Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI”

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 9 июл 2024

Комментарии • 81

  • @user-ix2ux5ss1b
    @user-ix2ux5ss1b 19 дней назад +5

    More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika

  • @EversDman
    @EversDman 18 дней назад

    Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯

  • @PeterKasiya
    @PeterKasiya 18 дней назад

    Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji 20 дней назад +1

    Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏

  • @LuyoloTlhapane
    @LuyoloTlhapane 13 дней назад

    A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila

  • @MomeryPhiri
    @MomeryPhiri 18 дней назад

    ❤❤❤❤❤❤❤ love it

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k 19 дней назад +1

    bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo

  • @user-xm5cq1fb8g
    @user-xm5cq1fb8g 18 дней назад

    Ulemu wanu big❤❤❤❤❤

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp 18 дней назад

    😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi

  • @neemahkapatamoyo9563
    @neemahkapatamoyo9563 19 дней назад

    Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @user-dj6rc3lc4t
    @user-dj6rc3lc4t 19 дней назад

    Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana

  • @FarookRaphael
    @FarookRaphael 19 дней назад

    More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem 19 дней назад

    Big up bro

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 19 дней назад

    Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂

  • @FlorryVugy
    @FlorryVugy 19 дней назад

    A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂

  • @UthmanKapungu
    @UthmanKapungu 19 дней назад

    Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife

  • @AffickChaona
    @AffickChaona 16 дней назад

    ❤❤❤❤❤

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j 19 дней назад

    Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima.
    Agalu a anthu ndithu

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w 20 дней назад +1

    Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 19 дней назад

    Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @NdawaPhillipfortunePhakatie
    @NdawaPhillipfortunePhakatie 19 дней назад

    Motor 💥 kalindoooo

  • @user-wm4rs4kd7d
    @user-wm4rs4kd7d 19 дней назад

  • @user-zt3gv7md6x
    @user-zt3gv7md6x 18 дней назад

    Zoona amwene

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 19 дней назад

    😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 19 дней назад

    Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂

  • @nicholasmutano6017
    @nicholasmutano6017 19 дней назад

    Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?

  • @PeterMaulana-qk5uq
    @PeterMaulana-qk5uq 19 дней назад

    Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!

  • @FwasanMwenefumbo-zq7sg
    @FwasanMwenefumbo-zq7sg 19 дней назад

    The DC 🔥

  • @BernadettaTengula
    @BernadettaTengula 19 дней назад

    Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂

  • @ericlarks8165
    @ericlarks8165 19 дней назад

    ,🔥🔥🔥🔥

  • @JoyceChitsulo-mw7wg
    @JoyceChitsulo-mw7wg 19 дней назад +1

    Makosana apa nde mwapita

  • @FrankMilias-og3js
    @FrankMilias-og3js 19 дней назад

    Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko

  • @user-hq8fw5hz2l
    @user-hq8fw5hz2l 19 дней назад

    Awa ndie mawu

  • @user-dm6xq6cp1m
    @user-dm6xq6cp1m 19 дней назад

    Ai zikomo 🥱

  • @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa
    @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa 19 дней назад

    Ambuye akudalitsen

  • @benjulius6070
    @benjulius6070 19 дней назад +2

    😂😂😂😂😂😂

  • @gerrardgladstone2473
    @gerrardgladstone2473 19 дней назад

    Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi 19 дней назад

    Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi

  • @ChisomoamitoniSauzandeamiton
    @ChisomoamitoniSauzandeamiton 19 дней назад

    bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu

  • @SmartMoles
    @SmartMoles 19 дней назад

    Zofunikila kulangura mwayangure kumene

  • @VincentMalika-w7x
    @VincentMalika-w7x 19 дней назад +1

    Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath

  • @directorkfuture118
    @directorkfuture118 19 дней назад

    Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂

  • @user-tw5iw7gf2v
    @user-tw5iw7gf2v 19 дней назад

    😂😂😂😂 mpaka muchenga license

  • @RamseyWasi
    @RamseyWasi 20 дней назад

    Blasa,
    Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC)
    My opinion:
    Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 19 дней назад

    Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 19 дней назад

    Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha

  • @user-kx4cj7iu9q
    @user-kx4cj7iu9q 19 дней назад

    Dc

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 19 дней назад

    Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk

  • @HendersonDziwa
    @HendersonDziwa 19 дней назад

    Dzelu zachepa kkkk

  • @DaudiAbdullah-o5l
    @DaudiAbdullah-o5l 19 дней назад

    Mumatiyimilila

  • @TshepoModise-xs4qu
    @TshepoModise-xs4qu 19 дней назад

    Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee

  • @maxwellcaptain3937
    @maxwellcaptain3937 19 дней назад

    Kalindo samaopa😂😂

  • @PeterGrant-ih1sr
    @PeterGrant-ih1sr 19 дней назад

    Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 19 дней назад

    😂😂😂😂😂 koma DC

  • @D.RJALLI-qo6yd
    @D.RJALLI-qo6yd 19 дней назад

    Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 19 дней назад

    Ati kutitola kapena chani

  • @JuliusMunthali-z7j
    @JuliusMunthali-z7j 19 дней назад

    Awuzeni

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward 19 дней назад

    Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto

  • @user-ls5zj8qn6k
    @user-ls5zj8qn6k 19 дней назад

    Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo

  • @AnthoniohMazengera
    @AnthoniohMazengera 18 дней назад

    Hahahahahahahahahaha😂😂😂

  • @Aluwenkareem-ev3ro
    @Aluwenkareem-ev3ro 19 дней назад

    😂🤣😂🤣

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko4534 19 дней назад

    😂😂 kung'alulatu

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 16 дней назад

    😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp

  • @GiftKulture
    @GiftKulture 19 дней назад

    🤣🤣🤣🤣 mipunga

  • @AaronLitete
    @AaronLitete 19 дней назад

    Kkkkk boma lopusa

  • @YonaMartin-kb3do
    @YonaMartin-kb3do 19 дней назад

    😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe

  • @user-yl3lg5fk8f
    @user-yl3lg5fk8f 19 дней назад

    Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-2001 19 дней назад

    Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo

  • @ikmusic-s9f
    @ikmusic-s9f 19 дней назад

    koma nde eeee mpaka licence mchenga

  • @YohaneMbewe-u4k
    @YohaneMbewe-u4k 19 дней назад

    😂😂😂😂

  • @user-ky8us1ff5b
    @user-ky8us1ff5b 19 дней назад

    😅😅😅😅

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya8577 19 дней назад

    Bigiliman naweni

  • @user-vn1wq6wg6i
    @user-vn1wq6wg6i 19 дней назад

    K.K😂

  • @PhillipMtonga-g7o
    @PhillipMtonga-g7o 19 дней назад

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance

  • @BenjaminKayembe-j7j
    @BenjaminKayembe-j7j 19 дней назад +1

    km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km

  • @Kachelephiri
    @Kachelephiri 19 дней назад

    Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam 19 дней назад

      Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam 19 дней назад

      Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe

  • @user-wz6jy3re8n
    @user-wz6jy3re8n 19 дней назад +1

    😂😂😂😂😂😂

  • @myheartforkids2876
    @myheartforkids2876 20 дней назад

    😂😂😂😂😂