on my way going to the shop kukagula mowa kut ndiufile y annabera amandipwetekesa mutu heve any question from joab chakhaza kumangot malamulo athu sakulora relo alikut 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Milandu yaku Malawi ikukhala bwanji this my first kumva kuti muthu wamangidwa kamba koti amafuna kuphwanya lamulo 😊 ma judge mulipo koma where did you get this power mudziwaletsako a mcp kuti malamulo anu samatelo👣🔊
Kungopanga zoti ena azidziwe basi ❤❤❤
Is good nice now Zikom mulungu asikudalisapo chakwera achoke 2025
Very good every body must register inorder to exercise his or her to vote.
Ili ndi dziko la Mulungu zikomo Ambuye ndinu Mokha mumakhala ndi mayankho anthu anu a Malawi ❤❤❤
Kma yesu ameneyu aaaaa watimenyera nkhondo ife tili chete
Amen nthawi ija yakwana yochoka pa pando Mr chikangawa wagwa nayo keasala nkumapita ku Court every week ya 2025 nyiiii
Amen mwatimenyele nkhondo ife tli chete chi satanacho chichite manyazi
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Democracy woyeee Mizimu ya anthu 9 aja uwuse mumtendere not forgetting Ralph Kasambala ,chonde timenyereni nkondo ,
Amen ambuye zikomo mwatiyakha pepho lanthu
Amen kumwamba kuli mulungu
Hallelujah 🖐️🖐️🖐️🖐️🖐️🖐️🙏🙏🙏
Mayi Joyce banda amamupotsa chalakwe poganiza.
UTM vote yangaaaaaa
Osaopa amalawi dzikoli ndilathu
Khoti layamba kuopa lawyer uja kuti awaulula
😂😂😂😂
Passports and driving licences belong to the government please.
The smoldering charcal👐👐👐
Kodi ndingalipeze kuti Buku la smoldering Charcoal 😂😂😂, nchere, Bota aaaaa you just reminding me in those good old days
@@JustinLipipa Tafufuzani mma book-shop Blantyre ko
Ambuye musasiile pomwepa chonde tioneni ife ana anu
Wagwa nayo Anabel izoooo usova 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Mulungu sichakwela kapene chimwendo ayi dzikoli ndilamuthu Wina aliye sidzimene amafuna makape enawa
Mulungu mutiyankhe tilimuwulamulilo asatana mcp yikutizuza amalawi
Chakwela ndi mbuzi yopanda zelu
Murungu aremekezeke ndizo timafuna zimenez
Aleluya
Zochitika kuno ku malawi ndingoti Dzuka MALAWI
Amen
MULUNGU SI JEMUSI!!!!!! KUMENYA KUGWETSA BASI
An assessment need to be done on condition known as dyslexia
Nkhani, yabwino kwa amalawi okonda ziko lawo salute
Zoona masten
❤❤❤❤yaah
Chilima musagone mwachangu paka tizavote chifukwa tizasowa zimu wanu pathawi yovota chakwela mazi basi
Mcp ija pa ulendo basi ma plan anu aduka,
Smartmatic isagwiritsidwe ntchito
Ameen
Nkhani kma imeneyo
Wagwa nayo.ndani
Chiletso sichintheke
Apa mudzi onse wakwathu tikavota basni kkkkk Moto kuti buuuui
MCP yomwe ikulamula panoyi ndi yomwe ijayi ya ku Ghana ya kamuzu banda.Chakwerayu wangokhalapo ngati chukwangwani chabe.🐊🐊🐊🐊🤦🤦
Atsogoleli athu simuchita manyadzi ponamiza anthu awo.
Ndipo watsalanso nzimai uja mtali manja atule pasi usindo hule ameneyo
Tili komweko bas 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Ndubwera lne ndzarembetse lme
Wina alira chaka chake nchino
Hahahah izi ndazikonda, odi nkalembese ine
Kumwamba kulandire ulemu
Vuto ndi kaphunzisidwe sikali bwino.
Ambuye tipatseni munthu ozatiimila 2025 popeza munthu tilibe
Kuyambila inuyo.
I can forsee the Rise and Fall of Eid Amin part 2, ahead 😅
Sono Za smartmatic zija zilipat guys 🤔
Ndipo live
Tikavota bas🤣
Ndazkonda zimenez
Pamenepa zili bwino kwambiri
Wina alila kkkk😂😂😂😂😂
Tipatseni ife chakudya chathu chalelo
on my way going to the shop kukagula mowa kut ndiufile y annabera amandipwetekesa mutu heve any question from joab chakhaza kumangot malamulo athu sakulora relo alikut 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Ali mmadzi ameneyo 😂😂😂😂😂😂
❤❤
😂😂😂😂mbuzi za amalawi.....
How do you recognise the citizen without ID.....
MCP inawina musavutike....
The entire mec is MCP family
Apa ndye zilibwino tsopano
This woman has lost her senses Joyce
Agwa nao akanganya amenewa
Nkhani yabwino kwambili
Indendizona
Zopusa basi makape inu
MEC chair finally defeated
CHITSIRU CHIJA CHI TONKHWE-TONKHWE
@@Kabwilachikangawakkkkkkkkkk 😂😂😂😂😂😂🎉
Koma kumeneko 😅😅😅😅
God and God alone😅😅😅
Kumwamba kudyele nyama
Moto kuti buuuu
Nthawani tidusa inu
Dusani bwana 😂
Hluuuuuuu ulemu wanu dutsani😂😂😂😂😂😂😂
Zilibwino
Milandu yaku Malawi ikukhala bwanji this my first kumva kuti muthu wamangidwa kamba koti amafuna kuphwanya lamulo 😊 ma judge mulipo koma where did you get this power mudziwaletsako a mcp kuti malamulo anu samatelo👣🔊
Deal
Tikavota 😂😂
Anabel 😂😂😂😂😂😂😂 dweku
Ndetika votela ndani umuvotela akusowa osewa zaozimozi
Iwe sukuona, sukumwa , kapena political blindness
Political blindness