LIMPOPO FM USIKU WA 26 JUNE 2024 NDALAMA ZA BON KALINDO ZOMWE ZINALI MA PHONE ONSE AWIRI ZABEDWAMO

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 1 окт 2024
  • LIMPOPO FM
    USIKU WA 26 JUNE 2024
    NDALAMA ZA BON KALINDO
    ZOMWE ZINALI MA PHONE
    ONSE AWIRI
    ZABEDWAMO NDI APOLICE

Комментарии • 162

  • @eliasMwamba-q5f
    @eliasMwamba-q5f 3 месяца назад +19

    Tiuzeni bho Za Uyo waku Capetown Ife tikamukonze tokha omrade

  • @HarryChindiwo
    @HarryChindiwo 3 месяца назад +30

    Let's act like Kenya Malawians..... Why we are sleeping

  • @alexandermwale4669
    @alexandermwale4669 3 месяца назад +6

    Pa sea point ndipafupi timusaka james ameneyo ifeso tili konkuno ku capetown

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa 3 месяца назад +5

    Mcp boma la ma savage thats why amangolimbana ndi anthu malo moti aziendesa dziko thats why zawakanika zitsiru za anthu

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 3 месяца назад +7

    How are you Mr Mtanyiwa, The fact is that we're in new generation we don't have any piece of time entice Chakwera government we're tired with him as soon as possible what happened in Kenya get prepared for Malawi

  • @PetroMatias
    @PetroMatias 3 месяца назад +8

    Osadandaura zophebwa ambuye alinawe ntanyiwa 🙏🙏🙏🙏

  • @Imraanjafali
    @Imraanjafali 3 месяца назад +8

    Boooon kalindo ndi muthu wa a Malawi ndalama waberazi wango zivutisa wabayo the dc ❤❤❤

  • @ShiraKasekaNyirenda
    @ShiraKasekaNyirenda 3 месяца назад +6

    Get well soon comrade

  • @ChomboNgosi
    @ChomboNgosi 3 месяца назад +5

    May God protect you Mr Man we lv u ntanyiwa

  • @kennethnasteve4721
    @kennethnasteve4721 3 месяца назад +2

    For the next generation yet unborn, whenever you come across this comment section, just know that we once alive this day to witness this masterpiece.

  • @gizzykondwani865
    @gizzykondwani865 3 месяца назад +3

    Osaopa comrade tili nanu limodzi makapewo sangapange kathu

  • @EdisonNakulenga
    @EdisonNakulenga 3 месяца назад +4

    Asanapagechoipapainu chiwachitikileiyowo paja yudasianaziona

  • @ZondoChirwa
    @ZondoChirwa 3 месяца назад +1

    Tell us everything ntanyiwa because you are not talking about one country talk about other countri❤❤❤❤❤

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 3 месяца назад +2

    Malawi kugona....i salute kenyans for standing up for there country

  • @JummahNelson
    @JummahNelson 3 месяца назад

    Lipopo
    ❤❤❤

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 3 месяца назад +7

    Ofunikano tiyambe kuwatengela a police ku court.

    • @ColetteMalunga
      @ColetteMalunga 3 месяца назад

      Amaonjeza amenewa, too corrupt. Abweze zimenezo

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 месяца назад +1

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 3 месяца назад

    Trully our own independent journalist #The truth always on point

  • @FreddieMatuta
    @FreddieMatuta 3 месяца назад +2

    Sea point, tithana naye timuyedzeka mwana opusa

  • @MoosaBanda-su3zp
    @MoosaBanda-su3zp 3 месяца назад +8

    Mr mtanyiwa mokupephani akamakusokonezani mungowulula zisisi zonse basi za if ya bale athu komaso chilima mukatelo ndiye kuti athu osewo mwawatha basi afiti amenewa , koma timakuyikizilan mapephelo basi ❤❤

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 3 месяца назад +1

    Ma gardener boy amu seapoint amenewo

  • @JefreyMtambo
    @JefreyMtambo 2 месяца назад

    They are fools we don't like them ntanyiwa we play for u nothing will never happen to you

  • @amosphakira7936
    @amosphakira7936 3 месяца назад +1

    Tipaseni phn yamunthu ymwe Ali ku seaport pls

  • @AdamNapwanga-ff2wm
    @AdamNapwanga-ff2wm 3 месяца назад +4

    Nthanyiwa God is neya with you 🎉

  • @GiftChiposi
    @GiftChiposi 3 месяца назад +4

    Timakunyadila ntanyiwa tili pa mbuyo pako

  • @moniqb7373
    @moniqb7373 3 месяца назад

    Zikomo pa ntchito yomwe mukuigwila bwana. Praying for your safety. Be protected!!

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 3 месяца назад

    Why bon kalindo himself never raise this issue of 25 million

  • @leviouslongwe2950
    @leviouslongwe2950 3 месяца назад

    Bambo Mtambo ndi HRDC yonse, bwererani mu mseu,
    Zinthu ziipitsitsa kuposa mnthawi ya Pitala.
    MCP ndi mkango wakudya nyama,
    Kodi isinthabe pano.
    Mwambi
    "Mhpaka samuuika mu jaketi, akupala mwiniwe"

  • @leviouslongwe2950
    @leviouslongwe2950 3 месяца назад

    Kodi Bakili Muluzi akuti chiani pa za Malawi Democracy imene anaibweretsa? Kodi
    Ithere mnjira imeneyi?
    Auzeni a Malawi zoona pa nkhaniyi
    Munthu wobadwa from 1990 mu Malawi akuti MCP ndi yabwino,
    A Bakili nenanipo kanthu zinthu zisanafike pa mwana akana phala

  • @SellarKasiya
    @SellarKasiya 3 месяца назад

    KOD antanyiwa tatifusiran kut kod a zodiaki omwe timkawadalira pa tiuzeni zoona program ndi kunena zachisisi bwAnj PANO kuli ziii ndipo akumaika chiprogram china chanchingrez chonyasa apo ayi akuzimitsa trassm8sions.tatifusiran kut bwanj kod mwakhala chete?

  • @nifachitima3477
    @nifachitima3477 3 месяца назад

    Osaopa ntanyiwa tili kumbuyo kwako chotigwera chitigwere titsatile chilima

  • @HusseinMoffatt-mi1fl
    @HusseinMoffatt-mi1fl 3 месяца назад +2

    Ulibho iweusazafeyi uzangosowa umaitha t

  • @liz9425
    @liz9425 3 месяца назад

    Athu aku Cape Town James yi musalore akhudze Comrade, ndipo tonse tieni timupange Comrade soak mu Mwanzi wa Yesu. A ndemvu za mwai it’s obvious anafumbatitsidwa, anasitha sakudzudzulaso, zoona kulolandalama za magazi kukutsekani pakamwa ? Shame !!! Mzimu wa Chilima uchita nawo athu amenewa

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 3 месяца назад

    Send his number ife tiliso nkonkuno ku capetown amtanyuwa Jem's kalazonga

    • @EllenPhiri-xt8pt
      @EllenPhiri-xt8pt 3 месяца назад

      Tumizani number yake ya Jem's kalozongayo azula amati wonke abantu lawo bebathi bahlanganiphile base matuneni

  • @GustoJuliusYobe
    @GustoJuliusYobe 3 месяца назад +3

    More fire

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 месяца назад

    Eishhhhhh 15 million yongogawa kufuna kuchotsa moyo wa nzawo kodi nde kuti anthu amene mumapanga ziwembu zopha anzanu inuyo mudzakhala pa dziko pano mpakana kale kale? Koma ndalama zukugawidwazi ndi zabwino bwino???????????

  • @YellowmanMalawi-qe8zh
    @YellowmanMalawi-qe8zh 3 месяца назад +1

    Tamuziwa ku capetown kuno,will show him

  • @Kst8an8yslag8Fobig
    @Kst8an8yslag8Fobig 3 месяца назад

    A Police kuba ndalama za Booon Kalindo? Zopatsa manhazi, manhazi, manhazi a Malawi. Zafika apa?. Kulira Kamuzu.

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 3 месяца назад

    even voice isamanveke bobo ife ndiosangalala Nanu comrade komaso wa Ku Capetown tipatseni number yake

  • @MaxwellBanda-xd6oh
    @MaxwellBanda-xd6oh 3 месяца назад

    Ntanyiwa anthuwa achulukila manthha chifukwa chilungamo chikunenedwa ndipo akudziwa kuti zawo zadela,komanso Ntanyiwa sangaphedwe mwachibwana ngati m'mene anamuphela chilima ndipo nzimu wachilima ukuyenda paliponse mulungu simunthu

  • @HaroonMaundala-lg5lg
    @HaroonMaundala-lg5lg 3 месяца назад

    Kunama amenewo ataya thawi yawo pachabe. Inu denkhani sangakupezeniyi.

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 месяца назад

    I think ndi ku sea point not sea port, Koma nde afera zainitu konseko kufuna ndlama? Koma nde ku Mcp kuli ndalama zogawatu m'malo mogulira mankhwala mzipatala

  • @kondwamlungu8384
    @kondwamlungu8384 3 месяца назад

    Ka James ndi muzeleza so ñganya leka kopa

  • @MelissaMondey
    @MelissaMondey 3 месяца назад +2

    Fire hit!! Ntanyiwa umakwana keep it up more 🔥🔥🔥🔥

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 3 месяца назад +7

    Proud of you mtanyiwa ❤❤

  • @wondermsibe1708
    @wondermsibe1708 3 месяца назад

    Ndipasengi number yake naneso ndine ntonga ndimagwira konkuno ku Cape town camp's sea point ndimafika ifweyo tithana nayo galu yoo

  • @JamesChiphwanya-m4v
    @JamesChiphwanya-m4v 3 месяца назад

    Koma boma ilili ayi zafika posauzana koma mukanazilemekeza matsiku akuthera ku chiseko

  • @mishecksipolo7153
    @mishecksipolo7153 3 месяца назад

    Abweze ndalama za bon kalindozo or else they will see Nairobi in Lilongwe

  • @thokogwebe2337
    @thokogwebe2337 3 месяца назад

    There is no secrete under the sun. Chilichonse chizaulurika

  • @EdisonNakulenga
    @EdisonNakulenga 3 месяца назад +2

    Mulunguakutetezani tilipokukupepelelani masalimo 91:1/15

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 3 месяца назад

    A Malawi tinabadwa ndi kukula mwa mantha kwambiri komanso umphawi

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 месяца назад

    Khani za awa bolaso boni kalindo sizimabveka kuti akutichani amangopeka khani lelo anena izi mawa anena izi palibe chomwe chimaoneka kuti ndichoona abale koma tchito ilipo

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 3 месяца назад

    Ayaluka sanati akazizi amenewa,,, Chilima R I P

  • @Costance-nf7ue
    @Costance-nf7ue 3 месяца назад

    No secret under the sun

  • @dunganyamwela7266
    @dunganyamwela7266 3 месяца назад

    Seapoint not seaport

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 3 месяца назад +1

    We love you comrade ❤❤❤❤❤ keep it up

  • @EstherBonga
    @EstherBonga 3 месяца назад +2

    Ndipo Nzimu wa chilima uwanyetsadi anthu God will protect you

  • @ZioneMkwanda-y6i
    @ZioneMkwanda-y6i 3 месяца назад

    I salute you, Achalume , kumtunda

  • @rexphiri7242
    @rexphiri7242 3 месяца назад +2

    Ntanyiwa umakwana bro mulungu azikudalitsa always

  • @AyakhaTom
    @AyakhaTom 3 месяца назад

    See point not see pot

  • @SamuelChiwere
    @SamuelChiwere 3 месяца назад

    Tingokonza dzinalo ndi Sea point not sea port l know the place

  • @ZioneMkwanda-y6i
    @ZioneMkwanda-y6i 3 месяца назад

    Get better Mr Com

  • @OmegaChingamuka
    @OmegaChingamuka 3 месяца назад

    Moyo wautali akupatseni mulungu

  • @kaungabondera892
    @kaungabondera892 3 месяца назад +2

    Amakhala ku sea point

  • @InnocentKandaya
    @InnocentKandaya 3 месяца назад

    😂😂🎉🎉🎉🎉 fire

  • @Deborah-b3k
    @Deborah-b3k 3 месяца назад

    Chokani apa agalu inu a LIMPOPO FM. Iwe ndiwe.mbuli yeniyeni, Tikudziwa kuti DPP inakupatsani ndarama ma million for propergander..

  • @NaduMbewe-zz6iw
    @NaduMbewe-zz6iw 3 месяца назад

    Muchile mwansanga chifuwacho

  • @EstherBonga
    @EstherBonga 3 месяца назад +2

    Ingong'alula kalikonse tikadziwa

  • @enochjacksonkhobili
    @enochjacksonkhobili 3 месяца назад +2

    Mtanyiwa more fire

  • @emilynthite6545
    @emilynthite6545 3 месяца назад +2

    Timakunyadira pazomwe mukuchita

  • @stevezulu2108
    @stevezulu2108 3 месяца назад +1

    Keep up with good job, sir. Never give up.

  • @JogaJoseph
    @JogaJoseph 3 месяца назад +1

    tiuzeni zooona bg tilinanu best tv ever 🎉

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 3 месяца назад

    Mwana uyu ndi mwana mmm wachep

  • @MercyChiwaya-um6us
    @MercyChiwaya-um6us 3 месяца назад +1

    mapephelo anthu ndi misozi yanthu ikutetezelani A ntanyuwa uyuyu uyu Mulungu amuone ndikumudzudzula ayelekeze aone

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 3 месяца назад

    Mbambande ntanyiwa

  • @robenallie6985
    @robenallie6985 3 месяца назад +1

    Tipatseni number yakhe kuno jozi

  • @CiprianoBindissone
    @CiprianoBindissone 3 месяца назад +1

    A cipriano mukuwononga dzina langa ndi khalidwe lá anthu amene ali dzina lá cipriano

  • @TongaiTixeiraMafungaMafunga
    @TongaiTixeiraMafungaMafunga 3 месяца назад

    Mbambande

  • @feehasaidid.r.d
    @feehasaidid.r.d 3 месяца назад +1

    Sangabisale pansi pa mtambo

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 3 месяца назад

    ndalama mwatchulayo siyilowa mu phone mmm boza basi.evin kunoko ku RSA KULIBE EWALLET YA 50PIN AMALAWI CHEPESANI BOZA

  • @kanowamndalaphiri2959
    @kanowamndalaphiri2959 3 месяца назад

    ine kupanda kumva audio yanu ndi abon kalindo komasso wa Bakili sindmva bwino plz ABOMA NDALAMA ZAKALINDO BOMA LIBWEZE

  • @AlickMDayi
    @AlickMDayi 3 месяца назад

    Comrede Ntanyiwa tiwuzeni zakape amene alikunoyo ku SEA POINT CAPE TOWN
    Tiwawuze kuno makaladi amukoze ameneyo ndi ngalu kwambiri munthu ameneyo

  • @khoviwaedward
    @khoviwaedward 3 месяца назад

    Koma uyu otchedwa James Khalasonga akuseweratu. Wangoona kudziyamba sea point no where to kubisala

  • @leviouslongwe2950
    @leviouslongwe2950 3 месяца назад

    Kodi katundu wa a Malemu a Chilima momwe anapemphela Aku banja Lao kuti awabwezere Aku banja, zinathekadi.

  • @GustoJuliusYobe
    @GustoJuliusYobe 3 месяца назад +1

    More fire,more

  • @OscarKathumba
    @OscarKathumba 3 месяца назад +1

    25 million ilowa mu fon? Azanthu airtel tiyakheni

    • @LindaMvula-w9n
      @LindaMvula-w9n 3 месяца назад

      Iwe national Bank more sukuidziwa et ndalama zikakhala mu fon

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 3 месяца назад

    Amtanyiwa ajems woo azisiya ndalama zomwe alandilazo jst send the number ifeso tilikuno ku captown mazula amati bonke lawo bebathi bahlanganiphile basematuneni

  • @Yabwata
    @Yabwata 3 месяца назад

    I always say Malawi is a peaceful country can't you see what's happening in malawi but only kalindo and little others are standing for the truth but if they say let's go pamademo wanthu wose wakukhala chete munyumba zawo nokufuma , but after mademo , nde amayambilaso hee njala hee mavuto aa vazii mademo simumatuluka , can't you see kenya today iyaa, mademo all the people went out no inside the house like Malawi nonsense malawi people..

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 месяца назад

    Tikamati uyu amangopeka khani moti 25 mita ingakhale 4n ya kalindo 😂😂😂😂😂😂😂😂 abale ndiye poti amalawi timasangalala ndimabodza ok tiye nazoni

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 3 месяца назад

    Kusunga ndalama zotero mu phone ndizotheka Inu. Sikuti zonse zingalowe pa kamodzi. You can have ma business and be doing transactions through Airtel money. Momweso amayendera madolo ndizabwino kukhala ndi dollar zambiri mu phone so that they can withdraw everywhere and anytime they need it than kudalira bank. Account siyimakhutatu kuti basi zakwana.

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 месяца назад

    😅😅😅😅😅😂😂😂😂 yomweyo galu iwe achina Sadam angomanga anthu opanda chifukwa aziwona sanati mizimu yakwiya

  • @HassanMbalaka-gb5sv
    @HassanMbalaka-gb5sv 3 месяца назад

    Antanyiwa kod mulibe mfut ija amat snaiper chonde ngat mulinaayo ndibweleken. Asatijaile

  • @MasterBlack-r2n
    @MasterBlack-r2n 3 месяца назад

    kukhale Ku (sea point) kumeneko kapena? kapena cos Ku sea port sinkukuziwa koma Ku sea point.

  • @kanowamndalaphiri2959
    @kanowamndalaphiri2959 3 месяца назад

    Acomrade Mtanyiwa ife aMalawi ochuluka tilipambuyo panu and Mulungu alinanu .ife tidzaimananu pamodzi.zaimfa yaa chilima ndyopweteka koopsa imene mmalawi izavuta kuiwala.

  • @mariamahamadu8402
    @mariamahamadu8402 3 месяца назад

    Ndipo mamulungu yeka atimenyela nkhondo ntanyiwa mulungu akudaliste kodi Boma limabanso

  • @JohnMakokola
    @JohnMakokola 3 месяца назад

    Mulungu si jemus ayise mtanyiwa uwoloka nafe limozi ndichikhulupiliro

  • @HaliJana
    @HaliJana 3 месяца назад

    KOMA PLEASE NDALAMA ZA BON KALINDO MPASENI MUSANAFE OSAKOZA SITIPANGASO ZA KUPOLIC CHIFUKWA KUMALAWI KULIBEKO POLICE KOMA MUSOWA TIKUTI BWEZANI NDALAMAZO TIKUTI AGALU INU

  • @HaliJana
    @HaliJana 3 месяца назад

    KODI AZIKHALI ,CHIMWENDO,KUKUYU CHAKWERA, KUFA KWA CHILIMA SIKUNAKUKWANENI ,MUKUFUNASO KUMAPHASO ANTHU ENASO KODI INU KUPHA SIMUMAPANGA MANTHA MUZAYANKHATU IZI KWA MULUNGU IZI AGALU INU

  • @BwanaGD
    @BwanaGD 3 месяца назад

    Kawawa pitilizani kutidziwitsa zomwe zikupanga zitsiluzi kuphedwa simugaphedwe mr tanyiwa komano zikuzuzika zonkha zitsiluzi tikati tantsala ndi wayires Malawi muno ndi Limpopo bas zinazose zagulidwa ndi mcp

  • @MineMoyo
    @MineMoyo 3 месяца назад

    Asamale jemus makaladi athana naye kuno achita masewela ndipo ayelekeze tiyambapo ndife kuthana naye....