A Michael Usi Alibe Impact Inaliyonse Ku UTM Olo Ukhansala Sangawine - UTM Member

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 14 окт 2024
  • On Nyasa VoiceBox, A UTM member says that Vice President Michael Usi has no real impact in UTM, he cannot even contest as a councillor and win.
    Pa Nyasa VoiceBox, membala wa UTM wati Vice President Michael Usi alibe chikoka mu UTM, sangapikisane nawo ngati khansala ndikupambana.
    #malawi

Комментарии • 62

  • @josephinemisomali6840
    @josephinemisomali6840 2 месяца назад +7

    Funso mkumati Kodi nsalu zikugawidwa lerozi Kaya ndingongole zomwe zikufuna kuperekedwa lerozi nthawi yonse zinali kt amadikila Chilima amwalire Kaye UTM gwilanani manja Zambiri zichitika Koma osafooka

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy 2 месяца назад +14

    And munthu otan oti nd mtsogoleri km ma meeting amwambo wamaliro osapanga attend kmnso akapanga attend osayankhulapo chonsecho nd mtsogoleri amathanthauza chan???

    • @chippakaribafox2865
      @chippakaribafox2865 2 месяца назад +4

      Mukufuna achite kukuwuzani yekha kuti ndi sellout?

    • @SalaJawali
      @SalaJawali 2 месяца назад

      Ndipo zodabwitsatu

  • @LamieTiger
    @LamieTiger 2 месяца назад +5

    Mbili ya usi amakhala president straight tithakuona khadza Za John Tembo

  • @DENSONZULU
    @DENSONZULU 2 месяца назад +4

    Rest in peace SKC , we shall always remember you, 2025 ndipafupi apa

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 2 месяца назад +4

    Well spoken

  • @SamuelMthengo
    @SamuelMthengo 2 месяца назад

    Very powerful message.

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 2 месяца назад +3

    Tidzadandaula akadzatuluka kaliati chifukwa ndi chipilala cha chipani

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 2 месяца назад +3

    Osamaphweketsa Bon Kalindo. Bon Kalindo analosera za imfa ya Chilima. Ndipo ananena pa 6th June 2024 kuti Chakwera wakonza plan yakupha Chilima ndi ndege. Ndipo anamuuza Chilima asakwere ndege. Pa 10 June ndege ya Chilima inagwetsedwa. Pa 15 June, MCP inamanga Bon Kalindo kamba ka ma audio.

  • @thomasphiri-zr3xs
    @thomasphiri-zr3xs 2 месяца назад

    Very true comrade le take on Nyalonje has no political impact indeed in her last constituency b4 her lost her seat pipo in the constituency booted her out bcos of her characters manners...........my plea to UTM G.members mama kaliati do a better research on mps to stand in 2025 elections don't just hand pick the rejects from other parties now are paying back what we sow in 2019.

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em 2 месяца назад +1

    Viva UTM viva

  • @JohnJohn-og8rt
    @JohnJohn-og8rt 2 месяца назад +3

    Zoona Mau abwino kwambili maso kusongolo

  • @beakab2378
    @beakab2378 2 месяца назад

    Good message, 👏👏👏

  • @khumalonyirenda4437
    @khumalonyirenda4437 2 месяца назад

    Morefire Dr, micheal usi

  • @thomasphiri-zr3xs
    @thomasphiri-zr3xs 2 месяца назад

    Lets allow new members why pipo r flocking to UTM now.....there is potential to win elections though reqiures proper partners.
    However let's give chance to madam Mary Chilima if so she can accept to compete any position now or later but God shows that in the years to come Shaun Chilima will bounce back into politics same UTM with powerful change and will rule the country.
    What late VP Chilima was doing hasn't been fulfilled so spiritually power is coming back to complete where left.

  • @Marymahendra
    @Marymahendra 2 месяца назад

    Thanks to god you have come out from the lion side completely different between evil people xx

  • @VincentMtambo
    @VincentMtambo 2 месяца назад

    Kaliati is Very loyal. Ndinaona nthawi ya Bingu sanathawe

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn 2 месяца назад

    UTM siinagawanike koma tsopano tingodziwa kuti ma utm members enieni ndi atiwo
    Ife till nganganga pa UTM

  • @DragoMchombo
    @DragoMchombo 2 месяца назад

    We want Kabambe

  • @daviskamonde4882
    @daviskamonde4882 2 месяца назад

    Reality!!

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gz 2 месяца назад +1

    Uku ndiye akuyakhula was wondering kuti guys how can u trust Micheal usiiiii???

  • @suzenzulu9412
    @suzenzulu9412 2 месяца назад

    UTM should support Kaliyati for presidency.

  • @alinafesalima5597
    @alinafesalima5597 2 месяца назад +2

    A Michael Usi ndi munthudi owumila koopsa ine ndagwirizana nanu ndipo sapasa munthu ndalama yake

  • @AbrahamTembo-z5k
    @AbrahamTembo-z5k 2 месяца назад

    Zikuwoneka kt alibe impact ku chipani, koma ku Dziko, alinayo. PENYETSETSANI KWAMBIRI OSANGOCHITA ZINTHU ZA PHUMA ndi MKWIYO. S.K.C. pomusankha, adawonamo NZERU ndipo ambiri tinakhutira. Dr Michael Usi, ali ndi popularity across the country. Mwina poti ife tikuziwonera patali mwina.

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 2 месяца назад

    Zoona abwana amene mukuyankhula,,pitilizani kulangiza anthu a UTM,,Bon Kalindo akufunila DPP iwine

  • @WinerdShadreck
    @WinerdShadreck 2 месяца назад

    This is good

  • @eliasmgala8469
    @eliasmgala8469 2 месяца назад

    Micheal Usi mukumunenayotu Chilima dolo amene timamunenayo, anamusankha iye kt akhale Vice wake enanu kukusiyani uko. And I think amaganizadi bwino munthu uja. Imagine akanasankha wina like this one or ena aja!

  • @JamesIngeni-ku3qj
    @JamesIngeni-ku3qj 2 месяца назад

    Manganya is a betrayer and I can believe kut munthuyu ndi oipa nchochi

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 2 месяца назад

    Vuto ku Malawi ndi kukoza or kiyanjanisa ayi ndithu koma kupasula ndi kibwelesa chidani pakati pa anthu or chipani UTM be careful mawa sikutali chilima anasankha usi chilipo chomwe anawona mwayiye

  • @AMONINICHOLAS-g2m
    @AMONINICHOLAS-g2m 2 месяца назад

    Masophenya andari ndi Chilima Inu aye Mp mikuyakhulani mulibe vision

  • @FrankSpison-o7o
    @FrankSpison-o7o 2 месяца назад

    Yudas 😢

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 2 месяца назад

    Usi si wa UTM ndipo kalikonse tikaonana pa 19 Friday li

  • @BellaMandala
    @BellaMandala 2 месяца назад

    Uncle shortawo bas angokhala ku MCP komko bas

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 2 месяца назад

    Onse ankayamba chonchi ndi pang'ono pang'ono uzakhumudwa atakhala nsogoleli wa ziko enanu muli ndi nkhwizi chabe ndi mzanu musiyeni ,gulu la kaliat likufuna kubwerera kwao paja ndi a dpp

  • @CharlesChagudubuka-rm6bh
    @CharlesChagudubuka-rm6bh 2 месяца назад

    Ndipo sidzawaonaso,apa mwayankhula bwino mwandilumbitsa mtima,anandinyasatu short one ameneyu

  • @JustusSNkhata
    @JustusSNkhata 2 месяца назад

    Komanso kuchoka mu mgwirizano chisalhale chifukwa kuti anthu a UTM asiye kutumikila a Makawi

  • @GracePendame
    @GracePendame 2 месяца назад

    Ndiwakabudura uyu usi simunthu wabwino ndi yudasi uyu osamusekerera

  • @LivaneMsyamboza
    @LivaneMsyamboza 2 месяца назад

    Ndipo mwayakhula bwino

  • @IsaacChapotera
    @IsaacChapotera 2 месяца назад

    Mau a mphamvu

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 2 месяца назад

    Anthu akonda ndrama ndi galimoto za Boma,,anthu Albie chikondi

  • @EliasKawuwa
    @EliasKawuwa 2 месяца назад

    Anthu a UTM mwadzadza ndi nkhwidzi pa wina ndi zake, mmalo mongwirizana chifukwa chopititsa patsongolo chipani chanu,mmalo mwatsongoza kuika patsongolo zofuna zanu,choncho mwaononga chipani Cha mwini wake Malemu SKC ,ndipo zimene mukuchitazi,anakakhara kuti SKC Ali moyo,nonse SKC anakakukwapulani kwambiri pazimene mukuchitazi,ngati mmene ambuye Yesu anachitira ataona anthu akungwiritsa tchalitchi kugulitsira malonda, the problem is,nonse mumafuna ma udindou Boma,nde mmalo mwake mwafuna kuuikira azanu ama udindo Boma, that's very bad, just feeling sorry for all UTM members kuti atsongoleri anu onse ndi adyera,ndipo chipani Cha UTM chitha movetsa Chisomo,chifukwa Cha dyera, that's why zipani zambiri Malawi muno ndi family parties,at least zimayendako, koma zinazi nde Kaya ndithu,dyera lakula mu UTM,mwaononga chipani chifukwa Cha Nsanje

  • @amosnyirenda-pl1ss
    @amosnyirenda-pl1ss 2 месяца назад

    wasanje ise nikaliyati wako musiyeni usi alamulile

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda 2 месяца назад

    Utn kuyaghayika

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o 2 месяца назад

    Akaliayati ndi nkhalidwe lawo atamwalila abingu anachita chi.mozi mozi kunyoza mai j b ndiye amene akuziwa mai kaliyati sakudabwa ayi

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 2 месяца назад

    anthu ofuna kugulisa utm aja ena ndakuluwa

  • @JoyceBanda-k8t
    @JoyceBanda-k8t 2 месяца назад

    Mau omveka bwino micheal utsi pomwe anaoneketa kuti si wa utm ndi nthawi ya maliro achilimA osayakhula chili conse kungofziwiratu kuti ndiyemwe anapereka chilima manja mwa chakwera ndiye manganya si wautm koma mcp

  • @SildaKatundu
    @SildaKatundu 2 месяца назад +1

    Tisankhe Patricia Kaliati kukhala president .Ndipo ndi munthu olimbikira ,opanda mantha komanso ochuluka mmalawi muno timamudziwa ndi kumukonda

    • @AishaChibwana-b8o
      @AishaChibwana-b8o 2 месяца назад

      Zoona Patricia Kaliati mpando omwe Ali akhale omweo

  • @GregoryMatambo
    @GregoryMatambo 2 месяца назад

    😂😂😂😂 uko kunali kulira kwa anamalra

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafrica 2 месяца назад +1

    Alindi impact mudziko lamalawj kuyambira kelekale. Sagawa masweet.

  • @hissimajohn965
    @hissimajohn965 2 месяца назад

    Za ziii

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o 2 месяца назад +1

    Inu ndi adpp msatisokose ife ayi adyela ndinuyo mmene anamzuzila adpp lelo adpp bdiabwino kwachilima poti wamwamwalila ayi kaya msanyoze ausi ayi i u ndiamene mkufuna kugulisa chipani kwa adani

    • @BenjaminKamanga-p8w
      @BenjaminKamanga-p8w 2 месяца назад

      Muziti poti mcp ysmupha nanga mukubisa chani

    • @AishaChibwana-b8o
      @AishaChibwana-b8o 2 месяца назад

      Ana anjoka inu mukhalira yomweyo

    • @beakab2378
      @beakab2378 2 месяца назад

      DPP mukuinyozayo inamusiya Chilima apite wamoyo, iye nkumainyoza nkupita ku ng'ona zokupha. Phunziranipo phunziro.

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di 2 месяца назад

    Say NO to Kabambe (utm presidency)

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di 2 месяца назад

    Awalandire alendo ofuna kulowa UTM koma osati zogulisa chipani kumpasa obwera (mlendo) kumpatsa u president kodi nkatimwanu mulibe angaimire u president? Mene mwavutikira basi mukagulisa chipani iyo ndi trick
    Say NO to Kabambe (UTM presidency) pls

  • @MackdBanda
    @MackdBanda 2 месяца назад

    Atumidwa ndi MCP awa