Размер видео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показать панель управления
Автовоспроизведение
Автоповтор
I ve followed the story am from Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲
Eishhhh God have mercy upon Malawi😢
Mmmmmmm Malawi, too bad watching from Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲
Achewa muli ndi ntchito choncho dziko lingatukuke sham
All very wonderful Malawi what's going on?
I pray for my brother sisters and my dad kuti mwina naonso angabwele coz sitikhutila nazo imfa zao
Kukhwima kwake kopusapusa nanga kulemela kwake kulipati nyumba yadothi lokhalokha
I pray my husband to come back five years now Koma still sindikhutisidwa mpakana pano
Ambuye sizingachitikileko ine izi adad kungotulukila mmmmm😭😭😭😭
Sonawonepo zolemela kungozizuzapo ndiza ziii
I have followed the whole story of Mr sato and the omighty Lord should drop more miracles to this village so that people there have to live without fear.
Malawi nkhanza
Att Ng'ombe 5🤣🤣🤣🤣
Amalawi nzoopsa.
amalawi muzipenpela kwambili🇿🇲🇿🇲🇿🇲😭😭🙏
mukufanana mphuno komanso nkhope..zomvetsa chisoni
Eyaa
Zosatheka ndi anthu zimatheka ndi ambuye ,,,may God reveal all the secrets in this world
Koma kulemela kuli pati apa umfiti si zithu sure
Wakufa sadziwa kanthu bii
Lord have mercy on us. May you deliver your people.
Oh my God!.. miracle working God please bring back his senses 🙏🙏
How are you ❤❤❤❤❤
Abale ndiluti sindikuvesesa momwe wamwalila mwana wanga yekha yekha ndinabeleka , Pano Ali ndi mwezi pasi, koma chomwe chikundidabwisa Amati apopano beseni lomwe amasambikira mtembo anangoliyika kusi Kwa bed kwawo , kuwauza andipase akukanilila abale ndithandizeni ndithu
Ambuye asala pang,one kubwera tiyyeni tirape a abare anga chance nthaw yantha
Amalimatu mesa amalimisa mizukwa anawachita bwino bambo akowo afit inu agalu mukuzuza amzanu kwambir
🙆🤷
Kma anthu mumalakwa ufit ilipo ndthu
Amalawi kodi mwatani kodi mulungu alimumalawi
Anthu Ali ndi nsambi ndinthu mmmmm
Amalawi azanga moyo wopepetula abale anu pofuna kulemera simoyo wabwino ndithu
Much respect boss ❤️
Koma anthu amaipatu
Eeeh Koma munthu !!!
Zaziiizo ng'ombe 5 zophela athuzo zaziiizo mxweuuuuuuuuuuu
Mr sato where are you now too bad from chama zambia
Tili masiku otsiriza nde zobisika zose zayanera kukhara pamtunda
Ndiye aziti ufiti kulibe
Komatu agogowo akufunika thandizo lakuchipatara
Palibeso kulemela apa munthuyu anangokhala chabe mfiti
Chofunika kuima pa maso pa mulungu
Zaka zadusapo zochepa kakumben manda mukawonemo mafupa
Koma mlungu. S mthu
That family needs a breakthrough and deliverance, God have mercy on this family.
Lunch time
Kodi bwanji kukumba mmandamo ndikutsimikiza ndithu
Akakakumba akampeza, it's spiritual thing u know
😢
Ufiti malawi
Shame
Ufiti ulipodi a Malawi mmmmmm
People are bad wichchruft is real
A chewa koma
Nanuso ndachewa amenewa?
Kom uphawi sizinthu kusowa zochita chifukwa cha uphawi
L
Ufit ulipod mmmmm
Ai ndimasiku yotsiliza,,
I ve followed the story am from Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲
Eishhhh God have mercy upon Malawi😢
Mmmmmmm Malawi, too bad watching from Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲
Achewa muli ndi ntchito choncho dziko lingatukuke sham
All very wonderful Malawi what's going on?
I pray for my brother sisters and my dad kuti mwina naonso angabwele coz sitikhutila nazo imfa zao
Kukhwima kwake kopusapusa nanga kulemela kwake kulipati nyumba yadothi lokhalokha
I pray my husband to come back five years now Koma still sindikhutisidwa mpakana pano
Ambuye sizingachitikileko ine izi adad kungotulukila mmmmm😭😭😭😭
Sonawonepo zolemela kungozizuzapo ndiza ziii
I have followed the whole story of Mr sato and the omighty Lord should drop more miracles to this village so that people there have to live without fear.
Malawi nkhanza
Att Ng'ombe 5🤣🤣🤣🤣
Amalawi nzoopsa.
amalawi muzipenpela kwambili🇿🇲🇿🇲🇿🇲😭😭🙏
mukufanana mphuno komanso nkhope..zomvetsa chisoni
Eyaa
Zosatheka ndi anthu zimatheka ndi ambuye ,,,may God reveal all the secrets in this world
Koma kulemela kuli pati apa umfiti si zithu sure
Wakufa sadziwa kanthu bii
Lord have mercy on us. May you deliver your people.
Oh my God!.. miracle working God please bring back his senses 🙏🙏
How are you ❤❤❤❤❤
Abale ndiluti sindikuvesesa momwe wamwalila mwana wanga yekha yekha ndinabeleka , Pano Ali ndi mwezi pasi, koma chomwe chikundidabwisa Amati apopano beseni lomwe amasambikira mtembo anangoliyika kusi Kwa bed kwawo , kuwauza andipase akukanilila abale ndithandizeni ndithu
Ambuye asala pang,one kubwera tiyyeni tirape a abare anga chance nthaw yantha
Amalimatu mesa amalimisa mizukwa anawachita bwino bambo akowo afit inu agalu mukuzuza amzanu kwambir
🙆🤷
Kma anthu mumalakwa ufit ilipo ndthu
Amalawi kodi mwatani kodi mulungu alimumalawi
Anthu Ali ndi nsambi ndinthu mmmmm
Amalawi azanga moyo wopepetula abale anu pofuna kulemera simoyo wabwino ndithu
Much respect boss ❤️
Koma anthu amaipatu
Eeeh Koma munthu !!!
Zaziiizo ng'ombe 5 zophela athuzo zaziiizo mxweuuuuuuuuuuu
Mr sato where are you now too bad from chama zambia
Tili masiku otsiriza nde zobisika zose zayanera kukhara pamtunda
Ndiye aziti ufiti kulibe
Komatu agogowo akufunika thandizo lakuchipatara
Palibeso kulemela apa munthuyu anangokhala chabe mfiti
Chofunika kuima pa maso pa mulungu
Zaka zadusapo zochepa kakumben manda mukawonemo mafupa
Koma mlungu. S mthu
That family needs a breakthrough and deliverance, God have mercy on this family.
Lunch time
Kodi bwanji kukumba mmandamo ndikutsimikiza ndithu
Akakakumba akampeza, it's spiritual thing u know
😢
Ufiti malawi
Shame
Ufiti ulipodi a Malawi mmmmmm
People are bad wichchruft is real
A chewa koma
Nanuso ndachewa amenewa?
Kom uphawi sizinthu kusowa zochita chifukwa cha uphawi
L
Ufit ulipod mmmmm
Kukhwima kwake kopusapusa nanga kulemela kwake kulipati nyumba yadothi lokhalokha
Ai ndimasiku yotsiliza,,