This is the best n' honest ever Hot Current ...Anthu adzikumadi mbali dzonse monga momwe mwapangira apamu. Apa mpomweno tikutha kudziwa kuti " Atambwali ndi atiwo kkkkk
For the first time I have to comment on this, from look of things onsewa ndi anthu oti palibe chomwe angapange kuti athandize dziko lino. Panopa from what I have Said palibe Ali ndi masomphenya ofuna kukonza dziko koma kutukula matumba awo. Sindikuwonapo munthu apa. Continue kutibela basi nthawi yanu. Inu a tonse alliance ibani monga momwe anzanuwo anabela zikuwawa nanuso a DPP mukalowa ibani basi osamangana
The main problem that these leaders have is they politicize everything...Instead of coming up with workable technical solutions they are just busy backing up their parties....This is sickening! It appears Malawians are not just poor economically but they are also poor mentally.. These leaders are not on their seats to fix Malawians problem but to fix their personal and party problems...
These men are well aware of the real reason our Country is poor. We're not utilizing Malawians. We're too busy acting like servants. Where's a real Gov't with chidwi and commitment to improve us? Our Politicians are embarrassing.
I think there is no need to b inviting these failed politicians... palibe chanzeru angatiuze adzingolozana chala basi.. continue your program mmene mumapangira kale
anuwake a program safunsa manfunso mwa intelegent amafunsa mwa ubulutu kapena mwa usavage Kodi mumapitadi Ku school kukaphunzira zapa wailes funsani munthu mpatseni mpata ayankhe
Koma mmene likuzunzira dziko ili,anthu tikuvutika day in day out mkumati tikulonza mavuto amene anzathu anasiya three years down the line,like really Mulungu akuyendereni mwapadera sure😢😢
Namalomba uli ndi nzeru koma wamushayinitsa Kinkuyu chifukwa uli ndi phuma next time uxizaupeza komaso kukhalitsa ndi APM sungakhale ndi nzeru bcz ija ndo mbatata ya mtsogoleri yomwe inkangona pa chiongolere,mwachidule nonse mbava zobera a malawi
I think Kunkuyu is clever enough however he doesn't have enough data to tell the nation how and what to do to improve our economy.He is a good politian to protect his superiors.If he can be honest he will admit the failures in the regime.Please accept you have failed guys.
Kunkuyu is just talking nonsense he don't know how anger is in Malawians 😢😢😢😢
More fire Nambalomba 🔥 🔥
This is the best n' honest ever Hot Current ...Anthu adzikumadi mbali dzonse monga momwe mwapangira apamu. Apa mpomweno tikutha kudziwa kuti " Atambwali ndi atiwo kkkkk
🤣🤣🤣Kukuyu ukuwona ngati malawi ndi wa Abambo oka achakwera et
Kkkk kmabe ngakhale dpp imapeleka ma figure olakwika ku imf kmabe dziko limayenda bwino kusiyana ndipano
Yeah zoona boma lomwe lilipanopa likuphweteka kwambiri ndibola dpp
🔥🔥🔥🔥🔥 namalomba on 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Wonder ur best ❤
Kkkkkkkk ndevu zamwayi 😂😂😂😂😂 apa ndiye mwaitha sindinayambe kunvera koma ndimmene ayambira akunkuyu aaaaaa
If they are failing to buy a packet of sugar why? Is not because of expensive
Kkkkkkkk koma mkukuyu zoti azabwelaponso apa ndakaika😄😄😄😄
Namalomba ndiwe galu kwabasi wandisangalatsa kwambiri uli ndi nfundo komaso phuma 😂😂😂😂 wakwana iweyo Namalomba Umatiyimilira tonse amalawi a DPP
ingoswananipo zithepo💪💪
Zoona zake
Ndevu za mwayi ndiwe wa mcp bola Brian ndi fire
A Shadreck namalomba kuwonesa kuchenjera satana akukugwitsani nchito koma one day is day muzakolora
Mmafuna munene kuti a Kumkuyu kapena aNamalomba? Chifukwa ine mkuona kwanga ndikuona kuti amene akuoneka kuchenjera kulankhula apa ndi akumkuyu chifukwa akuzembazemba pamene chilungamo akuchidziwa
Never trust any Politician
For the first time I have to comment on this, from look of things onsewa ndi anthu oti palibe chomwe angapange kuti athandize dziko lino.
Panopa from what I have Said palibe Ali ndi masomphenya ofuna kukonza dziko koma kutukula matumba awo.
Sindikuwonapo munthu apa. Continue kutibela basi nthawi yanu. Inu a tonse alliance ibani monga momwe anzanuwo anabela zikuwawa nanuso a DPP mukalowa ibani basi osamangana
Mungoona Mbava Mmene ikusekera Kusekelera 😂😂😂😂
Mr Wonder muziwapasa mpata olongosola kuti amalize osamangowadula pliz
The main problem that these leaders have is they politicize everything...Instead of coming up with workable technical solutions they are just busy backing up their parties....This is sickening!
It appears Malawians are not just poor economically but they are also poor mentally..
These leaders are not on their seats to fix Malawians problem but to fix their personal and party problems...
These men are well aware of the real reason our Country is poor. We're not utilizing Malawians. We're too busy acting like servants. Where's a real Gov't with chidwi and commitment to improve us? Our Politicians are embarrassing.
This was hot🔥🔥🔥🔥🔥
Akunkuyu ndalama zikubedwa muulamuliro wa MCP komaso njala yaphwi anthua kufa ndi njala
This government is a headless government
Mr wonder mukuyener mukapeleka funso muziwapatsa mpata kuti afotokoze cfkw zikuonets ngat mukufusa funso pamene yankho mulinalo kale
nde utolankhaniwo
Boma limene lasokoneza zinthu kwambiri ndilomweri la mcp
Both parties palibe chomwe amayakhula zogwiea mtima,mitima mwawo mwangozaza mikwiyo
Politicians😂 this is just a game 🎯🎮
Komatu eeeeee! Amalawi timadziwa kudzibakira
Hot current yalero ndiye yandiwaza nyatwa kkkk
Anthu amenyanatu awa ndikuona ngati aDpp zinawawa kwambiri samafuna kuchoka
I think there is no need to b inviting these failed politicians... palibe chanzeru angatiuze adzingolozana chala basi.. continue your program mmene mumapangira kale
Namalomba ndimwana pandale Ndipo muli makani opanda ntchito atakhala m'boma anthu awa sangamatsutsike
Koma ilyi ndi hot current for sure 😀😀😀😀
Definitely 😂
Program iyi ndiyandale amalawi muzisamala pomaoonera manyaka awa, this is another part of compaigning
kkkkkk Osokonedza abwera
Kod akukuyu kod wasowetsa sugar ndan mesa Inu atonse ( a mec akazangotulutsa kut mwawinaso muzaiputa khondo cuz mukuziwaso kut 3coters simukufunidwa dziko lino )
Kunkuyu siukuyankha mafuso Ungokamba mbalume zopusa
anuwake a program safunsa manfunso mwa intelegent amafunsa mwa ubulutu kapena mwa usavage Kodi mumapitadi Ku school kukaphunzira zapa wailes funsani munthu mpatseni mpata ayankhe
Wonder musiye kunkuyu alankhule
You must agree that the past affects the present.
Ntchito ikumuvuta uyu amene akuyendetsa program_yi kodi Brian Banda analikuti nthawi yomwe amamusiira mzake wa mcp_yu kuti apange Host program yofunika ngati imeneyi???
DPP inakanika kale now we are looking forward namalomba wawononga chipani Cha ambuye ake
Kkkkkk Koma wonder wandiseketsa 😂😂😂😂😂
Koma mmene likuzunzira dziko ili,anthu tikuvutika day in day out mkumati tikulonza mavuto amene anzathu anasiya three years down the line,like really Mulungu akuyendereni mwapadera sure😢😢
Wonder usamabwere utakhuta cyclone mbatata wamva, ukumagunda posagunda bwanji😂😂
akuonesa mbali
@@dyba-x9w
Ayi sanaonetse mbali koma inuyo muli ndi nkhawa ndi mbali yanu.
DPP ibwelele plz cement 20,000😮
Ndipo mavuto alipo nde mkuka voter so imbwaa zimenezo ayi zikomo mcp🙌🙌🙌
Kunkuyu amalawi tikufuna moyo wabwino osati zomwe ukulankhulazo
Izi zikadalongosoka chikhala Kuti khaniyi ikukambidwa mwadongosolo. Koma Vuto Lake zikukhala Ngati Wanda wabwela Atalawa.
sindikufuna kutaya nthawi yanga ndikumvetsera uyo wa mcp uyo palibe chimene anganene manyazi alibe galu waanthu
Those suits are our money
ineyo ndikuona molakwika kwambiri ndikukumbukira mau omwe bon kalindo anayankhula week yatha kuti times ikubakira kwambiri tonse adminstreation, ndikanakonda a Wonder wo akufusa mafuso awo ndi a indipendent balancing sikutheka . akhale neutralas ngati mtolankhani
mr msisya improve your questioning skills when you have big dogs
Namalomba uli ndi nzeru koma wamushayinitsa Kinkuyu chifukwa uli ndi phuma next time uxizaupeza komaso kukhalitsa ndi APM sungakhale ndi nzeru bcz ija ndo mbatata ya mtsogoleri yomwe inkangona pa chiongolere,mwachidule nonse mbava zobera a malawi
Koma akukuyu amatha osutsa satinthandiza
Big up Namalomba
Kumkuyu galu mutu oumawo
Kuchenjera kwatha mcp anthu oipa,
Kukela kwazinthu kukhala ngati munabadwa kwachinyama agalu achakwera ndi adzanuwo ndiposo kumkuyu ndiwe kape
DPP imakwana kkkkkkkkk keep it up.
Wander ndiwe Garu
munalakwa pochotsa dpp chomwe mwachita inu a mcp ndichani dpp imagulitsa feterizer 50 kg inu a mcp k90,000 anthu akumudzi angakwanitse kugula feterizer? mwaononga dziko a mcp anthu akuba okupha
Athu ...onsewa palimbe chomwe akuyankhula zomve saname angopanga ngti akupanga nthano awa a mcp nawo athu olephera ...padzaka zitatu apanga chani bolako Dpp ndithu tinkhodza kulodza zomwe apanga azaowo ❤❤❤ Dpp awo ziphuphu kuba kwambiri mcp
Brian alikut
Zitsiru Za anthu iziii muwatenga amalawi Ngati a kapolo
Masanje okhaokha
Namalonda sanakhakepo mbom
Koditu wakuba amayankha mwazelu cholinga awapusise amalawi pano nde tazukatu siife akale aja ayi
I think Kunkuyu is clever enough however he doesn't have enough data to tell the nation how and what to do to improve our economy.He is a good politian to protect his superiors.If he can be honest he will admit the failures in the regime.Please accept you have failed guys.
Nkukuyu or utakokera motani ,zakubvutani basi , palibe mukuchita ,komaso a wonder ndinu a MCP
Malawi feeling pains😢
Kumkuyuyu mkatundu
Ndikanakonda kuti msogolomo osamatenga andale kumapezeka pamenepo chifukwa wandale ndipovuta kuti azavomereze zolakwika zake, ndiye ife okonda dziko lathuli amatipwetekesa mitu.
Namalomba is well matured and he knows how to answer the questions, Big up Sir.
Zoonadi
Aaaaaa kuyankha mafunso mkumeneko kmno inu muona kut Tonse yu akuttenger kut.
These are crukes
A wonder ndachitsiru so buanj
This hot current for today there is nothing you 2 you answer Mr Namalomba and Kumkuyu
Palibe gvn imene idzabwele ndi chilungamo ku Malawi mbanva zonse
Namalomba ndiye dolo Akunkuyu sakundifikapo anta naye Wonder akuonena kuti sympathizer wa MCP
Political z a deaty game a can agree na
Kom Nyasa tim imakwanad
Kuposa Akt kul zodiac
Mpak mwakumanizad
Ulendo win mudzamuitan chilim ndi Atuper
Komanso chakwer ndi pit
I have personally liked this approach. These people must be accountable for whatever they are doing.
Kumkuyu ntchito yamukulira
Mungakweze bwanji lulimi pomwe feteliza ndalama mumapeleka kuma butchala ndi kuma Pharmacy anthu alimila chani mwalephela basi tatopa
Mbuzi za anthu Malawi tili pa moto dziko loti lingathe kusitha mosavuta koma dyera mbuzi za anthu izi shupiti
I think Wonder Msiska u are the one who is bringing chaos in this interview-U are very unprofessional
Ma trillion being mentioned like it’s nothing.
Kalonga Shawa uiwale za 2025 ndipo muyembekezele kumangidwa
Kunkuyu nchitsiru, chidzete, munthu opepera, nyapapi weniweni.
Namalomba amakhala nditimajoker, atha kupweteka gulu
This one the dog of the dogst🇲🇼👁
Kodi Mesa amatcalenger kt after 2years akhala atapanga client kukanika apamga lisine pano tree years apamga apamga chani mbava
Mbuzi zokhazokha zinakumana
Trillion kuitchula nganti pin
Mcp inatengadi mbuli
Wanda ndi wa MCP ...chitsiru cha agalu
Inde mchifukwa chake program iyiyi ikuveka monga akuyambana
Kkkkk sure anali ata coach na kale awa aaaa🔥
at the end am giving both of them 50/50.
mbamva ziwiri zidakumana zochokera ku ma group awiri a corruption. (DPP & MCP)
a wonder try your best to be neutral change your system, it seems something is not ok with you.
Waseka Namalomba 😂😂
Anamphedwa ndi ndan I?
Mukut anasakaza nanga inu?
And Mr Namalomba you was behaving why you don't wait to finish talk
Muzamenyanisa akulu akulu
Muzizikhoza bwino zithuzi