Kamlepo Kalua wayankhura mosaopa ndipo iye Wati wamvaso kuti they’re planning to kill his son

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 19 окт 2024

Комментарии • 164

  • @AlbertEngelbercht
    @AlbertEngelbercht 3 месяца назад +28

    Mwachitamakola kuwaphalila unenesyo, chiuta wamusungeni dada kamulepo,we are In democracy time!!!!.

    • @GoodlechaManda
      @GoodlechaManda 3 месяца назад +1

      Makolawaka 😊kwalinamwe manda
      6 jjjjjoo9ooj .0pll0
      V

  • @petermanMitambo
    @petermanMitambo 3 месяца назад +11

    Very powerful speech.long live Mr KALUA. may God protect you from these heartless swines

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem 3 месяца назад +10

    Good massage Mr u are the strongest man

  • @georgemsowoya6525
    @georgemsowoya6525 3 месяца назад +4

    Mcp pamoz ndi achakwera achepa there days are numbered....live long dad kaluwa and much love to fredo kiss ,,, I speak divinely protection in that family ,God be with you

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge 3 месяца назад +2

    Powerful massage bwana Mr KALUA ❤🎉🎉🎉

  • @AustinMhone-r3s
    @AustinMhone-r3s 3 месяца назад +3

    Mr kamlepo kaluwa one of the greatest politician in Malawi u fought for democracy MCP is getting us backwards to dictatorship arresting and killing innocent people this is not what the voters wanted.

  • @FrancisMbewe-xn2pl
    @FrancisMbewe-xn2pl 2 месяца назад

    Powerful Papa ❤ palibe wamuyaya tonse tizafa bas

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 месяца назад +8

    I support kamlepo munthu wa mkulu kwambiri mumakwanila.

  • @CliftonMaseya
    @CliftonMaseya 3 месяца назад +9

    Mvamvekatu ma words umu 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @PrinceernestBorniface-x1m
    @PrinceernestBorniface-x1m 3 месяца назад +6

    Apolisiwo ndi chakwela onse machende awo fotsek...

  • @normantondole2669
    @normantondole2669 3 месяца назад +4

    Why not taking them (police) to court Mr Kalua?

  • @brightsonsaidi
    @brightsonsaidi 3 месяца назад +2

    Pls bring out the CCTV footage here, ASAP. It will have a heavy impact on people's minds

  • @unitelectronicmedia4581
    @unitelectronicmedia4581 3 месяца назад +3

    This man is loaded!
    Wati ndigenda waponda MWALA

  • @JailosGazahBoica
    @JailosGazahBoica 3 месяца назад +4

    My Land 😢😢😢our warm heart of Africa 😢😢😢😢our peace,joy and harmony county has turned into Sodom and Gomorrah 😢😢😢😢

  • @shaffiejumah6385
    @shaffiejumah6385 3 месяца назад

    We respect you mr kalua we leant alot and we still learning much love...

  • @MikeMerecah
    @MikeMerecah 3 месяца назад +2

    Konwani kamponje ndiwe opusa kwabasi ukuona ngati kamlepo kalua ndi size yako, Bwana my God protect your family,,,,,,,,

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 3 месяца назад +1

    God is great be safe and your family Mr kamulepo

  • @tamandaninampinga
    @tamandaninampinga 3 месяца назад +1

    Thanks dada for the message

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 3 месяца назад +1

    Ayiwala zoti achoka pampando, shame on you. May God be with you Kamlepo

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 3 месяца назад +2

    🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏
    Father kamulepo kaluwa tili pambuyo panu

  • @MadalitsoMalamba
    @MadalitsoMalamba 3 месяца назад +6

    MCP makolo amkatiuza kuti ndi chipani chakupha ndiye tikutha kuonadi and I don't think wachinyamata ozindikira bwino mkumakaponyera vote MCP....

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw 3 месяца назад +2

    Good massage kalua

  • @StevenTembo-mb7rm
    @StevenTembo-mb7rm 3 месяца назад +2

    Well said I hope pala ni wanthu wa umunthu wawo wapulika and if they may attempt to kill Fredo this country will go beyond what happened in Kenya. We are ready

  • @alicegama8138
    @alicegama8138 3 месяца назад +2

    Apo ndipo wamanya kuti watumbuka wokhumba yay kuwaseweleska

  • @MichaelKwZgambo
    @MichaelKwZgambo 3 месяца назад +2

    What a powerful message

  • @ZikaniJere
    @ZikaniJere 3 месяца назад +1

    I love the the guy

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga 3 месяца назад +9

    WE LOVE U KAMLEPO...MCP YIKUTULUKA M'BOMA CHAKA CHA MAWA...

  • @PrinceThom-pe6ie
    @PrinceThom-pe6ie 3 месяца назад +2

    Don't worry dad 2025 mcp police tizayikhaulisa

  • @WillamChihana
    @WillamChihana 3 месяца назад +2

    Mwayowoya bwana ndipo nakondwa nazo fundo zino zose chiuta wakuona vose

  • @FrancisMbewe-xn2pl
    @FrancisMbewe-xn2pl 2 месяца назад

    We fear God not person 💪🔥

  • @JuliusChamwanje
    @JuliusChamwanje 3 месяца назад +3

    History we learn alot

  • @PrinceernestBorniface-x1m
    @PrinceernestBorniface-x1m 3 месяца назад +2

    This is very stupid insane 😠... Chakwela should resign galu wachabechabe

  • @ElemiahKavute
    @ElemiahKavute 3 месяца назад +1

    Mupheni kkkkkkk andale amwene 🤣🤣🤣🙌 atitu enawo anyumwe kkkk muphenitu akamlepo akusendeno muone

  • @DerickZiba
    @DerickZiba 2 месяца назад

    Yebo mwawanthu, don't touch Tumbuka people, we believe in Jesus

  • @JailosGazahBoica
    @JailosGazahBoica 3 месяца назад

    May God protect you and your family

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj 3 месяца назад +3

    Ndikukaika ngt anthu afike nthaw yovota bwinobwino ..zikundionekela ngat mavote azizizi akhoza kuchitika mu Mziko muno...

  • @HendrixGrem
    @HendrixGrem 3 месяца назад

    Wise speech Honourable

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 3 месяца назад

    Mmmm nde afika posausano... Kupha bas!!!!! Eeee why Malawi now

  • @zayedmitawa8345
    @zayedmitawa8345 3 месяца назад

    Andale amafuna kukhala pa mpando forever yet amapanga zoononga mu nthawi yochepa
    I don't understand then at all.
    Being good will not make you lose anything at all but being bad eeeh ndi izi za cheucheuzi

  • @lumbaninyirenda8223
    @lumbaninyirenda8223 3 месяца назад +2

    kumpoto MCP kulibe vote

  • @Amunandife3212
    @Amunandife3212 3 месяца назад

    Ing'aluleni bwana Kaluwa,,,,,,,,,,,,

  • @VincentTembenu-ip5ii
    @VincentTembenu-ip5ii 3 месяца назад +1

    Mmm mpaka I know akumidima omwe mumadalila 2025 Kuli ntchito

  • @AbdulSelemen-q5j
    @AbdulSelemen-q5j 2 месяца назад

    Osaopa osaopa palibe wambewu padziko pano, ndipo kalikonso kazalawa imfa.

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 3 месяца назад

    We love you Kamulepo Kaluwa

  • @kidneyblessingschilinguloj7292
    @kidneyblessingschilinguloj7292 3 месяца назад

    Rise up Kamlepo we want peace

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 3 месяца назад

    Kuyankhula kwabwino uku, nawo apolice alibe nzeru angowagwiritsa ntchito malipiro ochepa km kumangozunza anthu

  • @MusaMajudu
    @MusaMajudu 3 месяца назад +4

    Message ya mphamvu ❤

  • @zaitwazaitwa941
    @zaitwazaitwa941 3 месяца назад +1

    Koma ndiye Kwachema

  • @JaphetChimphepo
    @JaphetChimphepo 3 месяца назад +1

    😂 koma kwachema osapanga mantha aonese

  • @MussahWilliam-py1ff
    @MussahWilliam-py1ff 3 месяца назад

    Koma ndalama mani mmmmmh ay ndinthu mmmh anthuwa guyz samagona muja tigonera enafe

  • @johnmponda9070
    @johnmponda9070 3 месяца назад +1

    Oh my God Malawi police and Malawi defence force are just used they don't even know what they responsibility is really shame on them

  • @TryMoo-c1e
    @TryMoo-c1e 3 месяца назад +1

    *Amtumile mwenye* kwabasi nambo ngadandaula Mcp chipani changalumbana Ata panondi.

  • @OwenMajoni-qv3eg
    @OwenMajoni-qv3eg 3 месяца назад

    Osapita ku khothi bwanji a Kalua? Komanso ndalama zanga simunabwenze kuchoka 2019 paka lero mumaganiza bwanji bwana Kalua? Koma umunthu mulinawo?

  • @natashamathala8715
    @natashamathala8715 3 месяца назад +6

    Koma nde mwangoti 3stars apa pali nkhani apa tiuzeni zambili bwanaaa

  • @KateRose-sh8zl
    @KateRose-sh8zl 3 месяца назад +1

    Pathu sipadziko zoona but the voters are suffering bwana

  • @MirajLaja
    @MirajLaja 3 месяца назад

    Za phone iwalani asiyileni ikhale yawoo...

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 3 месяца назад

    Kamulepo kaluwa mumatiyomilira munatsala nokha (RIP chakufwa chihana)

  • @glynbulambo
    @glynbulambo 3 месяца назад +1

    Mwana wamupoka wayoghoya wa chewa mfela za Eni 😅

  • @SydneyChiphaka
    @SydneyChiphaka 3 месяца назад

    Why Mr Kamulepo want to kill his own son? Sad

  • @emanuelnziza1193
    @emanuelnziza1193 3 месяца назад

    Awawa ngat ali mau awodi. Aah the Man must be suspected sure

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 3 месяца назад

    Achilundi samalani, msaone ngati mwafika. Lindani madzi achilundi apite nde mziti mwadala, nzosiilanatu izi osasimbwa.

  • @IsaacTsinde
    @IsaacTsinde 3 месяца назад

    Mwayankhula abwana

  • @RABSONChisambi
    @RABSONChisambi 3 месяца назад

    30:24 my God protect you kamulepo and your family ilike what you saying

  • @JaxyKumwenda
    @JaxyKumwenda 3 месяца назад

    Munthu wamkulu wayankhura❤

  • @chifundochimenya6368
    @chifundochimenya6368 3 месяца назад

    😢 indeed this world it's not our home am crying Malawi

  • @wonganikaunda
    @wonganikaunda 3 месяца назад +2

    Mukapha uyu nde muyalukatu poyerayera

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim 3 месяца назад +6

    Chitukuko chA razalo ndikupha basi

    • @clesheinvestments
      @clesheinvestments 3 месяца назад

      Ngati muja Chinalilinso Chitukuko Cha Peter Mutharika pakupha Issah Twaib Njaujyu, Buleya, Masambuka, Tambala Family kutchulapo chabe ochepa

    • @isaacpelani
      @isaacpelani 3 месяца назад

      ​@@clesheinvestmentsmuli m'bomatu. Tengerani umboniwu kukhoti tidziwe zoona zenizeni. Mwina munkapha ndinu kuti muipise mbiri yaamnzanu

    • @LukaThawe
      @LukaThawe 3 месяца назад

      Yah ndimakape

  • @KhumboZimba-x1z
    @KhumboZimba-x1z 3 месяца назад

    Mawu amphamvu kwambiri chakwerayo ngati kulikumva wamva dziko ndilizungulira

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 3 месяца назад +1

    Tavuka na mcp onse wa mcp mavi yao (komaso inu akamulepo mukufoila kwambili mr kalua u sleep too much

  • @FiskaniTonymahone-vl3og
    @FiskaniTonymahone-vl3og 3 месяца назад

    Chakwera, don't know,do good, be good, live good, he's no good..

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 3 месяца назад

    Koma z..ikoli ...Amwene

  • @HarrietMtenje
    @HarrietMtenje 3 месяца назад

    Koma ndiye ndinthawiso yakamuzutu aaa

  • @BrightNkhoma-xz4bg
    @BrightNkhoma-xz4bg 3 месяца назад

    With heavy heart

  • @kondwanimandala4575
    @kondwanimandala4575 3 месяца назад

    Mawu a mphavu ,ana achepa

  • @edakweni
    @edakweni 3 месяца назад

    Voice sinali yanu kkkkkk. Apaso mukanaso kuti siyanu

  • @ednakaluwa5414
    @ednakaluwa5414 3 месяца назад

    Hon kaluwa🔥🔥🔥🔥

  • @BenjaminMoffat
    @BenjaminMoffat 3 месяца назад

    big boy ting set

  • @UbreyNicks
    @UbreyNicks 3 месяца назад

    Mwamuyambapo kaluwa amayabwatu chwe mwana chwe

  • @HawaiijeminieHawaii
    @HawaiijeminieHawaii 3 месяца назад

    Fact

  • @MrMagombo
    @MrMagombo 3 месяца назад

    Akapha mwana inunso tiyeni tikaphe awo.
    Ofunika kuyamba kubwenzera. Zatopetsa.
    Athuwa akufuta chifukwa amalawi sabwenzera.

  • @VincentSamson-q2j
    @VincentSamson-q2j 3 месяца назад

    Powerful

  • @MacdonaldMisomali-lt4wu
    @MacdonaldMisomali-lt4wu 3 месяца назад

    Aphe fredo awone

  • @AustinBornface
    @AustinBornface 3 месяца назад +3

    Tili mukati mweni mweni

  • @prettytambala5687
    @prettytambala5687 3 месяца назад

    Muzazisumire zimbava izi zidzakulipireni hiyaaaaa

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb 3 месяца назад +1

    Afa okha

  • @GibsonLackson
    @GibsonLackson 3 месяца назад

    Ayelekeze 😳😳😳😳

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 3 месяца назад +2

    Good Messnge Mr Kamulepo kaluwa ❤ Chakwela you mast go watikwana

  • @JoyMpinga
    @JoyMpinga 3 месяца назад

    Ntchana asamuyese ghetto azaimva

  • @MagretMvula
    @MagretMvula 3 месяца назад +1

    Dadi apa mwafikapo muuzeni zoonaasiye chibwanamooto uyake asazolowele

  • @ellenchipula9809
    @ellenchipula9809 3 месяца назад

    Chakwera pa m’tongo pa mako

  • @kelvinedson685
    @kelvinedson685 3 месяца назад

    That's fact's indeed

  • @TadalaMaumbo
    @TadalaMaumbo 3 месяца назад

    I support you

  • @giftwisdom-km7yh
    @giftwisdom-km7yh 3 месяца назад

    Mwachita makola mwawa phalila unenesho.
    Chiuta wakudangirileni.

  • @ShakiraOsman-e8g
    @ShakiraOsman-e8g 2 месяца назад

    Komanso katundu anaonongayo abweze

  • @Amunandife3212
    @Amunandife3212 3 месяца назад

    Leader

  • @zwdydigonia8730
    @zwdydigonia8730 3 месяца назад

    Ng'aluuulaaaa iwe

  • @MassaukoKintu-k7s
    @MassaukoKintu-k7s 3 месяца назад

    Following

  • @MosesShaba
    @MosesShaba 3 месяца назад

  • @ajasikalonga3210
    @ajasikalonga3210 3 месяца назад

    Auze ngati ali ndi mzerunso

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np 3 месяца назад +1

    Ndipo ndizoonadi zamawa siziziwika