Ogulitsa Ziwalo Xa Anthu Agwida Ku Thyolo.

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 20 окт 2024

Комментарии • 169

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 4 месяца назад +7

    TA you are more a patriotic citizen.May God bless you.Malawi is lacking such leaders even in religious and political fields.

  • @rosebanda3613
    @rosebanda3613 Год назад +1

    Ulemu wanu manjolo and hands up to Ta. TA you are wise like king Solomon may God bless you with more wisdom

  • @charlesmpaso2383
    @charlesmpaso2383 Год назад +8

    Anthu awa akuyenera kukwezedwa udindo komaso akufunika chitetezo.....mulungu oziwa kusamala akutetezeni mu zonse pamodzi ndi ma family anu.... AMEN AND AMEN.U DESERVE AWARDS GUYS.

  • @moseschizyibwa4463
    @moseschizyibwa4463 Год назад +3

    I like this program. Watching from zambia, Moses

  • @LawrentNgoma-o4o
    @LawrentNgoma-o4o Год назад +2

    Really appreciate nkhani izikhala in full video osabisa maina olakwayo ndiokhudzidwawo.

  • @AngellinaUsman
    @AngellinaUsman Год назад +3

    My God bless you mr manjolo ndi
    T/A mukhale ndi moyo fumu❤

  • @khoviwaedward
    @khoviwaedward Год назад +29

    This guy is really true Malawian legend.. Wapulumutsa moyo wamwana. The government should recognise him, awards is coming bro

    • @innocentjames_01
      @innocentjames_01 Год назад +1

      For sure 😊

    • @hanabrighton9903
      @hanabrighton9903 Год назад +1

      Koma zoona this man must be recognized as a legent

    • @PempheroMkusangombe
      @PempheroMkusangombe 7 месяцев назад

      Mulungu akudalitseni amfumu ndi manjolo

    • @JosephMkandawire-sq7uf
      @JosephMkandawire-sq7uf 6 месяцев назад

      Mumagula inu guys

    • @CatherineDesire
      @CatherineDesire 3 месяца назад

      Anakakhara Ngati Maiko anzathuwa aindithu anakapangapo kachithokodzo ndithu kooneka pa Mfumuyi NDI azakewa Koma🤔mmmm h Malawi a Magadzi mmmm ndukaika anakakhala mwina NDI dzina Lina otsati Malawi coz ma🔥gahena mmmmmh ayi ndithu kuteloko lakwiya bomalo akumipandoko 😂😂😂😂😂😂 Kuti ena apulumutsetso mwana?coz iwowo NDI👹👿👺kare kupha NDI kuononga 😂😂😂😂😂 wafikapo aise Ma🔥lawi iwe🙌ndakuponyera kukhara ngati unalengapo munthu Malawi👹👿👺🤔😔

  • @luciachimbalawala3545
    @luciachimbalawala3545 5 месяцев назад +1

    God bless you manjolo and the T/A for job well done im watching from lusaka zambia❤

  • @olivechikwindi9126
    @olivechikwindi9126 Год назад +7

    😭😭😭😭YESU akuchedweranji kubwera koma?AMBUYE akudalitseni A/T ndipo akupatseni moyo wautali and Mr manjolo God bless you mukhale wotetedzedwa anthuwa

  • @Hildamakebu
    @Hildamakebu 3 дня назад

    Tithokoze aT/A ndi Mr. Manjolo polimba mtima kupulumutsa moyo wa mwana ku imfa ngati imeneyi. Enatu anakakonda ndalama kusiyana ndi moyo wa munthu. God bless you.

  • @johndaka6368
    @johndaka6368 Год назад +2

    That's ws good pran AMALAWI
    Am John from Lusaka Zambia

  • @chifundomhango3324
    @chifundomhango3324 Год назад +9

    Good job Mr Manjolo & T/A❤

  • @princekabvina1718
    @princekabvina1718 Год назад +10

    Manjolo he deserve an award,,,well done Mr Manjolo and T/A

  • @ChimwemweNthukwa-fw3qj
    @ChimwemweNthukwa-fw3qj 7 месяцев назад +4

    Amen Ambuye alemekezeke, amfumu abwino okonda amalawi anzawo!! Ambuye akudalitseni a amfumu

  • @Davison-jr6ev
    @Davison-jr6ev 8 месяцев назад +1

    Yes this guy and the TA must gain some thing from the the government for rescued the boys who was about to lose his life,

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 Год назад +8

    long live amfumu ndi Manjolo..Ambuye akutetezeni

    • @Richardbanda-hg6pt
      @Richardbanda-hg6pt Месяц назад +1

      May God bless you all as well as the chief ❤in Aroma 13v1

  • @collinsassenga3711
    @collinsassenga3711 Год назад +2

    a T A Mr manjolo mulungu akudalitseni, a T A kuyambira lero ndinu mfumu Solomon.

  • @gkay-striker
    @gkay-striker 8 месяцев назад +2

    You did a great job

  • @chitimbethegreat8560
    @chitimbethegreat8560 Год назад +1

    Mr TA well done mwagwira ntchito mafumu ambiri amakonda ndalama and mchitidwe oterewu umakula chifukwa mafumu amatenga nawo gawo koma Inu simunatero ulemu wanu ndi Mr majolo

  • @collinsassenga3711
    @collinsassenga3711 Год назад +2

    Chilungamu chiyende ngati madzi, AT ndi mr manjolo mulungu akudalitseni.

  • @ChifundoJames-ks6pr
    @ChifundoJames-ks6pr 10 дней назад

    God bless u mr manjolo.

  • @johndaka6368
    @johndaka6368 Год назад +1

    Manjolo akhale wa police am JOHN daka from Lusaka Zambia

  • @ephraimnjikho9307
    @ephraimnjikho9307 Год назад +2

    If all Malawians were like Manjolo and the TA, such cases could have been on the decrease.
    People are very hard hearted.

  • @DenisAntonio-bn5ey
    @DenisAntonio-bn5ey 11 месяцев назад

    Big up to Mr manjolo and the t.a, 4such a good job done.❤

  • @PeacefulWildFlowers-sl8er
    @PeacefulWildFlowers-sl8er 9 месяцев назад +1

    Mafumu a smart❤❤❤

  • @ausbonchimgolo9984
    @ausbonchimgolo9984 Год назад +4

    Manjolo and T/A they deserve a medal

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 3 месяца назад

    😂😂,😂koma Lawez 🙌wafikapo eeeh!dzikomo amfumu Mlungu akupatseni moyo wautali ndithu

  • @HenryGulani-fq5js
    @HenryGulani-fq5js 5 месяцев назад

    Mlu dzikomo kwambili mulungu Akudalitseni 🙏🙏 ine ndili Joz

  • @lindsonexton8563
    @lindsonexton8563 Год назад

    Inu ndi akatundu odziwa kufufuza nkhani, you deserve a medal

  • @usherkays4379
    @usherkays4379 Год назад

    Thanks to the TA for exposing the criminals and protecting the nation

  • @chrissyamanda5510
    @chrissyamanda5510 Год назад

    Manjolo atetezedwe ndi mwazi wa Yesu
    Ndikutha kuwona kuti moyo wake uli pa chiopsezo koma Ambuye wanthu ngwa moyo ndipo ndi mgonjetsì

  • @PempheroMkusangombe
    @PempheroMkusangombe 7 месяцев назад +2

    T/A akutetezeni Mulungu ndi manjolo akupatseni moyo wautali

  • @FatimaBanda-b3s
    @FatimaBanda-b3s 7 месяцев назад

    😭😭😭😭😭 God bless you my brother all the best in your life 🙏

  • @jamesngalande4345
    @jamesngalande4345 Год назад +5

    thats true your heros boma likuyenera kukuthokozani kuti anthu ena akawona atengelepo phunziro

    • @bjmtalimanja5073
      @bjmtalimanja5073 Год назад

      Pakufunika apasidwe unduna wa za chitetezo mdziko mino.wosati zisilu zomwe chakwera azisankha zija

    • @fosterphiri5366
      @fosterphiri5366 Год назад

      Mulungu akukwezeni afumu ndakutukulilani muma ja a yehova

    • @juniorbvumbwe9822
      @juniorbvumbwe9822 Год назад

      Akanagwirisa mawu ot opha nzake aphedwe bas

  • @williamchanza5338
    @williamchanza5338 Год назад +3

    This guy s a hero

  • @MariaKamanga-u3p
    @MariaKamanga-u3p Год назад +1

    Keep it up Manjolo and T/A. May the almighty God, bless both of you.

  • @PeterMillionAntonio
    @PeterMillionAntonio Год назад

    Well done Mr T/A

  • @TiwongeLuwe
    @TiwongeLuwe Год назад

    Government give thanks to the people for sure they did great job 👏

  • @ThokoKaipa
    @ThokoKaipa 6 месяцев назад

    God is revealing himself to people,,,that child is just innocent and God is watching upon him

  • @mcdonaldkamanga6919
    @mcdonaldkamanga6919 7 месяцев назад

    Title of the song please

  • @janetmanda6412
    @janetmanda6412 Год назад +8

    After so many years now the secret is out, my question is is the police keep secrets also?

  • @noahmshanga-rb1xc
    @noahmshanga-rb1xc Год назад

    Mmmmm! MR MANJOLO and the headman they need to be on the better position and please my fellow youths do not be influenced in such calectors even if things can be bad in life try your best to do the right thing like what MR MANJOLO and the village HEADMAN.

  • @SurprisedBaseballEquipme-by6sp
    @SurprisedBaseballEquipme-by6sp День назад

    God bless you

  • @PeacefulWildFlowers-sl8er
    @PeacefulWildFlowers-sl8er 9 месяцев назад

    Ulemu wanu mr manjolo❤❤❤

  • @matiasncalaila4003
    @matiasncalaila4003 Год назад +1

    Nanga Judgement yatha bwanji? Nanga anthu 5 womwe akugulisapo ndi ati? Amagulitsira kuti? Nanga anthu amenene anagula Boma lichita nawo chiyani? We need Justice. Manjolo Ambuye Akudalitse komanso a T.A pamaganizo yawo ya bwino yofuna munthu wamoyo, tikana luza mwana.

  • @HawaChifi
    @HawaChifi 7 месяцев назад

    Strong man manjolo💪

  • @ChinsinsiMaseso
    @ChinsinsiMaseso Год назад

    Boma lichitepo kanthu, big up Manjolo and T/A

  • @Elvin-dr8tv
    @Elvin-dr8tv 6 месяцев назад

    Well-done Manojolo

  • @jamesngalande4345
    @jamesngalande4345 Год назад +3

    Jesus

  • @PeterMillionAntonio
    @PeterMillionAntonio Год назад

    Manjolo u are a king

  • @LenackMoyo-jz2fl
    @LenackMoyo-jz2fl 11 месяцев назад

    Please those who are doing this dirty thing should face the law.

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 4 месяца назад

    Malawi is no longer at ease.Laws have to revised

  • @RaphaelMusa-x5t
    @RaphaelMusa-x5t 3 месяца назад

    It's really fine

  • @dalitsochibisa2986
    @dalitsochibisa2986 Год назад +1

    Zikomo kwa bwana TA and the team who helped to rescue the boy

  • @officefileofficefile4771
    @officefileofficefile4771 Год назад

    Dziko la Malawi atulusidwa amenewo, chisanzo nachimpanti anamutulusa kale Ali kuno ku South Africa, nkhani ngati zimenezi athu m'boma zimakhala kuti zikuwakhuza

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 Год назад +2

    Chochi ndi kumati lamulolonyonga lichoke nooo am saying nooo!!!!! Athuawa akuenela kunyongedwaaja ndiawa for sure ❗❗❗❗❗❗❓❓

    • @hucklyrajabu7137
      @hucklyrajabu7137 Год назад

      That true my bro wapha mzake naye aphedwe chifukwa kuchotsa moyo wamzako sichinthu chapafupi

  • @kingmakala3919
    @kingmakala3919 Год назад +1

    GOOD JOB BRO🙏

  • @oliviasullivan1059
    @oliviasullivan1059 2 месяца назад

    Nkhani yogulisa ziwalo zinayamba kale kale ndipo ine ndikukumbukira boma likuopyeza anthu kuti anthu asiye kunena boza kuchitisa anthu anzao mantha. Pano anthu ngati Manjolo ndi a T/A ndi osowa. Nchitidwe umenewu uthe mulungu achite nao opha anthu .
    Zikomo a Ntola nkhani Ambuye akutsogolereni mu nchito imenei. Mwapulumusa ena.

  • @dolikakamanga203
    @dolikakamanga203 Год назад

    Good job may God bless you guys

  • @marynkhata9707
    @marynkhata9707 Год назад +3

    Afumu anzelu mulungu akudalitseni

  • @lestermhone2710
    @lestermhone2710 6 месяцев назад

    Amfumu ndi Manjolo apanga zaumunthu. Boma liwathokoze basi

  • @ECKRADEMZATI
    @ECKRADEMZATI 6 дней назад

    So touching

  • @kingkayaye
    @kingkayaye Год назад

    on my way to Mr manjolo and Mr T/A they deserve it🏃🏃

  • @charlurquhart5788
    @charlurquhart5788 Год назад

    Mwana obweresa nxakeyu asatuluke cz anauyamba kale

  • @MacDonaldkachala-cm5gc
    @MacDonaldkachala-cm5gc 4 месяца назад

    Don't forget the big buyer also hails from the same.........'.............

  • @steven22issah97
    @steven22issah97 Год назад

    Just a few people can manage it. Well deserved Mr Manjolo and T/A Ngomano

  • @PaulThawale-cq7ev
    @PaulThawale-cq7ev 6 месяцев назад

    Malawi akufunika atsogoleri ngati awa agog Mulungu akudaliseni

  • @EdsonSichali
    @EdsonSichali Год назад

    Munthu amene anafika kwa munthu wachilungamo amene anauza aT/A ndiye amene wachilungamo zikomo

  • @IshuzymtumaHussein
    @IshuzymtumaHussein 4 месяца назад

    Mukuloleranji ambuye anthu oipa mtima awa azichita bwino dziko lolenga nokha

  • @ChimzyBinali
    @ChimzyBinali 4 месяца назад

    Ine ndimaona kuti boma litenge mbali ogula ndiogulitsa azirandira chirango chachikuru

  • @greychizaka4088
    @greychizaka4088 7 месяцев назад

    True hero

  • @lukainnocent5380
    @lukainnocent5380 Год назад +1

    Thyolo chilazulo maboma aukape kwambiri kamalawi watunthu alomwe zisiru zokonda kupha anthu moyo wawo ndi waku Mozambique basi

    • @belindansona5296
      @belindansona5296 Год назад +1

      Kuyankhula mopusa kwinako anthu saphana mxieeee

    • @SirpromiseMatabwa
      @SirpromiseMatabwa 3 месяца назад

      Mbola yanu malowesa ndale ndikusankhana mitundu eti anthu akuchikwawatu kuthyolo ndikubwalo

    • @Felixbanda-q6p
      @Felixbanda-q6p 20 дней назад

      mboliyanu amwene dikila timuchose chakwela matumbo

  • @SirpromiseMatabwa
    @SirpromiseMatabwa 3 месяца назад

    Well amfumu amchacha

  • @chifundositolo5387
    @chifundositolo5387 Год назад

    Bwana minjolo ulemu wanu ndipo mu kufunika kukhala wa police

  • @paulkaunda6780
    @paulkaunda6780 Год назад +4

    Dziwalo zimapita ku boma asaname

  • @Davison-jr6ev
    @Davison-jr6ev 8 месяцев назад

    Anthu oterewa akuyenera kukalowa mundane moyo wawo onse chifukwa ndizoipa kupha munthu osalakwa

  • @MadalitsoMada-g3l
    @MadalitsoMada-g3l 11 дней назад

    . iyi ndi program ya bwino.isathere pa njila.( Ndine chikumbutso Sande : ck/T/A NGABU ,GVH SANDE ll SAOPA.

  • @BeautyMtambo
    @BeautyMtambo 7 месяцев назад

    Ineyo ndikuyamika a T/A ndi A police amumudzi mulungu awa tsogolele

  • @promisemakawa1556
    @promisemakawa1556 Год назад

    T/A ndi mr manjolo muyenera kulandila award, boma liyenera kukuganizirani, tsoka boma lathuli ndilopondereza

    • @pauldaka7966
      @pauldaka7966 Год назад

      Tikuyeneradi kudziwa mmene chigemulo chakukhoti chinayendera abale inu

  • @usherkays4379
    @usherkays4379 Год назад

    Manjolo deserves a reward from the government

  • @PiliranTChimalizen
    @PiliranTChimalizen 6 месяцев назад

    Km a T/A awa ngofunika award

  • @BeautyMtambo
    @BeautyMtambo 7 месяцев назад

    Amalawi tiyeni tigwilane manja kupewa nkadza Kwa abale athu tiyeni tikondani wina ndinzache

  • @AndréSeveni
    @AndréSeveni Год назад

    Mwanayo mudamupeleka kwa makolo wake?

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 Год назад +1

    Ooooo my god 🤔🤔🤔🤔kama amalawi 🇲🇼 mmmmm

  • @WysonJekapu
    @WysonJekapu 7 месяцев назад

    Nyamatayu Boma limupase kagalimoto

  • @blessingsmasakala3285
    @blessingsmasakala3285 Год назад

    Moti zigawenga zija zikanatutumuka manjolo anali pamavuto agulupu aja akanamutembenukilanso kt iweyo mission ija wailepheresa pazifukwa zilibwino ubale wamanjolo ndi a T/A panopa kamba mission yatheka nduthu

  • @EliasMtize
    @EliasMtize 6 месяцев назад

    Manjolo wanena zoona kuti boma ndilo vuto lalikulu anthu ena atagwidwa koma pano anamasulidwa

  • @JosephEthan-l6u
    @JosephEthan-l6u 8 месяцев назад

    Trader manjolo

  • @carlossadimba595
    @carlossadimba595 7 месяцев назад

    Koma nanga mabwana omwe amagula Ku nchalo Ku chikwawao tiwadziwe nawo ife kwathu mkomweko

  • @bobsaidi7691
    @bobsaidi7691 Год назад +1

    A tiye Wawa ndi anzelu kwambili

  • @geee7672
    @geee7672 Год назад

    Mwana, wapezayi ndi scoop. Atolankhani akuluakulu amagulidwa ndi mapoliticians to avoid this. Break into this industry. This is nothing but tip of iceberg. Mpakana umupeza amene amagula ma albino. Ine ndimakaikila mzimai wakumwanza uja

  • @harrisonmwanga9812
    @harrisonmwanga9812 Год назад

    Zimenezo zinali nthawi ya kamuzu,yemwe anali ndi lamulo okupha wina naye aphedwetso.democracy yafika ndi zithu zoipa kwambili.

  • @kedibonesegametsi2493
    @kedibonesegametsi2493 6 месяцев назад

    Mmmmmmm My god 😢😢😢

  • @ShownyYohane
    @ShownyYohane 4 месяца назад

    Malamulo nkhumi amulungu;Usaphe ";

  • @sydneykumisuku1380
    @sydneykumisuku1380 Год назад

    Few good men!

  • @janetnpaul426
    @janetnpaul426 Год назад +2

    Chonena ndilibe 😭😭😭

  • @RodneyMwapasa
    @RodneyMwapasa 7 месяцев назад

    Akanachulukira anthu oterewa bwezi zili bwino amfumu

  • @SheriefSaloominBanda-sv5ie
    @SheriefSaloominBanda-sv5ie Год назад

    Manjolo ✨

  • @GeorgeMakhalira
    @GeorgeMakhalira День назад

    Zikomo amfumu chauta akudalitseni

  • @abdulkatopola3612
    @abdulkatopola3612 Год назад

    Iweyo ukungofunika ulandile award ndiwe wekha ungakwanise