe sogoleri angakomele aliyese iwo ali ndi anthu owasata basi athandize iwo azawoso ali ndi anthu owathandiza ndiposo ubwino wake zipani zonse zidakhalapo ku opposition
Dzikomo my sister u b next president in malawi your future in my country god bless you
Miyimaso achemwali mumatiyi milira ndizowona tikudziwa andifuse ife ndizowona timapita ku school limozi ndimawona taphuzilalimozi mukunena zowona chitukuko tikuchiwona pantambanyama kuchoka phungu thoyolo thava zowonadi
Wishing you all the best for the position you are hoping for and am seriously praying for you mama
Love you dpp love you mom
Blessed woman of grace
Apm my vote 🗳
More fire
Hon Mary Navitcha kms Hon Sameer Suleiman ndi akatundu ku DPP ndipo ndi omwe akulimbitsa Chipani chathu chokondwa 🔥💙💙
Mau
I agree
God bless marry and dpp
Stay blessed mother
PAM my vote❤❤❤❤
Mai inuyo musazafe....ndipo..musazasowe...Ambuye Apitilize kukupasani...mtima wa Chifundo......okonda Amalawi...Azanu ndipo ife... business tinaduka....kare kare kma..pano.tili ndi Chikhulupiliro kuti sikulina..dzuwa liwaraso... Ambuye Akudalitseni....mai..🙏💪
Long live madam Mary Navitcha
Maonekedwe anu akusikimizila chomwe inu muli..Pokhala Hon koma nkumaonela mwa naturally as if mulibe khobili sichinthu chophweka iyo ndi mbali imodz yomwe ikukamba za kuzichepesa kwanu.....Muzilimbikila kupemphela musalowese ajuju mu machitachita anu..may the good Lord bless youmy dear sister
My model
may Mary navitcha mumakwana mam Mulungu akudaliseni APM my vote
So powerful
Mary Navicha woyeee
Mary Navitcha Woyeeeee❤❤❤
Chiphadzuwa❤❤❤❤
Dpp 💙💙✊ my vote 💙
Mama limbikani campaign mwamphanva.. ndimachikonda chipani chabwino.
❤❤❤❤
Nanunso2 inu amakosana ujeni yanu ndiyopoira kwambiri chifukwa ikumaduka duka conzani Studio yanu kuti idzimveka bwino
Amayi navicha mukunena zoona olo nkhope yanu ikuwoneka simunapange chibwana pitilizani ndipo dpp musayisiye.
Umakwana zofunikaa zimenezo
❤❤❤❤ my opinion
🎉❤
May navitcha muli ndi fundo zabwino kwambiri ndpo mulungu apitilixe kukupasan moyo wawutali ndpo muzatilamulila muzakhla presidential presidential president waziko la malawi love you mom❤❤
❤❤❤❤❤❤
Eeeeeee uyuyo ndi akatundu si anyapapi ngati kamajekete ndi chikangawa
Tatiphulani inu a dpp, tikuphula njerwa za moto a malawife, tili ku aigupto ifeee
Mayi Navitcha,am very impressed with ur back ground and what it has taken you to be where u are,thanks for the Education foundation u instituted and it has worked and its working for that Child coming from that poor family,May God bless you and continue helping the Less privileged
Powerful 💪
Fitness eeee, ndalama zamuyanjatu. She was cute then now it is a different story.
Finess...
Zoona mama tumikirani dziko ndi chikondi kwa Ali yense Malawi chonde pangani zinthu zokonda Malawi yathu
DPP imangopanga zakumwera bas nde mpovuta kwambiri kuti akumpoto akusapoteni
Koma kuyakhula mosaonjezera mau zimai Ali pa mabvuto kuposa ife abambo mai tiyeni nadzo 2025 tikupasani vote yokwanila mulowe boma
Zoona eneso ndine mboni mumene zinthu zililipano ayi ndithu mavuto afika pa mwana Akana phara panopa chilichose mavuto okhaokha palibe chomwe chikuyenda kukakhara kudya ndi kawiri pa week
I'm in love with her and I wish akanakhala MG2 wanga.
Dpp my vote💌
Mary Navitcha ❤❤❤❤
Nkhaniyi ndiyoona. Adaliyekha kwathu ku Nsanje North. Udzudzu wakwathu sadauope mayi ameneyu. Moti ine ndimadabwa mpaka pano kuti kodi u leader of opposition uja adamulandiranji? Mulungu adampasa mphatso ya utsogoleri mkazi ameneyu. Umboni wina ndi umenewu woti pakanthawi kochepa adabebetsa u Leader of opposition.
My vote Dpp
Welcome mayi
My vote 💙💙💙💙
Mai olimba mtima washing from Lusaka Zambia
Kodi mai Navitcha simungabweleko ku monkey bay kuno choonde?
Mama go to contest pa Vice President
Navitcha Suleiman 2025
Mbambande Asisj,inuyo ndi one
Panu muyambe kumapanga Ma Demo.
Anzanu anatenga ndi Ma Demo ndiye inu mukuti anthu awa angokupatsani Boma?
Kkkkkkkk
You want to come back and put nany people of DPP on Government pay Row . Wayilasha
Mzabwere kwa2 kuno ku Mzimba south east Khosolo mama Navitcha chonde chonde mama. Dpp woyeeee!!!!!!,,,,,voti yanu mdzatenge kuno.
😂😂😂😂 koma anthu simukhala serious, mpaka mayiyu mwati azakhale next president eish
Kukhala nkhalamba sivuto koma nzeru ndizomwe timanena,apeter tu kukalamba sikuti kwabwera lero ai, apeter anatengapo boma 2014 koma amalawi zikoli amalimva kukoma osati zaziiiii tikuziwona lerozi,nyamata wanuyo chakwerayo akupanga chani?nkhalambayotu zitukuko zake taziwona,nanga nyamata wanuyo chakwera wapanga chani?musawapotoze amalawi,amalawi akufuna apm osati chikangawa ai
Amen
Ndipo inuyo mulungu azikudalisani
Sameer Suleman ndi mery navicha ndimakufunani awilinu mulibwino kwambi ndiyimbileni ndikufuna wina akhale president wina VP
❤❤
Yes DPP ikubwelanso basi
Aaaaaaa kod gayz takozani TV yanuyo bwanj kod mubwezatu ndalama ansaaaah
Ndinu mai mbambande mama osililika,komano mukapita ku parliament musakaiwale nkhani yovotela chaunzika yokha pomwe chanzikacho chikuvuta kuti chituluke
Ndizoona Peter Wamuthalika his a good President koma kunena zoona munthu uja wakula kwambiri his 85 nde alamulire zaka 5 azakhala ndi 90 pamenepo ndekuti sitili serious a Malawi ngati 2017 to 2019 amangogona mpakana kumalamulidwa ndi bodyguard Bambo a Chisale mpakana kutisakhila Bwana Chimulirenji kutathauza kutha kwa nzeru akanapeleka udindo kwa munthu wachichepere ndikumamupanga guide, zithu momwe zikuyendera panopa padziko lapansi khalamba ngati imeneyo singakwanitse tiyeni tikonde dziko lathu a Malawi
Nzeru imagonjetsa chilichonse
Navicha mkatundu eshiiii
Mai awa alindimbalume ngati abusa eee🧢🧢🧢🧢
Ndimaikonda DPP ndimoyo wanga onse
ndakunyadirani love you Mami yes
Mayi navitcha ndiolimba mtima ndinawaona nthawi yomwe amqngwirilizira reader of opposition.mayiyu adzaimire u presdent malawi yizasinthqtu alindimfundo zothandiza malawi
Zoona.madamu
koma nafeso tikukufunani amayi ndingakupezeni bwanji mayi inu mzimayi muzathu ndakunyadirani
Mulungu salephera amai APM Bomaaaaaaa
sikonoyo mutu wake unataya kare ameneyo kuguritsa friend wake rero akunjoya chisiru ameneyo kufera vp
Nazoni mayi osafooka apm endanayeni
zofunika mama
ADAD woye, 2025
Nthwawi imene munali m,boma sumunkadziwa kuti azimai apolisi aphunzitsi salandila ndalamazokwana mwadziwa lelo mukunamatu nthwawi yatsalai ndiya UTM osati dpp
My vote
Mukapeza mpata munvereko nyimbo ya muchedwa ya kell Kay ija mwanva
muzikumbukilatu chomwe chinatulutsa Dpp boma 2019.timayikondatu Dpp koma mukasamale kukomveshoni osakasakhaso adad ayi zimenezo ife sitikufuna
Ukunama akamusakhe apm
Peter, Boma Boma Boma❤❤❤❤
Dpp ndi chipani chamadolo
Kkkkkkkkkk
DPP ayi ayi ayi ayi
Kkkkkkkkkkk
Mama inuyo mukukwana
Mbambande inuyo
Koditu ammalawi wake ndi nchewa,achewa ndi mbuzi
Inde nchipululu simofela awuzeni
Mulungu adzikudalitsani
Kutopa ndi zaka four nanga zaka 25 zapitazi simmatipa bwanji pot munali pa chinyezi eti
Za bwino zonse Mai navisha iwe mbambande
Zidakukanikani kale inu pano musatipusitse ingopangani masters yo basi osati muzitilongolora ife
Boma libwelera 2025 asiyeni achina sikonowo tizaonana
Km zonsezo zochokela kubanja losaukazo zisiyeni ilolo ndedziko km masopatsogolo aliyense alimbili yakeyake
My vote
Ukati uchisilu ukutanthauza chani
Mapoliticians ofoira mumati Boma lisiye kupeleka ngongole Kwa anthu kudikira Inu??? Mulibe mnzeru vuto Malawi muno si usogoleri Ayi.Koma stragety mmene mumapangira M'Boma zinthu.Mungonena kuti muzapitiliza kuononga pamene munalekezera
Wasowa zokambaso nawe khala chete usatukanise mafupa
@@FortunePhiri-kl7oe ukhalira ndale zomwezo
Very weak lady,
Uchisilu ndiye mumafuna kuti asiye kupereka ngongoleyo chifukwa cha inu bwanji osamapanga zanu bwanji
No matter what respect your mother kutukwanaku sizingathandize
@@AlfredMatthew-v4h Pali zoyakhula zina aziyamba aganiza polakhula chifukwa palibe amene sakuziwa chilungamo ndiposo Palibe sogoleri angakomele aliyese iwo ali ndi anthu owasata basi athandize iwo azawoso ali ndi anthu owathandiza ndiposo ubwino wake zipani zonse zidakhalapo ku opposition
Ngongole apatsa anthu angat???or 2000 aangakwane Malawi yonse...mmalo mopanga ncthito mkuwalemba
@@clashftm369ndpo ayamba liti kupeleka ngongolezo kkkk anthu saziwa zomwe akuyankhura zomwe ankapanga adpp amatha n chakwera anakati azisatira za chilima bwenzi akupanga zokomera amalawi koma kusamvetsesana ndzo palibe akupangapo
wa chikangawa ndakuona😂😂😂😂😂😂
Malawi yadzuka.dzikomo a mayi.
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
❤❤❤❤❤❤❤
❤❤❤❤❤
❤❤❤❤❤❤❤