A Michael Usi Alibe Impact Inaliyonse Ku UTM Olo Ukhansala Sangawine - UTM Member
HTML-код
- Опубликовано: 14 окт 2024
- On Nyasa VoiceBox, A UTM member says that Vice President Michael Usi has no real impact in UTM, he cannot even contest as a councillor and win.
Pa Nyasa VoiceBox, membala wa UTM wati Vice President Michael Usi alibe chikoka mu UTM, sangapikisane nawo ngati khansala ndikupambana.
#malawi
Funso mkumati Kodi nsalu zikugawidwa lerozi Kaya ndingongole zomwe zikufuna kuperekedwa lerozi nthawi yonse zinali kt amadikila Chilima amwalire Kaye UTM gwilanani manja Zambiri zichitika Koma osafooka
And munthu otan oti nd mtsogoleri km ma meeting amwambo wamaliro osapanga attend kmnso akapanga attend osayankhulapo chonsecho nd mtsogoleri amathanthauza chan???
Mukufuna achite kukuwuzani yekha kuti ndi sellout?
Ndipo zodabwitsatu
Mbili ya usi amakhala president straight tithakuona khadza Za John Tembo
Rest in peace SKC , we shall always remember you, 2025 ndipafupi apa
Well spoken
Very powerful message.
Tidzadandaula akadzatuluka kaliati chifukwa ndi chipilala cha chipani
Osamaphweketsa Bon Kalindo. Bon Kalindo analosera za imfa ya Chilima. Ndipo ananena pa 6th June 2024 kuti Chakwera wakonza plan yakupha Chilima ndi ndege. Ndipo anamuuza Chilima asakwere ndege. Pa 10 June ndege ya Chilima inagwetsedwa. Pa 15 June, MCP inamanga Bon Kalindo kamba ka ma audio.
Very true comrade le take on Nyalonje has no political impact indeed in her last constituency b4 her lost her seat pipo in the constituency booted her out bcos of her characters manners...........my plea to UTM G.members mama kaliati do a better research on mps to stand in 2025 elections don't just hand pick the rejects from other parties now are paying back what we sow in 2019.
Viva UTM viva
Zoona Mau abwino kwambili maso kusongolo
Good message, 👏👏👏
Morefire Dr, micheal usi
Lets allow new members why pipo r flocking to UTM now.....there is potential to win elections though reqiures proper partners.
However let's give chance to madam Mary Chilima if so she can accept to compete any position now or later but God shows that in the years to come Shaun Chilima will bounce back into politics same UTM with powerful change and will rule the country.
What late VP Chilima was doing hasn't been fulfilled so spiritually power is coming back to complete where left.
Thanks to god you have come out from the lion side completely different between evil people xx
Kaliati is Very loyal. Ndinaona nthawi ya Bingu sanathawe
UTM siinagawanike koma tsopano tingodziwa kuti ma utm members enieni ndi atiwo
Ife till nganganga pa UTM
We want Kabambe
Reality!!
Uku ndiye akuyakhula was wondering kuti guys how can u trust Micheal usiiiii???
UTM should support Kaliyati for presidency.
A Michael Usi ndi munthudi owumila koopsa ine ndagwirizana nanu ndipo sapasa munthu ndalama yake
Zikuwoneka kt alibe impact ku chipani, koma ku Dziko, alinayo. PENYETSETSANI KWAMBIRI OSANGOCHITA ZINTHU ZA PHUMA ndi MKWIYO. S.K.C. pomusankha, adawonamo NZERU ndipo ambiri tinakhutira. Dr Michael Usi, ali ndi popularity across the country. Mwina poti ife tikuziwonera patali mwina.
Zoona abwana amene mukuyankhula,,pitilizani kulangiza anthu a UTM,,Bon Kalindo akufunila DPP iwine
This is good
Micheal Usi mukumunenayotu Chilima dolo amene timamunenayo, anamusankha iye kt akhale Vice wake enanu kukusiyani uko. And I think amaganizadi bwino munthu uja. Imagine akanasankha wina like this one or ena aja!
Manganya is a betrayer and I can believe kut munthuyu ndi oipa nchochi
Vuto ku Malawi ndi kukoza or kiyanjanisa ayi ndithu koma kupasula ndi kibwelesa chidani pakati pa anthu or chipani UTM be careful mawa sikutali chilima anasankha usi chilipo chomwe anawona mwayiye
Masophenya andari ndi Chilima Inu aye Mp mikuyakhulani mulibe vision
Yudas 😢
Usi si wa UTM ndipo kalikonse tikaonana pa 19 Friday li
Uncle shortawo bas angokhala ku MCP komko bas
Onse ankayamba chonchi ndi pang'ono pang'ono uzakhumudwa atakhala nsogoleli wa ziko enanu muli ndi nkhwizi chabe ndi mzanu musiyeni ,gulu la kaliat likufuna kubwerera kwao paja ndi a dpp
Ndipo sidzawaonaso,apa mwayankhula bwino mwandilumbitsa mtima,anandinyasatu short one ameneyu
Komanso kuchoka mu mgwirizano chisalhale chifukwa kuti anthu a UTM asiye kutumikila a Makawi
Ndiwakabudura uyu usi simunthu wabwino ndi yudasi uyu osamusekerera
Ndipo mwayakhula bwino
Mau a mphamvu
Anthu akonda ndrama ndi galimoto za Boma,,anthu Albie chikondi
Anthu a UTM mwadzadza ndi nkhwidzi pa wina ndi zake, mmalo mongwirizana chifukwa chopititsa patsongolo chipani chanu,mmalo mwatsongoza kuika patsongolo zofuna zanu,choncho mwaononga chipani Cha mwini wake Malemu SKC ,ndipo zimene mukuchitazi,anakakhara kuti SKC Ali moyo,nonse SKC anakakukwapulani kwambiri pazimene mukuchitazi,ngati mmene ambuye Yesu anachitira ataona anthu akungwiritsa tchalitchi kugulitsira malonda, the problem is,nonse mumafuna ma udindou Boma,nde mmalo mwake mwafuna kuuikira azanu ama udindo Boma, that's very bad, just feeling sorry for all UTM members kuti atsongoleri anu onse ndi adyera,ndipo chipani Cha UTM chitha movetsa Chisomo,chifukwa Cha dyera, that's why zipani zambiri Malawi muno ndi family parties,at least zimayendako, koma zinazi nde Kaya ndithu,dyera lakula mu UTM,mwaononga chipani chifukwa Cha Nsanje
Mwana Wa njoka iwe kagwere
wasanje ise nikaliyati wako musiyeni usi alamulile
Utn kuyaghayika
Akaliayati ndi nkhalidwe lawo atamwalila abingu anachita chi.mozi mozi kunyoza mai j b ndiye amene akuziwa mai kaliyati sakudabwa ayi
anthu ofuna kugulisa utm aja ena ndakuluwa
Mau omveka bwino micheal utsi pomwe anaoneketa kuti si wa utm ndi nthawi ya maliro achilimA osayakhula chili conse kungofziwiratu kuti ndiyemwe anapereka chilima manja mwa chakwera ndiye manganya si wautm koma mcp
Tisankhe Patricia Kaliati kukhala president .Ndipo ndi munthu olimbikira ,opanda mantha komanso ochuluka mmalawi muno timamudziwa ndi kumukonda
Zoona Patricia Kaliati mpando omwe Ali akhale omweo
😂😂😂😂 uko kunali kulira kwa anamalra
Alindi impact mudziko lamalawj kuyambira kelekale. Sagawa masweet.
Za ziii
Inu ndi adpp msatisokose ife ayi adyela ndinuyo mmene anamzuzila adpp lelo adpp bdiabwino kwachilima poti wamwamwalila ayi kaya msanyoze ausi ayi i u ndiamene mkufuna kugulisa chipani kwa adani
Muziti poti mcp ysmupha nanga mukubisa chani
Ana anjoka inu mukhalira yomweyo
DPP mukuinyozayo inamusiya Chilima apite wamoyo, iye nkumainyoza nkupita ku ng'ona zokupha. Phunziranipo phunziro.
Say NO to Kabambe (utm presidency)
Awalandire alendo ofuna kulowa UTM koma osati zogulisa chipani kumpasa obwera (mlendo) kumpatsa u president kodi nkatimwanu mulibe angaimire u president? Mene mwavutikira basi mukagulisa chipani iyo ndi trick
Say NO to Kabambe (UTM presidency) pls
Atumidwa ndi MCP awa