How are you Mr Mtanyiwa, The fact is that we're in new generation we don't have any piece of time entice Chakwera government we're tired with him as soon as possible what happened in Kenya get prepared for Malawi
Mr mtanyiwa mokupephani akamakusokonezani mungowulula zisisi zonse basi za if ya bale athu komaso chilima mukatelo ndiye kuti athu osewo mwawatha basi afiti amenewa , koma timakuyikizilan mapephelo basi ❤❤
Kodi Bakili Muluzi akuti chiani pa za Malawi Democracy imene anaibweretsa? Kodi Ithere mnjira imeneyi? Auzeni a Malawi zoona pa nkhaniyi Munthu wobadwa from 1990 mu Malawi akuti MCP ndi yabwino, A Bakili nenanipo kanthu zinthu zisanafike pa mwana akana phala
KOD antanyiwa tatifusiran kut kod a zodiaki omwe timkawadalira pa tiuzeni zoona program ndi kunena zachisisi bwAnj PANO kuli ziii ndipo akumaika chiprogram china chanchingrez chonyasa apo ayi akuzimitsa trassm8sions.tatifusiran kut bwanj kod mwakhala chete?
Athu aku Cape Town James yi musalore akhudze Comrade, ndipo tonse tieni timupange Comrade soak mu Mwanzi wa Yesu. A ndemvu za mwai it’s obvious anafumbatitsidwa, anasitha sakudzudzulaso, zoona kulolandalama za magazi kukutsekani pakamwa ? Shame !!! Mzimu wa Chilima uchita nawo athu amenewa
Eishhhhhh 15 million yongogawa kufuna kuchotsa moyo wa nzawo kodi nde kuti anthu amene mumapanga ziwembu zopha anzanu inuyo mudzakhala pa dziko pano mpakana kale kale? Koma ndalama zukugawidwazi ndi zabwino bwino???????????
I think ndi ku sea point not sea port, Koma nde afera zainitu konseko kufuna ndlama? Koma nde ku Mcp kuli ndalama zogawatu m'malo mogulira mankhwala mzipatala
I always say Malawi is a peaceful country can't you see what's happening in malawi but only kalindo and little others are standing for the truth but if they say let's go pamademo wanthu wose wakukhala chete munyumba zawo nokufuma , but after mademo , nde amayambilaso hee njala hee mavuto aa vazii mademo simumatuluka , can't you see kenya today iyaa, mademo all the people went out no inside the house like Malawi nonsense malawi people..
Kusunga ndalama zotero mu phone ndizotheka Inu. Sikuti zonse zingalowe pa kamodzi. You can have ma business and be doing transactions through Airtel money. Momweso amayendera madolo ndizabwino kukhala ndi dollar zambiri mu phone so that they can withdraw everywhere and anytime they need it than kudalira bank. Account siyimakhutatu kuti basi zakwana.
Tiuzeni bho Za Uyo waku Capetown Ife tikamukonze tokha omrade
Let's act like Kenya Malawians..... Why we are sleeping
Koma ndipo live
Thats the only way
yes.. Koma amalawi mantha.. lets act like kukenya pls..
I support
Agree
Pa sea point ndipafupi timusaka james ameneyo ifeso tili konkuno ku capetown
Mcp boma la ma savage thats why amangolimbana ndi anthu malo moti aziendesa dziko thats why zawakanika zitsiru za anthu
How are you Mr Mtanyiwa, The fact is that we're in new generation we don't have any piece of time entice Chakwera government we're tired with him as soon as possible what happened in Kenya get prepared for Malawi
Osadandaura zophebwa ambuye alinawe ntanyiwa 🙏🙏🙏🙏
Boooon kalindo ndi muthu wa a Malawi ndalama waberazi wango zivutisa wabayo the dc ❤❤❤
Get well soon comrade
May God protect you Mr Man we lv u ntanyiwa
For the next generation yet unborn, whenever you come across this comment section, just know that we once alive this day to witness this masterpiece.
Osaopa comrade tili nanu limodzi makapewo sangapange kathu
Asanapagechoipapainu chiwachitikileiyowo paja yudasianaziona
Tell us everything ntanyiwa because you are not talking about one country talk about other countri❤❤❤❤❤
Malawi kugona....i salute kenyans for standing up for there country
Lipopo
❤❤❤
Ofunikano tiyambe kuwatengela a police ku court.
Amaonjeza amenewa, too corrupt. Abweze zimenezo
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you
Trully our own independent journalist #The truth always on point
Sea point, tithana naye timuyedzeka mwana opusa
Mr mtanyiwa mokupephani akamakusokonezani mungowulula zisisi zonse basi za if ya bale athu komaso chilima mukatelo ndiye kuti athu osewo mwawatha basi afiti amenewa , koma timakuyikizilan mapephelo basi ❤❤
Ma gardener boy amu seapoint amenewo
They are fools we don't like them ntanyiwa we play for u nothing will never happen to you
Tipaseni phn yamunthu ymwe Ali ku seaport pls
Nthanyiwa God is neya with you 🎉
Timakunyadila ntanyiwa tili pa mbuyo pako
Zikomo pa ntchito yomwe mukuigwila bwana. Praying for your safety. Be protected!!
Why bon kalindo himself never raise this issue of 25 million
Bambo Mtambo ndi HRDC yonse, bwererani mu mseu,
Zinthu ziipitsitsa kuposa mnthawi ya Pitala.
MCP ndi mkango wakudya nyama,
Kodi isinthabe pano.
Mwambi
"Mhpaka samuuika mu jaketi, akupala mwiniwe"
Kodi Bakili Muluzi akuti chiani pa za Malawi Democracy imene anaibweretsa? Kodi
Ithere mnjira imeneyi?
Auzeni a Malawi zoona pa nkhaniyi
Munthu wobadwa from 1990 mu Malawi akuti MCP ndi yabwino,
A Bakili nenanipo kanthu zinthu zisanafike pa mwana akana phala
KOD antanyiwa tatifusiran kut kod a zodiaki omwe timkawadalira pa tiuzeni zoona program ndi kunena zachisisi bwAnj PANO kuli ziii ndipo akumaika chiprogram china chanchingrez chonyasa apo ayi akuzimitsa trassm8sions.tatifusiran kut bwanj kod mwakhala chete?
Osaopa ntanyiwa tili kumbuyo kwako chotigwera chitigwere titsatile chilima
Ulibho iweusazafeyi uzangosowa umaitha t
Athu aku Cape Town James yi musalore akhudze Comrade, ndipo tonse tieni timupange Comrade soak mu Mwanzi wa Yesu. A ndemvu za mwai it’s obvious anafumbatitsidwa, anasitha sakudzudzulaso, zoona kulolandalama za magazi kukutsekani pakamwa ? Shame !!! Mzimu wa Chilima uchita nawo athu amenewa
Send his number ife tiliso nkonkuno ku capetown amtanyuwa Jem's kalazonga
Tumizani number yake ya Jem's kalozongayo azula amati wonke abantu lawo bebathi bahlanganiphile base matuneni
More fire
Eishhhhhh 15 million yongogawa kufuna kuchotsa moyo wa nzawo kodi nde kuti anthu amene mumapanga ziwembu zopha anzanu inuyo mudzakhala pa dziko pano mpakana kale kale? Koma ndalama zukugawidwazi ndi zabwino bwino???????????
Tamuziwa ku capetown kuno,will show him
A Police kuba ndalama za Booon Kalindo? Zopatsa manhazi, manhazi, manhazi a Malawi. Zafika apa?. Kulira Kamuzu.
even voice isamanveke bobo ife ndiosangalala Nanu comrade komaso wa Ku Capetown tipatseni number yake
Ntanyiwa anthuwa achulukila manthha chifukwa chilungamo chikunenedwa ndipo akudziwa kuti zawo zadela,komanso Ntanyiwa sangaphedwe mwachibwana ngati m'mene anamuphela chilima ndipo nzimu wachilima ukuyenda paliponse mulungu simunthu
Kunama amenewo ataya thawi yawo pachabe. Inu denkhani sangakupezeniyi.
I think ndi ku sea point not sea port, Koma nde afera zainitu konseko kufuna ndlama? Koma nde ku Mcp kuli ndalama zogawatu m'malo mogulira mankhwala mzipatala
Ka James ndi muzeleza so ñganya leka kopa
Fire hit!! Ntanyiwa umakwana keep it up more 🔥🔥🔥🔥
Proud of you mtanyiwa ❤❤
Q@a,
Ndipasengi number yake naneso ndine ntonga ndimagwira konkuno ku Cape town camp's sea point ndimafika ifweyo tithana nayo galu yoo
Koma boma ilili ayi zafika posauzana koma mukanazilemekeza matsiku akuthera ku chiseko
Abweze ndalama za bon kalindozo or else they will see Nairobi in Lilongwe
There is no secrete under the sun. Chilichonse chizaulurika
Mulunguakutetezani tilipokukupepelelani masalimo 91:1/15
A Malawi tinabadwa ndi kukula mwa mantha kwambiri komanso umphawi
Khani za awa bolaso boni kalindo sizimabveka kuti akutichani amangopeka khani lelo anena izi mawa anena izi palibe chomwe chimaoneka kuti ndichoona abale koma tchito ilipo
Ayaluka sanati akazizi amenewa,,, Chilima R I P
No secret under the sun
Seapoint not seaport
We love you comrade ❤❤❤❤❤ keep it up
Ndipo Nzimu wa chilima uwanyetsadi anthu God will protect you
I salute you, Achalume , kumtunda
Ntanyiwa umakwana bro mulungu azikudalitsa always
See point not see pot
Tingokonza dzinalo ndi Sea point not sea port l know the place
Get better Mr Com
Moyo wautali akupatseni mulungu
Amakhala ku sea point
😂😂🎉🎉🎉🎉 fire
Chokani apa agalu inu a LIMPOPO FM. Iwe ndiwe.mbuli yeniyeni, Tikudziwa kuti DPP inakupatsani ndarama ma million for propergander..
Koma ife timamufela bro
Muchile mwansanga chifuwacho
Ingong'alula kalikonse tikadziwa
Mtanyiwa more fire
Timakunyadira pazomwe mukuchita
Keep up with good job, sir. Never give up.
tiuzeni zooona bg tilinanu best tv ever 🎉
Mwana uyu ndi mwana mmm wachep
mapephelo anthu ndi misozi yanthu ikutetezelani A ntanyuwa uyuyu uyu Mulungu amuone ndikumudzudzula ayelekeze aone
Mbambande ntanyiwa
Tipatseni number yakhe kuno jozi
A cipriano mukuwononga dzina langa ndi khalidwe lá anthu amene ali dzina lá cipriano
Mbambande
Sangabisale pansi pa mtambo
ndalama mwatchulayo siyilowa mu phone mmm boza basi.evin kunoko ku RSA KULIBE EWALLET YA 50PIN AMALAWI CHEPESANI BOZA
ine kupanda kumva audio yanu ndi abon kalindo komasso wa Bakili sindmva bwino plz ABOMA NDALAMA ZAKALINDO BOMA LIBWEZE
Comrede Ntanyiwa tiwuzeni zakape amene alikunoyo ku SEA POINT CAPE TOWN
Tiwawuze kuno makaladi amukoze ameneyo ndi ngalu kwambiri munthu ameneyo
Koma uyu otchedwa James Khalasonga akuseweratu. Wangoona kudziyamba sea point no where to kubisala
Kodi katundu wa a Malemu a Chilima momwe anapemphela Aku banja Lao kuti awabwezere Aku banja, zinathekadi.
More fire,more
25 million ilowa mu fon? Azanthu airtel tiyakheni
Iwe national Bank more sukuidziwa et ndalama zikakhala mu fon
Amtanyiwa ajems woo azisiya ndalama zomwe alandilazo jst send the number ifeso tilikuno ku captown mazula amati bonke lawo bebathi bahlanganiphile basematuneni
I always say Malawi is a peaceful country can't you see what's happening in malawi but only kalindo and little others are standing for the truth but if they say let's go pamademo wanthu wose wakukhala chete munyumba zawo nokufuma , but after mademo , nde amayambilaso hee njala hee mavuto aa vazii mademo simumatuluka , can't you see kenya today iyaa, mademo all the people went out no inside the house like Malawi nonsense malawi people..
Tikamati uyu amangopeka khani moti 25 mita ingakhale 4n ya kalindo 😂😂😂😂😂😂😂😂 abale ndiye poti amalawi timasangalala ndimabodza ok tiye nazoni
Kusunga ndalama zotero mu phone ndizotheka Inu. Sikuti zonse zingalowe pa kamodzi. You can have ma business and be doing transactions through Airtel money. Momweso amayendera madolo ndizabwino kukhala ndi dollar zambiri mu phone so that they can withdraw everywhere and anytime they need it than kudalira bank. Account siyimakhutatu kuti basi zakwana.
😅😅😅😅😅😂😂😂😂 yomweyo galu iwe achina Sadam angomanga anthu opanda chifukwa aziwona sanati mizimu yakwiya
Antanyiwa kod mulibe mfut ija amat snaiper chonde ngat mulinaayo ndibweleken. Asatijaile
kukhale Ku (sea point) kumeneko kapena? kapena cos Ku sea port sinkukuziwa koma Ku sea point.
Acomrade Mtanyiwa ife aMalawi ochuluka tilipambuyo panu and Mulungu alinanu .ife tidzaimananu pamodzi.zaimfa yaa chilima ndyopweteka koopsa imene mmalawi izavuta kuiwala.
Ndipo mamulungu yeka atimenyela nkhondo ntanyiwa mulungu akudaliste kodi Boma limabanso
Mulungu si jemus ayise mtanyiwa uwoloka nafe limozi ndichikhulupiliro
KOMA PLEASE NDALAMA ZA BON KALINDO MPASENI MUSANAFE OSAKOZA SITIPANGASO ZA KUPOLIC CHIFUKWA KUMALAWI KULIBEKO POLICE KOMA MUSOWA TIKUTI BWEZANI NDALAMAZO TIKUTI AGALU INU
KODI AZIKHALI ,CHIMWENDO,KUKUYU CHAKWERA, KUFA KWA CHILIMA SIKUNAKUKWANENI ,MUKUFUNASO KUMAPHASO ANTHU ENASO KODI INU KUPHA SIMUMAPANGA MANTHA MUZAYANKHATU IZI KWA MULUNGU IZI AGALU INU
Kawawa pitilizani kutidziwitsa zomwe zikupanga zitsiluzi kuphedwa simugaphedwe mr tanyiwa komano zikuzuzika zonkha zitsiluzi tikati tantsala ndi wayires Malawi muno ndi Limpopo bas zinazose zagulidwa ndi mcp
Asamale jemus makaladi athana naye kuno achita masewela ndipo ayelekeze tiyambapo ndife kuthana naye....