Ndi plan yachikangawa imeneyo ndiyemwe wamuona Kut atha kumupasa bizy thaw ya kampeni ino.amanga bwanji Muthu opanda milandu, zake izo Ife nde boma tikusitha Patt!!?
Politics yo dyetsana Manyi.. .We ready to die for this flag Zachimizi .Lilongwe sewage kwacha down youth struggling...and you want to bring fear to my head...No ! This is not 1993
Anthu a MCP ma plan awo amakhala olephera nthawi zonse adapanga plan ya Chilima anthu adawatulukiranso mwachangu lero apangaso izi anthu awatulukiranso nonse a MCP mulibe m'zeru ndale zanu ndi za anadi nokhanokha
Adziwe akulu ake ati? There is no way MCP can stop Malawians from seeking justice. Awa akupita kumapeto a nthawi yawo. Apa Amalawi taphunzirapo kuti MCP siinasinthe.
Aaaa adzi ndidzimene kaliyati ndi malemu chilima amafuna onena analipo koma kutsamva MCP yoyipa koma kakaka idzi anthu ambili omangidwa pa dzifukwa dziiiii kufuna kuti MCP itsachoke boma koma dzilikotu
Dictatorship ya Chakwera ndi Usi,zabodza zones akufuna ku opyeza opposition,MCP ya bodza,kuba,kupha,kuyambira Kuma 1960s.Ma International Human Rights ,IMF,UN,World Bank ,EU,stop donating to Dictatorship Chakwera who has crippled Malawi and it's citizens,fuel crisis,poverty,no maize ,no fertilizer, and they killed VP Chilima and others,they are abusing Malawians.Free HON Kaliati,HON Navitcha and opposition.
Mayi a Kaliati munakatenga mfiti ku church kuti adzazunze anthu osaoka, onani akumakumangani komanso kumadyanso ena mwa inu. Munatenga zosayenela kuzibweretsa ku dziko.
Iyiyi ndi move akufuna asakayime nawo pa President adziyenda ndi Bello mu thumba... 🙆♀️🙆♀️🙆♀️
Eeeh Koma! There is just too much evil happening in this country. May the Almighty God come to our rescue.
Ine Joseph Mkuziwaduka Osadanda masten Sweet for sweat keep it up
BomA la MCP ,,, mwatasa kwambili... Kufuna kubisa imafa ya SKC
Koma ife nde zatizunga mutu msaname ,zungokhala ngati za ma aged person ndithu kuti mwina akula anthuwa abwelera ku wumwana aaaaah 😊
From Cape Town mitchells plain town centre. Chakwela ukufuna chiyani. Iweyo manganya ndimbuzi yamuthu kwambili ukuziwa kt upule sungatenge ndichingangawa wakoyo
Iyi ndi pulani kuti asaime pa koveshoni ndi Michael usi wagwirizana ndi chikangawa
Zoona akutiopa
Ndi plan yachikangawa imeneyo ndiyemwe wamuona Kut atha kumupasa bizy thaw ya kampeni ino.amanga bwanji Muthu opanda milandu, zake izo Ife nde boma tikusitha Patt!!?
Manganya ameneyo,,mafuta kulibe kummanga munthu wa utm akulira maliro achirima
Never give up pk
Komatu utsi sufuka opanda moto dziko lonseli sangangoma Mayi Kaliyati! Akulu anati kang'oma kolilitsa sikachedwa kung'ambika osangoti poti ndimzimayi koma ngati alakwa afunika akumane m'chigamulo osamangonyoza boma.
Kalindo adanena kale izi ,sizodabwitsa
Kalindo ndi Katundu he never disappoints
Angofuna kuti kweni asapedze ku convention it's like government want to finish U T M. But God is watching.
Koma ndi chani makamaka, God have mercy on us
But why mukumayika zithuzi nkhope yamagazi ngati munthuyo wakhapi propaganda
Our country now is more 𝕎𝕠𝕣𝕤𝕖 𝕥𝕙𝕒𝕟 𝕓𝕖𝕗𝕠𝕣𝕖
Mulungu si James pemphero mulungu amutetezere mai a kweni ndipo mzimu wa chilima uwakanthe anthuwo
Tru,,God z watching,,Mulungu awamenyera Mai kaliati nkhondo Ali cete
Perekani chifukwa chomangira ...kungoti felony...timve zifukwa... felony sichifukwa..mukutisokoneza...
Masiku atha kale awa tionana this coming year, kutha nzeru kwa Boma uku😢😢😢😢
Amawonjeza kma kupanga ndale sanyozana mayi uyu akhale nd displin
Politics yo dyetsana Manyi..
.We ready to die for this flag
Zachimizi
.Lilongwe sewage kwacha down youth struggling...and you want to bring fear to my head...No ! This is not 1993
Muja Paulos amanzunzira osatira Yesu ndi pamene Chikhristu chinafalikira kwambiri.Mungoonjejera mkwiyo wa pa 29 ndi 30 OCTOBER.
History is best teacher koma kusanva anthu
Mayi ameneyu nayeso ndiosokoneza achita bwno kumutapa mesa ndi amene anathandiza bomali kt likhale pa pando eya uliziwe ziko zomwevlimapanga mwina uleka
Ku Malawi timayankhula Chichewa,chitumbuka atinthandauzire mlandu wake timve bwino bwino
Ngat walakwa amangidwe basi bcoz nobody is above the law
Mbuzi yamunthu iwe
@@FanessayassinFanessayassinakuti ngati walakwatu. Nde mukufulumila kutukwana bwa
Ndingoziwa nawwo kuti azukako bwanji amai lero kuchitokolosi,ndadzuka ndi matha zedi😢😢😢,so God help us
Basi manyodza dpp ameneyo lelo adziwona okha kuti boma ndi dpp chipani cha ulemu
Good make it truth on one life
God deliver our beloved country whr r we going
Inka Malawian politics very few women speak out. Kaliati is a voice for women.
Politics in Malawi is cleartivity that dazzles
Manganya akudziwa za kumangidwaku, Mulungu akuona, opposition be careful about
Iri si boma ayi akufuna kuti kumbutsa nthawi ya kamuzu banda from mocambique
Anthu a MCP ma plan awo amakhala olephera nthawi zonse adapanga plan ya Chilima anthu adawatulukiranso mwachangu lero apangaso izi anthu awatulukiranso nonse a MCP mulibe m'zeru ndale zanu ndi za anadi nokhanokha
Michael Usi amadziwa kuti sangakhale president, Akweni for President,we are praying for you Akweni and our country Malawi
Mukamabweretsa nkhani zanuzo timaona ngati mwafufuza nkupeza chimene wamangidwira koma inunso muli mbuli pankhaniyiii moti mkumakasaka mma comments aanthu
Eti eti
Akaliyat amaonjeza kunyonza
Kodi akufuna kumpha athu angati chifukwa chani m dima umadana ndikuujika bas tikufunabe commission of equrery
JESUS JESUS INTERVINE IN THIS SITUATION 😢😢
Mulungu salakwitsa kalikose akuwoneni pokuyikani nose wokhudxidwa pa ifa ya chilima
No good,no rest for the wicked
Bwana Chakwera zomwe akupangazi adzafa ngati mwana ndipo sikale chifukwa pano anthu atopa nazo. Inu muzigona ndithu
Nde mukanangokhala chete osabwera ndi nkhani zossmveka spa mudziyamba mwafufuza kuti anthu adziwe chenicheni
Angofuna kupeza mpata osokoneza nsonkhano waukulu wa UTM pa 17 Nov. 2024
mulungu chonde chonde munarenga malawi ndiinu kodi dziko ra malawi muritetedze kuti anthu anu amene munawarenga akudzuzana okhaokha inu ndi chikondi kodi munarenga ndarama ndiinu chonde chotsani choipa ku malawi ko ngati mvuto ndiifeyo chonde tikhululukireni pomupanga chakwera kuti ariramurire mumava kurira kwa aphawi yakhani mulungu mwadongosoro ranu amen
Tupere ananena komaso phiter adadi wofa athu inu chaka chamawa uphusezo akumfunika tupere uzogoleri wabwino ❤
Ndale zaku Malawi
Boma limeneli ndi loipa kwambili tionetsana 2025
Boma ili ndiloyipa kwambili don't warry amalawi tiligwesa popanopopano Muthu sumaluma Chala chimene chimakudyesa phala
Manganya panga manyazi ulibe umunthu Chocho kumati muzakhale president
MCP yikuopa chisankho ndichifukwa ayamba musokoneza mwapha chilima mwayamba kaliati nikufuna kusokoneza UTM afiti imwe a satanic imwe ba MCP agalu inu from Zambia 🇿🇲
This is what we expected from Mcp with it's president too bad
Ukayenda usasiye mlomo amayiwa amazitenga ngati adzao alibe pakamwa
That's indeed
AMUCHITA BWINO HIM AND CHILIMA AMAYELEKEDWA KUMANYODZA MUNTHALI KA...IN SUPPORT OF CHIKWERA...LERO WADZIWONAH!!!!!!
Akufuna manganya kuti atenge chipani kuti chibwerere ku mcp a kunama tu manganya anthu savoteratu
Uku ndi kuwonjezela nkwiyo wa chikangawa airport.
Timaona ngati muzitifotokozera nokhatu nanga mukuwerenganso zomwe alanda anzanu ku page kwawo Ife tingopita ku page konko kaa
Pora moto
It's normal ngati walakwa amangidwa ndithu. It's not politics but normal.
Chilikwamzako mudzaziona man
Malawi
Wachpka pamaso pa Mulungu Tikuyeñda ndi zeru zathu sitinati.
Boma ili mulibemo democracy
Sanalakwitse adziwe kupeleka ulemu Kwa akulu akhale zaka 3
Adziwe akulu ake ati? There is no way MCP can stop Malawians from seeking justice. Awa akupita kumapeto a nthawi yawo. Apa Amalawi taphunzirapo kuti MCP siinasinthe.
Awa atitha onse😢
Azimai musanamizane zosayenda mbulanda coz mukangoziyalutsako
Zirikotu 🙌
Aaaa adzi ndidzimene kaliyati ndi malemu chilima amafuna onena analipo koma kutsamva MCP yoyipa koma kakaka idzi anthu ambili omangidwa pa dzifukwa dziiiii kufuna kuti MCP itsachoke boma koma dzilikotu
Kunzuza azimayi ndi mavuto akulu kwambili kaliati amatukwana bakili muluzi koma sanammange boma la chakwela ndi lolephela atetezeni azimayi onse nzdiko muno kusaziwa ndale ndi matenda
Strong we stand,free up PK
Mulandu waukulu oponsa wakugwa kwa ndege ?
As MCP tries to kill UTM and entire opposition using Kape manganya,, shame
Malawi is more fire apa ndeeeeeeee zativuta basssss
Ubwino wake bon kalido the dc mwama owooopsa kwambiri ananena kale Ndie sidzachilendo ai chikangawa paty
Akudziwana awa ndi momwe amadyera. Anthu a ndale zawo ndi zimodzi.
Munamutenga nokha Lazalo ku chipiku kuti akhale president wanu lero akumangansoni mukhaula naye Chikangawayo
Awamanga chifukwa Choti anawakana chibwenzi apule,zoona mungamalimbane ndi mzimai mukufuna muzikhala busy kumugwilira kumeneko
Kod tamakambani ndi PK apalamula mulandu waukulu mlandu wake uti felony simulandutu tanenani Mulandu wake
Azimai tiyeni tikayende mbulanda Ku mnsewu zanyanya
Ndi za ndale izi muzingovutika ndinu anthu ovutika, olo kaliyatiyo akuziwa chikuchitika
Mwatero? Mwinadi
Izo ndindare manganya ndichikangawa afuna kuzunza azawo mmalo mosakha njira zotesera mavuto mmalawi muli bize kukorezer mukwiyo amalawi
Can delay Change but cannot deny it.
Azimai boza osayenda maliseche muzangoyaluka musiyen ngat mukuona mavuto gulu lake ndilomweli lomwe linalimhlbikisa zisokonezo nthaw ya pita
Mmmm Kodi a MCP icho wakupenga nivichi
Zonse zikuchitikazi akufuna anthu azikhala busy ndi kuyankhula za Mai kaliyat kufuna kuwayiwalitsa anthu za commission of enquiry
Iwe kayaka tanena chifukwa chomwe mwawamangila sukunena bwanji...iwe ndi mnzako chikangawa matsiku anu awelengedwa mwazitenga ngati ndnu mashasha, daily kukacha tizimva nyasi za MCP ndi chikangawa mmmm mwanyanya😮😮😮😮
Manganya plan akufuna akweni asakayime ku convention 😢
Boma loyendesedwa ndi zigawenga komanso mbava chonchi tikavotere anthu okuti akumanga anthu popanda zifukwa zenizeni
amalawi sisamapange chochi zosezi wapanga ndi usi pofuna kumulepere kuti asamenyere ufulu wa malawi basi tiwuzeni chomwe a mcp mukufuna chencheni
Koma apolice amene mikugwirisidwa ntchito achipan tizaona boma likadzasintha ntchito za mcp ndizimenezo chipani chakupha iweso jezebelo ziwa kt paudindo umenewo uzachokapo
Izi wapanga. Ndi manganya kuti asazaime. Pampando wa upresident pajanso ndi yemwe adampeleka malemu. Chilima.
Nde bwanji mlandu woo sakuwutchula, iziituu khaza akupanga ,kod zonsezi akuchitachi akufuna chani kwenikweni
Dictatorship ya Chakwera ndi Usi,zabodza zones akufuna ku opyeza opposition,MCP ya bodza,kuba,kupha,kuyambira Kuma 1960s.Ma International Human Rights ,IMF,UN,World Bank ,EU,stop donating to Dictatorship Chakwera who has crippled Malawi and it's citizens,fuel crisis,poverty,no maize ,no fertilizer, and they killed VP Chilima and others,they are abusing Malawians.Free HON Kaliati,HON Navitcha and opposition.
Muthu aliyense niwofunika osamawonjeza malakhulidwe
Ngati alakwisa amangidwe basi palibe zoti ndi mzimayi LAMULO LIGWIRE NTCHITO
Bwanji osamanga anthu omwe anapha chilima nd anthu Ena aja Zinaz ndy ai srs please forgive God tichitiren chifundo mcp tatopa nay srs
🤣🤣🤣 10 ago ndamuona akuchoka kunyumba kwake amumanga nThawi yanji 🥺😂
Cholinga chawo akufuna asakayime nawo PA u president
The Elect the worst to lead us,kodi akuwona ngati dzikoli la ambuye awo
Kufuna kuwononga UTM uku, Eshhhh koma kumalawi amwene
Mayi a Kaliati munakatenga mfiti ku church kuti adzazunze anthu osaoka, onani akumakumangani komanso kumadyanso ena mwa inu. Munatenga zosayenela kuzibweretsa ku dziko.
But what's happening in Malawi
😊😊😊