BREAKING NEWS NAMIYANGO - MUNTHU WAPEZEKA ATAFA MNYUMBA KU NAMIYANGO.

Поделиться
HTML-код

Комментарии • 79

  • @patriciakanjanga1284
    @patriciakanjanga1284 5 месяцев назад +6

    anthu akachite lenti pakhomo panu ndinu makolo aanthuwo chonde mukaona kuti khomo silikutsegulidwa kwa masiku angapo chonde muzipita nkukaona chachitika ndi chani mpaka masiku angapo landlorad osadziwapo kanthu mzimu wao uuse mutendere

  • @Margaret-t7m
    @Margaret-t7m 5 месяцев назад +7

    Zomvetsa chisoni 😭😭😭😭😭😭 komanso titengelepo phunziro chifukwa tima wanzako ndi sidya lina, Rest in peace mama

  • @mphatsolupiabanda6910
    @mphatsolupiabanda6910 5 месяцев назад +4

    We love you Director wa mkhalango multimedia

  • @Cecilia-f9u5u
    @Cecilia-f9u5u 5 месяцев назад +5

    Malandlod muzikhala serious 4d

  • @collinstrevor
    @collinstrevor 5 месяцев назад +11

    Zimu wake sukhala chete wapanga zimenezi adziwika

  • @stephenschipolo5296
    @stephenschipolo5296 4 месяца назад +1

    Umatha Harry. Keep it up! Well covered and narrated

  • @AngungaThatcherNgoma
    @AngungaThatcherNgoma 5 месяцев назад +3

    Good Narrater

  • @ThembiweKapukayenda
    @ThembiweKapukayenda 3 месяца назад +1

    Eish too bad😢😢

  • @endphiri3933
    @endphiri3933 3 месяца назад +1

    Inna lilah wa inalahijuna

  • @Zamwano
    @Zamwano 5 месяцев назад +1

    Moyo ophana achinyama chepesani sibwino kuchosa moyo wamuzako ngati mwalakwilana kambilanani mwaufuna basi Chatha Chatha mukapeza wina,,,, landlord alibe vuto pamenepo sankaziwa chilichonse oipa ndiwakuphayo Ambuye Mulungu amukanthe komwe aliko Galu kwabasi

  • @khadjahmustafa8273
    @khadjahmustafa8273 5 месяцев назад +1

    My home land Namiyango

  • @AnitaChakwana
    @AnitaChakwana 3 месяца назад

    Ine mmoyo uno ndaphuzila zambili muthu ndimamuwopa ndipo sindidzakhulupilira muthu ndachita matha iiii😭😭😭😭

  • @DuncanMataka
    @DuncanMataka 4 месяца назад +1

    Ambuye amulankhule wapangazoterezi mwazisisi amuziwe yesu.

  • @Cynthia-gv9gh
    @Cynthia-gv9gh 4 месяца назад +1

    Imfa yomvesa chison pamaso ngat akukonda mtima muli nkhondo,rest well mama😭😭💔

  • @DorothyKamanga-l9j
    @DorothyKamanga-l9j Месяц назад

    RIP 💔💔💔💔

  • @phylessmphanda3251
    @phylessmphanda3251 2 месяца назад

    RIP 🙏

  • @AyandaTshontini
    @AyandaTshontini 5 месяцев назад +1

    Akapezeka munthuyo straight wakumaula munthu woipa kwambiri khalidwe laukape

  • @BillyKalambo-jx3vf
    @BillyKalambo-jx3vf 5 месяцев назад +1

    Tiuzeni malonda omwe amachita nsungwanayo osabisa tangonenani kuti anali hule bwanji???

  • @TyamikeTiyako
    @TyamikeTiyako Месяц назад

    Eish kulakwa

  • @StanleyMatewere
    @StanleyMatewere 3 месяца назад

    Eish....too sad

  • @NdazionaKumcheza
    @NdazionaKumcheza 3 месяца назад

    Landlord ogona osachita monitor wa lent wako

  • @bmbboymstyles5894
    @bmbboymstyles5894 4 месяца назад

    Eishhhh koma zinthu zake😢😥😥

  • @ABASHACeeMW
    @ABASHACeeMW 5 месяцев назад

    Ina Lillah waina ilaih rajuhunah 😢😢😢

  • @Yusufu-ul5ec
    @Yusufu-ul5ec 4 месяца назад

    Eish zosayenda mmmmm zosakhala bwino
    Mzimu wake uuse mu mtendere

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 4 месяца назад

    My Malawi 😭😭😭😭😭

  • @GeorgeKasambwe
    @GeorgeKasambwe 5 месяцев назад

    May her soul rest in peace

  • @janemanyamba7201
    @janemanyamba7201 4 месяца назад

    Kuyeza kwakanika?

  • @PempheroPaliani-ke3ez
    @PempheroPaliani-ke3ez 3 месяца назад

    So sad

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 5 месяцев назад

    Very sad 😢

  • @EmilyPade
    @EmilyPade 5 месяцев назад

    Sad news

  • @CharlesMadulira-px8yq
    @CharlesMadulira-px8yq 5 месяцев назад

    Mmmm very sad anthu tikulimba mtima moopsa

  • @sibokawana2358
    @sibokawana2358 5 месяцев назад

    So sad😢😢

  • @Franz5Khoriyo
    @Franz5Khoriyo 4 месяца назад

    Following

  • @nimrodkapingatheu5475
    @nimrodkapingatheu5475 4 месяца назад

    Eni ake nyumbawa nganzeru... Ndi munthu wachikuliledi

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 4 месяца назад

    Koma azimunafe eeeeeeeeeee zovuta zedi mmmm😢😢😢😢😢😢

  • @JunnieMulazie
    @JunnieMulazie 5 месяцев назад

    Mmmm Sad😭

  • @patricktembo1160
    @patricktembo1160 4 месяца назад

    Zomvesa chison kwambili 😢😢😢

  • @janemanyamba7201
    @janemanyamba7201 4 месяца назад

    Alandlod mumakaniza kii kwa m,bale wake????

  • @TelezaMzia
    @TelezaMzia 5 месяцев назад

    Eishii 😭😭😭😭

  • @VictoriaWilliam-ms2ft
    @VictoriaWilliam-ms2ft 5 месяцев назад

    Eish 😭😭😭 Kulakwa

  • @FrancePhangula
    @FrancePhangula 4 месяца назад

    Zomvetsa chisoni 😭😭😭😭

  • @Rhoda-g1y
    @Rhoda-g1y 5 месяцев назад

    😭😭zovesa chisoni

  • @GiboTakondwa
    @GiboTakondwa 5 месяцев назад

    Khalidwe lophanali silingasinthe khalidweli anthu akuchicha kuwonela chifukwa pano mulandu wakupha ulibe ntchito khalidweli labwela ndianthu andale able athu achialubino anatha milanduyake kukulibeko mpaka pano lelo ena ndiaja anapha witika nanga mayi wakulizevu banki uja Malawi tiyeni tsiku Lina tizikhalangati osamva tiyambe tokha kulañga anthu opanga chipongwe azawo tikawagwila chifukwa kupolisi kulibe chimene chiliko kukhoti nakonso kwangosala mapoto obowoka okha okha

  • @TracciaChizinga-o9d
    @TracciaChizinga-o9d 5 месяцев назад

    This is too bad

  • @MosesChileka
    @MosesChileka 3 месяца назад

    Dzimuwamunthu, ndioopya apezeka

  • @amoschilangiza
    @amoschilangiza 4 месяца назад

    Zachitika liti?

  • @RichardMwamadi
    @RichardMwamadi 3 месяца назад

    Zomvesa chison koma wapanga zimenezoyo mulungu amuwone

  • @ChifundoMwale-yp1iz
    @ChifundoMwale-yp1iz 5 месяцев назад

    😢😢😢 shem

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 4 месяца назад

    Azimunawo anagona nawowo anali angati??

  • @Takondwac
    @Takondwac 3 месяца назад

    😢😢😢😢😢😢

  • @egreymkumba-tj5ji
    @egreymkumba-tj5ji 4 месяца назад

    😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @issadinala125
    @issadinala125 5 месяцев назад

    Eeeee zosaendatu iz 😢

  • @AminSoko
    @AminSoko 3 месяца назад

    Zovutatu malawi mmmm

  • @chifundoalfred14
    @chifundoalfred14 4 месяца назад

    Zovuta kwambili

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 5 месяцев назад

    It's too bad eish kma zophanazi Eeeeee

  • @isaaczidana2914
    @isaaczidana2914 5 месяцев назад

    Mkulakwa kuchotsa Moyo wanzako

  • @zaithwachiwaya
    @zaithwachiwaya 5 месяцев назад

    😭

  • @PeterEriko
    @PeterEriko 5 месяцев назад

    Khalango maltimadia ndi dilu

  • @EmmanuelManiya-dz5ry
    @EmmanuelManiya-dz5ry 3 месяца назад

    Zoopsa kwabasi

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 4 месяца назад

    Malawi mmmmmmmmmmmmm

  • @KabayifaBilu
    @KabayifaBilu 26 дней назад

    Zo 😂😂

  • @BudaEarth
    @BudaEarth 2 месяца назад

    Zoopsa

  • @Lufeo-kx8kf
    @Lufeo-kx8kf 4 месяца назад

    Sizinthu zabwin koma 11:19

  • @TeresaSaudeNampalala
    @TeresaSaudeNampalala 4 месяца назад

    Eee zomvetsa chison

  • @BeatriceBiziweck
    @BeatriceBiziweck 5 месяцев назад

    Zosakhala bwino

  • @EnockMtengula
    @EnockMtengula 5 месяцев назад

    Eeeeee km

  • @gideonnyirongo2202
    @gideonnyirongo2202 3 месяца назад

    Manase

  • @CharlesMulikhiwa
    @CharlesMulikhiwa 4 месяца назад

    Akapezeks waphayo aotchedwe chifukwa akapita ku polisi kungopereka 3000 basi amutulutsa then aziphabe

  • @patricktembo1160
    @patricktembo1160 4 месяца назад

    Zomvesa chison kwambili 😢😢😢

  • @mercymagola
    @mercymagola 4 месяца назад

    😭😭😭😭😭😭

  • @ChrispinChikagwa
    @ChrispinChikagwa 5 месяцев назад

    Zosakhala bwino

  • @lingstonenagoli7729
    @lingstonenagoli7729 5 месяцев назад

    Zomvetsa chisoni kwambiri😢