Размер видео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показать панель управления
Автовоспроизведение
Автоповтор
Akuti mulanduwake amafuna kupha ndani? Khalani serious guys kodi amene anapha nzake ndi ndani?. Ndiolose ndikakutafune #TRAESON mugwadi ndi bp chaka chino
More 🔥 a Malawi tisafooke mpaka chilungamo chioneke
The country has really changed mulungu chitaniponi kanthu
Utm my vote osaopa osafoka osatopa anyani a mcp anthu ankhaza chipani chakupha
Boma Ili tinaliyika tonkha tichotsaso tonkha Chaka cha mawa
Bravo UTM and UDF Aford. God Bless
Yeah Ralph
Sukunama Raphael........🔥🔥🔥🔥🔥
Km raster uyoyo Ali nd confidence 😊atha kuthibura koopsa
Kodo apolice amathamangila kuponya utsikamba ka chani koma anyani awawaaa?
Apolice anthu ndiatinke nawo ngakhale mumange wanthu chikangawa sakupatsani kalikonse Apolice mukhangati sinu anthu nanu muvutika tidzikumenyani mamidzimu muzolowela zomamanga anthu dziko ndilanthu sikuti mukavala uniform tidzikuwopani sitikuchita mantha
The dc🔥🔥🔥❤️❤️
Dzikoli ena azimangidwa ena ayi chonsecho onse alakwa sizoona, aliyense akaphwanya lamulo azimangidwa
Ine ndimafuna nditatero km vuto ndikibe lawyer komanso kabunthabuya
Chakwera ndi mbuzi yamuthu muthu oyipa kwambili ngati idya amin koma thawi yake yasara pang'ono basi atuluke
Zoonadi the DC ifeyotu timakunyadilani
Ngati apolisi akuphulisa usi munseu amalawi pitani mukhaphulise usi ma office am.boma
Wanted woman can not be in custody for long time, which means can happen something
Muthamangitsa bwanji anthuwa pomwe akufuna amvere mtsogoleri wao ndipo sakupanga ma demo ayi,
Lilongwe wake uti wavutayo.aa.omwewo osowa zochitawo ndamene ali wekaweka.atoziwana.Lilongwe business usual.
Osaopa osafowoka osatopa 💪💪
Manganya akuona ngati 2025 azakhabe vice president galu kufupika
UDF igawanikaso pompano 😂😂😂
apolice musatero asiyeni anthu averere milandu mumaziyamba daratu
Osatopa osafowoka osaopa dziko ndi lathu ili a Malawi wo nde ndifeyo nde asatiopseze ngati ndife obwera ayi
Kaliati simunthu wamba aMCP munyera Naye ameneyu kaliati ndi President kale
Mwatizuza kwakwana tsopano muweluzidwa inu a mcp
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
Chakwera anapha chilima bwanji mlandu sakuyakha or kumangidwa a police osamakondera pomangaathu
Koma ndikutha kunvetsetsa, umangotolera zomwe anzako ayika kale
Chakwera amangidwa lit zaimfa yachilima
Imeneyi ndi plan ya Micheal Usi munthu oyipa uyu Manganya
Koma chilima ayi Zikomo kwambiri mulungu analola kuti mupite dziko lidziwe wabwino ndi oipa
Iwe kapolo tazingoyika osati kulankhuliralankhulura. Ukalemba zakwana basi
Dpp bwanji sinabwele kumeneku?😊
Chifukwa cha ndale akaliat sanalakwe
Koma Mulungu sangalole kut athu ake azivutika chifukwa cha M C P Mulungu akatha Chakwela posachedwa a Malawi khulupililani pepani a Mai Kaliati
Nthawi imene chilima ali moyo adamangidwa izi kudalibe tinene kuti zikuchitika chifukwa chani
Kodi ndekuti ndi one party system
osaopa osafowoka osatopa💪💪💪💪
Let's go DC more fire
Ukanenetsa kwambiri akutengeta ku chikangawa ohooooh
Khaza
Nanu muziponya khuni za Moto ayake amenewo omawaopa athu amenewo
Osatopa osaopa osafooka
Nkukuyu sakumumanga bwanji,,,,
Dziko ndi anthu ake
Osaopa osafoka mpak chimbaz adyacho asaze
More 🔥🔥🔥 DC
Mkutaya nthawi
Kuipa mtima kotani uku
Aponyeranji tiregus aaaaa
DC wenwen
The dc 🔥❤️
Athireni usiwooo. No future
Aone nyekweeeee!!!!!!!
UTM for life
Osaopa, osafooka n osatopa, it's fight for real democracy as real nation don't fear anyone just fear i will fight for and de reality will set Patricia kalita will set her free in Jesus name
Moto kuti booooooo😂😂😂😂😂😂🎉
Kwaola hvy
Osaopa, osafoka,osatopa
Koma pamene mwayima apo ndipa chitukuko Cha chakwera misewu yikubeba
Iwe chakwera wakokoyo ali ndi ndalama zomangire nsewu wasowa zokamba eti
Misonkho sindalama zachakwera wakoyo galu ngat amenei
Koma dziko lanthu likupita kuti esh
Kkk latchena kwambiri het? 😂
Sizona
Moto buuuu
DPP Kodi sonabweleko lelo
Mwina apita kukavelera mulandu wa ku mec paja amati chigamulo chiliko lero
Aliko,,achina sulemani
apapa ma demo ndiye ayamba mpaka pa 30 OSAOPA💪Alunta Continua 💪 (SKC💔)
Foseki
Anthu mukusowa zochita et 😂😂😂
Iwe uli nazo zoopha anthu
Osaopa osafooka osatopa
Akuti mulanduwake amafuna kupha ndani? Khalani serious guys kodi amene anapha nzake ndi ndani?. Ndiolose ndikakutafune #TRAESON mugwadi ndi bp chaka chino
More 🔥 a Malawi tisafooke mpaka chilungamo chioneke
The country has really changed mulungu chitaniponi kanthu
Utm my vote osaopa osafoka osatopa anyani a mcp anthu ankhaza chipani chakupha
Boma Ili tinaliyika tonkha tichotsaso tonkha Chaka cha mawa
Bravo UTM and UDF Aford. God Bless
Yeah Ralph
Sukunama Raphael........🔥🔥🔥🔥🔥
Km raster uyoyo Ali nd confidence 😊atha kuthibura koopsa
Kodo apolice amathamangila kuponya utsikamba ka chani koma anyani awawaaa?
Apolice anthu ndiatinke nawo ngakhale mumange wanthu chikangawa sakupatsani kalikonse Apolice mukhangati sinu anthu nanu muvutika tidzikumenyani mamidzimu muzolowela zomamanga anthu dziko ndilanthu sikuti mukavala uniform tidzikuwopani sitikuchita mantha
The dc🔥🔥🔥❤️❤️
Dzikoli ena azimangidwa ena ayi chonsecho onse alakwa sizoona, aliyense akaphwanya lamulo azimangidwa
Ine ndimafuna nditatero km vuto ndikibe lawyer komanso kabunthabuya
Chakwera ndi mbuzi yamuthu muthu oyipa kwambili ngati idya amin koma thawi yake yasara pang'ono basi atuluke
Zoonadi the DC ifeyotu timakunyadilani
Ngati apolisi akuphulisa usi munseu amalawi pitani mukhaphulise usi ma office am.boma
Wanted woman can not be in custody for long time, which means can happen something
Muthamangitsa bwanji anthuwa pomwe akufuna amvere mtsogoleri wao ndipo sakupanga ma demo ayi,
Lilongwe wake uti wavutayo.aa.omwewo osowa zochitawo ndamene ali wekaweka.atoziwana.Lilongwe business usual.
Osaopa osafowoka osatopa 💪💪
Manganya akuona ngati 2025 azakhabe vice president galu kufupika
UDF igawanikaso pompano 😂😂😂
apolice musatero asiyeni anthu averere milandu mumaziyamba daratu
Osatopa osafowoka osaopa dziko ndi lathu ili a Malawi wo nde ndifeyo nde asatiopseze ngati ndife obwera ayi
Kaliati simunthu wamba aMCP munyera Naye ameneyu kaliati ndi President kale
Mwatizuza kwakwana tsopano muweluzidwa inu a mcp
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
Chakwera anapha chilima bwanji mlandu sakuyakha or kumangidwa a police osamakondera pomangaathu
Koma ndikutha kunvetsetsa, umangotolera zomwe anzako ayika kale
Chakwera amangidwa lit zaimfa yachilima
Imeneyi ndi plan ya Micheal Usi munthu oyipa uyu Manganya
Koma chilima ayi Zikomo kwambiri mulungu analola kuti mupite dziko lidziwe wabwino ndi oipa
Iwe kapolo tazingoyika osati kulankhuliralankhulura. Ukalemba zakwana basi
Dpp bwanji sinabwele kumeneku?😊
Chifukwa cha ndale akaliat sanalakwe
Koma Mulungu sangalole kut athu ake azivutika chifukwa cha M C P Mulungu akatha Chakwela posachedwa a Malawi khulupililani pepani a Mai Kaliati
Nthawi imene chilima ali moyo adamangidwa izi kudalibe tinene kuti zikuchitika chifukwa chani
Kodi ndekuti ndi one party system
osaopa osafowoka osatopa💪💪💪💪
Let's go DC more fire
Ukanenetsa kwambiri akutengeta ku chikangawa ohooooh
Khaza
Nanu muziponya khuni za Moto ayake amenewo omawaopa athu amenewo
Osatopa osaopa osafooka
Nkukuyu sakumumanga bwanji,,,,
Dziko ndi anthu ake
Osaopa osafoka mpak chimbaz adyacho asaze
More 🔥🔥🔥 DC
Mkutaya nthawi
Kuipa mtima kotani uku
Aponyeranji tiregus aaaaa
DC wenwen
The dc 🔥❤️
Athireni usiwooo. No future
Aone nyekweeeee!!!!!!!
UTM for life
Osaopa, osafooka n osatopa, it's fight for real democracy as real nation don't fear anyone just fear i will fight for and de reality will set Patricia kalita will set her free in Jesus name
Moto kuti booooooo😂😂😂😂😂😂🎉
Kwaola hvy
Osaopa, osafoka,osatopa
Koma pamene mwayima apo ndipa chitukuko Cha chakwera misewu yikubeba
Iwe chakwera wakokoyo ali ndi ndalama zomangire nsewu wasowa zokamba eti
Misonkho sindalama zachakwera wakoyo galu ngat amenei
Koma dziko lanthu likupita kuti esh
Kkk latchena kwambiri het? 😂
Sizona
Moto buuuu
DPP Kodi sonabweleko lelo
Mwina apita kukavelera mulandu wa ku mec paja amati chigamulo chiliko lero
Aliko,,achina sulemani
apapa ma demo ndiye ayamba mpaka pa 30 OSAOPA💪
Alunta Continua 💪
(SKC💔)
Foseki
Anthu mukusowa zochita et 😂😂😂
Iwe uli nazo zoopha anthu
Osaopa osafooka osatopa