Это видео недоступно.
Сожалеем об этом.

Zomwe wayankhula Michael Usi Lero atangofika mu Mzinda wa Blantyre

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 25 авг 2024

Комментарии • 125

  • @benardisaac1986
    @benardisaac1986 Месяц назад +1

    Nyengo ndizosintha manvuto sankha moyo wose wamunthu koma Dr usi all the best

  • @user-zs6qc9dx8s
    @user-zs6qc9dx8s Месяц назад +5

    We all know kut anthu omwe avala makaka a UTM nd a MCP. Eni eni a UTM sitikupanga nawo zopusazo.

    • @JonesSiliya
      @JonesSiliya Месяц назад

      Zoona akufuna kupusitsa

    • @JonesSiliya
      @JonesSiliya Месяц назад

      Chilima nzake amane amakambilana naye ndi ndani nanga nthawi imene amakusekani pakamwa ndindani

  • @giftmasenti5732
    @giftmasenti5732 Месяц назад +3

    Manganya ndi wa MCP kuchokera kalekale

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Месяц назад +1

    Michael usi is a matured intellectual who doesn't entertain nosense.

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 Месяц назад +4

    Wachepa nao u vice president.waiwala imfa ya skc.

    • @LukeKalima
      @LukeKalima Месяц назад

      @@paulnyondo7572 aaaaaaaaaaa imfa ya skc ndiyotani anthu samamwalira kodi kapena munamuphera dala kuti muzipangira ndale imfa yake, kodi maliro akwanzanutu amaphweka chomchi akadzakhala akwanu zidzakuwawa kuti anthu azidzaseweretsa dzina la malemuwo

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 Месяц назад +3

    Ndimaona ngati adziyankhula zogwira mtima

  • @moyowrobert3331
    @moyowrobert3331 Месяц назад

    zoti akumanga thumba ngati Mphaka sukuziwa

  • @hastingskalambo8502
    @hastingskalambo8502 Месяц назад +2

    Ndekuti zoti UTM yatuluka ku alliance iyeyo sakudziwa

  • @JacobKasalika
    @JacobKasalika Месяц назад

    UTM ndimaikonda komano tikudzibalalitsa yokhatu.Uyu ndinthu ndinyamata wa SCK

  • @LukeKalima
    @LukeKalima Месяц назад +1

    Wandisangalatsa usi sakupanga nawo za mtopola ena achita manyanzi kumeneko ndiye kulankhulatu ambuye akudalitseni dr usi

  • @sanddaniweck2703
    @sanddaniweck2703 Месяц назад +2

    Zangongole ife tilibenazo ntchito nkhani musise zinthu zakwela kwambili coz za Neef zo anthu ena akumamizi kwina salandila koma mukasisa zinthu anthu onse athandizika

  • @FrankSpison-o7o
    @FrankSpison-o7o Месяц назад

    Mbuz yamunthu iyi yudasi ife a Utm zopusazo ayi sitikupanga nawo

  • @LeviBlackson
    @LeviBlackson Месяц назад

    Anthu sakumudziwa Kodi ku Blantyre kapana amapanga sewero

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Месяц назад +3

    Ngongole imeneyi udzabweza ndiwe .
    Fataleza udula konseko

  • @Jane-qb5qf
    @Jane-qb5qf Месяц назад +1

    Amalawi look sharp amalawi tilindivuto akati uku komweko uku komweko lekani timapemphera kukhala ndi chiganizo chokhazikika zimandimvesa chisoni kwambiri tisinthe mindset plz plz tizagwa chagada ndikati ndione amazayesa zida kuti kuli bwanji uku aaaa kaya Malawi

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses Месяц назад +3

    Muli mbali iti kodi Fada

  • @user-nu1dj3jh7b
    @user-nu1dj3jh7b Месяц назад +3

    Palibe azalande m'dalitso wamunthu, Dr usi ndiodalitsika muzonse komanso olimbika.

  • @joeldaniel-pc3ij
    @joeldaniel-pc3ij Месяц назад

    Mwapatsa anthu a MCP ma uniform a UTM kuti aziti chani?

  • @LeniaJosophat
    @LeniaJosophat Месяц назад

    Mukutipatsirazi ndizabwino zeedi koma you need to fix the sound kuti zizikomabe( this is the VP)

  • @user-vb1iq5un5p
    @user-vb1iq5un5p Месяц назад

    Kodi Usi ulimbali iti?. Koma umphawi luMalawi ukupepeletsa azibambo...

  • @VeronicaYohane
    @VeronicaYohane Месяц назад

    Mudyelen bambo wasikono akabwela osadziwa kuyankhula odvala madiresiyo

  • @JuniorKalipinde-gy7dx
    @JuniorKalipinde-gy7dx Месяц назад

    Usaone ngati ndi bugwe LA adla limenelo akupweteka

  • @johnbakali27
    @johnbakali27 Месяц назад

    Kodi iwe ukumenyera kampeni ya mco kapena UTM?

  • @user-hh4xg4hf2k
    @user-hh4xg4hf2k Месяц назад +2

    Enafe tisayankhire

  • @JonesSiliya
    @JonesSiliya Месяц назад

    Mwachedwa ndi chilima simunapange chifukwa chiyani

  • @FrankidEugenio
    @FrankidEugenio Месяц назад

    Ndale zayambika,Malawi ayiwale zambuyo.😂

  • @user-dv6rt6vb6e
    @user-dv6rt6vb6e Месяц назад

    Umbuli suzatha anthu munayambila kunamizidwa muja zilero changamukani

  • @constancemkandawire7378
    @constancemkandawire7378 Месяц назад

    You can't say that you love God if you don't love your nearby that's a total lie.You have failed to come together with your fellow utm members mukuti phala lomwe likudumpha mu mpoto lidumphe meaning you don't care ,ayi zikomo

  • @user-ni4nw1ee2f
    @user-ni4nw1ee2f Месяц назад

    Mwschedwa nayo ngongoleyo bwana kkkkkkk nyimbo ikhale ya mpaka malilo vinyo watha

  • @user-yq1mc3nm1f
    @user-yq1mc3nm1f Месяц назад +1

    Dziko la Malawi lafika pa uchitsiru weni weni

  • @CHRISSYBALALIKA
    @CHRISSYBALALIKA Месяц назад

    Tasisani fertilizer zinthu zisike agalu inu muona muwina mosavuta

  • @RossanaMitha-tl9in
    @RossanaMitha-tl9in Месяц назад

    Kodi akuti kwabwela ndani ?😂😂😂😂

  • @lumbaninyirenda8223
    @lumbaninyirenda8223 Месяц назад

    tamangopitani muzikapanga ma drama,mfundo palibe apa

  • @ChrisjuZiyaya
    @ChrisjuZiyaya Месяц назад

    Chizindikiro choti Usi siwa utm onani zomwe zavalidwazo , zomwe Malemu Sks sadapangepo. Tikufuna m'tsogoleri wa serious not this gys.

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g Месяц назад

    Lelo akunamizila chilima lelo ndi mbuzi yamunthu

  • @genesismbewe
    @genesismbewe Месяц назад

    genius

  • @jedoforsure2842
    @jedoforsure2842 Месяц назад

    Umakwana us

  • @joekamphulusa4767
    @joekamphulusa4767 Месяц назад

    Chitsilu chenicheni ichi watenga athu a mcp kumati a utm 🚮🚮🚮

  • @footballhighlightsofficial7248
    @footballhighlightsofficial7248 Месяц назад

    Missing Chilima Already😢

  • @MlecheFatch
    @MlecheFatch Месяц назад

    A manganya mmmh

  • @enockharry8039
    @enockharry8039 Месяц назад

    koma izi wina aziona

  • @joma5327
    @joma5327 Месяц назад

    champhamvu kopasa kale kuthanthauza chani

  • @KondwaniNdobvie-f4v
    @KondwaniNdobvie-f4v Месяц назад

    Komatu adzake afanazo

  • @user-qu9ww1cd1y
    @user-qu9ww1cd1y Месяц назад

    Anamizana zokuti akope Southern Region

  • @ellahmvula
    @ellahmvula Месяц назад

    Hahaha awa a mcp achina Eliza avala za utm

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 Месяц назад

    Wakupha iwe manganya

  • @AbdulrahimoMassamba
    @AbdulrahimoMassamba Месяц назад

    Satan ndiyemwe ali kutsogolo kwakoyo

  • @RobertChisenga-ci2mq
    @RobertChisenga-ci2mq Месяц назад

    BT chitsilu2 paja

  • @MerySaid-uw3cm
    @MerySaid-uw3cm Месяц назад

    Tikufelanji

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 Месяц назад

    Iweyo ukuti ukufuna ulongo sole, ndimaesa UTM yatuluka mungwirizano ukufuna kupusisanso Wanthu

  • @user-rs7vx6hc1k
    @user-rs7vx6hc1k Месяц назад

    Basi tizingokhalira ma handouts mpaka liti abale?

  • @NkosDysonNkosDyson
    @NkosDysonNkosDyson Месяц назад

    Tangotsitsani fertilizer muonanso mudzawina mosavuta ife amalawi sititichedwa kuiwala

  • @charlesmasauko4651
    @charlesmasauko4651 Месяц назад

    Wosokoneza uyu

  • @macdonaldchaonekera834
    @macdonaldchaonekera834 Месяц назад

    Kodi akupanga sewero la tikuferanji et?

  • @frankwilliam9844
    @frankwilliam9844 Месяц назад

    There's contradictory in his mind,chomwe amalawi akufuna singongole,tsitsani zinthu,chepetsani kudalira ngongole za IMF...koma ndithu 60yrs independent Malawi yukanikabe kudalira payokha pa nkhani ya zachuma? so sad...Kodi maiko amzathuwa amatani Kodi ..adatukuka bwanji atalandila ufulu???

  • @NELSONMULIMAH-fv6ub
    @NELSONMULIMAH-fv6ub Месяц назад

    Zauchisilu zaziii

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p Месяц назад

    Aaaaaaaaaaaaaaaaaaa chitsiru mbuzi garu nyani mfiti iwe

  • @jeymulima9664
    @jeymulima9664 Месяц назад +2

    Zaziiiiii

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g Месяц назад

    Anthu 4 okha bs

  • @florenceharawa519
    @florenceharawa519 Месяц назад

    Uku wapita uku wapita punsi anagwa chada😂😂😂😂

  • @user-rs7vx6hc1k
    @user-rs7vx6hc1k Месяц назад

    Koma zimenezi zitithandiza izi????

  • @user-ep7gu2td6y
    @user-ep7gu2td6y Месяц назад

    Sakudziwa zomwe a makawi akukumana nazo ....,

  • @MuhammadNyambalo
    @MuhammadNyambalo Месяц назад

    😅😮😢😅😅😅😅😂 patumbo pako iwe nyo

  • @NathanMaunda-dz8gc
    @NathanMaunda-dz8gc Месяц назад

    Awa sakuyankhula zotigwira mtima kodi nd wa chipani chanji ameneyi

  • @LottiAffati
    @LottiAffati Месяц назад

    kod akuyankhula kut chan apa guys aaaaaa, komanso amalawi ngoputsadi ndithu

  • @MarthaChintolo
    @MarthaChintolo Месяц назад

    Aaaaaa chifukwa chani Chilima unalakwitsa ee

  • @AbdullCassim
    @AbdullCassim Месяц назад

    Iweso ndiye kayatu

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r Месяц назад

    Ayakhura ali pat?

  • @chikondiyovita7210
    @chikondiyovita7210 Месяц назад

    My data hu!

  • @Vascomw
    @Vascomw Месяц назад

    Ïn̈ë n̈d̈ïm̈än̈g̈än̈ïz̈ä k̈üẗ äÿäk̈ḧür̈ä z̈äz̈ël̈üüü k̈m̈ ääää b̈ün̈d̈l̈ë ÿän̈g̈ä amayo

  • @momuumro
    @momuumro Месяц назад

    Situfuna kunva zimenezo Ife tufuna nkhani yotuluka mu tonse alliance

  • @charlesmasauko4651
    @charlesmasauko4651 Месяц назад

    Akufuna kugulitsa UTM KU MCP

  • @user-lu6nq9bs6w
    @user-lu6nq9bs6w Месяц назад

    Nde ku MCP' ko akuti chani kkkk 😂😂😂

  • @elizabethnkhata3438
    @elizabethnkhata3438 Месяц назад

    It's lik people are not happy

  • @MaryTchapo-py4hh
    @MaryTchapo-py4hh Месяц назад

    Ndimwana uyu alibe fundo

  • @QuotienieMw
    @QuotienieMw Месяц назад

    Tikufilanji episode 10

  • @user-ou4md5ud1u
    @user-ou4md5ud1u Месяц назад

    Sizikuveka ai komas sizikugwilizana ayi

  • @MaryTchapo-py4hh
    @MaryTchapo-py4hh Месяц назад

    Kupusa

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses Месяц назад

    Palibe kunyengelerana ndi ngongore nbuzi za anthu.

  • @ElizabethMwakamogho-x7j
    @ElizabethMwakamogho-x7j Месяц назад

    Sukuziwa make awo find alimbe

  • @user-zl1xz9kt5s
    @user-zl1xz9kt5s Месяц назад

    Amalawi mitu sigwiradi sure

  • @Vascomw
    @Vascomw Месяц назад

    Hhhhhhh

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p Месяц назад

    Palibe chanzeru waywnkhula

  • @FysonKaliba
    @FysonKaliba Месяц назад

    Kod ati Ali Mbali iti??????????

  • @SmithLikoswe
    @SmithLikoswe Месяц назад

    Zamasewelo bac

  • @jeymulima9664
    @jeymulima9664 Месяц назад

    Kkkkk ngabule moyo,thetsa,uthetsa suthetsa kkk yathayi kkk

  • @WindowSomanje
    @WindowSomanje Месяц назад

    Za ziii

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm Месяц назад

    Km malawi ndfe anthu opusa kwambiri tinakali kuvutika

  • @smartchitimbe2450
    @smartchitimbe2450 Месяц назад +1

    Za ziii tu

  • @MECChiona
    @MECChiona Месяц назад

    wamisara uyu 😂😂

  • @NATASHAChimtolo
    @NATASHAChimtolo Месяц назад

    Opepela uyu malemu amavala makaka achipani chake

  • @RighteousMhone
    @RighteousMhone Месяц назад

    Shimeyi atukwane😂😂😂

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Месяц назад

    Emeneyi si dyera koma

  • @ChrisNkhoma-i8m
    @ChrisNkhoma-i8m Месяц назад

    Mcp BOMA labwino kwamunthu woganiza mwazelu tiwone komwe tachoka .

  • @user-uq4hn4rp2j
    @user-uq4hn4rp2j Месяц назад +2

    Nice

  • @thokofodya1583
    @thokofodya1583 Месяц назад

    😢

  • @user-hl3vl9nt1b
    @user-hl3vl9nt1b Месяц назад

    Aaaa zazi bas

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko Месяц назад

    Sanje bac amalawi eeee

  • @sonkieleymanni6312
    @sonkieleymanni6312 Месяц назад

    ndiopusatu awawa,,,,,,,,,,,,,,,palibepo chanzeru anena apa

    • @LukeKalima
      @LukeKalima Месяц назад

      😂😂😂😂😂😂😂 mumafuna akanamanyonza kuteroko mwakhaula mindset change ikufunika ndithu

    • @LukeKalima
      @LukeKalima Месяц назад

      😂😂😂😂😂😂😂 mumafuna akanamanyonza kuteroko mwakhaula mindset change ikufunika ndithu

  • @SiphiweTonnyChidumayo
    @SiphiweTonnyChidumayo Месяц назад

    Anthu sakusangalaratu😂😂

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 Месяц назад

      Ndizawo zimenezo komanso musawapangire Zochita anthuwo . ngati inuyo simukusangalala basi

    • @SiphiweTonnyChidumayo
      @SiphiweTonnyChidumayo Месяц назад

      @@ancientnkhata1137 eh eh iwe im commenting according ndimmene zuonekera nsiye ine