Continu.. Part 2

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 4 фев 2023

Комментарии • 60

  • @estherlangson1789
    @estherlangson1789 4 месяца назад

    I ve followed the story am from Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲

  • @phylessmphanda3251
    @phylessmphanda3251 19 дней назад

    Eishhhh God have mercy upon Malawi😢

  • @ChakuVillage077
    @ChakuVillage077 Год назад +1

    Mmmmmmm Malawi, too bad watching from Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲

  • @paulkaunda6780
    @paulkaunda6780 Год назад +5

    Achewa muli ndi ntchito choncho dziko lingatukuke sham

  • @FartisonNjolomole
    @FartisonNjolomole 10 дней назад

    All very wonderful Malawi what's going on?

  • @estherlangson1789
    @estherlangson1789 4 месяца назад

    I pray for my brother sisters and my dad kuti mwina naonso angabwele coz sitikhutila nazo imfa zao

  • @gladyschisomo4324
    @gladyschisomo4324 Год назад +2

    Kukhwima kwake kopusapusa nanga kulemela kwake kulipati nyumba yadothi lokhalokha

  • @violethamidayassin
    @violethamidayassin 8 месяцев назад +3

    I pray my husband to come back five years now Koma still sindikhutisidwa mpakana pano

  • @RoseChirwaKhofi
    @RoseChirwaKhofi 2 месяца назад +1

    Ambuye sizingachitikileko ine izi adad kungotulukila mmmmm😭😭😭😭

  • @Mary-hx9fc
    @Mary-hx9fc Год назад +2

    Sonawonepo zolemela kungozizuzapo ndiza ziii

  • @petermtema5241
    @petermtema5241 Год назад

    I have followed the whole story of Mr sato and the omighty Lord should drop more miracles to this village so that people there have to live without fear.

  • @paulkaunda6780
    @paulkaunda6780 Год назад +2

    Malawi nkhanza

  • @danieldicksonmbetewa4911
    @danieldicksonmbetewa4911 Год назад +2

    Att Ng'ombe 5🤣🤣🤣🤣

  • @muiwalenjobvu9841
    @muiwalenjobvu9841 11 дней назад

    Amalawi nzoopsa.

  • @dainesmumba1101
    @dainesmumba1101 9 месяцев назад +1

    amalawi muzipenpela kwambili🇿🇲🇿🇲🇿🇲😭😭🙏

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 Год назад +3

    mukufanana mphuno komanso nkhope..zomvetsa chisoni

  • @ThokoKaipa
    @ThokoKaipa 3 месяца назад +1

    Zosatheka ndi anthu zimatheka ndi ambuye ,,,may God reveal all the secrets in this world

  • @mbawabuliyan9704
    @mbawabuliyan9704 Год назад +2

    Koma kulemela kuli pati apa umfiti si zithu sure

  • @sydneykumisuku1380
    @sydneykumisuku1380 Год назад +2

    Wakufa sadziwa kanthu bii

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 Год назад +2

    Lord have mercy on us. May you deliver your people.

  • @lifeofqueennagama1935
    @lifeofqueennagama1935 Год назад +5

    Oh my God!.. miracle working God please bring back his senses 🙏🙏

  • @YamikaniManyamba
    @YamikaniManyamba Месяц назад

    Abale ndiluti sindikuvesesa momwe wamwalila mwana wanga yekha yekha ndinabeleka , Pano Ali ndi mwezi pasi, koma chomwe chikundidabwisa Amati apopano beseni lomwe amasambikira mtembo anangoliyika kusi Kwa bed kwawo , kuwauza andipase akukanilila abale ndithandizeni ndithu

  • @SomtoochukwuNwokwe
    @SomtoochukwuNwokwe Год назад

    Ambuye asala pang,one kubwera tiyyeni tirape a abare anga chance nthaw yantha

  • @ChimtengoRabecca-lv2kc
    @ChimtengoRabecca-lv2kc Год назад

    Amalimatu mesa amalimisa mizukwa anawachita bwino bambo akowo afit inu agalu mukuzuza amzanu kwambir

  • @AustinGift-j5w
    @AustinGift-j5w Месяц назад

    🙆🤷

  • @sharonjalamu8657
    @sharonjalamu8657 Год назад +3

    Kma anthu mumalakwa ufit ilipo ndthu

  • @dainesmumba1101
    @dainesmumba1101 9 месяцев назад

    Amalawi kodi mwatani kodi mulungu alimumalawi

  • @Rashidmw79
    @Rashidmw79 Год назад +1

    Anthu Ali ndi nsambi ndinthu mmmmm

  • @maxwellmustafa3078
    @maxwellmustafa3078 Год назад

    Amalawi azanga moyo wopepetula abale anu pofuna kulemera simoyo wabwino ndithu

  • @shaibukeakeni6224
    @shaibukeakeni6224 Год назад +2

    Much respect boss ❤️

  • @mphatsochopenga6357
    @mphatsochopenga6357 Год назад +5

    Koma anthu amaipatu

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire Месяц назад

    Eeeh Koma munthu !!!

  • @brendatamlangani7823
    @brendatamlangani7823 Год назад

    Zaziiizo ng'ombe 5 zophela athuzo zaziiizo mxweuuuuuuuuuuu

  • @AlicePhiri-dp8ho
    @AlicePhiri-dp8ho 2 месяца назад

    Mr sato where are you now too bad from chama zambia

  • @LidasiKangwanda-dg6cx
    @LidasiKangwanda-dg6cx Год назад

    Tili masiku otsiriza nde zobisika zose zayanera kukhara pamtunda

  • @Mary-hx9fc
    @Mary-hx9fc Год назад +1

    Ndiye aziti ufiti kulibe

  • @ElinaMkandawire-hy1ct
    @ElinaMkandawire-hy1ct Год назад

    Komatu agogowo akufunika thandizo lakuchipatara

  • @chifunirosaka9077
    @chifunirosaka9077 Год назад

    Palibeso kulemela apa munthuyu anangokhala chabe mfiti

  • @user-xk9vs9qc2s
    @user-xk9vs9qc2s 9 месяцев назад

    Chofunika kuima pa maso pa mulungu

  • @MarkoMhango
    @MarkoMhango 11 месяцев назад

    Zaka zadusapo zochepa kakumben manda mukawonemo mafupa

  • @user-fe6pp9gc6u
    @user-fe6pp9gc6u 7 месяцев назад

    Koma mlungu. S mthu

  • @user-xf1gb5gu3z
    @user-xf1gb5gu3z 3 месяца назад

    That family needs a breakthrough and deliverance, God have mercy on this family.

  • @RabanaSani-pq6oh
    @RabanaSani-pq6oh 10 месяцев назад

    Lunch time

  • @esankalipande433
    @esankalipande433 Год назад

    Kodi bwanji kukumba mmandamo ndikutsimikiza ndithu

    • @tiwongemandala3140
      @tiwongemandala3140 9 месяцев назад

      Akakakumba akampeza, it's spiritual thing u know

  • @user-ps4hd6rs8k
    @user-ps4hd6rs8k 5 месяцев назад

    😢

  • @AbdulFernandoFernando-pr2nd
    @AbdulFernandoFernando-pr2nd 3 месяца назад

    Ufiti malawi

  • @aleksawilliams710
    @aleksawilliams710 Год назад +2

    Shame

  • @user-hw8ds8oy6i
    @user-hw8ds8oy6i 6 месяцев назад

    Ufiti ulipodi a Malawi mmmmmm

  • @clementmwiinga6145
    @clementmwiinga6145 Год назад +1

    People are bad wichchruft is real

  • @user-kh9cr9dl7x
    @user-kh9cr9dl7x 11 месяцев назад

    A chewa koma

  • @eunicemoyo6024
    @eunicemoyo6024 Год назад

    Kom uphawi sizinthu kusowa zochita chifukwa cha uphawi

  • @macksenphiri-lv1qy
    @macksenphiri-lv1qy Год назад

    L

  • @dicksonphili3466
    @dicksonphili3466 2 месяца назад

    Ufit ulipod mmmmm

  • @gladyschisomo4324
    @gladyschisomo4324 Год назад +2

    Kukhwima kwake kopusapusa nanga kulemela kwake kulipati nyumba yadothi lokhalokha