HOT CURRENT 14 JULY 2024 |

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 13 июл 2024

Комментарии • 97

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 Месяц назад +8

    Go on Guy's we wait to see the changes in Malawi eeeee from Bakili muluzi up to know am in RSA because of politics of Malawi throwing as away not thinking of coming back to home eeeeeeeeesh

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 Месяц назад +6

    Chilima was assassinated that's the truth what more do u want to hear?

  • @user-lj8ug5lq8c
    @user-lj8ug5lq8c Месяц назад +2

    Guys keep it like this ,this is Hot current we know from those days congratulations

  • @JamesIngeni-ku3qj
    @JamesIngeni-ku3qj Месяц назад +2

    Manganya ndi mcp anapha chilima.

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e Месяц назад +3

    Usi si wa UTM. Munamuwona muja amarandira udindo muja? UTM yachita bwino kuwaturuka.

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Месяц назад +2

    Ngozi ija singozi ngozi ,,komanso yonse taona ndimafinso

  • @BambordKabambe
    @BambordKabambe Месяц назад +6

    😂😂😂😂😂 chaka chino ndi CHONG'ALURA

  • @JohnNjerenga
    @JohnNjerenga Месяц назад +1

    Kkkkk akut ipondeni fadha

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 Месяц назад +1

    Apa ndiye mwabwelatu chilungamo chimenecho

  • @EstherChimombo
    @EstherChimombo Месяц назад +1

    🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💯💯

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk Месяц назад +5

    Times muziwe kuti chilima agwila bwanji ntchito ndi chakwela mu 4years

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Месяц назад +2

    Masapota a UTM tonse tatuluka ku mgwirizano Chifukwa tinkasapota Chilima.Usi alibe masapota.

  • @user-oh9bh1cl3b
    @user-oh9bh1cl3b Месяц назад +1

    Well spoken guy's adzimva akawalalawa

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 Месяц назад

    Walephera Chakwera kulamulira kuchedwa 4yrs ndipo akhala akungodandaula DPP mmalo mopanga ziganizo msanga

  • @OrtonKabbichi
    @OrtonKabbichi Месяц назад +2

    Sizachilendo olo pa ngozi ya ndege ija anachedwanso kukafufuza ayambe kuchotsa ameneo onwe amaenera kukafufuza za ngozi ya ndege

  • @patricksinyala1345
    @patricksinyala1345 Месяц назад

    Mtsukuluzi ukulankhula mopusa, kufooka kwa Ussi kunayamba Chilima alimoyo. Ndipo. Chilimma anali atamuzindikila Kale Ussi ukathyali wake.

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h Месяц назад +3

    Inu ussi siwa UTM 😂😂😂😂ameneuja ngawa MCP

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Месяц назад

    Chakwera so asamale zomwe wawona Nzake wa kwa merica zija zichitikanso kuno.

  • @symonmakata938
    @symonmakata938 Месяц назад

    Changucho chiyambile pa kafukufuku wa ndege inapha chilima kenako the public ikhala ndi changu

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v Месяц назад +3

    Dziko ndilathu osaonesa kutopa azibambo ipondeni thawi ino palibe kuopa ng,alulani basi ng,ambani

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d Месяц назад

    Usi atha ngati nankhumwa sure, olo kuthesako akufuna kukhaulisa manganya coz anamuziwa kuti uyu sitili limozi ndi wa mcp.

  • @JohnmarkNazombe-hi9xd
    @JohnmarkNazombe-hi9xd Месяц назад

    Dziko nkumasawukaaaaah!!!!!!!

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Месяц назад +1

    Masapota ake ati omwe atsatire Usi ku MCP. Musanamizane palibe yemwe angavotere MCP true member wa UTM

  • @EfeloYovita
    @EfeloYovita Месяц назад

    ngati bola Allience latha ndibwino kukhala opanda president cs chakwela polowa m boma unali mgwilizano maka utm inali ndimavoti ambiri kuposa mcp we must have emergency presidental election

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Месяц назад

    MCP yayambitsa nkhondo yoopsa yokha amalawi sangasangalale nazo izi
    Zotsatila results zangozi kuli ziiiii mpaka pano what do you do

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma Месяц назад +1

    Keep it up Guy's ife ndalama tidya koma sitidzawavotela talira kokwana sife opusaso pano

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy Месяц назад

    Akuchedwa Nd pule yomweyo😂😂😂😂😂

  • @imaculadaAndre-ns1py
    @imaculadaAndre-ns1py Месяц назад

    Fiti ndifiti basi awa sangaulule chilingamo kwao ndikunama basi koma ife chilingamo tinachipeza kale

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Месяц назад

    Akuti mbwexe😅😅😅😅😅😂😂😂

  • @catherineKalinga-m4c
    @catherineKalinga-m4c Месяц назад +2

    🤩

  • @AishaChipande
    @AishaChipande Месяц назад +2

    Chakwela azuzula bwanji pomwe iyeyo anaphaso muzake

  • @EsnartMbalale
    @EsnartMbalale Месяц назад

    Ipitilile ndiyabwino coz ikulakhula mosatenga bali

  • @imaculadaAndre-ns1py
    @imaculadaAndre-ns1py Месяц назад

    Tamusiyani maganya abakhala komweko adzatiuza zenizeni abawatola zifukwa adzapange sewelo mutu wake chakwera anapha zake chifukwa chaudindo

  • @OfwaMwambila
    @OfwaMwambila Месяц назад

    Alot of people re in marriages that ended a long time ago but due to kids u re forced to still living together that's what I think was the case of SKC&usi.

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki Месяц назад +1

    Akuyambisa kuchedwa ndi achakwela ndipo ife tinalakwisa kumuika munthu onamizila ubusa Ngati uyu pa mpando

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Месяц назад

    Mbwelera zokha zokha za mcp kkkkkkk koma pankuku!!!!!!

  • @BestonStima
    @BestonStima Месяц назад

    Mcp ivutika chifukwa isanalowe m'boma amalawi ankaopa nkhanza za mbiri yawo
    Lero in their 4yrs rule patuluka nkhanza.
    Do you think they can reign???????????

  • @robertnambazo9936
    @robertnambazo9936 Месяц назад

    President osaziwachomwe akuchita he is so relaxing President President uyu ndi bubu shatapu zake

  • @SteveKanongwa
    @SteveKanongwa Месяц назад

    Koma ma guys inuo hahaha munatopa nalo dzikoli simufunaso zachikape

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Месяц назад

    Manganya ndi wa mcp not utm

  • @johnmhango9405
    @johnmhango9405 Месяц назад

    Briefcase parties end just like that.

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Месяц назад

    Uyakhura za chidodoyo ndiye ili mbudzi yoyambisa chakwera samasata zinthu that’s y anyamata ake angomisewera basi.

  • @SteveChapola
    @SteveChapola Месяц назад +1

    A mcp chipani chokupha

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Месяц назад

    Sitizalola report. Wonder you are very Intelligent than pankukuyo

  • @GodfryMalishe
    @GodfryMalishe Месяц назад

    Salute u guys 😂

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy Месяц назад

    How many meetings manganya has been attending?? Can he allow to apart from the alliance coz it's obvious manganya it's won't allow

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 Месяц назад +1

    Eeeeeee yankhulani guys ❤

  • @lukedumbula2724
    @lukedumbula2724 Месяц назад

    Very true wonder and jona, a PULE akuchedwaa

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Месяц назад

    Pa nkhani yochedwetsa chitukuko, tingomuchotsa next year basi, sali fit Chakwera to be a President.

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Месяц назад

    A Usi si president wanthu,,munthu mkazi wake tamuziwa polumbilitsa mkumazitama kuti ine sindinayendepo ndi mkazi wanga,,muthuyu angayendese chipani

  • @RafiqueChibwana
    @RafiqueChibwana Месяц назад +1

    You guys u don't share kamba here really keep it up guys kkkkkkkkk

  • @JaphetSakala-pq4fl
    @JaphetSakala-pq4fl Месяц назад +2

    Kuchokela pa ifa ya VP chilima kufikila pasiku la mavoti UTM ILI PA TOP ONE. or Dpp ndi mcp ita phatikizana. UTM IKUTENGA BOMA TIZAIPEPESA NDI VOTE.

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr Месяц назад

    Lero munabweratu a jonah kkk wonder akuti back to sender eee Chakwera dzimvere mumtolo

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba Месяц назад

    Eni ake a UTM ndifeyo ovotafe Tatupu ndife awowo dyela Paolo asaleko tilibe nawo film

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi Месяц назад

    Osawopa ayi a malawi ambiri tikuyang'anira inu kut muziyakhura mosawopa apa

  • @CosimassShyman
    @CosimassShyman Месяц назад

    Wakulu andevu zamwayi amayankhura Chichewa cha boo

  • @YamikanChirwa
    @YamikanChirwa Месяц назад +1

    Ng'alula iwe

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Месяц назад

    😂😂😂😂😂 anyamata inu mwandisangalatsatu chikufunika ndichimenechi osanyangerera kulankhula chilungamo kubandaluka basi sizoopaso ayi

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p Месяц назад

    Kaya DPP kaya ilibe ndalama iwinabe 2025

  • @user-rd9pd9hr2l
    @user-rd9pd9hr2l Месяц назад

    Inuyo munabwera ngati coming 🔥

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Месяц назад

    A pule ayamba kupemphera ku CCAP kamutu kataya

  • @joneskalitsilo6556
    @joneskalitsilo6556 Месяц назад

    Exactly Wonder bambo wanzelu amakonza mavuto amu nyumba mwake not kutuluka nkumakadandaula panja or kubwalo kuti mnyumba mwanga sitikudya ana anga sakuvala bwino, sitikudya bwino! Nde ana Inu muzivala bwino, muzidya bwino, ukuganiza kuti anawo azitenga kuti?

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850 Месяц назад

    Nkhaniyo ndiyoona, a President akugona kwambiri pachiongolero, dziko silingatukuke ai

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Месяц назад

    Anaphedwa ku Mwanza aja ndiochepa.pano ayesetsetsa kupha ambiri.athakati sadzasintha.Malawi Congress of Perishers

  • @DarlingtonMaya
    @DarlingtonMaya Месяц назад

    Gyz mmmatha

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Месяц назад +2

    MCP ndi Yakupha

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi Месяц назад

    Iwe pankuku osamayakhura mowopa apa

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI Месяц назад +1

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @MuhamadYassin-ye4hn
    @MuhamadYassin-ye4hn Месяц назад

    Mumakwana mabigi

  • @Amos-tr6ro
    @Amos-tr6ro Месяц назад

    Koma makosana inu MMM mwanditha keen on on our behalf

  • @jackmambo2638
    @jackmambo2638 Месяц назад

    Kod amaphang’ombe ali kut😂😂

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o Месяц назад

    Did. Mcp ask Afford

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki Месяц назад

    Aganizq bwanji mwakuya kuposa anthu zosatheka ubongo unatha chifukwa ankadya zopasidwa Za chaulele

  • @user-tg7ni7wh2c
    @user-tg7ni7wh2c Месяц назад

    Eeh 😂

  • @johnmhango9405
    @johnmhango9405 Месяц назад

    A kaliati ndi a njawala nzokonza izi, akufuna apange handpick Kabambe, can't you read between the lines? Typical of atsogoleri a dyela.

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r Месяц назад

    Emusipi ofunika isale yokha. Anthu woipa awa

  • @frankdomingo1109
    @frankdomingo1109 Месяц назад

    Decisiveness palibepo

  • @yusufjab786
    @yusufjab786 Месяц назад

    Ndipo inuyo kumeneko mumaitha 😂😂😂 akuchedwesa ndi chakwera

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o Месяц назад

    You. are. wrong. it. Is. People. at. the. grassroots. who matters not individuals

  • @PartsonMdeza
    @PartsonMdeza Месяц назад

    🤣🤣🤣 iponden fadah kkk

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn Месяц назад

    Ofufuza ngozi akuti, khoswe akakhala pakhate sapheka

  • @SteveChapola
    @SteveChapola Месяц назад

    Asiyeni atuiuka chifukwa chake achakwera apha chirima ndipo ndizoona

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gf Месяц назад

    Osamayiwala ku mudzi kaamba kokomedwa ndi maidyaidya chifukwa tsiku Lina amadzakusandutsa mtsamiro wa mfumu ikadzamwalira.

  • @michealchaomba9761
    @michealchaomba9761 Месяц назад

    😂😂😂 President wake utiyo mukudikira kuti azuzuleyo

  • @MarthaBanda-ye4pt
    @MarthaBanda-ye4pt Месяц назад +1

    Koma Wonder Ati kukura mtima 😂😂😂😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥uyatseni basi ng'alulani basi

  • @user-ru4px8os2v
    @user-ru4px8os2v Месяц назад

    Anthu ake ndi chimwendo banda,howeh mkaka,zikhaleng'oma ndiomwe akuyenela kuchoka

  • @ThandiMbewe
    @ThandiMbewe Месяц назад

    Musamamuzile zochita president, yekha samawona???

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Месяц назад

      President wake uti
      Ma comments 100 wa MCP yekha .chita manyazi😅😅

  • @SteveChapola
    @SteveChapola Месяц назад

    Chakwera ndiwofoka koma kumagaanthu chimenecho ndiye chitukuko.chake

  • @NdazionaKumcheza
    @NdazionaKumcheza Месяц назад

    Ine dakalira malemu za chipani tizitaye uko aaa

  • @YusufuUsumani
    @YusufuUsumani Месяц назад

    agaluwa alilimosi ndi chachera

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi Месяц назад

    Osamayakhura ngat akupatsani za lent kung'alura basi ukuva iwe ndevuzamwayi !!

  • @user-ql8nf2vb8s
    @user-ql8nf2vb8s Месяц назад

    Inu a times muyang'ane mgwirizanou kuchokela mmbuyo inunomwe mumaunikira mgwirizanou mmene umayendela chilima asanamwalile asiyeni ausi ali ndigululawo odya zake alibe mulandu

  • @MuhamadYassin-ye4hn
    @MuhamadYassin-ye4hn Месяц назад

    Mumakwana mabigi