Chilima anagwa ndi ndege basi may his soul rest in peace Ngati anaphedwa anaphedwa ndi ndege, Kafukufuku wa nzelu ngoyamba uja azibusa amayidziwa ndege?
Why the president is choosing what or who must be involved in the committee, it should have been the Malawi eni ake and all non governmental institutions, why Jabba alide out of all the pple as a chair? Awagula kale kale
Chomwe munkafuna ndi inquiry ya ndege n akuikirani anthu omwe akhala akuyankhulitsa pankhaniyi like anamiwa ndiye pano mukutiso chani, anthu oipa inu, musa zomwe munkafuna akupangirani so mwayambaso kutukwana, chomwe mukufuna ndichani😂😂😂😂😂😂😂 chitani manyaziiii
inu akufuna atinameze uyu Kalu wakupha uyu anthu amene anapha chilima tikuwaziwa ena ndi akunja ena ndiyamalawi omwe Ali asikali komaso chilungamo chikubwela 2025 ndi chipani China osati MCP ayi
Akungofuna alepherese mademo akupusitsa anthu chabe MCP simukuidziwa mwina
Zoonadi
Kma sivikuveka kd anali kut nthawi yoyesi pangengo yose
Kma nizoona anthu awa aya nkhula nthawi yaitali ndye kuyankhapo kwawo kwalelo sikoveka pati tasowekemala mayankho awo nthawi yaitali ndye tatumizaniso zithu zoveka kwamalawi
Ku Malawi 🇲🇼 kulibe president ayi!!! Koma mbava ndi okupha anthu chikangawa
Km atulutse. Black box ndiyomwe ikufunika umboni uli mmenemo. Zopusa ayi osamatiputsa ife😢😢😢
No
Palibe chomwe Chitaphulepo inu izi ndikukuuzanitu
Kuopa mademo kumeneko, president opanda mnzeru.
Iwe umaganiza mopepera inquiry yakhazikitsidwa monga momwe anthu timafunira pano wayambapo kulubwalubwa nzeru ulibedi
Yabodza imeneyo nthawi yonsei amadikira chiyani?😭😭😭😭💔💔💔
I'm happy kuti Anamiwa alimo mwina winiko akhoza kuchita manyazi pamenepo
Asa khe anthu ochekela zipani zonse.ma church.kubanja la ofeledwa.ndi mabungwe osiyana siyananso komanso mukhale atola nkhani amaradio osiyana siyana ndi mamfumu osiyana siyana
Aku banja mulibemo Aku mpingo mulibe Aku chipani mulibemo and Mr kalindo mulibe asakheso bwino
Chakwera wakhazikitsa bwanji commission of enquiry koma wopha chilima niweyo usamale kwambiri
Komaso why have they prioritise kumanga Patricia Kaliati then nkumatulutsa Commission of inquiry. Why??
Osalola ayi adikile mademo kenako ikwaya yanuyo zopusa kuona kuti sizikugwilizanaso continue mademo asathe
Ngati ili ya Fake Commission Of Inquires imeneyo Malawi ayidziwa kudzera Ku BAKILI MULUZI TV NDI Limpopo FM WITH Mtanyiwa.
Ntanyiwa wanena kale dzulo kuti akhazikitsa enquiry imeneyo chifukwa chothawa ma Demo.
Ine Kawanga Makwacha from KU pamenepa apre apanga chiganizo chabwino kwambiri kuti nkhani ifufuzidwe mwamachawi chilungamo chiyende ngati madzi.
Azipani akhalemo,akubanjanso akhalemo ,winiko akhalemo amabungwewo akhalemo okwanila nt Anamiwa ndi akariwa okhao ai,even antolankhani akhalemo
I think the air which chakwera breath is mixed with weed
😂😂😂😂
@@Chancenyangulu 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣 bro serious am not lying why asakha commission of inquiry amayembekeza chan weed is breathing by chakwera
Namiwa usakhale Kuti akugula osalola Kuti upite wekha Aku banja ,Aku mpingo ,Aku chipani ndi zipani Zina atengekoso anthu
Wakopakopa athu omwe wasankhawo ameneyo
Voice ngati cardinal 🎉
Ayikemo inkosi ya makosi Gomani komanso akubanja a wina aliyense amene anafa pa ngozi ija otherwise ndi zopepera zeni zeni
Chilima anagwa ndi ndege basi may his soul rest in peace Ngati anaphedwa anaphedwa ndi ndege, Kafukufuku wa nzelu ngoyamba uja azibusa amayidziwa ndege?
Koma mademo alipobe palibe kusintha coz zifukwa zopangira mademo ndizambiri
Ndichifukwa chiyani sanayikemo aku Banja komanso a zipani zosusa
Kkkkkkkkkkkk km chakwel ndigalud srs thaw yosey munalikt kuwop maden kumenek
Ngati pali judge wa corrupt. Wokhalila milandu ndi amene akamupezayu kuti atsogolele commission of enquiry. Abale anga, musayembekezele zambiri. Mau anga mudzawakumbuka.
Afufuza bwanji opanda black box, akuthawa mademo omalawi osalora zopusa
Enawo akufuna ndalama pomwe akubanja, akufuna chilungamo. iyi osayikhulupilira ayi. koma boma lidziwe kuti God he's watching you.
Zaziii musiyeni mulungu ndamene akudziwa
😂😂😂😂
Odi ndipite mkauluke ine
Aaa zamanyi basi awopa mademo akubwerawo pantumbo panu nose a MCP
Congrats Mr President mmm anthuwa awonjeza
@@JafaliAdams-l5k nde akugulirani mashon? Za ziii
Too late it will not change anything
Km bwanji wachedwetsa chonchi ife chilungamo tinachiziwa kale zoti anapha
Why the president is choosing what or who must be involved in the committee, it should have been the Malawi eni ake and all non governmental institutions, why Jabba alide out of all the pple as a chair? Awagula kale kale
Zabodza izi cz it's part of campaign so tisamale kwambiri chifukwa asankha anthu ni iyeyo
Anamiwa musavomereze munthuyu Chakwerayu ndi mfiti
Zoti ku Malawi tili ndi mtsogoleri ine ndimatsutsa koma tilindi Mbava,chigawenga,Satanism Chakwera
Shabwino. Ine pheee kumastand kudikila report
Ndiye nanga buanj sanaikemo osusa boma kma chakwera akutitora kwambiri kma mulungu akuona chilichonse
Zaziii!!!!!!! Mbuzi zawathu,,,kutiveka chijuzi kumaso chofiira cholemba nambala 2.mwatitola.
Zikomo bwana Mtanyiwa poyineneratu nkhaniyi
Wina akuopa ma demo uku
iwowo apresident asankha bwanji komite yoti afufuze zirongosoka apa ndizowona koma akunama murungu simunthu
Chomwe munkafuna ndi inquiry ya ndege n akuikirani anthu omwe akhala akuyankhulitsa pankhaniyi like anamiwa ndiye pano mukutiso chani, anthu oipa inu, musa zomwe munkafuna akupangirani so mwayambaso kutukwana, chomwe mukufuna ndichani😂😂😂😂😂😂😂 chitani manyaziiii
Osaika azipani zinazo bwanji poti nkhondoyi amathandizana anamiwa ndi amzawo
Kkkkk koma chakwera ukutenga amalawi kupusa chani
Wa utm, dpp,udf,afford, akubanja a khalemo. Apo biiii, deeeeee
Ndiyamika Mulungu pakukhazikisidwa kwa commission imeneyi, bola anthu amenewa asagulidwe posokoneza choonadi. anthu mwasankhidwanu
Ngati simugwira ntchito ya ambuye muyembekezere chilago chosatha.
Ndukaika zoti anena chilungamo
What about achibare
Nthawi yonsei amadikira chan
Nanga brackbo
Zauchitsiru zimenezo Asia anthu ofunikila ochuluka
inu akufuna atinameze uyu Kalu wakupha uyu anthu amene anapha chilima tikuwaziwa ena ndi akunja ena ndiyamalawi omwe Ali asikali komaso chilungamo chikubwela 2025 ndi chipani China osati MCP ayi
Kodi MWATI mumafuna chani?
Inu a opposition ndale zakukanikani basi
Umakana paja lero ukuopa madem galu iwe utuluse black box zonse zili momo mpaka miyezi 4 woipa iwe
Zompusa bsi commission yanji yopandamo akubanja aathu omwe anafawo kungosakha athu oti sitikuwaziwa akanatenga akubanja ose aathu omwe anamwalilawo komaso akulu akulu achipani cha utm komaso a opposition akhale nawo mu commission imeneyo osati zimenezo zaziiii kufuna kupusisa amalawi bsi tizapanga commission yathu yeniyeni tikasitha boma 2025 pano musatipusise
Kkkkkkk koma maganya😅😅😅😅😅
Aaa nthawi yonsey analikuti
Bwanji achita izi kutsatila atamumanga Kaliati?
Adzifufuza atamumasula chifukwa pamenepa Pali ?
Mademo what's the way forward
Anthuwo achepa komaso posankhapo amaganizila kuti anthuwa athandiza nanga amabungwe enawa
Amalawi musakayike ziyenda ndithu, palibe za ma bread kukamwa apa
Akufuna ampake ndan ife tikuzwa kut ndiyeyo2 anapha
Anakasiya akumabanja nawoso akhare ndianthu awo momwemo afufuzire rimozi
Thawi yonseyi amadikila chani 🚮🚮🚮zikutathauza kut madandaulo ayise a Malawi tikamadandaula kut ife a Malawi tikuvutika amamva et
Pamene commission of inquiry ikuyamba ntchito yo fufuza kwinaku mademoso a nyoooooo!!! Azichitikaso. Palibe kugona.
Tiwone zimene mutazakambe , anamiwa anuwo ali momo
bwanji akubanja ra anthu ofedwa muikepo akuba rachirima osati mafumu ai mungawagure mafumu kuti akukonde mbava iwe
Akatero awapatsa zindalama zambiri kuti atinamizeso,mmxiee
Sorry is tooooo late looks like he is ignoring to do that,,,,😂
Akubanja bwanji 😢
ku Malawi nkosekesa kwambiri, nonsense 😢
Nde azipan otsutsa sanawayikeko bwanji
Nthawi yonseyi amatani? Ndipo wasankha anthuwa ndindani?
Inu mumafuna commission of enquiry Kuti I chitike ndipo inali topic mumisonkhano yanu ndipo mimati tiwapemphe a pile akhadzikitse commission of enquiry Ngati , pano akhadzikitse alakwanso mmm
Uku ndikuzemba chilungamo chowoneka,
Iyeyo amadikira chiyani nthawi yonseyi
😂😂😂 Chakwera ndi Machine
Ndipo afa imfa yomvesa chisoni😊
Chakwera pamtumbo pake ndithu ndichitsiru kwambri
Mademo koma akupitili mawarino ku ntchewu
Galu kobasi bwanji sadasange akubanja
Aiwalamo kuika modzi ka Bon kalindo
Kuchita kukakamidzidwa mwina wache sankafuna kaya amabisanji
Mademo alipo pa 30
Achita bwino kwambili apule pomvela pempho la amalawi pa nkhani ya ngozi ya ndegeyi mwina anthu angayankhule dzinza tsopano
anaikaposo any member from either dpp, udf utm or aford
Nkhaniyi ikufunika kuwafusa apule Kuti ndimwana wandani amawanamiza maboza Kuti ndege inafika ku mzuzu
Chiphimba mmaso ...
Kuopa mademo
Osafooka
Osaopa
Osatopa
Mademo alipo yes or not
Nthawi yoseyi umatani chakwela umatani kt ukhazikitse commission of Inquiry? Koma chakwela iweyo umulungu ulibe kat ulawe upuresdent chf chilima kupanda chilima mkanakhara ndani inu
Mpakananso a Namiwa??
Mukhale akubanja ndiomwe angatipatse chilungamo amalawi
Yemwe akuyimila akubanja ndindani?
Amafuna asaikemo patricia kaliati kkkkkkkk eeeeeeh
Km apange moopa mulungu
AAA akubanja alikuti????
Commission equire ya bodza
Apapa ife ngati amalawi,tikupepha anthu omwe asakhidwawo kuti akaunike mosamala kuti akamabweretsa feedback ikhale yoonad, kapena kut yazoonad zikomo
Kunena zoona nkhaniyi sitinayilandileyi.
Nanga mosemuja zoona?
Zamanyazi