When the manbwas asked kuti ndi mwana wao wa number chani he said ayenera kukhaka wa number 3....i can not believe this man he must have bought this girl from kwa msato
Mibawa pankhaniyi ndiyobasa chidwi koma wapakamwela sali bwino nkhani ikamafotokozodwa akamamuloza munthu kamela iziloza pamunthuyo, monga ngati ine ndimankhala chidwi ndikuonela pa on line
Munthu akaphedwa mwa nyanga ndiye munthu amene wamupha uja akafa nyanga zonse zimaululika komanso mankhwala onse amaululika ndiye anthu onse anaikidwa mnyumba ya a msato atulukira onse tsopano....please update what happened to those people who is their parents
Mwanayo ndi wa amayiwo, 100% actual truth coz there's no way kuti mwana wako akasowe kunyumba kwako. That man he's a ritualistic, ndi a msatowo they performed rituals that's why things are like that. Komanso as you can see, mwanayo was in a bondage she needs fasting and prayers to be set free indeed. I am Solomon in this case, the lost son in the bible returned to his family and by the grace of God the yoke is broked and now she has returned to her family. So let her be with her family where she belongs, that's her family. If you give the child to the man, you'll kill her and fulfill the man's rituals. Question; how did the man knows that the girl is in that village? Answer; the evil spirit of sato and the man that connects the two men, that yoke has to be completely broken. Please, don't take the daughter away from her mother family. Just keep the fasting and prayers for her, God must deliver her and set her free.
Let that man go back to his village and home to live with his life and family. He's a fool who even doesn't know kuti mwana wakeyo ndi number chani kubadwa and he doesn't know her. He might be sing'anga wa a Sato, just watch out. People are wicked nowadays, so let us keep on praying for others. Kuno ndiye tizipemphera mpaka ena anapangidwa chipongwe apezekenso.
When the manbwas asked kuti ndi mwana wao wa number chani he said ayenera kukhaka wa number 3....i can not believe this man he must have bought this girl from kwa msato
I do agree with you
M'dalayu ndi msing'anga akufuna atenge mwanayu akamubwezere komwe wathawa ndi mfiti uyu wa ku Mozambique
Mwanayo ndiwabambowo akufana naye awo zangolumikizana
Seems onsewa akukamba zolondora, enawa anachita kugula mwanayo, . Mkana funso loti ndimwana wawo wachingati alephera kuyankha.
Mkafutse maneba akwabambowo ,mthu Amazika Mdela
Kulibe munthu anauka kwa akufa boza mwana ndiwa abambo Zambia
Mene akuwonekeramo angakhale kt Ali nd mwana wa zaka 19 or Nat kt athu akubereka msanga mwanayo n wabambowo chabe muthu wamisala amawona zambili zachisis ndchofukwa amawona asatowo kmas zimay uja akt anafika n katund mujumbo ndy tizit anachoka nazo kwasatoko ay ameneyo ndwamisalad nd mwana wabamboyo
Mwana ndiwa bamboyo , amayio akunama dzaka 18 zadutsa angawoneke choncho 😊
😂😂😂 eti inu
Mwanayo ndi wamaiwo awasiyile
A chipatala ndiwo anganene zoona
Zinthuzi Mmmmm zovuta kotheka bambowo akuziwapo kenakache km mwana ndiwa mayiwo
Zowona ndiwabambowo
Kma ndzachisoni kmaso abambowa Akuti bwerani mumutenge Munthu wanuyi akundkanda😢😢😢😢😢😢
Mwanayu adamukhwimila abambo akewo akudziwapo kanthu
Musikana wabwino choncho kumalawi zachisoni akhodza kukhala ba banja bwinobwino
Abambo awo ndamene awasiyila zizimba zosunga anthu munyumba ndafiti iwoso mtsikanayo apasa mkakamila
Mwana ndiwambambowo adsowa loweluka wapezeka monday chilungamo chenicheni
Mwana ndiwabambowo nanga akuwakakamila choncho bwanji ndekt wawaziwa abambo ake
😂😂😂😂😂akukakamiladitu ndikuona kut abambowa adagula kwasato
Mwanayo akuwaziwa abambowo ndiwawo
Mwanayo ndiwa bamboyo plz give him
I agree with you coz akukamila and 18yrs ago mwanayo akuoneka wachichepelebe
If someone can help to do DNA test it will help but i am doubting the man
Abambo awo ndititi akufuna kuti asokonedze umboni wamwanayo chifukwa mnkhani sitinamve mwana awachula dzina .Bombo uyo amadziwana ndia fiti chinsato,mtsayerekedze kumsiyi mwana akampheratu msungwana wabwino .bvomeredzani kt mwana watopa nding'mbe.
Am watching from zambia make me to understand am behind .
This is complecated but you can only understand if you learn the language
@@berthakambwiri6288He's not Chewa like me....this is also our language in the eastern part of Zambia... Chipata/Katete, etc....
Chofunika kupita naye ku DNA then ku church orkuma prophet like bushili I'm from Zambia
Abambo anachita kuguladi mwanayo munthu sungayiwale mwana wako kt ndi wanambala chani
Ndimomwe ndikuyibverera nkhaniyi mwanayu ndi wamayiwa komano poti nkuluyu akuti ndiwakenso zosautsa mwinatu nkuluyu akudziwapo kanthu kuthetsa nkhani ndikoti apite ku hospital akayense magazi
Afufudzidwe bwino bamboyo chilipo chilipo chomwe akudziwa za imfa ya mwanayo
Mibawa pankhaniyi ndiyobasa chidwi koma wapakamwela sali bwino nkhani ikamafotokozodwa akamamuloza munthu kamela iziloza pamunthuyo, monga ngati ine ndimankhala chidwi ndikuonela pa on line
Satana akufuna kutisokoneza potumiza bamboyi cholinga tisakhulupilire ndalamayu si real human being ndiongotumidwa ndi Satana.
Mwana ndi wabambawo mayiyo wawo anamwalira
Koma njira yabwino guys D N A siyimafanana angokayeza kuchipatala basi
Za ufiti bas
Afananadi ndamayiwo ndiwawo m'dalayo amutuma
Lord have mercy
Amayiwo anavomeleza kale asiyireni abambowo.
Umfiti ulipo ndithu ndipo anthu akuikidwa mmanda amoyo
Bamboyo watumidwa nda asato plz chonde mwanayo asiyiren amayiwo ndiwawo abambowo ndimagwala amenewo apanga kut aziwakakamila Dala plz chonde mwana ndiwamai
Anamukwimila bamboyo akudziwapo kathu
Apopo chofunika ndi DNA
DNA TEST BASI osati kumakangana ngati a galu opanda nzeru
Kkkkkkkkkkk kukanganrana mwana kkkkkk kwamvuta
Akufanana ndi abambowo
Bqmboyo anamugura kubanjaku mmatsenga azimayiwo sakunama😅
Mwanayo ndi wa abambo awo mayi awo akubamwanayo
Am watching from kasama zambia
Akufana ndiabambo mwana uyu
Mwana WA bambo wo mayiwo siwawo ayi
Bambo amenewo ndi fiti mwana siwawo
Mamuna sabeleka mwana, mwanayo ndi amayiwo
Achikangawa
Mwanayo ndiwabambao, kumanso akulongosola bwino kuti sikoyamba mwanayu kusowapo, kusonyoza kuti anthu ammudzi mwabamboyu akumudziwa mtsikanayu, komaso ku police akuidziwa nkhaniyi
Nkhani yi yinatha bwanji
Iburahim jumms
Chiphaso cha kuchipatala chigwire ntchito
mwanao ndiwamayio bamboo ndiokhwima ameneo
mdarayo akuziwakanthu mesa
Osawafunsa kuti mayi ake a mwanayo ali kutoko? Bwanji sanabwere nawo.
Mayakho Ali kuchimpatala
Zovuta kwambir eish
Bamboyo ndi mfiti anamukhimila mwanayi satana mlungu akuone
Munthu akaphedwa mwa nyanga ndiye munthu amene wamupha uja akafa nyanga zonse zimaululika komanso mankhwala onse amaululika ndiye anthu onse anaikidwa mnyumba ya a msato atulukira onse tsopano....please update what happened to those people who is their parents
Fantastic story 😂
God protect them
É daquele senhor
Pakufunika experience doctor ayeze DNA
Abambowadi ndi mfitidi👹 ndiekuti amenewa amatumikira nawo zawozo
Wawo bamboyo zikavuta DNA bas
Ash koma yah
Muphen mdara ameneyo asiye soputsa kupha athu
Mwinaso zipserazo mwina ankayamwitsa ndondosha za abambowa
Musakaike ndichoncho ndithu.
Bamboyo ndi nsing'anga mwina amadziwana ndi gogo womwalirayo
Mfumu solomon bweran mzaveso khani yina kuno
Koma ndiponso
Remember, we are in the end-time
Uyo bambo ndi mfiti Ali ndi Malaya a msipu,itanani a singanga amuone
Mwanayo ndi wa amayiwo, 100% actual truth coz there's no way kuti mwana wako akasowe kunyumba kwako. That man he's a ritualistic, ndi a msatowo they performed rituals that's why things are like that. Komanso as you can see, mwanayo was in a bondage she needs fasting and prayers to be set free indeed.
I am Solomon in this case, the lost son in the bible returned to his family and by the grace of God the yoke is broked and now she has returned to her family. So let her be with her family where she belongs, that's her family. If you give the child to the man, you'll kill her and fulfill the man's rituals.
Question; how did the man knows that the girl is in that village?
Answer; the evil spirit of sato and the man that connects the two men, that yoke has to be completely broken.
Please, don't take the daughter away from her mother family.
Just keep the fasting and prayers for her, God must deliver her and set her free.
Kukanganirana munthu ouka. Kkkkkk
Koma fuso la2 zinatha bwanji koma
Zingatheke nimadiku osiliza ano
Ikuveka mopusa nkhaniyi, mot ngat mwana ndi abambowo bwanji akumudzi kwawoko ayikilepo umbon chifukwa it's obvious anthu kumudziko akumudziwa
Where is the mother of that girl
Jabesi
Dremo
Munthuyo abamboyo amusiye siwawo kutheka watumidwa kwa asato omweo
Just do DN test
DNA ndiyomwe iyenela kunena zowona kuti mwana mwini wake ndindani boma lichitepo kanthu pankhani imeneyo
Bamboyo obvious mwanayo ndi wake
Agalu nkhani za malilo basi
The man is responsible over the lost of a girl,it seems the man was incharge of the girl
Madala mwana ndwawo
Kodi eni mwana anadziwika?
zomvetsa chisoni
E able zamasiku osiliza
Good
Abambowa ndiwo akuyang'anila ana ku satanism,so atumiwa kuti amufune-fune,akalephera alpha iwowa ku satanic
Bamboyo akunama
Abel ulibho umatha kuitsata nkhani ndipo umatha kufunsa mafunso
amuwone achipatara ngati anabelekapo umbon ndiosavuta apa
Or apange DNA
❤❤❤❤
Sia
Let that man go back to his village and home to live with his life and family.
He's a fool who even doesn't know kuti mwana wakeyo ndi number chani kubadwa and he doesn't know her. He might be sing'anga wa a Sato, just watch out.
People are wicked nowadays, so let us keep on praying for others. Kuno ndiye tizipemphera mpaka ena anapangidwa chipongwe apezekenso.