AKUFUNA KUPANGA ALLIANCE NDI MCP ALI OLANDILIDWA |

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 25 окт 2024

Комментарии • 34

  • @Lingstone-r3z
    @Lingstone-r3z 2 месяца назад +2

    No more to join with MCP never

  • @Marymahendra
    @Marymahendra 2 месяца назад

    Sorry nobody else wants to join MCP party in the future until Jesus Christ comes back xx

  • @CharlesChagudubuka-rm6bh
    @CharlesChagudubuka-rm6bh 2 месяца назад

    Muisova amene akufuna kukafera ku chikangawa apite 😅😅😅

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 2 месяца назад +1

    Zisankho za Normal Simungawine a MCP, Mukamuzutse kaye Chilima ndi ena 8

    • @TracyBanda-i2g
      @TracyBanda-i2g 2 месяца назад

      Kwambili akadzuse chilima chifukwa adamupha chilima pofuna udindo ndiy asake owajoina munyaaaa

  • @Fatima-f5c
    @Fatima-f5c 2 месяца назад

    Wasowa n,tengo ogwila azionaa

  • @AkimumusaMusaakimu
    @AkimumusaMusaakimu 2 месяца назад +2

    Kk wachedwa utalawilila sister

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e 2 месяца назад

    😂😂😂😂mwaganiza bwanji MCP

  • @ShamilahSaizi
    @ShamilahSaizi 2 месяца назад +1

    Eeeeeeee mpaka alliance ndi mcp???? Koma kukhala kufunanji

  • @Fanzo-h2l
    @Fanzo-h2l 2 месяца назад

    Ndipo azipami musalore kugwiliza a ndi Malawi Chikangawa Party mukufuna zipani zilalowa mgwilizano muzawaphenso ngati Chilima agallu inu

  • @DixonChimanya
    @DixonChimanya 2 месяца назад +1

    Muiwale kuti mupanga gwirizano ndi ena
    Mwapha chilima

  • @DixonChimanya
    @DixonChimanya 2 месяца назад +1

    Mwapha chilima pofuna kuti chakwela wanuyo alamulitso

  • @JacquereenPereira
    @JacquereenPereira 2 месяца назад

    Eeee mwaphela chilima muja anga pite ndani eee ndinu oopsyaaa kwambilili

  • @DKMWALE-ew3lp
    @DKMWALE-ew3lp 2 месяца назад

    Allience ya ukapoloyo tiyeni nayoni ukoo

  • @brainsmkumbwa6267
    @brainsmkumbwa6267 2 месяца назад

    Agalu inu a MCP ,kuti kumene mukuyika moyo wa munthu wakumudzi patsolo,anthu akupha inu,palibe amene atapange nanu alliance ulendo uno, ndiponso chilungamo ndichoti popanda kubela simungawine zisankho,mukadzangowina tidzazwiilathu kuti mwabela

  • @PaxKinley
    @PaxKinley 2 месяца назад

    MCP MUKHAULA MUNYA MULIRA KUGWA KUJA NDI KUMENEKU PALIBE ANGALORE ZA UCHITSIRU UMENEWO.... KUBA, KUPHA

  • @JustinMdala-c1t
    @JustinMdala-c1t 2 месяца назад

    Kodi chipani chimenechi anthu Ake onse NDI osagwira Mitu bwino bwino pamwamba phaka kumutsi palibe amakamva zogwira mtima kumangoyankhula Ngati Ali maliseche

  • @mabvutochimkondenji910
    @mabvutochimkondenji910 2 месяца назад

    mcp bomaaa kuti buuuuuu 2030 woooo

    • @AkimumusaMusaakimu
      @AkimumusaMusaakimu 2 месяца назад

      @@mabvutochimkondenji910 iwe where where your mind.your not normal

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 2 месяца назад

    Mwanya mwadya chilima yemwe uja ndiolose ndikakutafune asaaa ndani akufunaso ku chikangawa

  • @mabvutochimkondenji910
    @mabvutochimkondenji910 2 месяца назад

    Ngozi ndi ngozi ku brazil adamwatila anthu 62 pa ndegenso

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga 2 месяца назад

      Kma sanavulidweko zovala ngakhale president wakonko sanaime kufufuza ngozi itachitika

  • @JorgeSacuate
    @JorgeSacuate 2 месяца назад

    Mayi oputsa iwe. Mufuna mupeze ngalawa yowolokera?? Muzawaphe kawiri mukazavoteredwa. Iwe ndi chakwera wakoyo cha.......................chanu

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 2 месяца назад +1

    Ntolankhani okongola km masamu anatulukira pawindo

  • @Rose-wu5ef
    @Rose-wu5ef 2 месяца назад

    Chipan cha magazi manja and khope yonse ya chakwela i kumaoneka magaz okha okh a achilima ndi athu ena 8

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 2 месяца назад +1

    palibe chipani chomwe chingapange alayance chifukwa mcp ndi chipani chokupha tawonera pa chilima mayi inu pantumbo panu ndithu munya muwona

    • @ManganiStanley
      @ManganiStanley 2 месяца назад +1

      agalu ngti inu Pali wina angalore kt ajoine anthu oipa ngti inu

    • @JoyceBanda-k8t
      @JoyceBanda-k8t 2 месяца назад

      Mcp iwalani zoti anthu akhonz ku join inuyo anthu ambiri akukuopani chifukwa ndinu okupha okupha oononga simusamala zaanthu

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 2 месяца назад

    Anthu okupha amene angachite nawo ubale ndani ....muona ndi ziko ili

  • @Ghama-k4i
    @Ghama-k4i 2 месяца назад

    Apiteso ndan angalore ndenge

  • @mabvutochimkondenji910
    @mabvutochimkondenji910 2 месяца назад

    Alimi afodya tanjoya boma lomweri basi mukatibera enanu

  • @EdsonKamwendo
    @EdsonKamwendo 2 месяца назад

    Inu palibe angakuyandikileni ufiti wanu uli pamtunda

  • @CharlesChagudubuka-rm6bh
    @CharlesChagudubuka-rm6bh 2 месяца назад

    Ndipo mukadakhala kuti mukufuna kulamuliranso next erections mukadasutsana kaya zopha chilima zija koma mudady mfulumila ndiye zikuvutani ndithu😊😢

  • @WachiyawoWangalusa
    @WachiyawoWangalusa 2 месяца назад

    Munya.inu.amcp.muona