THE COURT..(Malawi )🤔

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 12 сен 2024

Комментарии • 461

  • @MwaleYankhoKatanga-k3e
    @MwaleYankhoKatanga-k3e Месяц назад +14

    The second wife is fully genius,

  • @JamesMalemba-tx4uh
    @JamesMalemba-tx4uh Месяц назад +17

    Very beautiful I need kumva chigamulo

  • @ishmaelimani3779
    @ishmaelimani3779 Месяц назад +32

    Apatsidwe gawo lawo mayiwo ,komaso ndasangalala mwayamba kuzenga mulandi mchichewa osati kufuna otathauzila tonse ndachewa 😅😅😅

    • @aminamussa9835
      @aminamussa9835 Месяц назад +3

      Point of correction, tose ndamalawi

    • @marianamwanje8968
      @marianamwanje8968 Месяц назад

      ​@@aminamussa9835ndiposo yonse ndachewa ndiye kuti chani eti

    • @EvelynDamiano-zg9kn
      @EvelynDamiano-zg9kn 29 дней назад

      M'bambo akakhala pa mitala amayenera mkazi aliyense azimupangira zotsogolo payekha ndi ana ake..momwe zilili apapa palibe chifukwa chomwe mkazi wamkulu atengere chuma kugawira mkazi wamng'onoyi..angoyamikanso kut ntsungwana uja wanena kut azimusamala brother wakeyo

  • @ChrispoGawani
    @ChrispoGawani Месяц назад +6

    Mwanayu ndi wa m'ng'ono akuyenera kusamalidwa aphunzire school yabwino azigona pabwino chuma adzapanga yekha msogolo m'mayi wa mkuluyi wavuta sapereka gawo la chuma komanso bamboyu analakwitsa osalemba will iyeyo ndiyemwe anayenera kugawa chuma adakali ndi moyo azibambo anzanga tiphunzirepo apa nkhani izi always zimavuta kwambiri

  • @user-xz3nz7dy1f
    @user-xz3nz7dy1f Месяц назад +20

    Na ngati wakulu adavomera kt ndi mitala ali mwana wa bambo chuma amupase komaso amupase 25% yamwa make 10%nkhani yatha

  • @MwaleYankhoKatanga-k3e
    @MwaleYankhoKatanga-k3e Месяц назад +3

    She knows how to explain,this marriage issue

  • @IsumailaSalanje
    @IsumailaSalanje Месяц назад +4

    Kumupatsa gawo lachuma kukhoza kulimbikitsa antchito kumagwa muchikondi ndimabwana.Mngosokoneza mabanja amenewa

  • @user-vu4cz1mt4f
    @user-vu4cz1mt4f Месяц назад +7

    Apatsidwe chuma chifkwa kuli mwana komanso akaz akuluwo anavomeleza

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu Месяц назад +7

    Chonde tibweleseleni nkhaniyi timve kuti anagamula bwanji so interesting 😂😂😂
    Komabe mwanayo akuyenela kumugawilako chifukwa amayiwa anavomeleza mitala linali banja ndithu akanafuna akanakana kuti mitala sakuifuna kangachepe ampaseko mwanayo

  • @gremmerchris71
    @gremmerchris71 23 дня назад +1

    Nkazi wachiwiri uziyamika kuti uyu woyambayu anakulola kulowa m'banja lawo komaso pokutenga kuti uzikamugwilila ntchito chokhacho uzimuyamika...usazitenge wapamwamba kwambili kuti wabeleka mwana wamamuna nzakoyo sikufuna koma zidangochitika..
    Komaso iwe nkazi woyamba kuti ufike pomwe ulipo dzidatengela nzakoyo kukhetsa thukuta ndikudzichepetsa kwakwe kuti iweyo ukhale umoyo ofewawo muthokoze pomupatsa shop imodzi over time mudzapeza ina basi simple..mukutelo pokuti iye ndiyemwe wasunga nfunda wanu basi

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w Месяц назад +6

    Amen good wafunsa funso labwino mkazi wa mkulu mahule wa ndi anthu oyipa wake kunalibe

    • @MeltonMumba-rn9mf
      @MeltonMumba-rn9mf Месяц назад

      Exactly

    • @patrisiobinalison8476
      @patrisiobinalison8476 Месяц назад

      Uyutu sihule ,mkazi wamkulu pomwe analakwila ndi kuvomeleza mitala

    • @GiftCMlangeni
      @GiftCMlangeni Месяц назад +1

      Mind your tongue remember ngati pali hule ndi abambowo not mkaziyo. Am also aman how can idate wantchito wanga? Mesa amkagwirantchito nde amakapempha banja ngati? Wamkukuyo adavomeleza bwanji mitala nde chitavute nchani kungomugawirako kuti asathe nthawi yaboma?
      Kungoti ndikupatsa business imodzi or minibus imodzi basi nkhani yatha. Komaso akuiwalakuti chuma chimatha, dzina la abambowo lilindi wamwamunayo, enawo mawanja akakavuta adzamufuna nchimwene wawoyo?? Nanga mayiwa akadzakalamba akaziwa adzakwanitsa zonse zomwe zimafunika mamuna akhalepo?? Mmmmh kuipamtima kukuoneka apa

  • @MustafaAmeen-tb6wd
    @MustafaAmeen-tb6wd Месяц назад +15

    Ngat nkazi anavomeleza mitala akuyenela amugawileko nzakeyo chumacho, congratulations ku mboni athandizedi mlongo wakeyo kuti naye azafike ngati pomwe ali iyepo

  • @PeterJafari
    @PeterJafari 2 дня назад

    Kodi anagamula bwanji guys ine ndikusaka koma sikupezeka koma mkadzi wang,onoyi akuyenera amupase ngawo lake ndithu

  • @kesterkaunda
    @kesterkaunda Месяц назад +1

    This is true story or movie?

  • @user-ni2vm8zx9t
    @user-ni2vm8zx9t 26 дней назад +1

    Is this acting classes?

  • @FRANCISLIFFAH
    @FRANCISLIFFAH 3 дня назад

    odandaulidwa munamvomera kunkhala akazi awiri, kwa m'bambo mozi sono musachuluke mzeru cfk mamunayo wamwalila

  • @user-mm2ek3cx8l
    @user-mm2ek3cx8l Месяц назад +4

    PA ana atatuwo dzanja alipo mmozi uyu ndiye mwana wamamuna mpaseni zabamboake

  • @ShadreckKwelani
    @ShadreckKwelani 27 дней назад +1

    Second wife agawilidwe mbali yake.

  • @MarkoMsango
    @MarkoMsango День назад

    Wang'onoyo ndiopusa komaso alive nzeru

  • @NedsonKennedy
    @NedsonKennedy Месяц назад +2

    The best way is, write willo b4 pass away 😂

  • @user-xo6th8bx2p
    @user-xo6th8bx2p 11 дней назад

    I don't think kubeleka mwana wammuna chikhale chitonzo pa anzawo , iwo adakangopempha thandizo la mwana osati mpaka chuma chifukwa mkazi wankulu kuvomeleza mitala sindiye kuti chilichose chomwe ali nacho ndye kuti nkazi wango'ono akhale nazo

  • @user-rj8bv9cw1r
    @user-rj8bv9cw1r Месяц назад +5

    Zaziiii agawe chani,amkaleka kumpasa chumacho mamunayo alipo bwa mg2 anthu oyipa akhoza kukumpha akhaula

    • @MikeMwale-bw1xw
      @MikeMwale-bw1xw Месяц назад +2

      Umfiti suposa pamenepo,kumakhala ndi umunthu palibe amadziwa za imfa kuti ingachitike mwachangu kwa bamboyo,ndili sure naye gawo lake lipezekapo akagamula.

    • @user-cn7uu4mb5n
      @user-cn7uu4mb5n Месяц назад

      Agawe chumacho

    • @PociahMack
      @PociahMack Месяц назад

      ​@@MikeMwale-bw1xw wina wazuzika naye wina kungochoka uko Ali agawe zosathekatu

    • @MikeMwale-bw1xw
      @MikeMwale-bw1xw Месяц назад +1

      @@PociahMack Ayi agawane anapangira limodzi,sikuti wangochoka uko nayeso anali mrs

    • @mphatsokauta6387
      @mphatsokauta6387 Месяц назад

      @@MikeMwale-bw1xw kungoti kwanthu kuno ma banja samayenda mwadongosolo

  • @vestarmkandawire6138
    @vestarmkandawire6138 Месяц назад +4

    Mkazi wa chigololo ameneyo ndi mbuzi,, banja ndi ndalama ndi zinthu ziwiri zosiyana. Mkazi woyamba ayankha bwino kuti adavomereza mwamunayi akhale awose osati chuma. Ndiye huleyo chuma chake ndimwana wamwamunayo. 1 Akumbukire kuti anali wa ntchito wa mayi wamkuluyo 2 wamulakwira kumulanda mwamuna wamwini. Apapa kunena zoona chuma asamugawire ndi wakuba mayiyu. Zikuonesa kuti wapha mwamuna ndiye kufuna chumacho.

    • @user-rt3nx4dx1t
      @user-rt3nx4dx1t Месяц назад +1

      Wolakwisa ndi mayi oyambayo povomereza mitala,chuma chiyenera kugawidwa basi

    • @FatimaAyami
      @FatimaAyami Месяц назад

      Mwanvetsa koma inu kapena ndinu achibale a MG1

    • @macdonaldkorea2928
      @macdonaldkorea2928 Месяц назад +1

      Inutu ndiodwala, munkhaniyi mwakambidwa zoti wina ndihule? Iwe momwe umkabadwa makolo akowo anakwatirana mwadongosolo? Kumasata nkhani osati mopusa.....

    • @macdonaldkorea2928
      @macdonaldkorea2928 Месяц назад

      @@user-rt3nx4dx1t nkhani koma imeneyi ndithu.....

    • @johnssanamah1408
      @johnssanamah1408 Месяц назад

      Vuto lowakhira nkhani pali za uhule apa mesa akuti unali mgwirizano oti ayese zida abambowo amafuna mwana wa mwamuna ndye atafunsidwa amayi akuluwo anavomera kuti vuto palibe atha kukhala pa mitala mwayi uwo mimba mkubwera akabadwe mwana chimphongo ndye kuti mdala Ku khosi mbeeee kuti mission yatheka mwana wa mwamuna wapezeka.
      Ndye chomuchulira kt ndi hule mumakhala chili chani....?????

  • @HenryLaidon-pl9ly
    @HenryLaidon-pl9ly Месяц назад +5

    1st born wa Dzanja from MG 1 uli ndi umunthu coz pa dziko pano uli ndi brother wako mmodzi from MG 2 komanso ndi mwana musamalire, komano zolinga ZENIZENI za MG 2 PA mlandu wu aaaaaa chabwino tiyeni tione kuti MALAMULO akuti chiyani

  • @samsonmtumbati4855
    @samsonmtumbati4855 Месяц назад +7

    Chuma chigawidwe kwa mkazi wachiwiri chifukwa kumenekonso kuli mwana wabamboyo amayiwo asaphangile chifukwa chakutinso mkazi woyambayo adavomereza kukwatiwa kwamkazi wachiwiri

  • @user-rm4kr8dj1e
    @user-rm4kr8dj1e День назад

    Where is the ruling. I need it pliz. Give me a link 😂

  • @HaroonHaji-rp4if
    @HaroonHaji-rp4if Месяц назад +1

    Malamulo amatiuza momveka bwino zachuma chamasiye mwana wamng'ono komanso ndimwamuna akuyenera kupatsidwa gawo lake koma akharea ndimtsinkhu woyenera ndipo MG 2 sakulakwitsa sichifukwa MG 1 pamene amavomereza mitala anadziwa zoti ali ndi chuma chimene umwini waukulu umakhara kwa ana

  • @LonjezoSingano
    @LonjezoSingano 19 дней назад

    Vuto ndi mayi mkulu kuvomeleza mitala mgayren nzanuyo bs

  • @AshleyMbewe-k5z
    @AshleyMbewe-k5z 23 дня назад

    I second with you bro,the rulling is very important

  • @MwaleYankhoKatanga-k3e
    @MwaleYankhoKatanga-k3e Месяц назад +1

    The first daughter is coming with some juries and want to run away from this as solution

  • @GilbertKuziona
    @GilbertKuziona Месяц назад +2

    Ngati mkazi wankulu akuziwa ndipo anavomeleza zamitala ndipo akudziwadi kut kuli mwana kwa mkazi wachiwiri akuyenera kumupasa gawo lake mwanayo

  • @ChimwemweWanga
    @ChimwemweWanga Месяц назад +2

    Na ngati anavomeleza mitala amugaile gawo lachumacho

  • @McDonaldKanyinji
    @McDonaldKanyinji Месяц назад

    As long as the first wife accepted that they were on polygamy, the worth is suppose to be shared according to how many kids each wife has......... but not equal..... Court should observe this.❤

  • @Standwell78
    @Standwell78 Месяц назад +2

    Abombo tiziyika konse konse chuma tisanamwalile chifukwa izi nde eee

  • @johnssanamah1408
    @johnssanamah1408 Месяц назад +1

    Mboni yafotokoza bwino zedi moti ndikuona akulandira gawo la chuma brother wakeyu

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 Месяц назад +2

    MG2 kutha mantha mpaka ku khothi kutengela MG1.

  • @josephgondwe5829
    @josephgondwe5829 Месяц назад

    Nkhanizi ndi za kuMalawi konkuno, I like it kuti you are using Chichewa osati zokhala ndi interpreter.

  • @YohaneJabesea-s8k
    @YohaneJabesea-s8k Месяц назад +2

    Mkazi wang'ono azipepha kuti amupatseko Osat kugawana

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Месяц назад +3

    Kwakoma ndikuno😅😅😂😂😂😅😅

  • @ChimwemweEddimael
    @ChimwemweEddimael Месяц назад +1

    Aah ine I think this is just acting why do I see the same faces on different cases or maybe it's only me 😂😂😂

    • @corretabanda7685
      @corretabanda7685 Месяц назад

      Eyaka ndi acting. Akufuna kuti anthu adzipita ku khoti zikaavuta, komanso anthu tidzitengerapo phunziro.

  • @EricThanda-qo3jz
    @EricThanda-qo3jz Месяц назад +2

    Koma akhale ndi tv yankhongo yomweyo😂😂

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w Месяц назад +1

    Kkkkkkkk akazinso alinso ndi ntchito mesa ndi anthu

  • @BrendaSinoya
    @BrendaSinoya 20 дней назад

    Watchitoyo anafoira bamboo alimoyo,akanapempha zake zoti aziyendesa ekha abambowo asanamwalire koma pot mphuno salota

  • @elsontmsukwa4356
    @elsontmsukwa4356 Месяц назад +2

    Ine ndimaganiza kuti chuma chisungike bwino chingokhara ndimunthu yumozi azichiyanganira kenako aziwapasako azake asowekera chinachake chifukwa akapupuluma kugawana mwana tava ndi wamungono nde mwina nikutheka awagawira koma koma mutu wa business alibe apeza chonse chathaso nde mwanayo azapezachani akakula 😢😢😢😢

    • @macdonaldkorea2928
      @macdonaldkorea2928 Месяц назад

      Ayi agawane chifukwa azimai okha okha sangamachitire zinthu limodzi

  • @peterjoshua2595
    @peterjoshua2595 Месяц назад

    I just like the guy who’s sat behind the accused 😅

  • @Memorymillanzi
    @Memorymillanzi 22 дня назад

    Ngati anafika polemba wantchito ndie chuma anali atapanga kale palibeso chifukwa chogawira chuma

  • @graciousbwanali5079
    @graciousbwanali5079 Месяц назад

    Gyz if i can have chance to coach people before the court ambiri sibwenzi akuluza milandu❤

  • @MilwardChanza-mr4yr
    @MilwardChanza-mr4yr 27 дней назад

    Mkazi wachiwiri anakakonda anamkagaila ma percentage angat?

  • @AgnessMaumbo
    @AgnessMaumbo 22 дня назад

    Akafukule amunache ankamuuza kuti amupatsa chuma adzamupatse,vuto la tsikana amasiya chomwe apitira maso muchanya kwa zimuna aeni ake kkkkk,akamaona nkazi akuoneka bwino amaona ngati akumusamala ndi mwamuna nde kumakhala kuti ndipite nane ndizikaoneka ngati amene aja,osadziwa kuti munthu wamayi amazilombikira yekha kkkkkkk,kuphunzitsa kwabwino amene akuonera atsikana aphunzirepo sure

  • @user-pc1rx7uj3s
    @user-pc1rx7uj3s Месяц назад +2

    Odandaula munavomela banja ndinso kuwabelekela mwana ,osati chuma ai ngati bambo sadapange gongosolo chafa kwanu mai

    • @MikeMwale-bw1xw
      @MikeMwale-bw1xw Месяц назад

      Koma banja mukulidziwa inuyo kapena mukungolubwa?

    • @SteveriaNyalugwe
      @SteveriaNyalugwe Месяц назад

      Ndipo mwamunayo akanasiya wilu asanamwalire, ndiye ngati mwamunayo sanamugawire mwana wake alimoyo samamuwelengera. Amafuna mwana osati chuma

  • @marianyirenda
    @marianyirenda 19 дней назад

    Komano walembedwa ntchito mphaka kumasukilana ndi a bwana wosachita mantha mphaka kuvomeleza kuti mukwatilana yikhale mitala ndi mkazi wa bwana mmmmm koma azimayi muzikhala ndi mantha please

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 24 дня назад

    Nkadzi wa chiwiliyo chuma akanapasidwa ndi mamunawakeyo chifukwa chumacho ndi cha kubanja lalikululo mamuna wanzeru satenga wa kwa Nkazi winabkupitisa kwina akanapanga zawo nthawi imene amunawo Ali ndi moyo😢

  • @user-mx5cx3gl4h
    @user-mx5cx3gl4h Месяц назад +2

    Hule ameneyo 😂😂😂eyeyo amachayilila chuma cha bambowo chifukwa chake amakachindana ndi abwana ake 😂😂musamupase kalikonse

    • @user-og1nx7en7j
      @user-og1nx7en7j Месяц назад

      😂😂😂😂😂😂 ooooh?

    • @BrendaMwandumba
      @BrendaMwandumba 26 дней назад

      Ndie malemuwo si hule?

    • @user-mx5cx3gl4h
      @user-mx5cx3gl4h 26 дней назад

      @@BrendaMwandumba onse ndimahule,,,ndiye asavutise kuti amugayileko chuma,, chifukwa iyeso anali ndi nyumba yake,,,,amusiye kazi woyambayo akhazila patendele,,,

  • @HannockMesiwni
    @HannockMesiwni Месяц назад +1

    Apachumacho chinera kugawidwa ndipo nkhani iyi yikuoneratu chilungamo chake ngakhale mwana wamaiwa wakuluyo akuyakhula chilungamo ndinthu apase gawo lawo amai achiwiriwa

  • @FrankNyoni-pm3jz
    @FrankNyoni-pm3jz Месяц назад

    What was the final judgment ?

  • @HildaMachinjiri
    @HildaMachinjiri Месяц назад +3

    😮😮😮 ati ana akazi alibe ntchito nkhani ija waiononga 😂😂

    • @user-xo6th8bx2p
      @user-xo6th8bx2p 11 дней назад

      Ndipo kuyankhula bwinobwino koyambilira kenako nkudzangosokonezanso ekha 😅

  • @user-gu1id5xg6k
    @user-gu1id5xg6k Месяц назад

    Choyankhulila chizungu nd chan pomwe tonse nd a Malawi??

  • @OmexMainala
    @OmexMainala Месяц назад +3

    Maio ndiovuta amafunika nkazinzaoyo amupaseko chuma

    • @MgGondwe
      @MgGondwe Месяц назад

      Ayi asamugawiri arindi mwano 😂😂 Wang, Ono. Uyo

    • @GloryNyirenda-c3i
      @GloryNyirenda-c3i Месяц назад

      Ine sindikuona chifukwa chomugailira chuma , iyenso anali ndi nyumba yake ndiye ngati sanapange naye chitukuko kunyumba kwakeko awo ndi mavuto ake , asayangane za mnyumba mwanzake, and after all enawo komwe achoka ndikutali akufuna akhale ndi katundu ofana ndi iyeyo oti amupeza dzulo! Za mwana Ati asamala mpaka adzaziimire payekha .. nkhani ndiyoti apondeponde apeze zochita.

    • @chifundobanda6814
      @chifundobanda6814 Месяц назад

      amugawire Kuti watani
      akulu bwanji sapempha zawakwamkuluyo aaaaa she lost

  • @henrymwale8994
    @henrymwale8994 Месяц назад +1

    Kodi izizi zimakhala zenizeni kapena ndi mwa drama coz anthu ake ndimaona amodzimodzi

    • @SoniahMussah
      @SoniahMussah 29 дней назад

      Drama😅

    • @user-jg2py7jj8c
      @user-jg2py7jj8c 29 дней назад

      Ndi drama yomwe imaphuzitsa anthu zokhudza khothi, malamulo, kuweluza milandu

  • @DeviMono-gv6vz
    @DeviMono-gv6vz Месяц назад

    Aninkhidwe chuma mwanayu nayenso limodzi ndi amayi ake azimwa wamkaka eeee litima bwanji mayi akuluwa?

  • @CathyMasina-q5v
    @CathyMasina-q5v Месяц назад

    Koma nkazi wachiwiliyu ndoipa wadyela😢

  • @dyba-x9w
    @dyba-x9w Месяц назад +1

    muzimalizitsa mpaka chigamulo osamasiira panjira ai

  • @user-mi8cx2qz7n
    @user-mi8cx2qz7n Месяц назад +1

    Iwe nkazi wachiwiri ndi wopusa chifukwa court imafuna umboni munasaina pati kuti ndikadzafa nkazi wankulu adzakugaira chuma

    • @MikeMwale-bw1xw
      @MikeMwale-bw1xw Месяц назад

      Mukunama akanadziwa bwanji kuti adzayanbe kufa ndi iyeyo.

  • @ashadokhomzy5781
    @ashadokhomzy5781 Месяц назад +1

    Yalakwatu apa kaya tidikile final episode kuti zitha bwanji

  • @user-dg9bh2xo8x
    @user-dg9bh2xo8x Месяц назад +1

    Koma akazi olandawa ngokupangitsa munthu kugwila nyasi

  • @user-ym6xu3xt2i
    @user-ym6xu3xt2i Месяц назад +1

    Ama gawa chuma ndi a ku chimuna osati mnkanzi mzako ayi zimatero ndithu

  • @user-sd4jn8ef7e
    @user-sd4jn8ef7e Месяц назад

    ❤ Mai awa sakuyakhura mwanzeru'!!

  • @user-io2uw2me9f
    @user-io2uw2me9f Месяц назад +1

    Amugaileko mwanayo koma osat zimenezozo mesa anakwatila so komaso uyuyu wabereka boy akungoyenela

  • @user-bh7xq3wf1i
    @user-bh7xq3wf1i Месяц назад

    Zogawana palibe aliyense pamalo pake

  • @KondwaniHara
    @KondwaniHara Месяц назад +1

    Chagamulo bwanji?

  • @henrychikuse1543
    @henrychikuse1543 Месяц назад +1

    Uhule ulibe profit chemwali. Komaso kulibeko mau oti amuna athu koma amuna Anga. Mwana wanu ndiwakuchigololo ndiye mwana wakuchigololo sawerengedwa

  • @listonnantapo1670
    @listonnantapo1670 Месяц назад

    Tikudikira chigamulo. Chinapelekedwa, kapena sichinapelekedwe?

  • @neighbourfilms
    @neighbourfilms Месяц назад

    Sound track is too loud please

  • @lazaruschitsamba8394
    @lazaruschitsamba8394 Месяц назад +1

    no ngati anafikila zintu atagwila njito alibe chake

  • @jameswajumpha6790
    @jameswajumpha6790 29 дней назад

    Waiting for next part

  • @chimuemuechingagwe175
    @chimuemuechingagwe175 Месяц назад

    Milandu imeneyi imakhala yowona kapena amangoyerekeza?

  • @RobsaiSaidi
    @RobsaiSaidi Месяц назад

    Bwanji you don't fully finish your court trials... whats the point of not letting us know the judgement. I. USA they finish fully. We love watch such stuff

  • @RemitterFlik1130
    @RemitterFlik1130 Месяц назад +3

    Ndipo anthu musamangoti a agawe agawe muli inu mungapange zimenezo uyotu ndi hule apezaso bambo wina kuti abelekele mwana wa nkazi sinanga ali pa business yopangila ana kwa zibambo omwe akufuna ana osiyana m nyumba ine ndikuti asampase....

  • @judithchaima
    @judithchaima 26 дней назад

    Mwana wamkazi alibe phindu Mai uyu akuyankhula bwanji? Uyu uhule wake zimuonekera ndithu

  • @MCLoudZeka
    @MCLoudZeka Месяц назад +1

    chigamulo chikut bwanji tinveka

  • @AfonsoBenjamim-k6k
    @AfonsoBenjamim-k6k Месяц назад

    Munthu walembedwa ntchito chofunilanso abwana ndichani ? Musampase hule ameneyo

  • @TumpaleMsukwa-l4i
    @TumpaleMsukwa-l4i 29 дней назад

    Kma poti ana akazi alibe ntchitopo akurakwisa ana ndi ana zilibe ntchito kt ndiakazi or aamuna

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq Месяц назад +1

    You are excellent girl.

  • @KamongoNowa
    @KamongoNowa 19 дней назад

    Chuma chigawidwe basi

  • @user-jm7tv7rm7e
    @user-jm7tv7rm7e Месяц назад

    Azibambo muziwapatsiratu ma mg 2 gawo lawo musanafe

  • @bonfacekantwanje6223
    @bonfacekantwanje6223 Месяц назад

    Akuti akufuna chuma Cha chani? Koma guys😊

  • @mphatsokauta6387
    @mphatsokauta6387 Месяц назад

    palibe kumugawila koma kugawana...100% ya assets yo then awona anthu oyenela kugawana ndangati then aliyense atenge percentage yake. community of property ijayo

  • @IdrissahJames-gu2yo
    @IdrissahJames-gu2yo 25 дней назад

    Zinko nd Anthu ake....koma apopo plz plz 😢 Awapatseko Gawoo la Chumachoo plz plz

  • @KondwaniGumba
    @KondwaniGumba Месяц назад

    Ngati adali mkazi wa malemu ndikumuberekera mwana , akufunika kukhara ndi gawo la chuma Cha mamuna wawe. Ndikukhulupirira kuti pakutha pa khaniyi ikomera odandaula.

  • @SteveSangwa-tb7lk
    @SteveSangwa-tb7lk Месяц назад

    Wakuba ameneyo ku banjako anapitilako chumacho

  • @MagangaLeman
    @MagangaLeman Месяц назад +1

    Muzitipasilanso nthawi ya chigamulo kuti tizitengelapo phunzilo

  • @MonicaThocco
    @MonicaThocco Месяц назад

    Mwamuna wa mwini ndi wa mwini basi ,ndipo mwana ndi mwana posayang'ana kuti mwanayo ndi wa mkazi or wa mwamuna ,anali pa business acc wa ,aluza basi

  • @miryamkatundulu
    @miryamkatundulu Месяц назад

    Please men before you die, write your last testament and will so that life is not complicated.

  • @alnordtembo8930
    @alnordtembo8930 Месяц назад

    Yuleyo anamumangira kare nyumba yake naye nde chuma chakaicho

  • @gracejere452
    @gracejere452 Месяц назад +1

    Mboni yufanana ndi step mom😂😂😂

  • @rachelbanda-xh7iv
    @rachelbanda-xh7iv Месяц назад

    Agawireni chabe zapadziko izi ndizotsala

  • @ShamirahMakungwa
    @ShamirahMakungwa Месяц назад

    Munthu utha kuvomera mitala malingana ndinyengo mmene iliri...vuto ndimalemuo coz sitikuziwa kuti ankagwirizana chani ndiwantchito wawo akakhala awiri.kmanso ngati inali mitala mamuna amapanga equal popanga zithu.iwowo kod sanasiye will...

  • @user-zz4uj4yt7p
    @user-zz4uj4yt7p Месяц назад

    Balibe zogawana aliyense amagawa kantudu uyo ndi hule

  • @user-vu4cz1mt4f
    @user-vu4cz1mt4f Месяц назад +8

    Komatsu inu omwe mumapanga post muzimalizitsa mpaka kuchigamulo coz timaphunzilira momwemu

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw Месяц назад +1

    Kkkkkkkkkk koma apa zivuta