Размер видео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показать панель управления
Автовоспроизведение
Автоповтор
Mmmm shame 😢😢😢😢😢zovesa chisoni abale Mzimu wawo uwuse mu mtendele sure munthu anamfa imfa yowawa
Limbani mtima chemwali. Mlandu sumaora. Mudzasuma boma likadzasintha. Yembekezerani pa Yeheva basi. Pepani 😢😢😢
Ipakaso okupha kumachalenja ondandaula Malawi wakaka ndiuchi unja akupita kuti wasanduka wamangazi ndi misuzi? Zikomo Mulungu ndiamene akuziwa akuthandizani akumbanja sizinaenereke kutero ause mutndere chimwene waifeyo pooezaso amapita kukapanga zachalichi muyembekezere kuona zachilendo kwaoseo amen
Eish chilungamo chikuyenera chiyende ngati madzi apa amqbungwe pls athandizeni nkhani yokhuza iyi😢😢
Ndipo ndizooba 😢😢
Mulungu oziwa chilulungamo akukhuzeni ndi dzanja lake pemphero langa ndi kuthekera kwachofuna chanu (justice)
Mmm yandikhuza komanso kundililitsa Mulungu akukimbitseni mitima yanu nonse akubanja
Achakwela mungotipha amalawi tonse mutchuke ndinu,,, pepani akubanja.
Very sad 😭😭
Zomvesa, chisoni pepani ndithu.
ine ndingakaibwenze live imeneyo ndipo eish angamve kunyuunguunya
Ku police kunalowa chinyengo pano... Kumwamba kuli Mulungu onse apanga izi komaso akubisa chilungamo Mulungu akukatheni
Aeee zosankhala bwino hey km dziko kd likupitakuti😭😭😭 pepani pepani akubanja
Kodi mulibe anyamata oti atha kungobwezera okha zachambazi inuyo musadandauleyi ingobwezerani basi
Pepani ambuye alowelele
Farawo kkkkk mbambanfe
Zovetsa chisoni ndithu
This is very bad, I hope people in authority can help this family.Mr Mgombe why?
Ineyo vuto ndi mm'ang'anja ingotumani munthu akatape phazi basi tilange
Rest in peace
Ambuye akhururukre pepan akubanja
Sizoona ulamulilo uwuwu siulibwinoayi guys chakwela atimaliza guys tiyenitimpephelelechakwela amwalile guys atiphatuuyu
Anthufe koma chikondi chimatisowa kwambiri ambuye yekha ndiamene akuziwa koma
Too bad
Koma dziko iliri limakonderad anthu alemera komanso andale omwe akulamula pa nthaw imeneyoyo,,kumupha munthu opanda chifukwa aaah
Anthu kuyipa kuposa Satan 😭
Chipani cha mcp
Pepani akubanja very sad
Pepani
Mulungu amabweretsa zinthu poyera ndipo choonadi chidziwika komanso munthu umakolora chomwe wabzala. Mu mtima mwanga mukuwawa ndipo mulungu chitani mukuweruza kwanu
Pepani Mulungu atithangatire bas
Zikomo
Sorry
Uyuyu kungomuphanso pogwiritsa ntchito gulu
Very bad
Mmmm shame 😢😢😢😢😢zovesa chisoni abale Mzimu wawo uwuse mu mtendele sure munthu anamfa imfa yowawa
Limbani mtima chemwali. Mlandu sumaora. Mudzasuma boma likadzasintha. Yembekezerani pa Yeheva basi. Pepani 😢😢😢
Ipakaso okupha kumachalenja ondandaula Malawi wakaka ndiuchi unja akupita kuti wasanduka wamangazi ndi misuzi?
Zikomo Mulungu ndiamene akuziwa akuthandizani akumbanja sizinaenereke kutero ause mutndere chimwene waifeyo pooezaso amapita kukapanga zachalichi muyembekezere kuona zachilendo kwaoseo amen
Eish chilungamo chikuyenera chiyende ngati madzi apa amqbungwe pls athandizeni nkhani yokhuza iyi😢😢
Ndipo ndizooba 😢😢
Mulungu oziwa chilulungamo akukhuzeni ndi dzanja lake pemphero langa ndi kuthekera kwachofuna chanu (justice)
Mmm yandikhuza komanso kundililitsa Mulungu akukimbitseni mitima yanu nonse akubanja
Achakwela mungotipha amalawi tonse mutchuke ndinu,,, pepani akubanja.
Very sad 😭😭
Zomvesa, chisoni pepani ndithu.
ine ndingakaibwenze live imeneyo ndipo eish angamve kunyuunguunya
Ku police kunalowa chinyengo pano... Kumwamba kuli Mulungu onse apanga izi komaso akubisa chilungamo Mulungu akukatheni
Aeee zosankhala bwino hey km dziko kd likupitakuti😭😭😭 pepani pepani akubanja
Kodi mulibe anyamata oti atha kungobwezera okha zachambazi inuyo musadandauleyi ingobwezerani basi
Pepani ambuye alowelele
Farawo kkkkk mbambanfe
Zovetsa chisoni ndithu
This is very bad, I hope people in authority can help this family.
Mr Mgombe why?
Ineyo vuto ndi mm'ang'anja ingotumani munthu akatape phazi basi tilange
Rest in peace
Ambuye akhururukre pepan akubanja
Sizoona ulamulilo uwuwu siulibwinoayi guys chakwela atimaliza guys tiyenitimpephelelechakwela amwalile guys atiphatuuyu
Anthufe koma chikondi chimatisowa kwambiri ambuye yekha ndiamene akuziwa koma
Too bad
Koma dziko iliri limakonderad anthu alemera komanso andale omwe akulamula pa nthaw imeneyoyo,,kumupha munthu opanda chifukwa aaah
Anthu kuyipa kuposa Satan 😭
Chipani cha mcp
Pepani akubanja very sad
Pepani
Mulungu amabweretsa zinthu poyera ndipo choonadi chidziwika komanso munthu umakolora chomwe wabzala. Mu mtima mwanga mukuwawa ndipo mulungu chitani mukuweruza kwanu
Pepani Mulungu atithangatire bas
Zikomo
Sorry
Uyuyu kungomuphanso pogwiritsa ntchito gulu
Very bad
Zomvesa, chisoni pepani ndithu.