Akadakumbukira padzana ndi imwewa anawaliwetsa mmboma anagwira ntchito Mai awa ndipo kaya lakwachani akadaganiza mwaumunthu anawina ngati alliance because of these strong people,all the best akweni
Dr usi akudziwapo kathu , why am saying like that, just because adakakhala kuti sakudziwapo kathu ndipo ndidabwa bwezi iwowo ali munthu oyambirila kukaonekela Ku police koma angokhala chete why?
@@LouisKhomani ziikugwilizana chani? Anyozana pantendele so this is a big problem sakuyenela kusungilana nkwiyo koma zingoonetselatu kuti iyeyu usiyu nde driver wa zithuzi
Mwana akalilila nsasi musemele UTM inakana DPP ndigwilizana ndi MCP lelo ndizimenezi chisankho choipa is like a game of Chase u make a long move u face a panishiment akulilila kuusi zitengelepo phunzilo zipani zina tiyeni tizikonda zikolanthu
A stitch intime indeed serves nine ,this is time for all Malawians to take part ,,lets have a concrete decision by showing our deeply concern "demonstration" this is too much
MA plan a wanthu olephera amakhala ngati amenewa😂😂😂 apa mayiyu nde ampatsa MA vote ambiri ku convention, Amanganya ndi Mr chikangawa ndinu Ana pandale ngakhale sindine wa ndale😂😂😂😂ndale izi or mwana wakuwonelelani😂😂😂😂
Inu a utsi , know God first,Mulungu sanakusankhen ,simukwanilitsa mission iliyonse inu ,God has more powerful ,iwe utsi ndiwe amene udapereka chilima kut aphedwe ,ndiwe mfiti oyipa kwambiri,tsoka kwa ana Ako utsi
Ngakhale ine ndale sindimazitsata koma kumangidwa kwa kaliat pa mulandu wa treeson zandikhudza ndimulandu wakulu .koma zonsenzi zikuchitika pazifukwa zandale 😢😢😢koma bola musamuthile poison kumeneko kapena kumupha ku malawi kuyamba genoside srs😢😢
MCP ndi chipani cha nkhaza chokupha ndipo sichingasinthe sichizasintha and this is a fact its just unfortunate that Malawians sachedwa kuiwalira,why putting this party in government after all the athroceties they committed in our own eyes Dr Bakili once said kuvotera mcp ndiye kulozedwa I suppose a malawi analozedwadi ndiye muona mmene chizunzire anthu ndikupha komwe
Usi wationjeza kwambiri usaone ngati sitikudziwa walakhula dzana kwa Azima munawaveka ngati a UTM aja zonena a SG lero kuwapangiraso mulandu and usaone ngati kuti sitidziwa kuti unapanga nawo upo opha Dr Chilima pomatenga nkhani kwa Bwana kumakasiya kwa Dr Chikangawa one day uzatimve kuwawa mphamvu zimenezo zikazatha
Simukudziwa kuti kutero mukupeleka Moral Ku UTM;chifukwatu apolice alibe vuto coz , amangogwira ntchito yomwe atumidwa basi. Ndichifukwa chake a Police omweo mawa adzakumangeni ndiinuyo
If she committed a crime it doesn’t matter what her political stature and power are. Her supporters and Kaliati better hope that the police is lying that it has evidence.
Mulungu akhululukire utsogoleri wa dziko la Malawi. Mulingo womwe umamuyezera mzako Mulungu amagwiritsa ntchito womwewo pa moyo wina uli wonse. So let God intervin.
MCP! MCP! MCP! chonde khalani busy ndi kulongosola Economy yathu Not kukhala busy ndi Kumanga athu ( Iwe Richard Chimwemwe banda uli ndi masiku Owelengeka ndipo Mulungu achite nawe.)
Otchani police yo,mupitenso mmanyumba mwawo muotche nyumba zawo ndikuphanso wana wao Ngati m'mene achitira Wanthu aku Maputo Moçambique, apólice amocambique Ali Ndi Mantha Ndi Wanthu, Ngati MCP ikudalira apólice iphani apolisiwo Ndiye popeza Amalawi Ndi opusa khalani
Mulipambuyo paw pa social media po ? Mapazi Anu munya simunati shupt mayi uyu amayankhula ngati chumba kd bwanji mwana wake ndi nduna aliku china bwanji osamuchotsa kt tidziwe kt awawa akuyankhuladi chilungamo awamange awa fwetseke
Komatu kumangidwa kwa Akweni palib angapindule koma kungotenga minyama achipha bwanji Chi Chakwera chimayenda ndi asilikali 100milliona zaziiiiiiiiii UTM
Utm Lower Shire Youth wing, Ikupempha achinyamata onse kuti mmawa tili ndi mapemphero wopemphelera Hon: Secretary General wathu SKWENI , Kuti ambuye atithandize kt chilungamo chiyende ngati madzi. Wotsogolera ndi Evangelist Donias Kamwana, Wa mpingo wa UNITY IN CHRIST.
MCP is an example of Malawian evil political parties
Exactly mcp is more than evil
Aaa simulidziwa kanthu inu zomanganazi zidayambika kalekale
Mukamapalamula mudzimangidwa kumene , good job Malawi police.
Dr usi akudziwapo kanthu ndipo ndimunthu oopsa muopeni ndi udasi ameniyo afe sitingamusapite ndamene akumenya nkhondo yapamsi ndi MCP
Yes 💯
Eya zimenezo anayankhula kale ntanyiwa izi
Ndipo Live
Kukhale kuyamba kwa zionetsero basi osadkira pa 29 kapena pa 30 ayi, more fire 💪💪
Ndipo live dzuka Malawi dzuka
Mademo ayambe pompano basi
Ife tipita kudimba
Ine kuma demo@@DeveliousMasinja
@@mathewsnachuma8086 eya aliyese pamalo pake
Osawopa osafooka we are together with you almighty God will protect you this plan is for manganya
History ya mcp ndi ya chabe chabe from long time........mziko lawakanika awa ndiye angoganiza zomangomanga anthu ....
🙌🙌
Akufuna kusokoneza UTM Koma MCP Idziwe Kuti thawi ndikachitsilu
Akadakumbukira padzana ndi imwewa anawaliwetsa mmboma anagwira ntchito Mai awa ndipo kaya lakwachani akadaganiza mwaumunthu anawina ngati alliance because of these strong people,all the best akweni
That's true
Amanga bwanj muthu wopanda sifukwa koma sizoona ai izi komano mapulani achakwela ndi manganya akupanga bwino ai.
Ndipo eti inu mmmmm
God is with you Madam Kweni
Dr usi akudziwapo kathu , why am saying like that, just because adakakhala kuti sakudziwapo kathu ndipo ndidabwa bwezi iwowo ali munthu oyambirila kukaonekela Ku police koma angokhala chete why?
Mcp ndiye imeneyi mwina timangonva makolo anthu akamadandaula lelo tizionela tokha
Akamuone chifukwa chani mesa patricia amamunyozaso usi yo
@@LouisKhomani ziikugwilizana chani? Anyozana pantendele so this is a big problem sakuyenela kusungilana nkwiyo koma zingoonetselatu kuti iyeyu usiyu nde driver wa zithuzi
@@SaidSamuden vuto timakomedwa ndimawu osaona m'maso mwawo kuti ndizilombo
More fire UTM. Weniweni wa UTM waoneka lero. Osati ena onama aja... ovala zanyuwani aja
Zimene akupanga M.usi sure aononga chipani please muchotse uyu
Chiyambi chachimwemwe pamoyo wamunthu chimayamba ndimavuto ndipo osafooka zabwino zili mtsogolo
Mwana akalilila nsasi musemele UTM inakana DPP ndigwilizana ndi MCP lelo ndizimenezi chisankho choipa is like a game of Chase u make a long move u face a panishiment akulilila kuusi zitengelepo phunzilo zipani zina tiyeni tizikonda zikolanthu
Karma is real, zofuna izi. Amalawi ntendere sanawufune
Kusamva lero ndi izi
Micle usi ukupanga ndale zopusa tikuziwa kt iwe ndi wa mcp ndipo ukufuna ugulise chipan
Ndikamva nkhani zaku Malawi ndimafila pain kwambiri 😢😢
Like wise bro
Where are u let's do something
We malawians we are very quiet lets take action now
Akungofuna kungosokoneza conversation
Zonsezi akupanga ndi Michael Usi akuziwa kuti palibe angazamuvotere Usi
Don't worry Mamie God is with you all time
MCP sangasithe oro patachedwa bwanji athuwa alindiziwatha zoipa opanda chisoni ndi azawo akweni alakwa chani anyamata anachita kuswa magalimoto Dpp sakuwamanga phakalelo amalawi tilindimafuso ambili
Zonsezi ndi nthira kuwiri maguya ndiyemwe akupangitsa .usamaletu koma.uona Zokhoma walakwanji kaliyatu.
A stitch intime indeed serves nine ,this is time for all Malawians to take part ,,lets have a concrete decision by showing our deeply concern "demonstration" this is too much
Mmmm campaign yose ija UTM , lero zafika pomaphana, kumangana Kodi mwaiwala Ntchito inagwirika ija kuti MCP mupezeke mboma
MA plan a wanthu olephera amakhala ngati amenewa😂😂😂 apa mayiyu nde ampatsa MA vote ambiri ku convention, Amanganya ndi Mr chikangawa ndinu Ana pandale ngakhale sindine wa ndale😂😂😂😂ndale izi or mwana wakuwonelelani😂😂😂😂
More fire 🔥 🔥 Utm
Everything you do, remember, there is tomorrow....
Be very careful...
Kodi a MCP m'malo mothesa njala ndi vuto lakusowa kwa mafuta, muli busy nso kumanga anthu?? Are serious? Kod kutuluka mu alliance ndichifukwa?
Whats wrong she did to arrest her innocent woman this plan it wont work guys
Mayi Kaliati is a threat to the government , mayi Kaliati ndi katundu , chakwera will fail
Chipani choipa ichi , chokhetsa mwazi wa a2 osalakwa... Eeeesh ooh God have mercy with us!
A dikira bwanji 48hrspowamanga ndimayesa Anali at amaliza ma investigation? Tikuyatsirani ma candles
It's too bad kumanga akweni to silence opposition?it's not good
Inu a utsi , know God first,Mulungu sanakusankhen ,simukwanilitsa mission iliyonse inu ,God has more powerful ,iwe utsi ndiwe amene udapereka chilima kut aphedwe ,ndiwe mfiti oyipa kwambiri,tsoka kwa ana Ako utsi
Nde kuti chipani chathu cha utm athuwa chikuwaopya kuesela Mbali zonse kuchifinya ummmmmm 😢😢 amanganya muliko mulungu akuoneni
Ntchito za Usi zayamba kuonekera poyera.
Pochosa Chilima amaganiza ngati athana nayo utm koma azindikila kuti mitu idakalipobe choncho akufunafunabe njila yowamaliza
Ngakhale ine ndale sindimazitsata koma kumangidwa kwa kaliat pa mulandu wa treeson zandikhudza ndimulandu wakulu .koma zonsenzi zikuchitika pazifukwa zandale 😢😢😢koma bola musamuthile poison kumeneko kapena kumupha ku malawi kuyamba genoside srs😢😢
Time is coming when Babylon will fall drastically
Komatu mulingo omwe umamuyezela nzako siku lina anzakuyedza iweyo manganya akuziwapo kanthu
Ausi akudziwapo kathu
Manganya ndi chani? Same boma same Malawi nkhondo ndi mnasi, saulos anaphedwa ndi ma friends
Anthu Ali ndi Mantha ndi UTM. Cholinga chowamangila mayi Kaliati sangafotokoze chifukwa palibe mlandu. Akungofuna kupeleka mantha kuti anthu azikhala ngati nkhosa komanso tikamayenda tidziyenda ngati nkhanu dziko lathu lomwe. Zochititsa manyazi. Ndipo amene wapanga izi mulungu achita naye.
Mwazi wa skc ndi anthu 8 kuchikangawa uyende Malawi yese ndiku zunza onse wochitira choyipa chipani Cha UTM. A usi inu munthu woyipa nkhope ndi mtima womwe munapera chilima adafa pano mwapeleka kaliat inutu ndi dyabulosi
A usi ngatidi Ali dolo osangoyambisa chawo chipani bwanji or kungo joiner MCP yo
M.usi,chakwera,chimwendo,,kunkuyu,ndi Team Yake ndamene adapanga chiwembu kuchikangawa,amaonamgati akaphapha chilima basi sapezekaso wina owasokoneza,komwe kulikulakwisa.achitazi sindaleayi .Akanangovomereza kuti zawavutabasi.
Akulu akulu apa MCP yawonjeza .
Tilinanubmai kaliat sitikusiyani tikaona Inu timakumbukila tsogoleri wathu Dr skc chilima
i'm with you 💗 a.k.a kweni
Michael Usi ndiyemwe adapha nawo Chilima ndiyemwe akupanga izi kuti Mayi Kaliyati amangidwe
🔥 utm osaopa osatopa osafooka muotche police imeneyo.
😢😢 zikufunika ma demonstration izi anyamata ndi anthu wokonda dziko tiyeni tigwilane manja amalawi
MCP ndi chipani cha nkhaza chokupha ndipo sichingasinthe sichizasintha and this is a fact its just unfortunate that Malawians sachedwa kuiwalira,why putting this party in government after all the athroceties they committed in our own eyes Dr Bakili once said kuvotera mcp ndiye kulozedwa I suppose a malawi analozedwadi ndiye muona mmene chizunzire anthu ndikupha komwe
Amene timamangidwafe ndizinyama aliyese azimangidwa basi akalakwa
a Matthews Kabambe ndiye atinso? utolankhani winawu eeesh
MCP you will be rewarded it's very soon
Usi wationjeza kwambiri usaone ngati sitikudziwa walakhula dzana kwa Azima munawaveka ngati a UTM aja zonena a SG lero kuwapangiraso mulandu and usaone ngati kuti sitidziwa kuti unapanga nawo upo opha Dr Chilima pomatenga nkhani kwa Bwana kumakasiya kwa Dr Chikangawa one day uzatimve kuwawa mphamvu zimenezo zikazatha
Tikamatche basi anthu amenewa atitopetsa serious,,usi akusewera yapansi
Simukudziwa kuti kutero mukupeleka Moral Ku UTM;chifukwatu apolice alibe vuto coz , amangogwira ntchito yomwe atumidwa basi. Ndichifukwa chake a Police omweo mawa adzakumangeni ndiinuyo
Osatopa asagonja mai ndimuthu modzi olimba mtima ngati umapita kuleba ndiye muthu ukaope kumenyela ufulu wathu
Yooo my country is finish😢😢😢
If she committed a crime it doesn’t matter what her political stature and power are. Her supporters and Kaliati better hope that the police is lying that it has evidence.
Amalawi tili ndi mvuto chilichose timachilowetsa ndalale muthu akamangidwa samangidwa asanapalamule anatani kumanga akabambe or kambala tisatsogoze ndale iyiyi ndi nkhani ya police asiyeni agwire tchito yawo
Atuluke pompapomano
Usi ndi chakwera wakoyo somewhere you
AMichiel usi ndi chakwera
Mukuputayo ndiye timati
NKHONDO
MWAMVA?
Athu a UTM tinkakuuzani kuti Congress ndi yoipa. Lero ndi izo.
Ndipo ngati simuwamasula amai tiotcha paliament muonatso tatopa nawe chikangawa wakupha iwe😊
Mulungu akhululukire utsogoleri wa dziko la Malawi. Mulingo womwe umamuyezera mzako Mulungu amagwiritsa ntchito womwewo pa moyo wina uli wonse. So let God intervin.
MCP! MCP! MCP! chonde khalani busy ndi kulongosola Economy yathu Not kukhala busy ndi Kumanga athu ( Iwe Richard Chimwemwe banda uli ndi masiku Owelengeka ndipo Mulungu achite nawe.)
Komatu asamuphe please please Ambuye mukhale nafe akweni alakwa chiani abale
Koma tilinanu secretary general
Manganya injunction ya convention yamuvuta
Masiku amathela ku chiseko asiyeni azayaka
Mpana mathews Kabambe.. Kof aliyese ku utm ndi Kabambe eti😂😂😂
Otchani police yo,mupitenso mmanyumba mwawo muotche nyumba zawo ndikuphanso wana wao Ngati m'mene achitira Wanthu aku Maputo Moçambique, apólice amocambique Ali Ndi Mantha Ndi Wanthu, Ngati MCP ikudalira apólice iphani apolisiwo Ndiye popeza Amalawi Ndi opusa khalani
Ku boma kwangodzadza Zitsiru, kuyambira mtsogoleri kufika omutsatira onse zitsiru zokhazokha. Dziko lanji loyenda ngat lilibe Mtsogoleri? Chitukuko mwaona inu mkumanga anthu? Osamamanga misewu bwanji? CONGRESS Chipani cha mbunde zokhazokha
Matthew's kabambe nde uti kape iwe😂
Asazitengele one party azazuzika nazoizi panali azawo pamenepo asayiwale or amanganyawo ngati ili pran yofinaku nthana ndi utm kambaka u vp wawowo azawona polekela ndale zotele zakele kwambili osati pano ndetizizi chilima sana chite kuphedwa milanduyo ayipeza lilti kuti amange nthu lelo mawa kuli meeting yayikulu yachipani akuwopa chani phamvu kuchuluka eti azawona polekela asiyeni
Muthana nokha paja campaign wa tonse alliance munkapangira limodzi
Remember kusunga munthu mokakamiza ndimulandu so why police department akupanga zinthu zachibadzi iiiiii koma moyo ukuwawa
Tinadziyikira dziko lathu pa Moto,,,, MCP ndi yakupha amalawi kuyiwala mwachangu,💔💔
Mulipambuyo paw pa social media po ? Mapazi Anu munya simunati shupt mayi uyu amayankhula ngati chumba kd bwanji mwana wake ndi nduna aliku china bwanji osamuchotsa kt tidziwe kt awawa akuyankhuladi chilungamo awamange awa fwetseke
Chosecho apolisi akuyenda ndisapato yophulika. Dzukani apolisi muyambe kuvhala sapato zabwino!!!
Kodi a Usi apitako ku Police?
Chonde a Usi. Pokhala Presdent wa UTM pitani m'kamuone Secretary wanu.
Mdima umakulirakulira pomwe kunja kukucha. Yehova pitirizani kutsogolera ana wanu mu nyengo zowawitsazi.
Km MCP ikuziwa kuti Malawi ndi ziko la democracy komatu mwala obwezela kuwawa muzalira Anu a mcp
Munthu akalakwila malamulo walakwa basi amayenera kumangidwa Kodi atsogoleli samamangidwa?
Nde bwanji simudamange nduna ija idapezeka ndi ma million ku airport ija bwaa??
Panyopako chakwera pamodzi ndi nonse ku state house
Lero ndakwera transport mtengo double koma agaru awa andikwana za mamina basi, kaya alamulira zaka 1million koma azayakha
Kod inu mukumawona ngat kt tikhala mbuli mpaka lit nikuwuzen ichi anthu andale dxikoli ife nianthu atendele ngat simokufuna kt ku Malawi kuyake moto muwamasule cifukwa zosezi tadxidziwa ifeso nianthu
Kugoluza mcp muli madzi nonse tidzabweza khaza zimenezo😊
Tiyeni kuzioneselo apa zayambika kulingazi ini go konko kuyambalelo mpaka pa 31 owo dairy abon kalindo mumachedwesa masiku zioneselo zayambalelo
Komatu kumangidwa kwa Akweni palib angapindule koma kungotenga minyama achipha bwanji Chi Chakwera chimayenda ndi asilikali 100milliona zaziiiiiiiiii UTM
Amay kaliyati amasuleni sitikuwona chowamangila apa
Koma amalawi tikanaziwa sitikanayika MCP pa mupando this is not freedom guys zimenezi ndi khaza ndithu
A MCP momoti awone mmene zinthu zkuyendera dziko muno ali busy kumanga anthu kumeneko ndkukonza kwa zinthu dziko chibwana achyambachi
Ausi azapitako ku mcp okha ngati akuona ngati athu angamusate walemba madzi
Boma kumalimbana ndi zimai kuyiwala komwe munatulukila 😢😮
Mathews kabambe ndye utiyo
MCP ili ndi mabvuto ocholuka m'malo moti mukonze zithu mukungopitiliza kuipira ipirabe Usi ndichilombo chopha athu yooo