hot Current..Kumkuyu Vs Namalomba

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 22 июл 2023

Комментарии • 220

  • @shakajudahTV
    @shakajudahTV 11 месяцев назад +6

    Kunkuyu is just talking nonsense he don't know how anger is in Malawians 😢😢😢😢

  • @georgesmart3791
    @georgesmart3791 11 месяцев назад +9

    More fire Nambalomba 🔥 🔥

  • @mkhulukinyata5198
    @mkhulukinyata5198 11 месяцев назад +2

    This is the best n' honest ever Hot Current ...Anthu adzikumadi mbali dzonse monga momwe mwapangira apamu. Apa mpomweno tikutha kudziwa kuti " Atambwali ndi atiwo kkkkk

  • @dicksonilimbani3443
    @dicksonilimbani3443 11 месяцев назад +9

    🤣🤣🤣Kukuyu ukuwona ngati malawi ndi wa Abambo oka achakwera et

  • @ismailkhuneya3346
    @ismailkhuneya3346 11 месяцев назад +7

    Kkkk kmabe ngakhale dpp imapeleka ma figure olakwika ku imf kmabe dziko limayenda bwino kusiyana ndipano

    • @samsonmtumbati4855
      @samsonmtumbati4855 11 месяцев назад +1

      Yeah zoona boma lomwe lilipanopa likuphweteka kwambiri ndibola dpp

  • @user-og4oe5yp4w
    @user-og4oe5yp4w 11 месяцев назад +3

    🔥🔥🔥🔥🔥 namalomba on 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @alinafeanderson3065
    @alinafeanderson3065 11 месяцев назад +2

    Wonder ur best ❤

  • @user-og4oe5yp4w
    @user-og4oe5yp4w 11 месяцев назад +1

    Kkkkkkkk ndevu zamwayi 😂😂😂😂😂 apa ndiye mwaitha sindinayambe kunvera koma ndimmene ayambira akunkuyu aaaaaa

  • @collinsmbewe3109
    @collinsmbewe3109 11 месяцев назад +1

    If they are failing to buy a packet of sugar why? Is not because of expensive

  • @ThoccoBondo-mx7vt
    @ThoccoBondo-mx7vt 11 месяцев назад +2

    Kkkkkkkk koma mkukuyu zoti azabwelaponso apa ndakaika😄😄😄😄

  • @lewisbonongwe8518
    @lewisbonongwe8518 11 месяцев назад +2

    Namalomba ndiwe galu kwabasi wandisangalatsa kwambiri uli ndi nfundo komaso phuma 😂😂😂😂 wakwana iweyo Namalomba Umatiyimilira tonse amalawi a DPP

  • @Andrew-nz9sh
    @Andrew-nz9sh 11 месяцев назад +5

    ingoswananipo zithepo💪💪

  • @user-fp2qj6vm4d
    @user-fp2qj6vm4d 11 месяцев назад +2

    Ndevu za mwayi ndiwe wa mcp bola Brian ndi fire

  • @user-mx5zy7ci3y
    @user-mx5zy7ci3y 5 месяцев назад +1

    A Shadreck namalomba kuwonesa kuchenjera satana akukugwitsani nchito koma one day is day muzakolora

    • @ShabaniKuswere-cp7ss
      @ShabaniKuswere-cp7ss 4 месяца назад

      Mmafuna munene kuti a Kumkuyu kapena aNamalomba? Chifukwa ine mkuona kwanga ndikuona kuti amene akuoneka kuchenjera kulankhula apa ndi akumkuyu chifukwa akuzembazemba pamene chilungamo akuchidziwa

  • @robertrichman9376
    @robertrichman9376 11 месяцев назад +3

    Never trust any Politician

  • @dominicmphepo-jk8lk
    @dominicmphepo-jk8lk 11 месяцев назад

    For the first time I have to comment on this, from look of things onsewa ndi anthu oti palibe chomwe angapange kuti athandize dziko lino.
    Panopa from what I have Said palibe Ali ndi masomphenya ofuna kukonza dziko koma kutukula matumba awo.
    Sindikuwonapo munthu apa. Continue kutibela basi nthawi yanu. Inu a tonse alliance ibani monga momwe anzanuwo anabela zikuwawa nanuso a DPP mukalowa ibani basi osamangana

  • @Marialongwe-nzlib
    @Marialongwe-nzlib 11 месяцев назад +2

    Mungoona Mbava Mmene ikusekera Kusekelera 😂😂😂😂

  • @vincentkamangamr9062
    @vincentkamangamr9062 11 месяцев назад

    Mr Wonder muziwapasa mpata olongosola kuti amalize osamangowadula pliz

  • @FefieTenisha-du7ge
    @FefieTenisha-du7ge 7 месяцев назад

    The main problem that these leaders have is they politicize everything...Instead of coming up with workable technical solutions they are just busy backing up their parties....This is sickening!
    It appears Malawians are not just poor economically but they are also poor mentally..
    These leaders are not on their seats to fix Malawians problem but to fix their personal and party problems...

  • @WakuMalawi
    @WakuMalawi 11 месяцев назад +1

    These men are well aware of the real reason our Country is poor. We're not utilizing Malawians. We're too busy acting like servants. Where's a real Gov't with chidwi and commitment to improve us? Our Politicians are embarrassing.

  • @stanleyfraction539
    @stanleyfraction539 11 месяцев назад

    This was hot🔥🔥🔥🔥🔥

  • @lewisbonongwe8518
    @lewisbonongwe8518 11 месяцев назад +2

    Akunkuyu ndalama zikubedwa muulamuliro wa MCP komaso njala yaphwi anthua kufa ndi njala

  • @collinsmbewe3109
    @collinsmbewe3109 11 месяцев назад +1

    This government is a headless government

  • @user-ed1rr2pw2t
    @user-ed1rr2pw2t 11 месяцев назад +1

    Mr wonder mukuyener mukapeleka funso muziwapatsa mpata kuti afotokoze cfkw zikuonets ngat mukufusa funso pamene yankho mulinalo kale

  • @ChisomoMsiska-oi2vg
    @ChisomoMsiska-oi2vg 11 месяцев назад +2

    Boma limene lasokoneza zinthu kwambiri ndilomweri la mcp

  • @fatimautilah5648
    @fatimautilah5648 Месяц назад

    Both parties palibe chomwe amayakhula zogwiea mtima,mitima mwawo mwangozaza mikwiyo

  • @GloryKhondiwa
    @GloryKhondiwa 27 дней назад

    Politicians😂 this is just a game 🎯🎮

  • @pauldaka7966
    @pauldaka7966 11 месяцев назад

    Komatu eeeeee! Amalawi timadziwa kudzibakira

  • @ganetkanzeru5153
    @ganetkanzeru5153 11 месяцев назад

    Hot current yalero ndiye yandiwaza nyatwa kkkk

  • @johnman4619
    @johnman4619 6 месяцев назад

    Anthu amenyanatu awa ndikuona ngati aDpp zinawawa kwambiri samafuna kuchoka

  • @piliranimphepo1920
    @piliranimphepo1920 11 месяцев назад

    I think there is no need to b inviting these failed politicians... palibe chanzeru angatiuze adzingolozana chala basi.. continue your program mmene mumapangira kale

  • @victorbanda9039
    @victorbanda9039 11 месяцев назад +1

    Namalomba ndimwana pandale Ndipo muli makani opanda ntchito atakhala m'boma anthu awa sangamatsutsike

  • @frstyhavoc6678
    @frstyhavoc6678 11 месяцев назад +1

    Koma ilyi ndi hot current for sure 😀😀😀😀

  • @thomasgamah764
    @thomasgamah764 11 месяцев назад

    Program iyi ndiyandale amalawi muzisamala pomaoonera manyaka awa, this is another part of compaigning

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw 11 месяцев назад

    kkkkkk Osokonedza abwera

  • @ThomasChiwaya-qx9mf
    @ThomasChiwaya-qx9mf Месяц назад

    Kod akukuyu kod wasowetsa sugar ndan mesa Inu atonse ( a mec akazangotulutsa kut mwawinaso muzaiputa khondo cuz mukuziwaso kut 3coters simukufunidwa dziko lino )

  • @louisgolden
    @louisgolden 11 месяцев назад +1

    Kunkuyu siukuyankha mafuso Ungokamba mbalume zopusa

  • @JohnNsona
    @JohnNsona 11 месяцев назад

    anuwake a program safunsa manfunso mwa intelegent amafunsa mwa ubulutu kapena mwa usavage Kodi mumapitadi Ku school kukaphunzira zapa wailes funsani munthu mpatseni mpata ayankhe

  • @AbleGondwe
    @AbleGondwe 14 дней назад

    Wonder musiye kunkuyu alankhule

  • @victormmbewe961
    @victormmbewe961 11 месяцев назад

    You must agree that the past affects the present.

  • @ShabaniKuswere-cp7ss
    @ShabaniKuswere-cp7ss 4 месяца назад

    Ntchito ikumuvuta uyu amene akuyendetsa program_yi kodi Brian Banda analikuti nthawi yomwe amamusiira mzake wa mcp_yu kuti apange Host program yofunika ngati imeneyi???

  • @user-xs3pk1vp8i
    @user-xs3pk1vp8i 4 месяца назад

    DPP inakanika kale now we are looking forward namalomba wawononga chipani Cha ambuye ake

  • @user-he6zq5iu5r
    @user-he6zq5iu5r 20 дней назад

    Kkkkkk Koma wonder wandiseketsa 😂😂😂😂😂

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 11 месяцев назад

    Koma mmene likuzunzira dziko ili,anthu tikuvutika day in day out mkumati tikulonza mavuto amene anzathu anasiya three years down the line,like really Mulungu akuyendereni mwapadera sure😢😢

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 11 месяцев назад +2

    Wonder usamabwere utakhuta cyclone mbatata wamva, ukumagunda posagunda bwanji😂😂

    • @dyba-x9w
      @dyba-x9w 11 месяцев назад

      akuonesa mbali

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 11 месяцев назад

      @@dyba-x9w
      Ayi sanaonetse mbali koma inuyo muli ndi nkhawa ndi mbali yanu.

  • @user-rd4lf2gg7g
    @user-rd4lf2gg7g 11 месяцев назад +4

    DPP ibwelele plz cement 20,000😮

    • @eliffagondewe8214
      @eliffagondewe8214 11 месяцев назад

      Ndipo mavuto alipo nde mkuka voter so imbwaa zimenezo ayi zikomo mcp🙌🙌🙌

  • @collinsmbewe3109
    @collinsmbewe3109 11 месяцев назад +1

    Kunkuyu amalawi tikufuna moyo wabwino osati zomwe ukulankhulazo

  • @molicieeosama8877
    @molicieeosama8877 11 месяцев назад

    Izi zikadalongosoka chikhala Kuti khaniyi ikukambidwa mwadongosolo. Koma Vuto Lake zikukhala Ngati Wanda wabwela Atalawa.

  • @dinganinedsontchongwe610
    @dinganinedsontchongwe610 6 месяцев назад

    sindikufuna kutaya nthawi yanga ndikumvetsera uyo wa mcp uyo palibe chimene anganene manyazi alibe galu waanthu

  • @ackimmunthali7886
    @ackimmunthali7886 11 месяцев назад

    Those suits are our money

  • @dyba-x9w
    @dyba-x9w 11 месяцев назад

    ineyo ndikuona molakwika kwambiri ndikukumbukira mau omwe bon kalindo anayankhula week yatha kuti times ikubakira kwambiri tonse adminstreation, ndikanakonda a Wonder wo akufusa mafuso awo ndi a indipendent balancing sikutheka . akhale neutralas ngati mtolankhani

  • @phanuelgryn858
    @phanuelgryn858 2 месяца назад

    mr msisya improve your questioning skills when you have big dogs

  • @EmercianahKasiku-en6hl
    @EmercianahKasiku-en6hl 11 месяцев назад

    Namalomba uli ndi nzeru koma wamushayinitsa Kinkuyu chifukwa uli ndi phuma next time uxizaupeza komaso kukhalitsa ndi APM sungakhale ndi nzeru bcz ija ndo mbatata ya mtsogoleri yomwe inkangona pa chiongolere,mwachidule nonse mbava zobera a malawi

  • @kho7676
    @kho7676 11 месяцев назад +2

    Koma akukuyu amatha osutsa satinthandiza

  • @ThoccoBondo-mx7vt
    @ThoccoBondo-mx7vt 11 месяцев назад +1

    Big up Namalomba

  • @user-gu5fy3tg2u
    @user-gu5fy3tg2u 4 месяца назад

    Kumkuyu galu mutu oumawo

  • @MikeMerecah
    @MikeMerecah 2 месяца назад

    Kuchenjera kwatha mcp anthu oipa,

  • @user-hp7xe2nu6w
    @user-hp7xe2nu6w 11 месяцев назад

    Kukela kwazinthu kukhala ngati munabadwa kwachinyama agalu achakwera ndi adzanuwo ndiposo kumkuyu ndiwe kape

  • @hopeskafumbiphiri6011
    @hopeskafumbiphiri6011 11 месяцев назад

    DPP imakwana kkkkkkkkk keep it up.

  • @harrisonnavayah6480
    @harrisonnavayah6480 11 месяцев назад

    Wander ndiwe Garu

  • @EfeloYovita
    @EfeloYovita 11 дней назад

    munalakwa pochotsa dpp chomwe mwachita inu a mcp ndichani dpp imagulitsa feterizer 50 kg inu a mcp k90,000 anthu akumudzi angakwanitse kugula feterizer? mwaononga dziko a mcp anthu akuba okupha

  • @serakillo8668
    @serakillo8668 11 месяцев назад

    Athu ...onsewa palimbe chomwe akuyankhula zomve saname angopanga ngti akupanga nthano awa a mcp nawo athu olephera ...padzaka zitatu apanga chani bolako Dpp ndithu tinkhodza kulodza zomwe apanga azaowo ❤❤❤ Dpp awo ziphuphu kuba kwambiri mcp

  • @Theheritage86
    @Theheritage86 11 месяцев назад +1

    Brian alikut

  • @nelsonkanjira2400
    @nelsonkanjira2400 11 месяцев назад

    Zitsiru Za anthu iziii muwatenga amalawi Ngati a kapolo

  • @ronaldsinjeni7823
    @ronaldsinjeni7823 11 месяцев назад +1

    Masanje okhaokha

  • @petersoko4283
    @petersoko4283 4 месяца назад

    Namalonda sanakhakepo mbom

  • @user-hp7xe2nu6w
    @user-hp7xe2nu6w 11 месяцев назад

    Koditu wakuba amayankha mwazelu cholinga awapusise amalawi pano nde tazukatu siife akale aja ayi

  • @user-yp3um6mf8d
    @user-yp3um6mf8d 11 месяцев назад

    I think Kunkuyu is clever enough however he doesn't have enough data to tell the nation how and what to do to improve our economy.He is a good politian to protect his superiors.If he can be honest he will admit the failures in the regime.Please accept you have failed guys.

  • @thomchinjoka177
    @thomchinjoka177 11 месяцев назад

    Nkukuyu or utakokera motani ,zakubvutani basi , palibe mukuchita ,komaso a wonder ndinu a MCP

  • @JOHNMARK-sl5ff
    @JOHNMARK-sl5ff 11 месяцев назад

    Malawi feeling pains😢

  • @millionsenenje5010
    @millionsenenje5010 11 месяцев назад +1

    Kumkuyuyu mkatundu

  • @stubish0p-fl2zf
    @stubish0p-fl2zf 11 месяцев назад

    Ndikanakonda kuti msogolomo osamatenga andale kumapezeka pamenepo chifukwa wandale ndipovuta kuti azavomereze zolakwika zake, ndiye ife okonda dziko lathuli amatipwetekesa mitu.

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 11 месяцев назад +14

    Namalomba is well matured and he knows how to answer the questions, Big up Sir.

  • @meditationmusic293
    @meditationmusic293 11 месяцев назад

    A wonder ndachitsiru so buanj

  • @simonpaul6567
    @simonpaul6567 11 месяцев назад

    This hot current for today there is nothing you 2 you answer Mr Namalomba and Kumkuyu

  • @alihibrahim
    @alihibrahim 11 месяцев назад

    Palibe gvn imene idzabwele ndi chilungamo ku Malawi mbanva zonse

  • @TrysonChimenya4-fm8nt
    @TrysonChimenya4-fm8nt 11 месяцев назад

    Namalomba ndiye dolo Akunkuyu sakundifikapo anta naye Wonder akuonena kuti sympathizer wa MCP

  • @shupikayintuwaluwa-5899
    @shupikayintuwaluwa-5899 11 месяцев назад

    Political z a deaty game a can agree na

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 11 месяцев назад

    Kom Nyasa tim imakwanad
    Kuposa Akt kul zodiac
    Mpak mwakumanizad
    Ulendo win mudzamuitan chilim ndi Atuper
    Komanso chakwer ndi pit

  • @user-ki3zi9qj3i
    @user-ki3zi9qj3i 11 месяцев назад

    I have personally liked this approach. These people must be accountable for whatever they are doing.

  • @adamkudzala186
    @adamkudzala186 11 месяцев назад +1

    Kumkuyu ntchito yamukulira

  • @donnexmgabe4355
    @donnexmgabe4355 11 месяцев назад

    Mungakweze bwanji lulimi pomwe feteliza ndalama mumapeleka kuma butchala ndi kuma Pharmacy anthu alimila chani mwalephela basi tatopa

  • @andrewngowe8836
    @andrewngowe8836 11 месяцев назад

    Mbuzi za anthu Malawi tili pa moto dziko loti lingathe kusitha mosavuta koma dyera mbuzi za anthu izi shupiti

  • @kennedychinguwo1640
    @kennedychinguwo1640 Месяц назад +1

    I think Wonder Msiska u are the one who is bringing chaos in this interview-U are very unprofessional

  • @MotivatedI
    @MotivatedI 11 месяцев назад

    Ma trillion being mentioned like it’s nothing.

  • @user-ne7rn4ki3c
    @user-ne7rn4ki3c 11 месяцев назад

    Kalonga Shawa uiwale za 2025 ndipo muyembekezele kumangidwa

  • @user-xi2ue2yq7b
    @user-xi2ue2yq7b 11 месяцев назад

    Kunkuyu nchitsiru, chidzete, munthu opepera, nyapapi weniweni.

  • @kennethmakweya3561
    @kennethmakweya3561 11 месяцев назад

    Namalomba amakhala nditimajoker, atha kupweteka gulu

  • @enockjailos6233
    @enockjailos6233 11 месяцев назад

    This one the dog of the dogst🇲🇼👁

  • @StevekantickKantick
    @StevekantickKantick 11 месяцев назад

    Kodi Mesa amatcalenger kt after 2years akhala atapanga client kukanika apamga lisine pano tree years apamga apamga chani mbava

  • @sjrecordschannel7687
    @sjrecordschannel7687 11 месяцев назад

    Mbuzi zokhazokha zinakumana

  • @harrisonnavayah6480
    @harrisonnavayah6480 11 месяцев назад

    Trillion kuitchula nganti pin

  • @CRMTV-pw9jt
    @CRMTV-pw9jt 2 месяца назад

    Mcp inatengadi mbuli

  • @thelondonbridge6605
    @thelondonbridge6605 11 месяцев назад +2

    Wanda ndi wa MCP ...chitsiru cha agalu

    • @pauldaka7966
      @pauldaka7966 11 месяцев назад

      Inde mchifukwa chake program iyiyi ikuveka monga akuyambana

    • @eliffagondewe8214
      @eliffagondewe8214 11 месяцев назад

      Kkkkk sure anali ata coach na kale awa aaaa🔥

  • @melodybashiriahmad914
    @melodybashiriahmad914 11 месяцев назад

    at the end am giving both of them 50/50.
    mbamva ziwiri zidakumana zochokera ku ma group awiri a corruption. (DPP & MCP)

  • @dyba-x9w
    @dyba-x9w 11 месяцев назад +2

    a wonder try your best to be neutral change your system, it seems something is not ok with you.

  • @lewisbonongwe8518
    @lewisbonongwe8518 11 месяцев назад +1

    Waseka Namalomba 😂😂

  • @PatrickMulangala-os4by
    @PatrickMulangala-os4by 11 дней назад

    Anamphedwa ndi ndan I?

  • @simonpaul6567
    @simonpaul6567 11 месяцев назад

    And Mr Namalomba you was behaving why you don't wait to finish talk

  • @frankphiri257
    @frankphiri257 11 месяцев назад

    Muzamenyanisa akulu akulu
    Muzizikhoza bwino zithuzi