Koma pali ndalama Palibe chisoni, apa anthu enanu mukuchita kuwonekera tu kuti mukhonza kupha m bale wanu chifukwa cha ndalama. Boni kalindo ife timamusapota chifukwa amanena chilungamo, amatiyimilira anthu osaukafe, akanakhala kuti ndi munthu opanda chilungamo, bwezi atadya chibanzi kale kale chifukwa anthu ena amamunyengerera ndi ndalama koma iye amakana. Bon kalindo is the best our president❤❤❤❤❤❤
Sukudziwa kanthu iwe, akumanga nyumba Pano Chifukwa cha ndalama Zama bans zimene ukunenazo, uyu timakhala naye Ku machinjiri area 8 ngati ufuna Umboni ubwere tikakuonese Kwa njilika komwe akumanga nyumba
Koma pali ndalama Palibe chisoni, apa anthu enanu mukuchita kuwonekera tu kuti mukhonza kupha m bale wanu chifukwa cha ndalama. Boni kalindo ife timamusapota chifukwa amanena chilungamo, amatiyimilira anthu osaukafe, akanakhala kuti ndi munthu opanda chilungamo, bwezi atadya chibanzi kale kale chifukwa anthu ena amamunyengerera ndi ndalama koma iye amakana. Bon kalindo is the best our president❤❤❤❤❤❤
Sukudziwa kanthu iwe, akumanga nyumba Pano Chifukwa cha ndalama Zama bans zimene ukunenazo, uyu timakhala naye Ku machinjiri area 8 ngati ufuna Umboni ubwere tikakuonese Kwa njilika komwe akumanga nyumba
❤❤❤❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉 Booooon kalindoooo 🔥
🤔
Tiyankhulilen bs we love you always
Ndizovala za utm sikut anthuwo nda utm , MCP ikuva kuwawa kwambili coz sizomwe amayembekezera
Pitirizani kuyima pachilungamo bwana.
President wathu ife anthu osaukafe.Manganya ndi Yudasi yemwe anamupeleka SKC.kwa Lazaro.
Kodi Chakwerayu chomwe akufuna ndichani anamupha SKC. Koma pano akudana nayebe .Ambuye atithandize ndithu ndipo alowelerepo.
Zosezi ndi ndi mamganya kamuthu koipa kapeneka
Manganya ndi masterminder wa imfa ya Chilima
Palibe amene angagulitse UTM ukunama ,,,,,,
Manganya anatenga nawo mbali yopha Chilima kumene zimachita kuwoneka ndi timaso take twani twani olo kuyankhula po pangozi zinachitika ija shame Mr zakeyu
Ndiye mumafuna athu asauke chifukwa chani aaaa moyo wa masiku ano ndikokera kwako aripo angakane ndarama apa olo bonikalindoyo sangayikane
Wa UTM MENE APHELA CHILIMA. MUJA ANGAYIMBILA.MANJA FITI ANTHU AWA A MCP DZOSEDZI CHISILU MANGANYA APA NDIPAMENE PAKUDZIWIKA KUTI MANGANYA ANATENGAPO GAWO KUPHA CHILIMA AAAA KOMA MENE ACHITILEMO KAYA UTM ITHA KOMABE MCP 2025 TITHANA NAYO KULAMULILA MALAWI AYI ANTHU OWONONGA AWA
mbuli iwe galu
mulomwe ozelezeka lwe kulongolola ngati mzimayi
Muhlomwe chisiru uyu akuoneka kuti uhlomwe wake ndiwaku Mozambique eeeeeeh satopa ndikulongolora
The DC Boooon Kalindo the truth and justice speech 🔥🔥❤❤
Bwana mtendere simuzaupezaso even mutazasiya pansi udindo simuzarandila uremu chifukwa moyo wanu anthu awuona
Utm ipange zotheka kumuletsa Manganya kuchititsa msokhano in the name of utm other wise Manganya agendedwe
Opusa ndi amene alondola manganya
Iwe UTM SIINGAGULITSIDWE NEVER NEVER AKUGULITSIDWA NDI ANTHUWO
Mwagula chipani osati mitima ya anthu ife sitingapite ku MCP ngakhale panti atasandusidwa kabudula
Omwe akuvala za UTM nkumapita ku MCP asiye zimenezo
Ena sinu a UTM Kalindo sukunama 😮
Ubwino wake iweso ukudya ndalama zopatsidwa kuchokela kwa anthu akukutumawo, ndani samadziwa kuti iweyo ndi wa dpp
Ok
Iwe kalindo umanena chilungamo
Ndiwo ubale weniweni otukula dziko zabodza izi osadzigwiritsa ntchito
nose ndinu zisilu kuvela chisilu chizanu chi
Kkkkkkkkk awuzeni big
NDIPO USI 😭😭😭😭 WAMPELEKA NZAKE
Zowonadi bon kalindo
Kodi Imfa ya Chirima muzipangira campaign
-Kung'alura mopanda mantha kumene
Kafukufuku waonetsa kuti D.P.P 2025 boma
Chisiru Bon Kalindo
Boni kalindo nd chounikira changa
We are proud of u kalindo
KUPANDA KUTERO OSAWSPATSA MPATA CHAKWERA NDI MANGANYA MUDZIKO MUNO APA NDIYE ZAWONETSADI KUTI MANGANYA ANALI MGULU LAKUPHA NAWO CHILIMA
agalu achabechabe😢
UTM si ya Catholic koma msogoleli wake was a Catholic member
Apule nawoni tixiwe
Makape
❤❤❤❤❤
Akulu UTM sichipani koma kaganizidwe sangatigule musavutike ata!
Ndizoonadi yagulitsidwadi ndili ndi umboni gyz U.T.M yathapodi zosadabwitsa yudasi anapeleka yesu chilima may u soul rest in peace
Yeah money is a problem
Boniiiiiiii k the Dc❤❤❤❤
Manganya ndi joker wa imfa ya chilima
kalindo ndiwa DPP
Usi satana yunda sikaliotiii
Akangopanga convention a utm, tione mmene zikhalire tisamangovera zopanda pale bwanji asatanawo osawatchula maina kupatula yemwe tikumudziwa kaleyo
adzagonjetsa ndi mphamvu ya ku madzi
Bon kalindo on fire
Ana a satana awa MCP chipani cha satanic ichi nonse amene mudavotele MCP ndinu dzisilu mwationongela dziko tionana 2025
Amenewa Si a UTM ndi MCP yangovala zivala za UTM
Nonse amene mwatuluka ku utm ndipo mupita ku mcp mzimu wa chilima ukukanteni
Musamachuluse zichewa zowonjezera kapena kuti zokomesera,
Muzingopita papoint yeniyeniyo basi
Ndipo ndizoona Ife timadabwa amanganya ndichani koseko kufuna ndalama muyaluka koma simungaphe utm koma ili ndiziko muziona mwamba mwathambo tiyamika mukukathani ndipo ndikusavuka bwino akabwila tiyenaoni Ife phe pa gabiloni
KUMIPEZA MANGANYA AKUCHITSA MSONKHONO MENYANI NDICHITSILU PAKUFUNIKA MANGANYA APEZE MAVITO MDZIKO MUNO NDIMUNTHU MODZI ANAPHANAWO CHILIMA MANGANYA MWAZIEONA TIYENI TIKUTHE MANGANYA AMALAWI NDI KAMBERE MBERE
Koyipa
Zoona bwana
Koma ukhala uchitsilu wa usi chifukwa MCP ili ndi vp wake kale ndi thawi yot akanamanga chipani chawo
utm siinagulisidwepo and utm siingagulitsidwepo never
Movement sigulitsidwa
Tangoyambisan chipan chanu a kalindo
Tipaseni ma hint who they’re
Manganya chitsiru kwambili,
❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉
MANYANYA ATAWAMO MUNO MALAWI ATATENGERE ZIBWANA OLO KUFA KUMENE
Pangolini kuyankhula mosaopa
Yudas wooneka ndi maso
Kalindo chamba chidamupweteka. He is mentally ill. Opusanso ndi anthu omwe akutengeka nayewo, mnzawo ndi ntchito imeneyi akudyerapo mwana wa adad, zochita zopezera ndalama zikumusowa, akudyera momwemu. Amangondimvetsa chisoni kuti sukulu siidamupindulire. Timanena kuti sukulu imangochotsako umbuli wokha siichotsa uchitsiru koma zimandimvetsa chisoni kuti Kalindo siidamuchotse ndi umbuli womwe; zonse umbuli ndi uchitsiru zidamutsalira Kalindo sukulu siidamupindulire adakangotayako ndalama. Ndalama ankalipirira fizizo mwina akanangoyambira bizinezi kapena kuzilowetsa kumunda bwenzi ali pena, sibwenzi akavutika ndi zopusa akuchita panozi ayi.
😮😮😮😮😮😮😮😮
Ndipo kalindo umandinyasa olo ndimau omwe anakumana
Kape mdi u
Ndipo live jisse ndibuli zooondi
CHIMENE CHIKUFUNIKA KWAMBILI LIPOTI LA NDEGE LITULUKE MWACHULUKA CHIBWANA MUDZIKO MUNO
Guys muzikha ndi zeru muwone aliyese kumneko angovala ma glass muziwe kt imneyo ndye satanic yaxungulila
Komatu wina apusa nazo izi
Galu iwe za ziiiiiiiii ndi jealous yakoyo
Iwe chifundo samakhala opanda zelu usinthe dzinalo , iwe unthan kumpha mwana wako chifukwa chandram zovetsa chison.
Kkkk a matchalitchi chikuwagunda ndichani uyaluka winiko matako ako
Iweyo ndie akuchita kuonekeratu kut iweyo ndi mmodzi wa chikangawa satanic party koma nonse munya 2025
Akugwetsani asatanic mukwele galimoto mawali umfa
L
Kalindo umbuli ukumuzuza zedi ngati sudziwa kathu ungokhala Basi ulila mpaka liti?
Mbuli ndiwe nyani
Wa youth sasowa
Usasokoneze maganizo anthu ndi nkhani zako zonamazo Nonsense,,,Wekha ukunena akuvala ma t shirt ndi a Mcp
Kaya UTM yagulitsidwa kaya ai Ife sizikutinkhudza, izoso ndizawo, chomwe tikudziwa nchakuti andale ndiamodzi. Iweyo born kalindo ngat Uli munthu oima pachilungamo n siupanga zandale, n'chifukwa chani umakamba zandale? Ndie ingoima ndiweyo ukhale president ndiweyo udzayendetse dzikoli osati uzingotiuza zopusazi chifukwa ndiwe yemwe unkanyoza DPP nkuwatsogolere anthu ku MCP n lero ukunyozaso MCP nkumawatsogolera anthu ku DPP komwekuja, kod amalawife mumafuna kutitenga ngat zitsiru? Kupusa
Mbuzi iwe kodi ukuti chani, tayankhula zonveka
@@KhooMadex mbuzi ndi amako aise
@@KhooMadex ngat siunanve nkhala nkusanva kwakoko popeza ndiwe gonthi nchifukwa chake siunva
A Bon a Chilima alimoyo ankati ndiwopusa, lelo akuti anali wanzeru timve ziti
MANGANYA MASENDE YAMAKO TIRHANA NAWE
Ndipo manganya munthu oipa
Iweyo ungakane galimoto chitsilu iwetu
😏😏😏😏😏😏😏
Anatiuza kuti tilandire koma vote ndiya DPP
Pambuyo panu bwana
Ndan asakonde ndalama wausiru iwe
Aaa iweyo uthadi kupeleka mai ako chifukwa cha ndalama asatanik inu unya
Idya ndalamazo koma ndizasatanic uzingomwalira ayise
Ife monga akubanja tikuti pepani munthuyu anadwalako misala akuyenda ndi ma paper aku mental ndiye zonse zomwe akulankhulazo ndizamisala, muziona amangolumikiza nkhani zopanda mutu zosadziwa kuti akupita nayo kuti, pepani aMalawi munthu ndiwamisala uyu
Bolo yàko
Iwe unatikwana ndi mau ako onyasawo
Ndiwe chitsilu kwambiri ungamunene kalindo moteromo uzikhala ndi umunthu mene akuphera chakwelamu ungamayakhule Zoputsa
Musiyeni akakwela galimoto upita ndi asatanic akugwetsa
Ndiye iweyo Bon kaliwondewonde chikukhudza ndichani ngati chipanicho nchakwanu
Ana achikangawa awa asakuziwa ndan
Kkkkk atagendeyo ndani machende ako
Kalindo ndiwaboza iiiiii
I blame manganya
Akalindo, doda la boza ili
Kalindo. Chitsilu iwe mesa naweso ukulandila ndalama ku DPP ndiye ukufuna kuti azako asadye money
Mupwetekana 😮
Galu iwe uyu sasankha angalula wina aliyese
❤❤❤❤